KUCHIPANI CHA UTM CHADABWITSA ANTHU🤔🤔

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 21 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 169

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt หลายเดือนก่อน +17

    SKC was a general fitter analibe kuyankhula za munthu koma maso ake anali ku dziko la malawi kuti lizakhare pabwino, now Usi amayenera kuwafikira a U TM amnzake powawuza za kusankhidwa kwake

  • @user-ui7wv1mb4g
    @user-ui7wv1mb4g หลายเดือนก่อน +6

    No need for imposing Usi on UTM. Usi has been so slippery in UTM. Let him go and we shall see if he is going to survive in MCP. UTM Executive may opt to accomodate him but as for ordinary members its a big NO! Why this time? Where was he all that time when our dear president was alive? Zachibwana a ayi. Usi safunika. Apite akachite zake aone ngati angadzatione.

    • @StewartMustafa
      @StewartMustafa หลายเดือนก่อน

      Yes Usi can't survive in MCP if he doesn't know. But let's give him chance to proof him self whether he z an UTM member or not?

  • @yohaneben5452
    @yohaneben5452 หลายเดือนก่อน +4

    I think most of the people don't know more about usi,although he is vp of UTM but originally he is a member of MCP.

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb หลายเดือนก่อน +23

    Chitsiru manganya ndiwa MCp anampha chilima ameneyo anakambapo Chan Za lfa yachilima galu uyo ndi chakwera

    • @princedetbozsmallboy1749
      @princedetbozsmallboy1749 หลายเดือนก่อน +3

      Tikudabwa nawo anthu ena usiyu anaphanawo Chilima shame on him galu

    • @jelsonmlowoka8611
      @jelsonmlowoka8611 หลายเดือนก่อน

      Usova iwe ndiwe ndani kumuletsa usi kusakhala vp wa dziko, why did the utm owner appoint him as his runningmate at first, leaving you with no any position in the party?

    • @GibsonBanda-ey2gc
      @GibsonBanda-ey2gc หลายเดือนก่อน

      umbuli

  • @AckimMhango-v1x
    @AckimMhango-v1x หลายเดือนก่อน +9

    Vuto lalikulu ndi boma chifukwa linayamba kukhala ndi Usi before Chilima asanamwalile

  • @leonardzchavula3139
    @leonardzchavula3139 หลายเดือนก่อน +21

    Its unfortunate that UTM has not shown any excitement on the appointment of Dr M B Usi,however constitutionally he was the appropriate choice.Had Chilima won the presidency in 2019 Usi was to be State Vice President. UTM has just to accept the situation.

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 หลายเดือนก่อน +2

      I am on one of MCP whatsapp groups. I know that Usi is MCP. I am also an MCP member but I don't like Chakwera

    • @MirriamKambale
      @MirriamKambale หลายเดือนก่อน +4

      He deserve deserve the appointment coz he was utm vp but it doesn't mean utm could have been overjoyed coz they're still in mourning time

    • @Betty-fe9ql
      @Betty-fe9ql หลายเดือนก่อน +4

      His conduct from the 10th leaves a lot to be desired, your senior dies and you don't say a single word what's that

    • @chimwemwedulla6760
      @chimwemwedulla6760 หลายเดือนก่อน +1

      Inu zomwe usi anayalkhula komulunbiritsa kuja amaoneka ngati anali namalira amene uja?

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 หลายเดือนก่อน

      Anamalira munali inuyo​@@chimwemwedulla6760

  • @DysonKamama-yh7hq
    @DysonKamama-yh7hq หลายเดือนก่อน +7

    Zitheka bwanji munthu anzako akulila koma osakakumana ndiakuchipani chanu before kulumbilisidwa, iye nkumakasangalala chilipo

    • @CharityChikomo-hl1gz
      @CharityChikomo-hl1gz หลายเดือนก่อน

      My question exactly was he never suppose to ask his fellow utm members before making his mind???anywy zoona zidzaziwika mu nthawi yamulungu

    • @PociahMack
      @PociahMack หลายเดือนก่อน

      ​@@CharityChikomo-hl1gz zimene a mayakhula a UTM munthu amene anali ndi umunthu kunali kovuta kumakhala nawo, even akubanja paja anatulusa chikalata chowadzudzula.

