Chisomo Nyamalikiti Nthiwatiwa Mdala - Barabas

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 48

  • @yaobleestelle2513
    @yaobleestelle2513 5 ปีที่แล้ว +3

    40. Abale a ku Africa, Asia, Europe ndi America! Inu mwina munali kuyembekezera Uthenga wa Mateyu 25:6 mwinamwake mu dziko lanu koma Mulungu anachita izo mosiyana. Kumbukirani Ambuye wathu Yesu Khristu! Pokhala mkulu wa ansembe Melkizedeki, achirabi ndi alembi anaona kuti Iye adzachokera ku fuko la Levi. Koma Iye adachokera ku fuko la Yuda. Ndiye, Uthenga Wake ndi ntchito Zake zinatsimikizira kuti Iye anali Mesiya. Ndipo lero pa nkhope yonse ya dziko lapansi, ngati iwe uli mwana wa Mulungu, malo ako awa ali pano ndi m’neneri wa nthawi yako, M’neneri Kacou Philipe. Ndipo amene ali ndi makutu akumva amve.

  • @estherwawa8439
    @estherwawa8439 5 ปีที่แล้ว +5

    18. Uthenga uwu ukunena kuti mabungwe onse, magwirizano ndi zitaganya za mipingo, m’maiko kapena padziko lonse, ndi zimbalangondo, zithunzi za satana kugwirira ncthito chifukwa cha Satana.

  • @medsonboti1984
    @medsonboti1984 4 ปีที่แล้ว +1

    Here comes my best poet. He is he best.

  • @jemimaahemin8359
    @jemimaahemin8359 5 ปีที่แล้ว +4

    40. Ndipo wa chi Aarabu anandiuza ine, "Kodi chili choipa kuti galu wako atembenukire ku chipembedzo chako?" Iye adzakutumikira bwinoko!“ Ndinamufunsa wa Chiarabu uyu ngati agalu ake angakhale imam kapena Ayatollah wake? Ndipo iye anati, "Bwera udzalalikire kuno ku Iran". Ndipo ndinamuuza kuti: Inu komanso Akhristu, Ahindu, Mabuddha ndi Ayuda mumakhulupirira chipembedzo ndi m'mabuku opatulika koma simumakhulupirira mwa Mulungu chifukwa Mulungu amangolankhula kudzera mwa aneneri amoyo. Ndipo ine, Kacou Philippe, amene akulayankhula ndi iwe, si kwa inu achipembedzo komwe ine ndatumizidwa ndipo Uthenga wanga ndi mkate wopatulika, si chakudya cha chipembedzo. Ndipo ndine wanzeru mokwanira kusapereka mkate wopatulika uwu ku Iran, nyama yomwe ingatafuniretu ziwiri zonse mkate ndi zala.

  • @bensondumbo4336
    @bensondumbo4336 ปีที่แล้ว

    Mwini nsinjiro zachiyakhulo Nyamalikiti ,awa ndi akatundu

  • @richardkamwezi9297
    @richardkamwezi9297 4 ปีที่แล้ว

    Probably the best piece by Nyamalikiti

  • @georgechifundochiwaula3846
    @georgechifundochiwaula3846 ปีที่แล้ว

    Nyamalikiti ndi katswiri wa a katswiri.🙌

  • @godfreylungu
    @godfreylungu 5 หลายเดือนก่อน

    Abwana kwambili koma ndakatulo zanu tikuzifuna pano pa you tube

  • @kalvetegoman4256
    @kalvetegoman4256 4 ปีที่แล้ว +2

    big up
    kulumikiza mau mwaluso

  • @samuelkasonya4975
    @samuelkasonya4975 4 หลายเดือนก่อน

    Eeeh chichewa chomwechi? 🙌🏽

  • @malingaliro
    @malingaliro 4 ปีที่แล้ว +1

    N.Y.A.M.A.L.I.K.I.T.I. a class apart!

  • @JimmyMpinda
    @JimmyMpinda 24 วันที่ผ่านมา

    Respect

  • @bogasarasylvana1004
    @bogasarasylvana1004 5 ปีที่แล้ว

    2. Chabwino. Dziko lonse lapansi limapempherera chitsitsimutso. Ndipo malingana ndi kufunika kwa pempho lotero, Mulungu adzayankha. Tsopano chitsitsimutso chimabwera kokha kupyolera mu Mawu a chibwezeretso. Ayuda anali kuyembekezera chitsitsimutso koma molingana ndi kalawidwe kwawo.

