Mkangano wa Lucius Banda ndi Bingu

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 30 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 150

  • @sammalvitha
    @sammalvitha  7 หลายเดือนก่อน +18

    Remember to subscribe ❤

    • @werlemsitima
      @werlemsitima 7 หลายเดือนก่อน +2

      😊

    • @werlemsitima
      @werlemsitima 7 หลายเดือนก่อน +1

      😊

    • @werlemsitima
      @werlemsitima 7 หลายเดือนก่อน

      😊

    • @werlemsitima
      @werlemsitima 7 หลายเดือนก่อน

      😊

    • @twenage
      @twenage 3 หลายเดือนก่อน

      Q😊😊q​@@werlemsitima

  • @DeboraNembele-ri3bh
    @DeboraNembele-ri3bh 7 หลายเดือนก่อน +15

    Freedom fighter anali Evison Matafare oyamba komanso osiriza anthu opanga za person siabwino nthawi zonse

    • @Jermah51kennias
      @Jermah51kennias 4 หลายเดือนก่อน +1

      Inu ndi anthu aja okonda munthu ukufaaaa

  • @giddymarley112
    @giddymarley112 7 หลายเดือนก่อน +6

    Bingu nd great man. Amaona patali. Malawi pano akuvutika coz Bingu sanamalize tym yake

  • @JamesjamesJames-w3l
    @JamesjamesJames-w3l 2 หลายเดือนก่อน +4

    Lucius banda sanali munthu wa freedom fighter Malawi koma freedom fighter wozipezela chuma yekha

  • @HandyChipets
    @HandyChipets 2 หลายเดือนก่อน +2

    Not 1997 but after the UDF convention in 1994 at NRC Bingu made his UP.

  • @chiefjusticie
    @chiefjusticie 7 หลายเดือนก่อน +5

    Lucia's Banda anayesesa mokwanila kutimenyela khondo ndipo oyimba ambiliwa akutchuka chifukwa cha iye he is bg boss

  • @davidwakhokamoto1124
    @davidwakhokamoto1124 7 หลายเดือนก่อน +6

    I hate Lucius Banda ndipo ndiwadyera kwambiri amkagofuna kumamudyera bingu nde ataona kut bingu simuthu oti akhoza kumupusisa ayi

  • @nysonzeperiana9869
    @nysonzeperiana9869 7 หลายเดือนก่อน +2

    Munthu oipa uyu ndiokonda ndalama nthaw amadana bdi bingu chifukwa samaonapo cholowa...ngati ali munthu osaopa why now ogokhala or nyimbo kuimba ..sakuona anthu kuti akuzuzika

  • @simphiwenyirenda2392
    @simphiwenyirenda2392 หลายเดือนก่อน

    Za dziko lapansi ndizovuta...lero ndi mbiri..rest well legends.

  • @patricgama4788
    @patricgama4788 7 หลายเดือนก่อน +2

    ali biz kuba ndalama dza boma ndi mcp iweso masu mutu wako sugwila ncthito iwe ungamayamikile galuyu

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 7 หลายเดือนก่อน +9

    Ndie ngat siwantha bwanji relo asalakhula namapwalayu alikut

  • @Ghama-k4i
    @Ghama-k4i 2 หลายเดือนก่อน +1

    Koma ngat uziopa kutchula zomwe ukuziwa bola usamapange

  • @DAVIESMDIMBA-ob9vq
    @DAVIESMDIMBA-ob9vq 29 วันที่ผ่านมา

    He mentioned Bingu wa Munthalika in his song called Ndisiyileni kanga

  • @BushiriliveTV
    @BushiriliveTV 7 หลายเดือนก่อน +4

    Lucias Banda ndi wadyera komanso munthu waziphuphu kwambiri amayendera MSCE yabodza cholinga chofuna kulemera, pano siuyu aChakwala ampasa mpando wakhala pheee

  • @forbesslemusani3601
    @forbesslemusani3601 หลายเดือนก่อน

    Mumaitha bwana ndipo mwafotokoza moveka bwino.

  • @franciskameko2586
    @franciskameko2586 7 หลายเดือนก่อน +4

    Lucius Banda munthu woipa kwambri but he's a pretender ngat ndwa bhobho

    • @FredodHawadi
      @FredodHawadi 7 หลายเดือนก่อน +1

      Zowona zake waononga anthu ambiri galu ameneyi🤔😢

  • @FredodHawadi
    @FredodHawadi 7 หลายเดือนก่อน +6

    Ndy Pano akuti chani agalu okonda ku dyesa mimba zawo😢

  • @NzeruDesign-ut1go
    @NzeruDesign-ut1go 7 หลายเดือนก่อน +2

    Mot uzingofotokoza apa ndye ukuopa zchan?