  • @user-ko2yv4gi5y
    @user-ko2yv4gi5y หลายเดือนก่อน +4

    Chilungamo ndi amanganya anatengapo gawo lakuphedwa kwa saulosi chilima ndingakhale pakwanu pa inu mukuyakhula pali munthu amene anatenga nawo chigawo kuwapasa udindo iwowo kulibe kathu koma chilungamo anthu aku utm akudziwa kuti panali ngwilizano pakati pa manganya ndi chilima

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma หลายเดือนก่อน +3

    Koma anthu Inu muli ndi nzeru?a utm apita bwanji kukaombela mmanja ali pa maliro?Kodi malamulo ake amtundu wanji week sinathe ena ayamba ukuvina kulumbilitsana a Malawi?which means it was planned this b4 imfa ya chilima khalani ndi nzimu waumunthu eeti

  • @RonicSouza-sk5ux
    @RonicSouza-sk5ux หลายเดือนก่อน +3

    Usi didn't consult the party when he was told about the news of his presidency

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 หลายเดือนก่อน

    I cant believe malawi judges still wears whiteman hair....
    "I once thought that educated pple are wiser"

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon หลายเดือนก่อน +4

    Nonse munakonza program iyi ndinu anthu opanda nzeru mukuonesakuti muli mbali ya mcp mumafuna kuti a utm akapeze ku parliament chosecho president wao wangoikidwa kumene m'manda, athaphedwa ndi mcp agalu kwabasi zikanakhala kuti zachitika mnyumba mwanu sibwezi mukukamba uchisiru mukukamba apau anthu opusa opanda chisoni

    • @user-un6qv6sj3h
      @user-un6qv6sj3h หลายเดือนก่อน

      True bro

    • @rodgerskatengeza1903
      @rodgerskatengeza1903 หลายเดือนก่อน

      Constitution imapeleka masiku ochepa president or vice president akamwalira kuti asankhe wina

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb หลายเดือนก่อน +4

    Inuso mphokoso kusowa zakamba position ndikuluza munthu malamuro ndichani zachamba et manganya amafuna Kare uvp Kare that way anamupereka chilima kwa mikangoyo mukusokosa kusowa zakamba

    • @user-ez4ru5sk2l
      @user-ez4ru5sk2l หลายเดือนก่อน

      The truth is that SKC shoes are unfittable in all the alliance...and entire country leadership currently....but the country has to move forward.....ndale sizinthu zamuyaya ... it's about servanthood ... service to the people

  • @user-xz7mo8zy8f
    @user-xz7mo8zy8f หลายเดือนก่อน +5

    Cheap propaganda. UTM mukuganiza bwino kwabasi

  • @hagayichiluwe
    @hagayichiluwe หลายเดือนก่อน +2

    It's just reminding me that sanje kapena nkhwidzi exist

    • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
      @CHIFUNDOCHINA-lp9lg หลายเดือนก่อน

      Vuto la USI anazionetsera KUTI Sali ku UTM,ATANGOMWALIRA CHILIMA,Nde chipani chisangalala bwanji

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p หลายเดือนก่อน

    What is Dr. Usi bringing to the leadership of VP and UTM. will be the question.

  • @mathewssimbi3052
    @mathewssimbi3052 หลายเดือนก่อน +2

    Koma ngakhale palibe umboni okwanira mafedwe a chilima ndiwonkhumudwitsa kwambiri ndipo ndiwokayikitsa kotero mkovuta Kuti lero ndi lero akulu akulu a UTM adzikapezeka akuyimba nthungululu pamwambo wosankhidwa Kwa Ausi kotero kusapita kwao kumwamboku mkovetsetseka zongofunika tsopano kuwona kutsogolo

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f หลายเดือนก่อน +2

    Kusankhidwa kwa Michael usi wasatila ndondomeko yake chifukwa iye anali osatila wa the late SKC.komano tingodziwa kuti usi ali ku UTM kapena ali ku mcp?

