Mpungwepungwe pa kudwala kwa Mary Chilima ''zowona mpaka 312 million''

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 27 ต.ค. 2024
  • The K311 million doesn't include medical bills, folks. It's just pocket money.

ความคิดเห็น • 36

  • @overcomers909
    @overcomers909 2 ปีที่แล้ว +2

    If thats what his condition of service since he is vice president of Malawi and if your currency is devalued badly K312m malawi currency

  • @ahamadulmbishana6629
    @ahamadulmbishana6629 2 ปีที่แล้ว +4

    Komad ndilamayo yachuluka osangowasiya afe bwanji ndilamazo akagulile Fertiliser wadulayu

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 2 ปีที่แล้ว +2

    Eish komatu Malawi ndiye wafikadi pa worse But i curse the coming of Lazarus Chakwera God is Watching you guys 😫😫

  • @emmanuelweja9606
    @emmanuelweja9606 2 ปีที่แล้ว +2

    Kodi alibe medical aid?sagwada zomwe amuthyolazo apite ku mwai wathu hospital or Adventist ,osati zowatengera amalawi kuntoso ai

  • @blandinabonaventure5474
    @blandinabonaventure5474 2 ปีที่แล้ว +3

    Iwowo salary zawo ntchito yake ndichani mmmmmm kma misokho yathu mmmmm mavuto kwambiri

  • @brendadumisan2526
    @brendadumisan2526 2 ปีที่แล้ว +3

    Mmmmmm koma nde mwatiseweresa ife amalawi zafikapa mukutiuza kuti muzipataramo odwara ndi nkazi chilima yekha kuti muziseweresa ndarama chonchi mmalo mokonza mavuto koma mwatizunza ife amalawi Mulungu akakulangani inu

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 2 ปีที่แล้ว +2

    Zikuchita kuwoneka kuti anthuwa ndi akumazidi wotumidwa ndi satana, munthu wamzelu sungawononge ndalama yoseyi pamene athu akulila za njala, mankhwala muzipatala, kukwela kwa zinthu, feteleza, koma ndiye yah asiyeni gahena linayasama kale kudikilila anthu ankhazawa,
    Chilimayo malipilo ake akugwila ntchito yanji? Shame to my fellow poor Malawians

  • @hanafi4766
    @hanafi4766 2 ปีที่แล้ว +2

    Chilima hemust youz money from in his pocket this politicals the don't think for athars there Sany Of davors

  • @blandinabonaventure5474
    @blandinabonaventure5474 2 ปีที่แล้ว +2

    Zitsiru zimenezi misokho yathu kma aliyese Ali ndi ufulu zikomo kwambiri mbuzi a utm nonse, +mcp tonse zipani 9 zero

  • @charlesmuyaya8839
    @charlesmuyaya8839 2 ปีที่แล้ว +3

    Iwe voice yako si yabwino, ma videos akonso umawapanga mopusa. No interesting at all

  • @chifundonkhoma3642
    @chifundonkhoma3642 2 ปีที่แล้ว +2

    But these are their entitlements, don't compare the amount of money to the living standards of a commoner.... Guys we need to think, asagwiritse ntchito ma entertainments awo chifukwa wina aganiza kuti a kuwononga ndalama, izi ndi chimodzi modzi kuti musawalipire ogwira ntchito m'boma chifukwa a Malawi ena omwe Sali pa ntchito akuvutika ku mudziku... Ayi it's high time we need to change thinking like idiots....

  • @robenallie6985
    @robenallie6985 2 ปีที่แล้ว +2

    312milion thats tonse alliance

  • @JohnMatope49
    @JohnMatope49 2 ปีที่แล้ว +2

    Anthuwatu ali pa pikisanu and zawathu sakuwelengaso ayi

  • @jimmyzgambo9928
    @jimmyzgambo9928 2 ปีที่แล้ว +2

    Akupanga zopusa kwambiri

  • @customer4784
    @customer4784 2 ปีที่แล้ว

    Mukuononga ma millions koma kukanika kutsitsa mtengo wa fertilizer....😩

  • @dysonmbizi9734
    @dysonmbizi9734 2 ปีที่แล้ว +2

    Wanthu wanyakhe wonjoya mchalo muno mweee mmmm

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 2 ปีที่แล้ว +2

    No sense full

  • @dijayusuf2918
    @dijayusuf2918 2 ปีที่แล้ว +2

    This is not fair

  • @emmakamwendo1370
    @emmakamwendo1370 3 หลายเดือนก่อน

    Awesome

  • @alickhassan181
    @alickhassan181 2 ปีที่แล้ว +2

    Kalanga ine malawi ine chete🇬🇹

  • @stevinmuhone877
    @stevinmuhone877 2 ปีที่แล้ว +2

    Akwanilitse zimene akufuna

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani 4 หลายเดือนก่อน

    Amalawi ochuluka akungodzifera mudzipatalamu kamba kosowa mankhwala pamene boma likukhuthula ndalama dzankhaninkhani pa munthu mmodzi😢😢😢

  • @OjesYahaya-zl4rx
    @OjesYahaya-zl4rx 4 หลายเดือนก่อน

    Athu akumwalila zimpatalamu kamba kosowa Panado ndiye Muthu mozi ndalama zosezo kusonyeza kuti miyo yanuyo ndiye yofunikila mumwalilabe mutisiya aphawife mulungu sowona chuma

  • @lawrencenoson9777
    @lawrencenoson9777 2 ปีที่แล้ว +3

    Mbola Kwantele boma

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 4 หลายเดือนก่อน

    Musiyeni akwere ndege agwe naye afeso ngati chakwera wamuloza kaziyo.kuti apite

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 5 หลายเดือนก่อน

    Ai zikomo Mulungu azikuonani

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 4 หลายเดือนก่อน

    Inu chakwera niamene wamuroza kuti afe dikirani muva kuti nayeso wamwarira

  • @henzomanzo9158
    @henzomanzo9158 2 ปีที่แล้ว

    That's bull sh*t

  • @bonifacekanyinji2517
    @bonifacekanyinji2517 2 ปีที่แล้ว

    Yemwe azavotere chilima ndi chule

    • @hanifamw
      @hanifamw  2 ปีที่แล้ว

      iiiii zomwezi lol