  • @ChrispinKaundama
    @ChrispinKaundama หลายเดือนก่อน

    Bingu amadya mkaz wa soja

  • @mathewstembo1778
    @mathewstembo1778 2 หลายเดือนก่อน +1

    So far so good

  • @jamessaiti
    @jamessaiti 7 หลายเดือนก่อน +6

    Pano anampasa bazi ameneyo

  • @patricgama4788
    @patricgama4788 7 หลายเดือนก่อน +1

    amadana ndi chilungamo wautsilu ananga pano akuti chani ku mcp chifukwa ampasa mpando kumalawi balibe amene angaipitse bungu

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 7 หลายเดือนก่อน +1

    N hate Lucius munthu woipa kwambiri

  • @SamSinoya
    @SamSinoya 27 วันที่ผ่านมา

    Zanziko lapansi izi

  • @MartinLuther-o2z
    @MartinLuther-o2z 7 หลายเดือนก่อน +2

    Pano zikumuvuta pati kuzuzura Boma la mcp

  • @AmadumtungasudiSudimtungaamadu
    @AmadumtungasudiSudimtungaamadu หลายเดือนก่อน

    Ky zaw izo aona kt atan😂😂

  • @mosesharoldngolombe
    @mosesharoldngolombe 7 หลายเดือนก่อน +4

    Pano zinthu nde zikuyenda bwino? Ali kuti nanga bwanawa 😂😂😂

  • @MackKalilombe
    @MackKalilombe 8 วันที่ผ่านมา

    Malawi

  • @ClementKampaka
    @ClementKampaka 7 หลายเดือนก่อน +1

    Kudali Billy kaunda yemwe adalimbana ndi bakili kapena mudali muli ana

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 7 หลายเดือนก่อน +1

    Munthu wadyera uyu galu

  • @madalitsochabwera5903
    @madalitsochabwera5903 7 หลายเดือนก่อน +2

    Ndisiyireni ena amati amanena Mulli kaya kkkk

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 7 หลายเดือนก่อน +1

    Mmmmmm lusius wakupha uyu anapha oyimba azake ambiri ATI asachuke kuposela iye

    • @chiefjusticie
      @chiefjusticie 7 หลายเดือนก่อน

      No mukulakwisa mukatelo kod mayiko enawa anthu samafa nakha anthu ena osayimba ndipo sanatchuke komwe anthu akumuzi samafa ndi infa za m'zizizi munganene kuti ndi bwana Lucia's Banda. No come on guys let's us learn to respect our favorite artist from our country because if we could no palibe Munthu yemwe angawalemekeze

    • @zionekanjoka7575
      @zionekanjoka7575 7 หลายเดือนก่อน

      Mmmmmm

  • @Ndendendlovu
    @Ndendendlovu 7 หลายเดือนก่อน +2

    Uyu ndigalu wadyela

  • @kingwaltermdezo
    @kingwaltermdezo 2 หลายเดือนก่อน

    My opinion Lucius sanakhalepo freedom fighter, unali chabe mukwiyo after bingu kuchoka ku UDF plus ma personal issues awo.
    Uyu kumapetoku atapasidwa udindo anangoti ziii kumanyambita misonkho ya amalawi

  • @CharityChinoko
    @CharityChinoko 2 หลายเดือนก่อน +1

    Lucius tikukulira ife amalawi

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj 7 หลายเดือนก่อน +1

    Boss apa ndie meatinamiza zoti Lucius dagulidwazo mmm

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 หลายเดือนก่อน

    Banda anali kape dissed nsanje port calling it dziwe la mng'ona....bingu was genius

  • @NicholasKwajama
    @NicholasKwajama 7 หลายเดือนก่อน +3

    Mukutiwuza zinthu zoti tikudzidziwa kuposa inunso

  • @ZahirZaheer-h3d
    @ZahirZaheer-h3d 7 หลายเดือนก่อน +1

    Don’t talk lies now

  • @edinabornface
    @edinabornface 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe ukukana kung'alula chifukwa choti ulibe lawyer nde ife tipange suggest lawyer timutenga kutu?

  • @ArexBright
    @ArexBright 3 หลายเดือนก่อน

    Sorry wapita mwachangu coz timadikila kt ayibe nyimbo mubo lilipoli koma ay zidko limatha bas kulimbanila nkazi kaya zichani tilibe nazo ntchito koma ife tingoti abuye wayakha bas RIP BINGU MUTHALIKA

  • @MrChimtengo
    @MrChimtengo 2 หลายเดือนก่อน

    Lucius anali wadyera amadana ndi bingu chifukwa sanamupasa mpando,

  • @KikaImran
    @KikaImran 2 หลายเดือนก่อน

    Sukutchula maina ndie chomatizuzir kumvera nchiyani?