    • @user-un6qv6sj3h
      @user-un6qv6sj3h หลายเดือนก่อน

      Adalowa kalekle MCP

    • @user-ik5sz8hc6f
      @user-ik5sz8hc6f หลายเดือนก่อน

      @@user-un6qv6sj3h vuto ndilimenelo.Anayenela kukhalabe wa UTM kuti alemekeze ukuru former president of UTM

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 หลายเดือนก่อน +1

    Nonse ndinu wanzeru zochepa mulankhuranu a UTM atiuzeso chani poyera zaku lephera kwao kosapezeka kolumbilitsa, pomwe anjawala adanena kale tikadalira nde mufuna atiuzeso chani za milandu basi

  • @lucksonnyirenda1168
    @lucksonnyirenda1168 หลายเดือนก่อน

    with UTM Dr Usi has failed as leader, he always sideline himself from his fellows, previously he dont associate with Utm members to please the president, even in this dark period he has failed to take a balance step by being to the part side & government side
    Usi has failed as a leader

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l หลายเดือนก่อน

    UTM this is your good time and best Future be united guys chipani chizalowa muboma pachokha don't expect kuzalamulira Malawi

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f หลายเดือนก่อน +2

    Anthu amene aludandaula zanthawi sakudziwa zamalamulo amdziko

    • @IdrisYousuf
      @IdrisYousuf หลายเดือนก่อน

      Àluthu aluamenewo aludandaulawo alukuti taludziwe😅😅😅😅😅😅

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Kuteleko achakwera atafa lelo manganya akhala president.......nonononono...
    Manganya sakuyenela kukhala president ....munthu wamfupi ngati ameneyi ngakhale phazi lake ayi ndithu simunthu oti anthu onse aziyang,ana
    Iye

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p หลายเดือนก่อน +1

    Malamulo amanena kuti for 7days pasankhidwe munthu wina,,komaso sakanankhidwa wina koma Usi chifukwa anali vp wa chipani cha UTM,,so guys I don't know why we don't understand for this issues,,,we suppose to understanding because it's a rule,, it's not opinion for someone

  • @NefassiNefitarZaqueioZaqueio
    @NefassiNefitarZaqueioZaqueio หลายเดือนก่อน +1

    Ngati palakwika kulumbilitsa a Usi nsanga ,tilolerane inuyo mukudzidzulanu sindinu angwiro muli ndi zofooka zanu choncho ngati late Chilima adasankha a Usi adaona kuthekera komwe kuli mmenemo. Kaya wina afune kaya asafune zili choncho basi olo mutukwana olo mutakhala chete ,zichitika zomwe mulungu wavomereza

  • @RaphaelMaunde
    @RaphaelMaunde หลายเดือนก่อน

    The appointment is right decisions but there is some issues between Dr Usi and UTM party Dr Usi was not royal to the party

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p หลายเดือนก่อน

    Malamulo are there but we pick and choose what to enforce in Malawi" s constitution.

  • @StewartMustafa
    @StewartMustafa หลายเดือนก่อน

    Gentlemen plzzz lets take this issue very seriously.
    Dr Usi z not wrong kulandila udindo kapena kuti VP. Ndizoona kuti Dr Usi anayamba kukhala ndi boma more especially president of the republic kalekale komano chomwe tingadziwe ndichakuti even The laye Dr Saulos Chilima adali pafupi ndi boma more especially to the President of the Republic.
    Now gents if u digest all of these it means these pple r wel organised coz they both take one step at a time.
    Now lets not talk a lot of things when its not time to do so. Time will tell whereby will will proof Dr Usi that is a member of MCP or He z still with us in Almighty UTM.

