Gogo Rodgers Zuze (74) battles inflammation of the manhood

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 58

  • @HawaMamo-q2v
    @HawaMamo-q2v 2 หลายเดือนก่อน +9

    Koma nkhani ndiyakuti bolani kwathandiza apite akakhale ndi abale awo .koma ambuye apamene mukuchilitsa onse odwala osayiwale abambo amenewa🙏🙏

  • @ChifundoJeffrey
    @ChifundoJeffrey 2 หลายเดือนก่อน +5

    Ambuye mene mukuchilitsa ena gogo Rodgers Zuze musawapitilire 🙏😢

  • @BlessingsMalunga-d8o
    @BlessingsMalunga-d8o หลายเดือนก่อน +1

    Iiii koma pepani agogo anga

  • @ScillaMau
    @ScillaMau 2 หลายเดือนก่อน +1

    Monga mmene anachilitsira Yobu, Ambuye awachilitsanso a Lupiya
    Amen 🙌

  • @Mavitoabdulla
    @Mavitoabdulla 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mr lumbe please yingo kwathandiza transport yokafikira kwawo ku mulanje is best way

    • @lastondaniel6697
      @lastondaniel6697 2 หลายเดือนก่อน

      Akamutafunako bola apite ku hospital

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 2 หลายเดือนก่อน +1

    So sad😢

  • @DrolieDongowa
    @DrolieDongowa หลายเดือนก่อน

    Ambuye achilitseni bambowa "komaso achibale ndi ana chonde komwe muliko athandizeni bambowa

  • @Rhoda-g1y
    @Rhoda-g1y 2 หลายเดือนก่อน +1

    yehova mulungu ndiwachikondi wachifundo mopepha awachosele ululu kwa lupiya🙏🏻🙏🏻🙏🏻

  • @mimizammimba7506
    @mimizammimba7506 2 หลายเดือนก่อน

    Abale may God see him through 🙏🏾

  • @nerrcejngulube
    @nerrcejngulube 4 วันที่ผ่านมา

    Mulungu woziwa kuchilisa achiliseni abambo wa😢😢😢😢

  • @bernarddaniel4413
    @bernarddaniel4413 2 หลายเดือนก่อน +1

    Eish zosayendatu,,, ambuye akuoneni mukhale bwino

  • @Lloyd-gd6pu
    @Lloyd-gd6pu หลายเดือนก่อน

    Eeeeiiish ambuye achitireni chifundo bambowa

  • @dorothymanda9106
    @dorothymanda9106 2 หลายเดือนก่อน

    God have mercy 😢

  • @yaokingdailess
    @yaokingdailess 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye muchitilen chifundo mwana wanu

  • @JaydreamDream
    @JaydreamDream 2 หลายเดือนก่อน

    Lord have mercy 😭😭🙏🙏

  • @SankpA-t9
    @SankpA-t9 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zokhudza😢

  • @BenjaminMtima
    @BenjaminMtima 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mmmm gogo ali mmavuto uyu ambuye awakhuze

  • @isaacfesani2357
    @isaacfesani2357 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye tipempha nkono wanu wamachilitso🙏🙏

  • @BazlioDenja
    @BazlioDenja 2 หลายเดือนก่อน

    Pamene kumwamba mukukambilana zoyendela ena awaso muwayendele Ambuye

  • @ManuelMalunga-j3l
    @ManuelMalunga-j3l 2 หลายเดือนก่อน

    Mulungu adalitse bambo Rhodgers ndidzanja lamachilitso

  • @MarkGonda-qr4vm
    @MarkGonda-qr4vm หลายเดือนก่อน

    Koma achibale awo akudziwa za m'bale wawo mene alili

  • @PriscillaKamkuzi
    @PriscillaKamkuzi 2 หลายเดือนก่อน +1

    Eeeeee koma ana amenewo amati bamboo awo Ali kut😭😭😭

  • @MadalitsoBokosi-j3u
    @MadalitsoBokosi-j3u 2 หลายเดือนก่อน

    Old age azibambo ambiri amagwidwa ndi matenda amenewa koma kuchipatala amangchila koma nkhani ndi chisamaliro alibe owasamala ..... Ambuye awakhuze

    • @lastondaniel6697
      @lastondaniel6697 2 หลายเดือนก่อน +1

      Kuchila imakhala mwai chabe

    • @LekeThomson
      @LekeThomson 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo inu ,bambo anga nthenda yomwe anamwalilira ndiyomweyi ndendende

  • @vatineseduwin
    @vatineseduwin 2 หลายเดือนก่อน

    nkhani zi zimandivesa chison ,muyendelekoso ku nkhatabay kwa TA malenga mzoma village lichenga Cheyeka kuli mayi loyina Ali ndi ana olumala ndi azibale akeso ngolumala ,mayuka, Jojo chutuwep osewo ngolumana ayendelen ndithu