  • @MarthaKhumbanyiwa
    @MarthaKhumbanyiwa หลายเดือนก่อน

    Likw

  • @AlexKaunda-x3p
    @AlexKaunda-x3p 7 หลายเดือนก่อน +2

    Pano bwanji wangoumba mlomo akuziwa kuti chakwera amudula machende

  • @giftjimu6685
    @giftjimu6685 2 หลายเดือนก่อน

    Lucius anali osokonedza komanso wadyera, amalimbana ndi boma lomwe sakupindula kanthu

  • @PqapTheOnly-r2p
    @PqapTheOnly-r2p 2 หลายเดือนก่อน

    6

  • @chisalebeston
    @chisalebeston 7 หลายเดือนก่อน +1

    I like you Sam a historian

  • @raymondchautsi6282
    @raymondchautsi6282 7 หลายเดือนก่อน

    Nde Pano sakuyankhula ndizopusa zomwe akupanga achakwelazi??🙄

  • @mariamhassan4089
    @mariamhassan4089 7 หลายเดือนก่อน +1

    Tadziwa nao

  • @SérgioFernandoKangombe
    @SérgioFernandoKangombe 2 หลายเดือนก่อน

    Uyu anali munthu oipa kwambili ndipo kufa kwa bingu amadziwako kanthu

  • @isaacdemba2401
    @isaacdemba2401 7 หลายเดือนก่อน

    Umangoyamba nkhani ukudziwa kuti suyimaliza nanga chomabisira mayina ndichani?

  • @JanetJamesMachila
    @JanetJamesMachila 7 หลายเดือนก่อน

    Lucius banda dyera amafuna bazi koma anaona kuti bingu anali dolo sanamupatse 😂😂palibenso president angazafanane ndi bingu 😢😢alucius nanga lero muli kuti dziko lili pa moto ili

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe 3 หลายเดือนก่อน

    The woman probably was Calista as all these were parliamentarians. Not so ?

  • @robertmakupe2863
    @robertmakupe2863 7 หลายเดือนก่อน

    Ase iwe ukumutama galu uyu alikuti luciac freedom fighter wakunyumba kwako tu

  • @AndrewChasweka
    @AndrewChasweka 7 หลายเดือนก่อน

    Komanso ngat kumalawi kuli andale osadziwa chomwe akupanga one of them ndi Lucius

  • @MacloudKasawala
    @MacloudKasawala 7 หลายเดือนก่อน +1

    Amanena bingu emweyo

  • @JasperKaleni-dx6nn
    @JasperKaleni-dx6nn 7 หลายเดือนก่อน +3

    😂sam iwe umandiwaza 😊

  • @BornMandala-rz1dk
    @BornMandala-rz1dk 7 หลายเดือนก่อน +1

    Ndisiyileni kanga nyimbo ija imanena Bingu😊

    • @ChifundoSikelo
      @ChifundoSikelo 7 หลายเดือนก่อน

      Amanena bingu kuti watani?

  • @patricgama4788
    @patricgama4788 7 หลายเดือนก่อน

    bingu anapotsa kamuzu muzochitika pa 7eyes yake ndiye mungama fanidze ndi galu yo lus

  • @JessicaChabwera
    @JessicaChabwera 6 หลายเดือนก่อน

    Ndipo ameneyu anamunyoza bingu kwabasi pano akukanika kuyankhula mmene anthu akuvutikila

  • @websterkausiwa8919
    @websterkausiwa8919 7 หลายเดือนก่อน

    Nawesotu nyimbo zachamwiniyoo usamangochaputaa ndiza Tygrin zoo

  • @HenryChunga
    @HenryChunga 6 หลายเดือนก่อน

    Soja wa mphawi , speaking on behalf of the poor masses

  • @ErnestKanthiti
    @ErnestKanthiti 7 หลายเดือนก่อน

    Ine zambiri ai guys ngati mukuidziwa kanyimbo kameveka kumapeto koo ndiuzeni kuti anayimba ndindani chonde

    • @sammalvitha
      @sammalvitha  7 หลายเดือนก่อน

      Search nyimbo ya Sam Malvitha youtube chanel...
      muipedza ...pa youtube pomwepa boss
      Anaomba ndi Yb Africa ndi Kikey Malawi

  • @WisdomKmsiska
    @WisdomKmsiska 3 หลายเดือนก่อน

    Anapangitsa kuti mnyenyembe afe si uyu mkumutama apayi?

  • @MphatsoSoko-p3l
    @MphatsoSoko-p3l 2 หลายเดือนก่อน

    Mavicha kape waboza iwe wasowa zokamba

  • @MoosahMtambo
    @MoosahMtambo 2 หลายเดือนก่อน

    Tilibe any suggetion tell us please

  • @LouisJamali-z7v
    @LouisJamali-z7v 2 หลายเดือนก่อน

    Bola Bikili muluzi t.v.

