No mukulakwisa mukatelo kod mayiko enawa anthu samafa nakha anthu ena osayimba ndipo sanatchuke komwe anthu akumuzi samafa ndi infa za m'zizizi munganene kuti ndi bwana Lucia's Banda. No come on guys let's us learn to respect our favorite artist from our country because if we could no palibe Munthu yemwe angawalemekeze
My opinion Lucius sanakhalepo freedom fighter, unali chabe mukwiyo after bingu kuchoka ku UDF plus ma personal issues awo. Uyu kumapetoku atapasidwa udindo anangoti ziii kumanyambita misonkho ya amalawi
Sorry wapita mwachangu coz timadikila kt ayibe nyimbo mubo lilipoli koma ay zidko limatha bas kulimbanila nkazi kaya zichani tilibe nazo ntchito koma ife tingoti abuye wayakha bas RIP BINGU MUTHALIKA
Lucius banda dyera amafuna bazi koma anaona kuti bingu anali dolo sanamupatse 😂😂palibenso president angazafanane ndi bingu 😢😢alucius nanga lero muli kuti dziko lili pa moto ili
Remember to subscribe ❤
😊
😊
😊
😊
Q😊😊q@@werlemsitima
Freedom fighter anali Evison Matafare oyamba komanso osiriza anthu opanga za person siabwino nthawi zonse
Inu ndi anthu aja okonda munthu ukufaaaa
Bingu nd great man. Amaona patali. Malawi pano akuvutika coz Bingu sanamalize tym yake
Lucius banda sanali munthu wa freedom fighter Malawi koma freedom fighter wozipezela chuma yekha
Not 1997 but after the UDF convention in 1994 at NRC Bingu made his UP.
Lucia's Banda anayesesa mokwanila kutimenyela khondo ndipo oyimba ambiliwa akutchuka chifukwa cha iye he is bg boss
I hate Lucius Banda ndipo ndiwadyera kwambiri amkagofuna kumamudyera bingu nde ataona kut bingu simuthu oti akhoza kumupusisa ayi
Si wabwino Lucius Banda
Munthu oipa uyu ndiokonda ndalama nthaw amadana bdi bingu chifukwa samaonapo cholowa...ngati ali munthu osaopa why now ogokhala or nyimbo kuimba ..sakuona anthu kuti akuzuzika
Za dziko lapansi ndizovuta...lero ndi mbiri..rest well legends.
ali biz kuba ndalama dza boma ndi mcp iweso masu mutu wako sugwila ncthito iwe ungamayamikile galuyu
Ndie ngat siwantha bwanji relo asalakhula namapwalayu alikut
Aaaaaaa!
Koma ngat uziopa kutchula zomwe ukuziwa bola usamapange
He mentioned Bingu wa Munthalika in his song called Ndisiyileni kanga
Lucias Banda ndi wadyera komanso munthu waziphuphu kwambiri amayendera MSCE yabodza cholinga chofuna kulemera, pano siuyu aChakwala ampasa mpando wakhala pheee
Mumaitha bwana ndipo mwafotokoza moveka bwino.
Lucius Banda munthu woipa kwambri but he's a pretender ngat ndwa bhobho
Zowona zake waononga anthu ambiri galu ameneyi🤔😢
Ndy Pano akuti chani agalu okonda ku dyesa mimba zawo😢
Mot uzingofotokoza apa ndye ukuopa zchan?
Bingu amadya mkaz wa soja
So far so good
Pano anampasa bazi ameneyo
amadana ndi chilungamo wautsilu ananga pano akuti chani ku mcp chifukwa ampasa mpando kumalawi balibe amene angaipitse bungu
N hate Lucius munthu woipa kwambiri
Zanziko lapansi izi
Pano zikumuvuta pati kuzuzura Boma la mcp
Ky zaw izo aona kt atan😂😂
Pano zinthu nde zikuyenda bwino? Ali kuti nanga bwanawa 😂😂😂
Achitsiru aja
Malawi
Kudali Billy kaunda yemwe adalimbana ndi bakili kapena mudali muli ana
Munthu wadyera uyu galu
Ndisiyireni ena amati amanena Mulli kaya kkkk
Ineso namva chomcho
Muli ankayenda ndi ndani
Mlaka ndi bernadetter?
Mmmmmm lusius wakupha uyu anapha oyimba azake ambiri ATI asachuke kuposela iye
No mukulakwisa mukatelo kod mayiko enawa anthu samafa nakha anthu ena osayimba ndipo sanatchuke komwe anthu akumuzi samafa ndi infa za m'zizizi munganene kuti ndi bwana Lucia's Banda. No come on guys let's us learn to respect our favorite artist from our country because if we could no palibe Munthu yemwe angawalemekeze
Mmmmmm
Uyu ndigalu wadyela
My opinion Lucius sanakhalepo freedom fighter, unali chabe mukwiyo after bingu kuchoka ku UDF plus ma personal issues awo.
