ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Koma nkhani ndiyakuti bolani kwathandiza apite akakhale ndi abale awo .koma ambuye apamene mukuchilitsa onse odwala osayiwale abambo amenewa🙏🙏
Ambuye mene mukuchilitsa ena gogo Rodgers Zuze musawapitilire 🙏😢
Iiii koma pepani agogo anga
Monga mmene anachilitsira Yobu, Ambuye awachilitsanso a LupiyaAmen 🙌
Mr lumbe please yingo kwathandiza transport yokafikira kwawo ku mulanje is best way
Akamutafunako bola apite ku hospital
So sad😢
Ambuye achilitseni bambowa "komaso achibale ndi ana chonde komwe muliko athandizeni bambowa
yehova mulungu ndiwachikondi wachifundo mopepha awachosele ululu kwa lupiya🙏🏻🙏🏻🙏🏻
Abale may God see him through 🙏🏾
Mulungu woziwa kuchilisa achiliseni abambo wa😢😢😢😢
Eish zosayendatu,,, ambuye akuoneni mukhale bwino
Eeeeiiish ambuye achitireni chifundo bambowa
God have mercy 😢
Ambuye muchitilen chifundo mwana wanu
Lord have mercy 😭😭🙏🙏
Zokhudza😢
Mmmm gogo ali mmavuto uyu ambuye awakhuze
Ambuye tipempha nkono wanu wamachilitso🙏🙏
Pamene kumwamba mukukambilana zoyendela ena awaso muwayendele Ambuye
Mulungu adalitse bambo Rhodgers ndidzanja lamachilitso
Koma achibale awo akudziwa za m'bale wawo mene alili
Eeeeee koma ana amenewo amati bamboo awo Ali kut😭😭😭
Old age azibambo ambiri amagwidwa ndi matenda amenewa koma kuchipatala amangchila koma nkhani ndi chisamaliro alibe owasamala ..... Ambuye awakhuze
Kuchila imakhala mwai chabe
Ndipo inu ,bambo anga nthenda yomwe anamwalilira ndiyomweyi ndendende
nkhani zi zimandivesa chison ,muyendelekoso ku nkhatabay kwa TA malenga mzoma village lichenga Cheyeka kuli mayi loyina Ali ndi ana olumala ndi azibale akeso ngolumala ,mayuka, Jojo chutuwep osewo ngolumana ayendelen ndithu
Ambuyee😢😢😢
Mulungu wachisoni mukhala bwino agogo inshallah
oooh Allah make easy for him heal him give him good health😢😢😢 u know everythings 🤲🤲🤲🤲
Ambuye khuzani mwana wanu amene akuvutika ndi matenda ambuye dzanja lanu silalifupi kut simungakhudze chitan nawo abambo awo amene akumva ululu wa siku ndi siku ndkuziwa ine mbuye wanga mukayamba ntchito mumayimaliza
Akuyenela chisamaliro athandizidwe kut azipita kwawo penanso koma limatha kukhala Vuto lamtima akaunikidwe moyenela😢😢😢
Too bad koma mulungu ndiwadongosolo amen.
Mulungu aikepo zanja
May the Almighty God heal you in Jesus' name amen.
Ambuye akumbukireni bambowa ndi machiritso anu
Atengereni kuchipatala inkhonza kunkhala prostate cancer..komanso apite kwao.
eish💔koma makolo osamafika powataya chonchi ana awowo akunva bwanji💔😭ndiakumudzi kwathu kumulanje mmh
Sanawataye mwina bambowa anachoka kale kalemwinaso kumudzi kwawo anthu akwawo sakudziwa mene alili tikamakhala koyenda nthawi Zina kumudzi tizikumbukirako abale chifukwa zimathandiza kuti tizidziwana mene moyo ukuyendera pena zimavuta achibale kusamala matenda kutengera mene zinalili mbuyomo
😭😭😭
Ambuye ndiwabwiño😢😢😢
Ambuye tumizani machiriso chilichonse munathana nacho pa mtanda paja ndinu yemweyo zulo lero ndi kunthawi zonse
Ambuye awachitile chifundo
Amen
EISH Koma mulungu achitileni chifundo
Ambuye oziwa kuchilitsa mkhuzeni mwana wanu ndimkono wamachilitso paikha sangathe🙏🙏
God help this man to recover from the disease he is suffering from 🙏
Chachikulu angopta kwawo ndithu mmm
Anthu akuvutikatu 😢😢😢
Murungu aikirepo dzanja
eish
Ambuye awakhuze chonde😥
Achibale akutipo chani alipo or ayi Mulungu achitapo kathu
Penatu umakhala vuto la mtima bambo anganso ankadwala choncho
Eeeeee zokhuza kwambiri
Boni kalindo bwa
