It is a political song, he was advising people to choose wisely in reference to what happened in the Scriptures like those people in times of Moses. Some men wanted to rule others without the blessings of Lord. So this angered Lord and He killed them by demanding the land open and swallow all who dared
Nkasa you are the best artist ever love your songs very meaningful
Mumakwana big man nkasa❤❤
I have been looking for song for very long time thank you for uploading this album great job ❤️
Nyimboyi ikungombusa Amalawi ufumu omwe ulipo panopou mkasa is the best keep it up good work 👌
So happy to hear this song today
Phungu ndi opanda nzake very talented Man ❤❤❤❤❤❤ mibado yonse idzamukumbukira nkasa
Your number one very nice song 2004 nthawi imeneyo
This man is great, and blessed
Koma adawawa amatha composition
The legendary Phungu Joseph Nkasa
Very prophetic
Music that stands out for ever and shall never die
ZAMUUDZA BRIAN BANDA KUTI AZITIIKILA IMENEYI
Kkkkkkkkk
🎉 tizivera zimenezi
If I could only have a chance to meet this great musician!!!! #phungu Joseph Nkasa
I shed tears in joy listening to this.
Nkasa Ndimakukonda ndipo ndidzakukonda mpaka kale coz umagwetsa nice tune
At last I was looking for this song for a long time thanks for uploading it
Ndmamkonda kwambil mkasa for ever
Mr Nkasa you right l like this song and keep telling Malawian that this is rong 😢
I don't hear the language but l like the rhythm
Ok he's says nkhope ili pa ndalama ndiyandani? whose face is on the money? it's like Ceazar's story
😂😂😂😂😂
It is a political song, he was advising people to choose wisely in reference to what happened in the Scriptures like those people in times of Moses. Some men wanted to rule others without the blessings of Lord. So this angered Lord and He killed them by demanding the land open and swallow all who dared
Would I give you in English?
Iwe ndi zoba eti😂
Legend in making,, pure talent
Am so happy to listen to this song again
Nkasa mmati yimirira pa chilungamo go on
Uyutu ndi Legend.amalemba lyrics
It reminds me of my early days in Malawi
PURE TALENT,ULEMU WAMU ANKASA
Ulemu wanu a nkasa this album munatswa zeni zeni, you will remain legend musician
My favorite truck from Tigwirane Manja album it was on repeat the time i had tape player
Ulemu wanu a nkasa
Phungu ndamunadi💪
Ine ndingopeleka ulemu kwa Nkasa
Nkulu uyuyu amatha
munthu oziwa chimene akuimba
Surefire!!!!!
Khaaaaa
Tidafela ubusa lero ndiizo
The song was targeting Bingu but look at Malawi situation now😅.... Tinasankhadi olakwika😂
Zinthu zikati zitembenuke 😂
😂😂😂
U are very right ASE .. actually looking for this type of comment ..the song was for bingu😂😂😂
Munthu wabwino mkasa , amandisangalatsa pamayimbidwe
Vunga dada umakwana hvy
Koma ndiye opandadi mfundo
😂😂😂
Zikomo kwambiri
Quality sounds, please keep it up
Ilike this guy
Thanks for this song, been looking for it
It was time bambo nkasa
i was cry thinking of my background when this song plays
Wuuuuuuuuuu don't remind me this song guys well composed
😂😂😂😂😂Tinasankhadi Chakwera wamisala mfiti nthakati lero tikulira coz chosankha olakwika
🎉❤
Pankhani yanyimbo awandiabwna
NICE SOUND
Machine
Timakunyadilani a mkasa
Fitting Chakwera nw
Munthu wankulu phungu
Katundu uyu
nomber one nkasa
🔥🔥
Who else is here for comments 😅
Nice
Nyimbo yabwino yakale iyi tisamve kuti mwamumangaso mwamva a ng'ona inu??
The song was for late bingu
Chisuro chanjanji
Abwanawa amatha
Chopanda fundo ngat chakwera
Nkasa ndi nkasa, osamuntenga mulungu ngati nsiweni wanu
Tidasankhad olakwika 😂😂😂
Heavy weight
Chakwera 🤣🤣