LIMPOPO FM 05 JULY 2024 NDI COMRADE NTANYIWA, ANTHU OSAZIWIKA BWINO ANAPEZELEDWA MALO OGONA ALENDO

แชร์
ฝัง

ความคิดเห็น • 190

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 10 วันที่ผ่านมา +20

    Koma ntanyiwa. Respect to you May the almighty God protect you wherever you will go

    • @petroszgambo9949
      @petroszgambo9949 10 วันที่ผ่านมา

      Keep up the good work comrade 💪💪

    • @BeliLikhola
      @BeliLikhola 10 วันที่ผ่านมา

      Ulemu wanu comrade Ntanyiwa.

  • @LoydKamtedza
    @LoydKamtedza 10 วันที่ผ่านมา +5

    Munandisangalasa yomweo chikangawa❤️❤️❤️🇿🇦🇿🇦🇿🇦🇿🇦 osavera Riiimpopo ndi ndimakhala ngati ndataya kofunikila

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8d 10 วันที่ผ่านมา +3

    Salute comrade ntanyiwa,we love you and all Limpopo FM

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo 10 วันที่ผ่านมา +3

    Limpopo FM live from south Africa Durban Pietermaritzburg auzeni zoona amenewa

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 10 วันที่ผ่านมา +4

    Panopa ine ndinasiya kuvela ma redio ena panopa ndili limpopo yokha basi

  • @mustafailanga2585
    @mustafailanga2585 10 วันที่ผ่านมา +2

    Ulemu wanu big mani mmatimvesa kukoma kwambili god bless you all the time ❤❤❤❤❤❤

  • @bytonalfred5844
    @bytonalfred5844 10 วันที่ผ่านมา +2

    Ntanyiwa and your fellow comrades excellent well done, and keep it up for the battle you are fighting for Mw nation

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 10 วันที่ผ่านมา +2

    Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu asinkuphasa moyyo wabwinno ndawi sonse I pray for you all the time amalawi tili phamoto 🤲🤲🤲🙏🙏🙏mulungu dalisani Malawi

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 10 วันที่ผ่านมา +2

    Respect bwana Ntanyiwa 🔥🔥🔥

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 วันที่ผ่านมา +2

    Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 วันที่ผ่านมา +4

    Ine mchifukwa chake ndinakana ntchito ya usilikali ndiyapolisi coz fans ya madepartiment amenewa ndiyombwambwana kwambiri, zigawenga zaku Israel and Ruanda zikungolowa mdziko mwathu ngat zikulowa mmanyumba mwawo, chomvesa chisoni kwambiri ndichoti asilikali ndi apolisi angoti vyooooo , vyooooo , osapangapo kanthu

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala 10 วันที่ผ่านมา +2

    Chifukwa iyeyu..akupanga zinthu zomwe south African ikhoza kukwiya nanzo.zomwe zingaikidze miyoyo yanthu ife amalawi pa chiswe😢

  • @jamiajafali6619
    @jamiajafali6619 10 วันที่ผ่านมา +2

    Antuwo zisilu kwabasi ...Antanyiwa gwilani nchito blo❤

  • @Jimmy-m4z
    @Jimmy-m4z 9 วันที่ผ่านมา +1

    My brother your number one keep it up

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 10 วันที่ผ่านมา +2

    May good God knows everything and palibe chingabisike Mulungu ateteze malawians

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 10 วันที่ผ่านมา +2

    Mtanyiwwa osawopha mulungu adalise inuyyo mulungu adalise inuyyo nosse

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j 10 วันที่ผ่านมา +1

    Tikuziwa zambiri GUYS mmmm Limpopo FM ndikatundu number 1

  • @LoydKamtedza
    @LoydKamtedza 10 วันที่ผ่านมา +1

    Comrade ntanyiwa mulungu azikupasa moyo wautali azikusogolera ndipo mupitiliza kuti pasila choona chamalawi Allah azikuteteza kulikose ukuyenda Limpopo FM ndimanyoya nayo ndikamavera

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 10 วันที่ผ่านมา +2

    Limpopo inabwera kuzakhala

  • @ibrahimalex7137
    @ibrahimalex7137 10 วันที่ผ่านมา +1

    Ulemu wanu from Limpopo south Africa 🇿🇦

  • @HanaNyasulu
    @HanaNyasulu 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mumatiimirira acomrade timakunyadilani❤