  • @chauncychauncy1683
    @chauncychauncy1683 7 หลายเดือนก่อน

    Uztchula Maina iwe ase aah ukuopa chan

  • @PaulkapesiPhirijunir-kh7vc
    @PaulkapesiPhirijunir-kh7vc 7 หลายเดือนก่อน

    Alucias inu ndinu achitsilu inu mulibe nzeru

  • @KalipentalaFred
    @KalipentalaFred 2 หลายเดือนก่อน

    Dorangoni wilison

  • @PatrickIman-n2u
    @PatrickIman-n2u หลายเดือนก่อน

    Fantastic . Big up!!

  • @HestingsChapola
    @HestingsChapola 6 หลายเดือนก่อน

    Mumatiuza zomwe sitimaziwa bwana mupitilize

  • @MORESSRAJABOCINGANO-rz1lt
    @MORESSRAJABOCINGANO-rz1lt 3 หลายเดือนก่อน

    I'm sorry forget you

  • @mayesohenry
    @mayesohenry 3 หลายเดือนก่อน

    Which freedom has he fought ?

  • @livisonchinsamba5655
    @livisonchinsamba5655 2 หลายเดือนก่อน

    Anali SOJA wa amphawi

  • @lingstonenagoli7729
    @lingstonenagoli7729 7 หลายเดือนก่อน

    That's why Lucious Banda panopa sakuyimba nyimbo zolongosoka,, mmbuyomu album yonse imakhala nyimbo zonena Bingu yekhayekha

    • @loidchikoti9338
      @loidchikoti9338 6 หลายเดือนก่อน

      Abodza inu munene kuti inuyo mzanu ndi bingu osati bandayo

  • @AshrafuKalimula
    @AshrafuKalimula 6 หลายเดือนก่อน

    Tay green aise

  • @Mickeykasambula265
    @Mickeykasambula265 7 หลายเดือนก่อน

    Ndepano lucius banda wanuyo sanagudwe ndi ndalama?

  • @WilliesMasanjala
    @WilliesMasanjala หลายเดือนก่อน

    Umakwana brother

  • @yamikanifischer
    @yamikanifischer 7 หลายเดือนก่อน

    If he is strong why now

  • @ChiwalePhade
    @ChiwalePhade 3 หลายเดือนก่อน

    Tsoja wampaw

  • @DamianoEdward
    @DamianoEdward 7 หลายเดือนก่อน

    Soja ndi soja basi

  • @beardmakwale-r8n
    @beardmakwale-r8n 3 หลายเดือนก่อน

    Sam mavita kapenso

  • @FrancisMusonda-h7p
    @FrancisMusonda-h7p 3 หลายเดือนก่อน

    Sir Paul banda is alive

  • @MemoryTambula
    @MemoryTambula 2 หลายเดือนก่อน

    Rest well soldier

  • @alexnyirenda123
    @alexnyirenda123 3 หลายเดือนก่อน

    Imfa ya Munyenyembe imandiwawa

  • @HarrisskudzaiLimula
    @HarrisskudzaiLimula หลายเดือนก่อน

    Nice

  • @Daneck-rm1gg
    @Daneck-rm1gg 3 หลายเดือนก่อน

    Rest in peace

  • @JonathanHenry-e9e
    @JonathanHenry-e9e 2 หลายเดือนก่อน

    Mumakwana inuyo

  • @MussaHassani-zg1hm
    @MussaHassani-zg1hm 2 หลายเดือนก่อน

    Thanks Good 👍

  • @DoricaMzeweza
    @DoricaMzeweza 7 หลายเดือนก่อน

    I like some navter go ahead

  • @brendaMkandawire-n2m
    @brendaMkandawire-n2m 2 หลายเดือนก่อน

    I like

  • @al-sudigang3299
    @al-sudigang3299 3 หลายเดือนก่อน

    Rip

  • @HenlyTiyesi
    @HenlyTiyesi 4 หลายเดือนก่อน

    Muli

  • @FRIDAYBANDA-m8i
    @FRIDAYBANDA-m8i 2 หลายเดือนก่อน

    Good

  • @Mphamdala
    @Mphamdala 7 หลายเดือนก่อน

    Kachunyau kunena nyau king?

    • @sammalvitha
      @sammalvitha  7 หลายเดือนก่อน

      Kkkkkkkk

  • @EdinahPhiri-z5o
    @EdinahPhiri-z5o 7 หลายเดือนก่อน

    Amati yimilira wulemu wawo

  • @MusaKim-l3s
    @MusaKim-l3s 2 หลายเดือนก่อน

    G up

  • @FrancisMusonda-h7p
    @FrancisMusonda-h7p 3 หลายเดือนก่อน

    Paul banda alipo