Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention
Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi
Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???
Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one I'm not just taking this is prophetic word Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu
Ntanyiwa mwathatu mungonena za security yanu tsopano kusonyeza mantha. Muzikhala ngati Bon Kalindo olo wa Bakili TV amabwera ndi nkhani ndi pfundo. Inu ndiye a DPP angowonongapo ndalama tsopano. Mukunena kuti muliku Botswana koma ma discussion anu onse mukunena kuti ku ku South Africa😂😂
I hate the late chilima and his members to make join and put MCP in government then anamutembenukila lero Ali Manda kusiya dziko la Malawi ndi anthu Ake mavuto 😂😂😂😂 in shot anafana oganinza kwambili rest in peace but you leave us in heavy fire 🔥🔥🔥🔥🔥
Koma ntanyiwa. Respect to you May the almighty God protect you wherever you will go
Keep up the good work comrade 💪💪
Ulemu wanu comrade Ntanyiwa.
Munandisangalasa yomweo chikangawa❤️❤️❤️🇿🇦🇿🇦🇿🇦🇿🇦 osavera Riiimpopo ndi ndimakhala ngati ndataya kofunikila
Ndipo kwambiri tu mmm
Salute comrade ntanyiwa,we love you and all Limpopo FM
Limpopo FM live from south Africa Durban Pietermaritzburg auzeni zoona amenewa
Panopa ine ndinasiya kuvela ma redio ena panopa ndili limpopo yokha basi
Ulemu wanu big mani mmatimvesa kukoma kwambili god bless you all the time ❤❤❤❤❤❤
Ntanyiwa and your fellow comrades excellent well done, and keep it up for the battle you are fighting for Mw nation
Mtanyiwwa ulemu wanuw mulungu asinkuphasa moyyo wabwinno ndawi sonse I pray for you all the time amalawi tili phamoto 🤲🤲🤲🙏🙏🙏mulungu dalisani Malawi
Respect bwana Ntanyiwa 🔥🔥🔥
Agape khombe amandibowa bwanjii eish!, i dont feel good wen i heard names like agape, kumkuyu, chimwendo, chakwela, zikhale, yolamu, vetino phiri, pter kalaya, billy malata, layitoni mangochi, ben longwe too many to mention
Ine mchifukwa chake ndinakana ntchito ya usilikali ndiyapolisi coz fans ya madepartiment amenewa ndiyombwambwana kwambiri, zigawenga zaku Israel and Ruanda zikungolowa mdziko mwathu ngat zikulowa mmanyumba mwawo, chomvesa chisoni kwambiri ndichoti asilikali ndi apolisi angoti vyooooo , vyooooo , osapangapo kanthu
Dzitsiru
Chifukwa iyeyu..akupanga zinthu zomwe south African ikhoza kukwiya nanzo.zomwe zingaikidze miyoyo yanthu ife amalawi pa chiswe😢
Antuwo zisilu kwabasi ...Antanyiwa gwilani nchito blo❤
My brother your number one keep it up
May good God knows everything and palibe chingabisike Mulungu ateteze malawians
Mtanyiwwa osawopha mulungu adalise inuyyo mulungu adalise inuyyo nosse
Tikuziwa zambiri GUYS mmmm Limpopo FM ndikatundu number 1
Comrade ntanyiwa mulungu azikupasa moyo wautali azikusogolera ndipo mupitiliza kuti pasila choona chamalawi Allah azikuteteza kulikose ukuyenda Limpopo FM ndimanyoya nayo ndikamavera
Limpopo inabwera kuzakhala
Ulemu wanu from Limpopo south Africa 🇿🇦
Mumatiimirira acomrade timakunyadilani❤
Tafika ndithu kuzamvera our very own limpopo Fm
Ndili pambuyo pako mtanyiwa
Mulungu akuulura chinachilichonso ku dziko langa koma vuto dziko langa linasankha kusamva koma limamva china chake chitachitika...Ambuye athandize Malawi
boma la zitsiru apolice army chakwera mitumbo ya chamanu
Mulungu wayitenga nkhondo imeneyi kukhala yake ndipo palibe yemwe angamenyane ndi MULUNGU.
OKHA OKHA A MCP AMENYANA NDIPONSO AWULULANA POSACHEDWAPA. IFE TINGOTI PHEEEEEE KUDIKIRA
Musalimbane ndi manyi woo aaaa muti asilikali alikuti??
Agalu osaziwa ntchitowo? ntchito zigololo bas.
ife tiibe ma ninja mmalawi muno aaaa
Chakwela sawina wapangila ena kapeni
Ndipo kwambiri tu mmm
LIMPOPO FM PALIBESO IFE TINGOTI NYADU
God's good always Amen
Mcp ikupanga zinthu zoopsyeza kwambiri ndipo zamdikwana mmmh
I salute you comrade, you are genius
Pangolin ..ntanyiwa ....
Tinakusowan Mr Mtanyiwa muli bwanji kumeneko kuno tili bwino ndithu
Wailesi yokhayo yomwe ambiri akuikonda kunvera panopa
Ndikuuza girl
Mutitumizire zithunzi za anthu omwe agwidwa ku South Africa.
It's only champion station in limpopo fm
Tchimo limayitana Lin,zache
Mcp mulungu walange ndinthu ndipo apange kanthu mudzina layesu akutitenga ngat chisiru ndinthu
🔥🔥🔥🔥Ana Wachepa awa Zina amangoziyambadi...