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 10 วันที่ผ่านมา +1

    Tafika ndithu kuzamvera our very own limpopo Fm

  • @user-uj9st8zp7v
    @user-uj9st8zp7v 10 วันที่ผ่านมา +2

    Ndili pambuyo pako mtanyiwa

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 10 วันที่ผ่านมา +2

    boma la zitsiru apolice army chakwera mitumbo ya chamanu

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 10 วันที่ผ่านมา +2

    Mulungu wayitenga nkhondo imeneyi kukhala yake ndipo palibe yemwe angamenyane ndi MULUNGU.
    OKHA OKHA A MCP AMENYANA NDIPONSO AWULULANA POSACHEDWAPA. IFE TINGOTI PHEEEEEE KUDIKIRA

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 10 วันที่ผ่านมา +2

    Musalimbane ndi manyi woo aaaa muti asilikali alikuti??
    Agalu osaziwa ntchitowo? ntchito zigololo bas.
    ife tiibe ma ninja mmalawi muno aaaa

  • @MaxwellManual
    @MaxwellManual 10 วันที่ผ่านมา +4

    Chakwela sawina wapangila ena kapeni

  • @nyanguoipa6996
    @nyanguoipa6996 10 วันที่ผ่านมา +1

    LIMPOPO FM PALIBESO IFE TINGOTI NYADU

  • @lottiempata2487
    @lottiempata2487 10 วันที่ผ่านมา +1

    God's good always Amen

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo6251 10 วันที่ผ่านมา +2

    Mcp ikupanga zinthu zoopsyeza kwambiri ndipo zamdikwana mmmh

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk 10 วันที่ผ่านมา +1

    I salute you comrade, you are genius

  • @user-iv4dj1pi3b
    @user-iv4dj1pi3b 10 วันที่ผ่านมา +2

    Pangolin ..ntanyiwa ....

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 10 วันที่ผ่านมา +1

    Tinakusowan Mr Mtanyiwa muli bwanji kumeneko kuno tili bwino ndithu

  • @RachealHarawa-xc9gs
    @RachealHarawa-xc9gs 10 วันที่ผ่านมา +2

    Wailesi yokhayo yomwe ambiri akuikonda kunvera panopa

  • @user-wb9ji3oe5o
    @user-wb9ji3oe5o 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mutitumizire zithunzi za anthu omwe agwidwa ku South Africa.

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 10 วันที่ผ่านมา +1

    It's only champion station in limpopo fm

  • @charlesjimu6054
    @charlesjimu6054 10 วันที่ผ่านมา +1

    Tchimo limayitana Lin,zache

  • @StellaCharles-dq8db
    @StellaCharles-dq8db 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mcp mulungu walange ndinthu ndipo apange kanthu mudzina layesu akutitenga ngat chisiru ndinthu

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 10 วันที่ผ่านมา +1

    🔥🔥🔥🔥Ana Wachepa awa Zina amangoziyambadi...

  • @charlesjimu6054
    @charlesjimu6054 10 วันที่ผ่านมา +1

    God bless you ❤

  • @EsnartMalewa
    @EsnartMalewa 8 วันที่ผ่านมา +2

    😂😂😂

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 10 วันที่ผ่านมา +1

    Zigawenga zosadziw dziko akadziwe munthu ali kudimba zoon

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x 10 วันที่ผ่านมา

    Buddy Ntanyiwa ‼️
    Always proud of you ♥️🔥

  • @Angolnanjilayusufu
    @Angolnanjilayusufu 9 วันที่ผ่านมา

    God bless you comrade

  • @gifthara2460
    @gifthara2460 10 วันที่ผ่านมา +1

    Koma braz mumakwana athawa a mcp

  • @FaressPatel
    @FaressPatel 10 วันที่ผ่านมา +2

    Kkkkkkkkkk yomwe mwaiputayo chakwera ikuphulikikani

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 10 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi agapeyu ndindani nanga tundu wanji wamunthu ku malawi kuno agalu kwabasi ndi MCP yawoyo

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 10 วันที่ผ่านมา +1

    Ndipo anapa chilima ndi ameneyo lelo chikuza mawu ndi iyeyo aziwona ndithu atule pasi udindo

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 10 วันที่ผ่านมา +1

    Guz Malawi ndiwatu if anyone ali okudzidwa ndikulephera kwa Chakwera tiyen paunsewu tonse pa 10 July

  • @StevenFombe
    @StevenFombe 9 วันที่ผ่านมา

    Even Tv,Radio stations in Malawi are getting lessons though they are silent bravo