  • @ezekielvitsitsi4155
    @ezekielvitsitsi4155 หลายเดือนก่อน

    Wow

  • @user-nc2hz1yp9g
    @user-nc2hz1yp9g ปีที่แล้ว

    My role model keep it up bid🎉🎉

  • @homersonkachere2009
    @homersonkachere2009 6 ปีที่แล้ว +4

    Thank you for uploading, can you please upload more of his poems please

  • @philippegnoumoutv3984
    @philippegnoumoutv3984 5 ปีที่แล้ว

    10. Ngati utumiki wa Aefeso 4:11 sukugwira ntchito, dongosolo la Mulungu lidzakwaniritsidwa. Koma Mulungu sangathe kuchita kapena kusinthitsa mneneri wam’thenga. Muloreni iye akane monga Yona, Mulungu adzamugwiritsa ntchito iye ... Ndipo m’neneri wam’thenga sadzakhala ndi mpingo wina waukulu koma bukhu mofanana monga Mose, Yesaya, Yeremiya ... Ndipo lero Lamlungu lino, Mamiliyoni a maulaliki apatsidwa padziko lonse lapansi m'zilankhulo zonse za padziko lapansi komanso pakati pa mamiliyoni ambiri a kulalikira padziko lonse lapansi, umodzi wokha idzasungidwa ndipo udzakwezedwa kosatha pamwamba pa anthu m'zilankhulo zonse za dziko lapansi. Ndipo ku kam’badwo kufikira ku kam’badwo, kulalikira uku sikudzaiwalika. Ndipo kulalikira uku ndiko kwa m’neneri wam’thenga wa kam'badwo. Ichi ndi chinthu chokha chimene Mulungu angachizindikire. M'masiku a Yeremiya panali mabuku ambiri, panali mau ambiri a Mulungu, panali aneneri ambiri, koma mawu a m’neneri m’modzi adakhala kwa ife zaka mazana ambiri, ndipo awa ndi mawu a Yeremiya . Ndipo kotero izo zinali kuchokera ku kam’badwo kufikira ku kam’badwo, kuchokera ku maziko a dziko. [Mawu a Mkonzi: Ameni! "].
    #PKPCHANNELTV

  • @andrewbanda9231
    @andrewbanda9231 2 ปีที่แล้ว

    I like the guy.....he is more creative..he recites well 💥💥

  • @mphaacbanda911
    @mphaacbanda911 5 ปีที่แล้ว

    Uwo ndiwo ulakatuli ndiwudziwa ine sawatcha uncle inu ndi 1 u always ipress me madala

    • @yaobleestelle2513
      @yaobleestelle2513 5 ปีที่แล้ว +2

      40. Abale a ku Africa, Asia, Europe ndi America! Inu mwina munali kuyembekezera Uthenga wa Mateyu 25:6 mwinamwake mu dziko lanu koma Mulungu anachita izo mosiyana. Kumbukirani Ambuye wathu Yesu Khristu! Pokhala mkulu wa ansembe Melkizedeki, achirabi ndi alembi anaona kuti Iye adzachokera ku fuko la Levi. Koma Iye adachokera ku fuko la Yuda. Ndiye, Uthenga Wake ndi ntchito Zake zinatsimikizira kuti Iye anali Mesiya. Ndipo lero pa nkhope yonse ya dziko lapansi, ngati iwe uli mwana wa Mulungu, malo ako awa ali pano ndi m’neneri wa nthawi yako, M’neneri Kacou Philipe. Ndipo amene ali ndi makutu akumva amve.