  • @tamalangoma2765
    @tamalangoma2765 หลายเดือนก่อน +2

    May be you should blame late VP for choosing Usi ngati VP wake.
    Please stop making too much noise.

  • @ishmaelsiffah9900
    @ishmaelsiffah9900 หลายเดือนก่อน

    Ussi samapanga za UTM n the sad point ndizomwe timaziona munthawi yomwe anthu amapanga zamaliro a SKC ndi ena,iwo aja being munthu wamkulu wachipani pambuyo pakumwalira kwa achilima iwowo ndamene timayembekezera kuti ndiomwe azititonthoza ndikumatipatsa ma update amomwe tiyendere koma mmalo mwake anamusiira mzimai kumapanga zazimenezo n zinatengera kulimba mtima kwamai Kaliyati osatopa,osafooka kumatiyankhula amalawi nthawi ndinthawi,mukumbukirenso kuti ndi a Ussi omweo akuwafunsa zakuimila kwao kwaku Blantyre anakanitsitsa kutchula kuti akaimila chipani chanji yet munthuyo mukuti ndiwa UTM pamabvuta pati kunena zokuti akaimila UTM izo ndizachidziwikile kuti akulu amenewa UTM anaituluka kumangotsala kuti officially alengedze kuti atuluka

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 หลายเดือนก่อน

    Onse Ali apa ndi zitsilu , how Catherine be sitting and talking while the responders they say ,they are still mourning and it's true Malawian are mourning ndale zophana basi achewa opanda Pache inu

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 หลายเดือนก่อน

    Choyamba tidziwe kuti mu zipanimu utsogoleri umasankhidwa through convention nde kusankhidwa kwa usi sikutanthauza kuti ndi mtsogoleri wa utm. By the way the government could write aletter to utm based on their agreement to prove that the alliance is still valid. Koma kungotenga munthu personally uuùuuu it's clear usi si wa utm

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Anthu anakwiya chifukwa amene anapangisa kuti chilima aphedwe ndi micheal usi....manganya

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Anamupeleka saulosi chilima ndi Micheal usi ....manganya chisilu cha munthu.....manganya ku mcp wapitako yekha chisilu cha munthu

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 หลายเดือนก่อน

    A Usi akafike,,amawaposa Mr Njawala zochita

  • @user-eb2yo9bc9k
    @user-eb2yo9bc9k หลายเดือนก่อน

    I doubt of all this, am confused but what I know is that utm is not happy with that

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo2972 หลายเดือนก่อน

    Don't just say this...who do you think kuti akanamusakha? Mention her or him....

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Nkhani iyi yakupha chilima sizatha mumtima mwathu .....mcp muziwe chilima apangisa kuti mcp ivutike osati masewela .....chipani chokupha ....amalawi sitizayiwala ayi

  • @RoseLameck-ub7sq
    @RoseLameck-ub7sq หลายเดือนก่อน

    Ine dakalila malilo achilima singakambe kathu ndingodikila chaka chamawa ka vote bas chiweluzo nkaweluzila komweko ndichala changa😢

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v หลายเดือนก่อน +1

    Koma tu anthu mcp mukamapanga zithu mudziziwa kuti mawa ndi tsiku Lina

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 หลายเดือนก่อน

    It can stay kufika pa 2 July ndipo panakhala popanda vice Kwa chaka bwa a Chilima atamangidwa

  • @Stewartchikoja
    @Stewartchikoja หลายเดือนก่อน

    Kodi ngat wina adakhala Dzaka 4 osapenza mpumulo pa office yake how about 1 Yr chingasithe ndi chani ?

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm หลายเดือนก่อน

    Move yonse yakuphedwa kwa Chilma amayiziwa asapuse fans.