  • @AlinafeChimoto-pp7wp
    @AlinafeChimoto-pp7wp 10 วันที่ผ่านมา +1

    Pa 10 akuchoka bas

  • @mikephiri4092
    @mikephiri4092 10 วันที่ผ่านมา +1

    Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 10 วันที่ผ่านมา +1

      Not ulemu as such bro, amalawife ndombwambwana kwambiri man, mtanyiwa and bakili muluzi tv alongside bon Kalindo are doing their part for sure

  • @user-vw7tj2ss3l
    @user-vw7tj2ss3l 10 วันที่ผ่านมา +1

    Yomwey gulu iwe

  • @user-pl2lj6mh1z
    @user-pl2lj6mh1z 10 วันที่ผ่านมา +1

    Koma athu aku mcp mulungu achitepo kathu

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah 10 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwera wamupa chilima kuvuna akhale president galu kwabas

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 10 วันที่ผ่านมา +1

    Bambo mu mtanyiwa ulemu ndi wanu mulungu apitirize kukuyang'anirani

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 10 วันที่ผ่านมา +2

    Achita bwino 😂😂😂arirata😂😂

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 10 วันที่ผ่านมา +1

    Zoonadi brother mtanyiwa ifetinapanga mistake kuvotera Chakwera ndigululake komano chakwera aziwekuti wasalandi madzi amodzi

  • @user-vw7tj2ss3l
    @user-vw7tj2ss3l 10 วันที่ผ่านมา +1

    Yomwey galu iwe umakwan

  • @philonampha
    @philonampha 10 วันที่ผ่านมา +1

    27:11 ❤❤❤❤❤

  • @user-vl9se5bl9s
    @user-vl9se5bl9s 10 วันที่ผ่านมา

    Limpopo FM is number one

  • @SindawaPelekamoyo
    @SindawaPelekamoyo 10 วันที่ผ่านมา

    Respect to you bro nthanyiwa keep the 🔥 buuuuuu

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg 10 วันที่ผ่านมา +1

    Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu
    Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu
    Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu
    I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one
    I'm not just taking this is prophetic word
    Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu

  • @MervisYobe
    @MervisYobe 10 วันที่ผ่านมา +2

    Chikangawa Ali madzi😅😅😅

  • @ThoccoKakowa
    @ThoccoKakowa 10 วันที่ผ่านมา +1

    Osasiya kunena zowona

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by 10 วันที่ผ่านมา +1

    Walemphela udindo

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 10 วันที่ผ่านมา

    We need some more teachings brother man !!

  • @user-yu4np2wq4s
    @user-yu4np2wq4s 10 วันที่ผ่านมา +1

    😂😂😂😂😂😂😂musandikomole antanyiwa ine lero Koma kulizithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @PetroJack
    @PetroJack 10 วันที่ผ่านมา +1

    Limpopo ndi katundu uyu😂😂😂😂

  • @MosesLackson-l4f
    @MosesLackson-l4f 10 วันที่ผ่านมา

    Comrade umakwana bigup

  • @JefulyPesulo
    @JefulyPesulo 10 วันที่ผ่านมา +1

    Mumakwana ntanyiwa

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 10 วันที่ผ่านมา

    God bless you mr ntanyuwa ❤❤❤

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 10 วันที่ผ่านมา +1

    Komatu ndiye nyama ya malemu Chilima mwasavuka nayo afiti inu muyaluka simunati akanyimbi

    • @KenHaji-z3q
      @KenHaji-z3q 10 วันที่ผ่านมา

      Ipaseni moto nkulu

  • @EyobeAyala
    @EyobeAyala 10 วันที่ผ่านมา

    Ife kuno ku South Africa kungochotsedwa chifukwa Cha zomwe akupanga chakwela😢azaona konko ku Malawiko zomwe tizapange

  • @ZondoChirwa
    @ZondoChirwa 10 วันที่ผ่านมา

    Ntanyiwa more 🔥🔥🔥🔥🔥 fire

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 10 วันที่ผ่านมา +1

    My channel ❤❤❤

  • @user-vb5dh8ip6g
    @user-vb5dh8ip6g 10 วันที่ผ่านมา

    Our channel Malawian channel we love you comrade together with your people ❤❤❤

  • @martinaustin-qm9yp
    @martinaustin-qm9yp 10 วันที่ผ่านมา +1

    Kkk koma ntanyiwa usazamwalire uzangosowa mumat tsegula maso ndikutichosa khawa ndikavera mtima kut miyaaah