Mukhara bwn madala
So sad
Koma nkhani ndiyakuti bolani kwathandiza apite akakhale ndi abale awo .koma ambuye apamene mukuchilitsa onse odwala osayiwale abambo amenewa🙏🙏
Ambuye mene mukuchilitsa ena gogo Rodgers Zuze musawapitilire 🙏😢
Iiii koma pepani agogo anga
Monga mmene anachilitsira Yobu, Ambuye awachilitsanso a Lupiya
Amen 🙌
Mr lumbe please yingo kwathandiza transport yokafikira kwawo ku mulanje is best way
Akamutafunako bola apite ku hospital
So sad😢
Ambuye achilitseni bambowa "komaso achibale ndi ana chonde komwe muliko athandizeni bambowa
yehova mulungu ndiwachikondi wachifundo mopepha awachosele ululu kwa lupiya🙏🏻🙏🏻🙏🏻
Abale may God see him through 🙏🏾
Mulungu woziwa kuchilisa achiliseni abambo wa😢😢😢😢
Eish zosayendatu,,, ambuye akuoneni mukhale bwino
Eeeeiiish ambuye achitireni chifundo bambowa
God have mercy 😢
Ambuye muchitilen chifundo mwana wanu
Lord have mercy 😭😭🙏🙏
Zokhudza😢
Mmmm gogo ali mmavuto uyu ambuye awakhuze
Ambuye tipempha nkono wanu wamachilitso🙏🙏
Pamene kumwamba mukukambilana zoyendela ena awaso muwayendele Ambuye
Mulungu adalitse bambo Rhodgers ndidzanja lamachilitso
Koma achibale awo akudziwa za m'bale wawo mene alili
Eeeeee koma ana amenewo amati bamboo awo Ali kut😭😭😭
Old age azibambo ambiri amagwidwa ndi matenda amenewa koma kuchipatala amangchila koma nkhani ndi chisamaliro alibe owasamala ..... Ambuye awakhuze
Kuchila imakhala mwai chabe
Ndipo inu ,bambo anga nthenda yomwe anamwalilira ndiyomweyi ndendende
nkhani zi zimandivesa chison ,muyendelekoso ku nkhatabay kwa TA malenga mzoma village lichenga Cheyeka kuli mayi loyina Ali ndi ana olumala ndi azibale akeso ngolumala ,mayuka, Jojo chutuwep osewo ngolumana ayendelen ndithu
Ambuyee😢😢😢
Mulungu wachisoni mukhala bwino agogo inshallah
oooh Allah make easy for him heal him give him good health😢😢😢 u know everythings 🤲🤲🤲🤲
Ambuye khuzani mwana wanu amene akuvutika ndi matenda ambuye dzanja lanu silalifupi kut simungakhudze chitan nawo abambo awo amene akumva ululu wa siku ndi siku ndkuziwa ine mbuye wanga mukayamba ntchito mumayimaliza
Akuyenela chisamaliro athandizidwe kut azipita kwawo penanso koma limatha kukhala Vuto lamtima akaunikidwe moyenela😢😢😢
Too bad koma mulungu ndiwadongosolo amen.
Mulungu aikepo zanja
May the Almighty God heal you in Jesus' name amen.
Ambuye akumbukireni bambowa ndi machiritso anu
Atengereni kuchipatala inkhonza kunkhala prostate cancer..komanso apite kwao.
eish💔koma makolo osamafika powataya chonchi ana awowo akunva bwanji💔😭ndiakumudzi kwathu kumulanje mmh
Sanawataye mwina bambowa anachoka kale kalemwinaso kumudzi kwawo anthu akwawo sakudziwa mene alili tikamakhala koyenda nthawi Zina kumudzi tizikumbukirako abale chifukwa zimathandiza kuti tizidziwana mene moyo ukuyendera pena zimavuta achibale kusamala matenda kutengera mene zinalili mbuyomo
😭😭😭
Ambuye ndiwabwiño😢😢😢
Ambuye tumizani machiriso chilichonse munathana nacho pa mtanda paja ndinu yemweyo zulo lero ndi kunthawi zonse
Ambuye awachitile chifundo
Amen
EISH Koma mulungu achitileni chifundo
Ambuye oziwa kuchilitsa mkhuzeni mwana wanu ndimkono wamachilitso paikha sangathe🙏🙏
God help this man to recover from the disease he is suffering from 🙏
Chachikulu angopta kwawo ndithu mmm
Anthu akuvutikatu 😢😢😢
Murungu aikirepo dzanja
eish
Ambuye awakhuze chonde😥
Achibale akutipo chani alipo or ayi Mulungu achitapo kathu
Penatu umakhala vuto la mtima bambo anganso ankadwala choncho
Eeeeee zokhuza kwambiri
Boni kalindo bwa
Mukhara bwn madala
So sad