  • @AnnesBaulen
    @AnnesBaulen หลายเดือนก่อน

    Zankutu,ngatiakutumani machende Anu ndi abwana Anu omweo kuphatikiza manganyayo

  • @wellosmbewe6820
    @wellosmbewe6820 หลายเดือนก่อน

    Who is the president of UTM now and what is his speach

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l หลายเดือนก่อน +3

    This is talking reality... Kodi ndani sakuziwa ngozi vuto ndilakuti ndi ndege yoyamba kugwa ku Malawi. Komaso DPP yokusonkheza moto kwambiri kuti utm isokonekere

    • @princekandulu4542
      @princekandulu4542 หลายเดือนก่อน

      Mmenenso MCP n imakokomeza mikangano ku Dpp

    • @chimwemwedulla6760
      @chimwemwedulla6760 หลายเดือนก่อน

      Ndiwe mbuzi

    • @spargomw
      @spargomw หลายเดือนก่อน

      Mwana wa Ng'ona iwe, khakhakha. Za DPP zikukukhudxa chaaa, zipangan zanu. Ife tili ku ma stand

  • @OmexPoisonkaombe-cf7bz
    @OmexPoisonkaombe-cf7bz หลายเดือนก่อน

    Kusapanda nseru anapha bwanji vice president wathu ameneyo bas

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 หลายเดือนก่อน

    A UTM ku sapita kolumbilitsa a Usi nkutheka sadalakwise mwina sadayitanidwe patha kukhara padalibe consultations,

  • @humphreysidie4747
    @humphreysidie4747 หลายเดือนก่อน

    Guys ineso ndufuna kumangidwa, this Usi guy knew everything, he sold Chilima

  • @ChisomoPound
    @ChisomoPound หลายเดือนก่อน

    Khaniyi mutati muyione ndiyovutirapo vuto Lili APA anthu ambiri andale amafuna maudindo ngat awa ndiye pamakhala kuyang'anizana ndi diso lofila ngat iweyo sunasakhidwe,choti muziwe Pali zina zimachitika mwamalamulo tiyeni tibwelere mbuyo 2012 bingu wa muthalika atamwalira Ku dpp kunali ambiri amafuna udindo koma anayiwala kut Kuli lamulo lot ngat president watisiya vice ndi yemwe akuyenera kukhala mlowa mmalo ndiye izizi zomwe zikuchitikazi khani siyina ayi maudindo amenewa Kuli kapezedwe Ka ndalama mwaulesi

  • @williamsjonazie5764
    @williamsjonazie5764 หลายเดือนก่อน

    Choyamba tiwunikile Kaye kuti Kodi chakwera poziwa kuti usi ndi vice president wa UTM anawawuza za appointment ya usi? Ngati adatelo ndiye a UTM analakwisa kusapita koma ngati sadawauze za kusakhidwa Kwa usi adachita bwino kusapita chifukwa usi wangokhala vice president wa UTM koma ndi member wa UTM,executive ikanaziwisidwa mwa dongosolo and then invited kukalumbilitsa vice president. Nde anthu musamangofutsa mafutso mwina mufutse chakwera yo. Ndamene angalongosole momwe adayendesela ndondomeko yake.

  • @EsnartMartin
    @EsnartMartin หลายเดือนก่อน

    Ineso Manganya simnamulandire ku UTM

  • @AllaniWilesi
    @AllaniWilesi หลายเดือนก่อน

    Ausi achita bwino inde koma asamanyengane nda azimayi ayeni pakuti Ali ndimbili yonyasa kwambili

  • @yasitafuphiri-nw2he
    @yasitafuphiri-nw2he หลายเดือนก่อน

    If Usi was never a UTM member, y Chilima appointed him as party VP?

    • @jelsonmlowoka8611
      @jelsonmlowoka8611 หลายเดือนก่อน

      Your question is very straight and correct

  • @Moffat-oi4yx
    @Moffat-oi4yx หลายเดือนก่อน

    Akanganya inu mwalandila banzi chakwelayo akalemekeze malamulo osankha vp bwanji sanalemekeze malamulo Osaka ndegeija kumawalozela anthu kolakwika akudziwa chilungamo

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw หลายเดือนก่อน

    Amalawi zinawamvesa chisoni kwambiri powona kuti ausi sanali busy ndi ifa yachilima ndipo analibeso chisoni chaifa imeneyi ndamene apeleka chilima ndipo nchochodi udasi

  • @stevenbanda-zp7ie
    @stevenbanda-zp7ie หลายเดือนก่อน

    Is Michael USI Acting president of UTM??