Uyu kumapetoku atapasidwa udindo anangoti ziii kumanyambita misonkho ya amalawi
Lucius tikukulira ife amalawi
Boss apa ndie meatinamiza zoti Lucius dagulidwazo mmm
Banda anali kape dissed nsanje port calling it dziwe la mng'ona....bingu was genius
Mukutiwuza zinthu zoti tikudzidziwa kuposa inunso
Don’t talk lies now
Iwe ukukana kung'alula chifukwa choti ulibe lawyer nde ife tipange suggest lawyer timutenga kutu?
Sorry wapita mwachangu coz timadikila kt ayibe nyimbo mubo lilipoli koma ay zidko limatha bas kulimbanila nkazi kaya zichani tilibe nazo ntchito koma ife tingoti abuye wayakha bas RIP BINGU MUTHALIKA
Lucius anali wadyera amadana ndi bingu chifukwa sanamupasa mpando,
Sukutchula maina ndie chomatizuzir kumvera nchiyani?
Likw
Pano bwanji wangoumba mlomo akuziwa kuti chakwera amudula machende
Sam mavitha umakhwana
Lucius anali osokonedza komanso wadyera, amalimbana ndi boma lomwe sakupindula kanthu
6
I like you Sam a historian
Nde Pano sakuyankhula ndizopusa zomwe akupanga achakwelazi??🙄
Tadziwa nao
Uyu anali munthu oipa kwambili ndipo kufa kwa bingu amadziwako kanthu
Umangoyamba nkhani ukudziwa kuti suyimaliza nanga chomabisira mayina ndichani?
Lucius banda dyera amafuna bazi koma anaona kuti bingu anali dolo sanamupatse 😂😂palibenso president angazafanane ndi bingu 😢😢alucius nanga lero muli kuti dziko lili pa moto ili
The woman probably was Calista as all these were parliamentarians. Not so ?
Ase iwe ukumutama galu uyu alikuti luciac freedom fighter wakunyumba kwako tu
Komanso ngat kumalawi kuli andale osadziwa chomwe akupanga one of them ndi Lucius
Amanena bingu emweyo
😂sam iwe umandiwaza 😊
Ndisiyileni kanga nyimbo ija imanena Bingu😊
Amanena bingu kuti watani?
bingu anapotsa kamuzu muzochitika pa 7eyes yake ndiye mungama fanidze ndi galu yo lus
Ndipo ameneyu anamunyoza bingu kwabasi pano akukanika kuyankhula mmene anthu akuvutikila
Nawesotu nyimbo zachamwiniyoo usamangochaputaa ndiza Tygrin zoo
Soja wa mphawi , speaking on behalf of the poor masses
Ine zambiri ai guys ngati mukuidziwa kanyimbo kameveka kumapeto koo ndiuzeni kuti anayimba ndindani chonde
Search nyimbo ya Sam Malvitha youtube chanel...
muipedza ...pa youtube pomwepa boss
Anaomba ndi Yb Africa ndi Kikey Malawi
Anapangitsa kuti mnyenyembe afe si uyu mkumutama apayi?
Mavicha kape waboza iwe wasowa zokamba
Tilibe any suggetion tell us please
Bola Bikili muluzi t.v.
Uztchula Maina iwe ase aah ukuopa chan
Alucias inu ndinu achitsilu inu mulibe nzeru
Dorangoni wilison
Fantastic . Big up!!
Mumatiuza zomwe sitimaziwa bwana mupitilize
I'm sorry forget you
Which freedom has he fought ?
Anali SOJA wa amphawi
That's why Lucious Banda panopa sakuyimba nyimbo zolongosoka,, mmbuyomu album yonse imakhala nyimbo zonena Bingu yekhayekha
Abodza inu munene kuti inuyo mzanu ndi bingu osati bandayo
Tay green aise
Ndepano lucius banda wanuyo sanagudwe ndi ndalama?
Umakwana brother
If he is strong why now
Tsoja wampaw
Soja ndi soja basi
Sam mavita kapenso
Sir Paul banda is alive
Rest well soldier
Imfa ya Munyenyembe imandiwawa
Nice
Rest in peace
Mumakwana inuyo
Thanks Good 👍
I like some navter go ahead
I like
Rip
Muli
Good
Kachunyau kunena nyau king?
Kkkkkkkk
Amati yimilira wulemu wawo
G up
Paul banda alipo