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 10 วันที่ผ่านมา +1

    Koma a mcp dzikoli ndiye mwalipezelera bwanji pasana panu nonse a mcp ndi masapota anu nonse zitsiru za anthu inu

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 10 วันที่ผ่านมา

      @@EdwardMathuwa Ndipo mbalame zokhazokha

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 10 วันที่ผ่านมา

    Great Job Ntanyiwa

  • @user-yi2fg1lh8x
    @user-yi2fg1lh8x 10 วันที่ผ่านมา

    Be blessed

  • @EmanMiles
    @EmanMiles 10 วันที่ผ่านมา

    🎉🎉🎉 to Limpopo FM

  • @LoveKhobiri
    @LoveKhobiri 9 วันที่ผ่านมา

    God be with u brother

  • @CatherineNkhala
    @CatherineNkhala 10 วันที่ผ่านมา

    Be protected sir

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 10 วันที่ผ่านมา

    Ulemu wanu Comrade ❤

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 10 วันที่ผ่านมา

    Chakwera woyeeeeeee! Mutu waima, ndipo a Malawi tisalole zopusa

  • @GeorgeChakuamba
    @GeorgeChakuamba 10 วันที่ผ่านมา +2

    Auze zoona a Malawi iwe umakwana ndipo ndimachita kukuika PA Bluetooth kut maneba amve nawo kkkkkk

    • @SmileMalanda
      @SmileMalanda 10 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 10 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 10 วันที่ผ่านมา

      umachita bwino

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 วันที่ผ่านมา

    South Africa ikangomuphulisa wagule uja basi, walowa mkati mwana wang'ona ameneyu

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by 10 วันที่ผ่านมา

    Respect for you

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 วันที่ผ่านมา

    Amuchita bwino kumuthyola msagwadazo on top of dat mapwala ake , atilakwisapo apaa kafucheche ameneyuu eish

  • @marthablessings1314
    @marthablessings1314 10 วันที่ผ่านมา

    Inde bwana wathu❤❤❤

  • @user-mo5od8cy3n
    @user-mo5od8cy3n 10 วันที่ผ่านมา

    No matter anyone to hate but the truth i talk.

  • @PatrickChirwa-cv5cd
    @PatrickChirwa-cv5cd 10 วันที่ผ่านมา

    Ntanyiwa mwathatu mungonena za security yanu tsopano kusonyeza mantha. Muzikhala ngati Bon Kalindo olo wa Bakili TV amabwera ndi nkhani ndi pfundo. Inu ndiye a DPP angowonongapo ndalama tsopano. Mukunena kuti muliku Botswana koma ma discussion anu onse mukunena kuti ku ku South Africa😂😂

  • @user-ky2fs3zr8y
    @user-ky2fs3zr8y 10 วันที่ผ่านมา +1

    Musamaname bwanji sitinaone pa sabc or ma channels ena kuti kwagwidwa zigawenga zotumizidwa ndi chakwera sizoona izi

    • @user-jm8kw9gw2d
      @user-jm8kw9gw2d 10 วันที่ผ่านมา +1

      Foolish young man, mcp the demonic party

    • @ChrifordBiziel
      @ChrifordBiziel 10 วันที่ผ่านมา

      Akufuna kumasochelesa anthu koma ife 203 wooooo uzingoseguea m'mimba

  • @user-vl8uw8mc3u
    @user-vl8uw8mc3u 9 วันที่ผ่านมา

    Mcp ikupangila kapeni Apm ngati sakuziwatu

  • @BMDMasulani
    @BMDMasulani 10 วันที่ผ่านมา

    Ntanyiwa umakwana Malata amayelekedwa mulungu amakumenyera nkhondo ntanyiwa kkkkkkkkkk

  • @ChiefJustin-cl8jl
    @ChiefJustin-cl8jl 10 วันที่ผ่านมา

    Limpopo fm ❤

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 10 วันที่ผ่านมา

    Malawi chikangawa party MCP .

  • @user-mo5od8cy3n
    @user-mo5od8cy3n 10 วันที่ผ่านมา

    I hate the late chilima and his members to make join and put MCP in government then anamutembenukila lero Ali Manda kusiya dziko la Malawi ndi anthu Ake mavuto 😂😂😂😂 in shot anafana oganinza kwambili rest in peace but you leave us in heavy fire 🔥🔥🔥🔥🔥