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona หลายเดือนก่อน

    Olakwa ndi usi chifukwa ngati achakwela anamufonela za nkhani iyeyo akanadziwitsa anthu achipani chake kuti zili motele titani amve maganizo awo

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm หลายเดือนก่อน

    Manganya he is a snake ndiwa Mcp .every knows about that, chitsilu cha munthu

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q หลายเดือนก่อน

    Manganya sanali wa UTM analowa MCP kale kale mosadziwa anthu mumtima mwake anali wa MCP

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 หลายเดือนก่อน

    It not alaw, kut you must choose the vice president wachipani, that is a trap iwe manganya akupasa zingati why you didn't have time to settle and see it with your utm people

  • @HellenKanyemba
    @HellenKanyemba หลายเดือนก่อน

    Atolankhani thawing zina ndinu anthira kuwili achakwera sanamusankhe usi koma achilima ndio anasankha a usi koma achakwera angitsatira lamulo basi

  • @RonaldGama-gz9ug
    @RonaldGama-gz9ug หลายเดือนก่อน

    Kodi a UTM wo mukuwafuna kuti atanipo Pa nkhaniyi coz they can't reserve the time anayankha zomwe iwo Ali ndiye chinanso ndi chani

  • @Happy-e8d
    @Happy-e8d หลายเดือนก่อน

    Ndinakakhala ine ndikanaka kukhala VP

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 หลายเดือนก่อน

    Dziko La malawa amipingo ndamene anasokoneza ndi athila kuwili amasokoneza athu iwo ananena sakhani tsogoleri asakha akubweraso mwasakha thawi yolakwika kkkk koma guys mavuto Eni Eni and manganya anali wachiwili kwa wachiwili anayenera akhala iye kaya😢

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau หลายเดือนก่อน

    Ndichimodzi modzi bingu atamwalila sitinakhale ndi pulezident wanyowani

  • @MikeKatola
    @MikeKatola หลายเดือนก่อน

    Inenso sindikuona vuto bcz olo ufumu amalonga wina mfumu asanaike.so why utm akuonesa kukwiya.akukwiya ndi anthu oti sakuziwa kuti chilima ndi usi amagwirizana chani.

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td หลายเดือนก่อน

    Munena angati mutukwana angati anzathu patsogolo Ife basi zaziii nthawi ikupita tichedwa zinenani bola chakwera sadandaula anaona kale Kuti sanje zilipo kuteloku Wena mtima uwawa Kuti basi manganya wapita basi ayi zosiyilana mawa ndinu pepani mulungu akusungeni

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r หลายเดือนก่อน

    Awusi anarephera kutengapo gawo, kufa kwa skc relo palibe sngakondwe nazo asiyen azipanga zomwe amatha ndi kongweresi yakeyo

  • @SuzgoMunthali
    @SuzgoMunthali หลายเดือนก่อน

    Awa so akukamba no nonse

  • @TaniaMphalumo
    @TaniaMphalumo หลายเดือนก่อน

    Zauchisilu basi wasangalalanazo ndani utm muyisiye agaru inu

  • @user-sh6gi5uq3l
    @user-sh6gi5uq3l หลายเดือนก่อน

    Amalawi let's move on zinazi tichedwa nazo mulungu salakwisa kodi amalawi mpaka liti tijusungabe mangawa look at APM for not accepting the fact someone is ruling now aaaa moti a UTM amafuna kufunsidwa maganizo pomwe thawi yochita appoint veep itakwana and azichedwa ndizosangala munthu mmmmmm. Malawi my country learn to accept God's plan