  • @witmanlumwira2743
    @witmanlumwira2743 ปีที่แล้ว

    Nyamalikiti legendary💣💥

  • @kouassiyvonne8538
    @kouassiyvonne8538 5 ปีที่แล้ว

    1. Ine ndikufuna kuyankhula za Mateyu 25:6. Tikudziwa kuchokera pa Mateyu 24:27 kuti Uthenga unachokera kwa Amwenye. Uthenga unabwera kuchokera Kum’mawa ndi Mtumwi Paulo. Mtundu wa dzuwa potuluka uli wachikasu, ndipo anthu a ku Amwenye, monga a Chitchaina, ali ndi mawonekedwe a khungu lachikasu. Kenako dzuwa, Uthenga Wabwino unabwera ku Ulaya kumene dzuŵa limasanduka loyera. Panali amuna aakulu a Mulungu ku Ulaya monga Martin Woyera wa kwaTours, Irenaeus, Columban, Martin Luther, John Wesley, ndi ena otero. Ndipo kumeneko tikudziwa kuti iwo amene amakhala ku Ulaya ali ndi khungu loyera. Kenaka dzuŵa linatsikira cha kumadzulo pa kukulowa kwadzuwa ndiko kunena kuti America. Ndipo madzulo, pa kulowa kwa dzuwa, dzuwa limakhala lofiira ndipo oyambirira okhala ku America iwo ali ndi khungu lofiira, Amwenye. Uko kunali William Branham ndi kuwala kwa madzulo. Ndipo William Branham anasonyeza kuti iye anali ndi magazi a Chimwenye kupyolera mwa agogo ake aakazi. Ndipo lero, pa nthawi ya kwa Afrika, Ewald Frank, munthu woyera akuyankhula za Mfuu la pakati pa usiku. Choncho, ife tikudziwa kuti kuchoka nthawi ya madzulo, iyo ilipakati pausiku, anthu a Chikuda, Africa, Iyeasanabwererenso Kum’mawa ndi mboni ziwiri za Chivumbulutso 11.
    2. Ngakhale pa msinkhu wachithupi-thupi, tikuwona achikuda pa olemekezeka onse a padziko lapansi. Ndipo ngakhale kwa nthawi yoyamba, tikuwona munthu wakuda ku likulu la UN. Ndipo zaka zaposachedwapa, tawona anthu akuda a ku America ali ndichidwi kwambiri ndi ku Africa, ngakhale kumafufuza za komwe anachokera. Pobwera kuzacheza ku Africa, Mulungu akudzakumbukira ana a Toussaint Louverture, Wilberforce, Martin Luther King ndi ena.
    3. Pamene Frederik de Klerc, mzungu ndi Nelson Mandela, yemwe ali munthu wakuda, adagwirana manja pamaso pa dziko lonse mu 1993 pamene awiriwa adapatsidwa mphoto ya Ntendere ya Nobel, komwe kunali kutha kwa tsankho, ndi kwa nthawi. Ichi chinali chizindikiro chaching'ono chimene chimabisa mbali yofunikira ya uzimu.
    4. Tsopano malinga ndi Mateyu 25:6, pakati pa usiku Mfuu lidzamveka, Ulaliki wa ufupi womwe udzakondoweza ndi kudzutsa anamwali a maulonda asanu ndi awiri. Ndipo kuwuka uku kudzatsogolera Mkwatibwi ku Mkwatulo. Yesu Khristu adzachezera Africa. Pambuyo pa dzuwa ndi kung’anima kwa Mateyu 24:27, mwezi ndi nyenyezi zidzawala. Yesaya 30 adzakwaniritsidwa. Ndipo aneneri ambiri amavomereza kuti kudzutsidwa kudzatulukira ku Ivory Coast. Kwa odzichepetsa m'mitima ndi malingaliro, kwa iwo amene akudikira mkwatulo wa oyera mtima, ichi sichilinso ulosi koma cheni-cheni.
    5. Tsopano pamene Mulungu ali kuchita, chochitika chirichonse chimathandizira ku zabwino. N'chifukwa chiyani vutoli ku Ivory Coast? N’chifukwa chiyani kusuntha uku kukulunjika ku Abidjan? Kodi chikoka ichi ndi chotani? Onani kuti mu Luka 2:1-7, Mfumu Kaisara Augusto adalamulakuti aliyense apite kumudzi kwawo kuti akawerengedwe. Chifukwa chiyani? Iye mwini sanadziwe, koma izo zinali choncho kuti Ambuye Yesu Khristu akhoze kubadwira ku Betelehemu ndi kuti maulosi asasokonezedwe. Tamva, tafika kudzawona ndipo tawona kudzera m'Malemba kuti mlaliki uyu ndi amene analonjezedwa mu Mateyu 25:6 ndi kuti tiyenera kumutsatira. [Mawu a Mkonzi: Msonkhano anati, "Ameni! "].
    6. ... Mfuu la pakati pa usiku lirindi maziko akulu a Baibulo, koma pamalo pomwe ife tafika, kwa osankhidwa, izo zangobwera ngati zowonjezera ku zimene iye akudziwa kale. Ndipo pamene ana a mdierekezi akukoka zingwe ndi maphunziro a malingaliro awo, osankhidwa akutenga ulamuliro wa zinthu.
    7. Ndipo ine ndikhoza kunena kuti, monga mitundu ina ya padziko lapansi, Mulungu wakumbukira zidzukulu za Simoni wa ku Sirene. Iwo omwe sanayambepo atenga dziko kapena kulamulira koma alandira chisomo cha Chipulumutso kwa Iye amene alibe kulemekeza munthu ndipo dziko lonse lapansi liyenera kuvomereza izo! [Mawu a Mkonzi: Gulu likuti, "Ameni!"]