  • @BridgetKasira-bi2js
    @BridgetKasira-bi2js 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ambuyee😢😢😢

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 2 หลายเดือนก่อน

    Mulungu wachisoni mukhala bwino agogo inshallah

  • @tambalahaggebunaya
    @tambalahaggebunaya 2 หลายเดือนก่อน +3

    oooh Allah make easy for him heal him give him good health😢😢😢 u know everythings 🤲🤲🤲🤲

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye khuzani mwana wanu amene akuvutika ndi matenda ambuye dzanja lanu silalifupi kut simungakhudze chitan nawo abambo awo amene akumva ululu wa siku ndi siku ndkuziwa ine mbuye wanga mukayamba ntchito mumayimaliza

  • @NaomiMoyo-x2r
    @NaomiMoyo-x2r 2 หลายเดือนก่อน

    Akuyenela chisamaliro athandizidwe kut azipita kwawo penanso koma limatha kukhala Vuto lamtima akaunikidwe moyenela😢😢😢

  • @LazarousKasambala
    @LazarousKasambala 2 หลายเดือนก่อน

    Too bad koma mulungu ndiwadongosolo amen.

  • @BakaliJustice
    @BakaliJustice 2 หลายเดือนก่อน

    Mulungu aikepo zanja

  • @Wyson-bo3sp
    @Wyson-bo3sp 2 หลายเดือนก่อน

    May the Almighty God heal you in Jesus' name amen.

  • @ChisambaChidzungu
    @ChisambaChidzungu 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye akumbukireni bambowa ndi machiritso anu

  • @ericchilinjala481
    @ericchilinjala481 2 หลายเดือนก่อน

    Atengereni kuchipatala inkhonza kunkhala prostate cancer..komanso apite kwao.

  • @PatienceMaere
    @PatienceMaere 2 หลายเดือนก่อน

    eish💔koma makolo osamafika powataya chonchi ana awowo akunva bwanji💔😭ndiakumudzi kwathu kumulanje mmh

    • @MarkGonda-qr4vm
      @MarkGonda-qr4vm หลายเดือนก่อน

      Sanawataye mwina bambowa anachoka kale kalemwinaso kumudzi kwawo anthu akwawo sakudziwa mene alili tikamakhala koyenda nthawi Zina kumudzi tizikumbukirako abale chifukwa zimathandiza kuti tizidziwana mene moyo ukuyendera pena zimavuta achibale kusamala matenda kutengera mene zinalili mbuyomo

  • @JanettWesly
    @JanettWesly 5 วันที่ผ่านมา

    😭😭😭

  • @GraceLobart
    @GraceLobart 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye ndiwabwiño😢😢😢

  • @FrankLeckson
    @FrankLeckson 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye tumizani machiriso chilichonse munathana nacho pa mtanda paja ndinu yemweyo zulo lero ndi kunthawi zonse

  • @RuthMatimba-l1d
    @RuthMatimba-l1d 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye awachitile chifundo

  • @austenmalawi
    @austenmalawi 2 หลายเดือนก่อน

    EISH Koma mulungu achitileni chifundo

  • @ShakiraBiton
    @ShakiraBiton 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye oziwa kuchilitsa mkhuzeni mwana wanu ndimkono wamachilitso paikha sangathe🙏🙏

    • @Oliver-2019
      @Oliver-2019 2 หลายเดือนก่อน

      God help this man to recover from the disease he is suffering from 🙏

  • @AlinafeMoses
    @AlinafeMoses 2 หลายเดือนก่อน

    Chachikulu angopta kwawo ndithu mmm

  • @WenaniMwenda
    @WenaniMwenda 2 หลายเดือนก่อน +1

    Anthu akuvutikatu 😢😢😢

  • @MaliamuSikawa
    @MaliamuSikawa 2 หลายเดือนก่อน

    Murungu aikirepo dzanja

  • @GiftChimtedza
    @GiftChimtedza 2 หลายเดือนก่อน +1

    eish

  • @CatherineMustafa-dq4qm
    @CatherineMustafa-dq4qm 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye awakhuze chonde😥

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 2 หลายเดือนก่อน

    Achibale akutipo chani alipo or ayi Mulungu achitapo kathu

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw 2 หลายเดือนก่อน

    Penatu umakhala vuto la mtima bambo anganso ankadwala choncho

  • @RhodneyBwa3
    @RhodneyBwa3 2 หลายเดือนก่อน

    Eeeeee zokhuza kwambiri

  • @HawaMamo-q2v
    @HawaMamo-q2v 2 หลายเดือนก่อน

    Boni kalindo bwa

  • @edgarmax-pi1bx
    @edgarmax-pi1bx 2 หลายเดือนก่อน

    Mukhara bwn madala

  • @BrightLuciano
    @BrightLuciano 2 หลายเดือนก่อน

    So sad