God bless you ❤
😂😂😂
Zigawenga zosadziw dziko akadziwe munthu ali kudimba zoon
Buddy Ntanyiwa ‼️
Always proud of you ♥️🔥
God bless you comrade
Koma braz mumakwana athawa a mcp
Kkkkkkkkkk yomwe mwaiputayo chakwera ikuphulikikani
Kodi agapeyu ndindani nanga tundu wanji wamunthu ku malawi kuno agalu kwabasi ndi MCP yawoyo
Ndipo anapa chilima ndi ameneyo lelo chikuza mawu ndi iyeyo aziwona ndithu atule pasi udindo
Guz Malawi ndiwatu if anyone ali okudzidwa ndikulephera kwa Chakwera tiyen paunsewu tonse pa 10 July
Even Tv,Radio stations in Malawi are getting lessons though they are silent bravo
Pa 10 akuchoka bas
Amalawi let’s gather together and fight like our fell Kenya’s bakili tv and Limpopo fm thy are doing there parts ife tonse tikutani kapena yathu ija ya Ulemu???
Not ulemu as such bro, amalawife ndombwambwana kwambiri man, mtanyiwa and bakili muluzi tv alongside bon Kalindo are doing their part for sure
Yomwey gulu iwe
Koma athu aku mcp mulungu achitepo kathu
Chakwera wamupa chilima kuvuna akhale president galu kwabas
Bambo mu mtanyiwa ulemu ndi wanu mulungu apitirize kukuyang'anirani
Achita bwino 😂😂😂arirata😂😂
Zoonadi brother mtanyiwa ifetinapanga mistake kuvotera Chakwera ndigululake komano chakwera aziwekuti wasalandi madzi amodzi
Yomwey galu iwe umakwan
27:11 ❤❤❤❤❤
Limpopo FM is number one
Respect to you bro nthanyiwa keep the 🔥 buuuuuu
Eyetu ameneyo nde mulungu inuyo ngati mukukwanitsa kutseka anthu pakamwa ndindalama ndiomwewo opusa osusuka achina yudasi Ana anjoka inuuuuu
Malawi mizimu yambiri ikuzunzika kusowa chisamaliro zinthu zinakwera kuli okalamba Ana amasiye nzipatala kundende ndi anthu onseee mdzikomu ofuna zabwino koma ayi zikuvuta kwacha mwagwetsa mwagwetsanso ma million mukukhonyolera m'matumba mwanu kukhutisa mimba zanu
Nde pemphero la olira ovutika Mulungu samalisiya amayankha mwachangu nde anthu ayamba kugwidwawa nchiyambi chowululika zinsisi zanu
I'm repeating all most each and every day kuti you will pay one by one
I'm not just taking this is prophetic word
Mulungu ndiokwiya nanuuuuuu anthu amagazi m'manja inu
Chikangawa Ali madzi😅😅😅
Kkk
Osasiya kunena zowona
Walemphela udindo
We need some more teachings brother man !!
😂😂😂😂😂😂😂musandikomole antanyiwa ine lero Koma kulizithuuuu 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Limpopo ndi katundu uyu😂😂😂😂
Comrade umakwana bigup
Mumakwana ntanyiwa
God bless you mr ntanyuwa ❤❤❤
Komatu ndiye nyama ya malemu Chilima mwasavuka nayo afiti inu muyaluka simunati akanyimbi
Ipaseni moto nkulu
Ife kuno ku South Africa kungochotsedwa chifukwa Cha zomwe akupanga chakwela😢azaona konko ku Malawiko zomwe tizapange
Ntanyiwa more 🔥🔥🔥🔥🔥 fire
My channel ❤❤❤
Our channel Malawian channel we love you comrade together with your people ❤❤❤
Kkk koma ntanyiwa usazamwalire uzangosowa mumat tsegula maso ndikutichosa khawa ndikavera mtima kut miyaaah
Koma a mcp dzikoli ndiye mwalipezelera bwanji pasana panu nonse a mcp ndi masapota anu nonse zitsiru za anthu inu
@@EdwardMathuwa Ndipo mbalame zokhazokha
Great Job Ntanyiwa
Be blessed
🎉🎉🎉 to Limpopo FM
God be with u brother
Be protected sir
Ulemu wanu Comrade ❤
Chakwera woyeeeeeee! Mutu waima, ndipo a Malawi tisalole zopusa
Auze zoona a Malawi iwe umakwana ndipo ndimachita kukuika PA Bluetooth kut maneba amve nawo kkkkkk
😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
umachita bwino
South Africa ikangomuphulisa wagule uja basi, walowa mkati mwana wang'ona ameneyu
Respect for you
Amuchita bwino kumuthyola msagwadazo on top of dat mapwala ake , atilakwisapo apaa kafucheche ameneyuu eish
Inde bwana wathu❤❤❤
No matter anyone to hate but the truth i talk.
Ntanyiwa mwathatu mungonena za security yanu tsopano kusonyeza mantha. Muzikhala ngati Bon Kalindo olo wa Bakili TV amabwera ndi nkhani ndi pfundo. Inu ndiye a DPP angowonongapo ndalama tsopano. Mukunena kuti muliku Botswana koma ma discussion anu onse mukunena kuti ku ku South Africa😂😂
Musamaname bwanji sitinaone pa sabc or ma channels ena kuti kwagwidwa zigawenga zotumizidwa ndi chakwera sizoona izi
Foolish young man, mcp the demonic party
Akufuna kumasochelesa anthu koma ife 203 wooooo uzingoseguea m'mimba
Mcp ikupangila kapeni Apm ngati sakuziwatu
Ntanyiwa umakwana Malata amayelekedwa mulungu amakumenyera nkhondo ntanyiwa kkkkkkkkkk
Limpopo fm ❤
Malawi chikangawa party MCP .
I hate the late chilima and his members to make join and put MCP in government then anamutembenukila lero Ali Manda kusiya dziko la Malawi ndi anthu Ake mavuto 😂😂😂😂 in shot anafana oganinza kwambili rest in peace but you leave us in heavy fire 🔥🔥🔥🔥🔥