  • @letoiledafriquetv3821
    @letoiledafriquetv3821 5 ปีที่แล้ว

    11. Pamene mtumiki wam’thenga akutumizidwa kudziko lapansi, ndichifukwa chakuti palibe choonadi padziko lapansi ndipo uthenga wake ndiwo wokhawo woona wa nthawi yake. Iye ndiye choyimira cha choonadi. Iye ndi woweruza wa Mawu a Mulungu mu nthawi yake. Inu mukuwona? Pamene Nowa ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Nowa. Pamene Yeremiya ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Yeremiya. Pamene Eliya ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Eliya. Pamene Ambuye Yesu Khristu ankalalikira kumeneko m'misewu ya Yerusalemu, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Ambuye Yesu. Iye anati, "Palibe amene amabwera kwa Atate koma kupyolera mwa Ine." Inu mukuwona? Pamene Martin Luther anali kulalikira mu Germany, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Martin Luther. Pamene John Wesley ankalalikira, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa pa nkhope yonse ya dziko kupatula mwa Uthenga wa John Wesley. Pamene William Branham ankalalikira mu Amerika, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa pa nkhope yonse ya dziko kupatula mwa Uthenga wa William Branham. Ndipo lero inu simungathe kupulumutsidwa koma kupyolera mu uthenga wa m’neneri Kacou Philippe. Ngati inu munali mwana wa Mulungu m'nthawi yawo, inu mukanakhulupirira mwa iwo ndipo ndi zofanana lero.[mkonzi: wosonkhana anena, “Ameni! "].

  • @sergeolivierbaba6243
    @sergeolivierbaba6243 5 ปีที่แล้ว

    #PROPHETKACOUPHILIPPE
    1. Monga aneneri a M’baibulo, mu Epulo 1993, ine, Kacou Philippe, mwamuna amene ndinali ndisanakhalepo ku mpingo, kupyolera m’masomphenya, ndinachezeredwa ndi M’ngelo amene anapereka kwa ine Uthenga wa kwa dziko lonse lapansi kukwaniritsa Mateyu 25:6 ndi Chivumbulutso 12:14. Iyi ndi nkhani ya kutembenuka kwanga, komanso masomphenya atatu a maitanidwe ndi utumiki wanga:

  • @crvl7288
    @crvl7288 4 ปีที่แล้ว

    Salute... This is great

  • @innocentjonathan8415
    @innocentjonathan8415 5 ปีที่แล้ว +1

    Mnyamatayu ali ndi luso

  • @user-on3yu7wt9o
    @user-on3yu7wt9o 11 หลายเดือนก่อน

    Nyamalikiti dolo km panopa ndy wasowa mu industry mu

  • @ThokozaniLosani-lr9ls
    @ThokozaniLosani-lr9ls ปีที่แล้ว

    Nyamalikiti ada kkkk

  • @YamikaniThirdson-jx7wn
    @YamikaniThirdson-jx7wn 9 หลายเดือนก่อน

    Dolo

  • @paulalfred7974
    @paulalfred7974 4 ปีที่แล้ว

    Ulemu wanu malume makwana

  • @joelmatchindu1738
    @joelmatchindu1738 6 ปีที่แล้ว +3

    Ndavula chisoti

  • @Ufulu
    @Ufulu 4 ปีที่แล้ว

    Where can I find the text for this poem. Would like to learn some chewa

    • @vidmore2180
      @vidmore2180 4 ปีที่แล้ว

      Check this guy on FB or Instagram

  • @cedricmakiyi1728
    @cedricmakiyi1728 ปีที่แล้ว

    ndakatulo zanu zikusowa boss

  • @rebeccamunguluma1516
    @rebeccamunguluma1516 4 ปีที่แล้ว

    Tipaseni zina please ,uyuyu amatha

  • @wiseyk1435
    @wiseyk1435 4 ปีที่แล้ว

    Ndakatulo or msonkhano?

  • @fexterkatungwe5998
    @fexterkatungwe5998 ปีที่แล้ว

    Luso losilirika

  • @samum3959
    @samum3959 6 ปีที่แล้ว +1

    Wanditsutsumutsa

    • @nouratana6463
      @nouratana6463 5 ปีที่แล้ว

      11. Pamene mtumiki wam’thenga akutumizidwa kudziko lapansi, ndichifukwa chakuti palibe choonadi padziko lapansi ndipo uthenga wake ndiwo wokhawo woona wa nthawi yake. Iye ndiye choyimira cha choonadi. Iye ndi woweruza wa Mawu a Mulungu mu nthawi yake. Inu mukuwona? Pamene Nowa ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Nowa. Pamene Yeremiya ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Yeremiya. Pamene Eliya ankalalikira, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Eliya. Pamene Ambuye Yesu Khristu ankalalikira kumeneko m'misewu ya Yerusalemu, palibe amene akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Ambuye Yesu. Iye anati, "Palibe amene amabwera kwa Atate koma kupyolera mwa Ine." Inu mukuwona? Pamene Martin Luther anali kulalikira mu Germany, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa kupatula mwa Uthenga wa Martin Luther. Pamene John Wesley ankalalikira, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa pa nkhope yonse ya dziko kupatula mwa Uthenga wa John Wesley. Pamene William Branham ankalalikira mu Amerika, palibe yemwe akanakhoza kupulumutsidwa pa nkhope yonse ya dziko kupatula mwa Uthenga wa William Branham. Ndipo lero inu simungathe kupulumutsidwa koma kupyolera mu uthenga wa m’neneri Kacou Philippe. Ngati inu munali mwana wa Mulungu m'nthawi yawo, inu mukanakhulupirira mwa iwo ndipo ndi zofanana lero.[mkonzi: wosonkhana anena, “Ameni! "].

  • @yaokacoudja9969
    @yaokacoudja9969 5 ปีที่แล้ว

    Kc.19:69 Q-A. N°28/ M'bale Philippe, kodi Satana angapereke vumbulutso kwa munthu wa Mulungu wodzazidwa ndi Mzimu Woyera?
    O m'bale, kulandiridwa kwa Mzimu Woyera sikumatiyika ife pamwamba pa Mulungu! Kodi munawerengapo Yobu 1? Dikirani! Tenga Mateyu 4, chinachitika ndi chiani? "Pomwepo mdierekezi anamunyamulira Iye mumzinda woyera, namuyika Iye pamwamba pa kachisi, ndipo anamuuza Iye ichi komanso icho." Inu mwawona? "Mdierekezi adamutengera Iye pa phiri lalitali, ndipo amamuwonetsa Iye maufumu onse a dziko komanso ulemerero wawo, ndipo akunena ichi komanso icho kwa Iye ...". Inu mwawona? Kodi chili chiyani? Zinali m'masomphenya omwe satana adamuwonetsa zinthu izi kwa Ambuye Yesu. Ndipo ngati inu simukumvetsa, dziwani kuti watchito siali wamkulu kuposa mbuye. Ngati satana wamunyamula Ambuye Yesu Khristu, ndipo kumufikitsa apa komanso apo, kumuwonetsa masomphenya, ndiye ine ndine yani mneneri Kacou Philippe wopulumutsidwa mwachisomo?

  • @carlobamusi9763
    @carlobamusi9763 5 ปีที่แล้ว

    Mmmmh salute rm

  • @edsonmasamba9631
    @edsonmasamba9631 5 ปีที่แล้ว

    Ulemu wanu abwana

    • @yaobleestelle2513
      @yaobleestelle2513 5 ปีที่แล้ว +1

      40. Abale a ku Africa, Asia, Europe ndi America! Inu mwina munali kuyembekezera Uthenga wa Mateyu 25:6 mwinamwake mu dziko lanu koma Mulungu anachita izo mosiyana. Kumbukirani Ambuye wathu Yesu Khristu! Pokhala mkulu wa ansembe Melkizedeki, achirabi ndi alembi anaona kuti Iye adzachokera ku fuko la Levi. Koma Iye adachokera ku fuko la Yuda. Ndiye, Uthenga Wake ndi ntchito Zake zinatsimikizira kuti Iye anali Mesiya. Ndipo lero pa nkhope yonse ya dziko lapansi, ngati iwe uli mwana wa Mulungu, malo ako awa ali pano ndi m’neneri wa nthawi yako, M’neneri Kacou Philipe. Ndipo amene ali ndi makutu akumva amve.

  • @alexandermasozgho4414
    @alexandermasozgho4414 7 ปีที่แล้ว

    Awa ndi amfumu ndithu

  • @beinhardkausiwa7107
    @beinhardkausiwa7107 6 ปีที่แล้ว

    I we ndi biggy