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika หลายเดือนก่อน

    Anachita bwino a UTM munangagulitsa chipani mwaganiza bho

  • @HanifiYaumu
    @HanifiYaumu หลายเดือนก่อน

    Kape manganya akudziwapo kathu pa infa skc

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft หลายเดือนก่อน

    Usi siwa utm ndiwa mcp uja musatinamizepo apa

  • @user-ql8sj4jj3y
    @user-ql8sj4jj3y หลายเดือนก่อน

    Total lay dpp sizikuwakhuza

  • @TsholofeloTong
    @TsholofeloTong หลายเดือนก่อน

    Usi please just go to your MCP because we already know that you're mcp member

    • @Maliet-nh6kf
      @Maliet-nh6kf หลายเดือนก่อน

      Uyanya mcp kupha

  • @user-ql8sj4jj3y
    @user-ql8sj4jj3y หลายเดือนก่อน

    Manganya ndi mcp,, if he was vice wa chilima, atamwalira dr chilima was just qite why

  • @MarkGonda-qr4vm
    @MarkGonda-qr4vm หลายเดือนก่อน

    Koma ndiye azingopanga zamasewerotu amanganyawa

  • @user-sh6gi5uq3l
    @user-sh6gi5uq3l หลายเดือนก่อน

    Akapusa a UTM a muluza manganyawo atuluka

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs หลายเดือนก่อน

    A UTM ananyanyaladi ndizona Koma anakakhala kt asakha aliyese akanavomelabe chifukwa andalewa amafuna ndalama osati kutisogolelai ndichifukwachake zipani zikungobadwabe aliyese akufuna kukhala pamwamba

  • @user-vr5jn8sz5r
    @user-vr5jn8sz5r หลายเดือนก่อน

    Manganya ndi wa MCP ngati inunomwe a ZBS musamati pepelese.

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau หลายเดือนก่อน

    Kodi akankhala kuti anali apulezident kuti ndiomwe atisiya Chilima automatically akanakhala pulezident Kodi kolumbilitsa sakanapita

  • @MerryWayson
    @MerryWayson หลายเดือนก่อน

    Musakhale ndimafunso inu omwe mukuzitcha boma lachakwera cos mukufunsa mukuziwa kut Usi ndi chakwera ndiwomwe anapanga plan yopha chiluma anthu akupha inu. Mukuona ngat sitikuziwa kut Usi analu akulumikizana nseli ndi chakwera . Kut aphe chilima ndawi yomwevali moyo agalu

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w หลายเดือนก่อน

    Palibe chimene angachite Usi, and Malemu ndiamene adatsogolera kubweretsa mavuto ali ku Malawi lero.

    • @user-ui7wv1mb4g
      @user-ui7wv1mb4g หลายเดือนก่อน

      What mavuto are you talking about . Was he on the driving seat? Kufooka kwa wina osaloza chala ena

  • @saidimwanyali8969
    @saidimwanyali8969 หลายเดือนก่อน

    Kodi pofuna kusanga ausi achakwera adayitana ausi oka kapena adayitana chipani chonse ndikumasanga kapena anawasanga kuseri

  • @user-oe1lg4xo7w
    @user-oe1lg4xo7w หลายเดือนก่อน

    Mamembala a UTM akuziwa kuti Razalo wasankha nkhwali kuti ikhale pampando wa vp

  • @RonaldGama-gz9ug
    @RonaldGama-gz9ug หลายเดือนก่อน

    Ndiye pano galu zanuwo akulemekeza malamulo ngati momwe mukuneneramo

  • @ChisomoPound
    @ChisomoPound หลายเดือนก่อน

    Komaso kod tikumuyamikila chilimba kut anali Muthu wabwino ndipo oganiza boo funso langa Lili APA kod chilima anaona chani Kwa usi ?

  • @AmusedDimSum-hd5yp
    @AmusedDimSum-hd5yp หลายเดือนก่อน

    how did you know that those who were not happy were utm members of the pary banzi mwadyayo musasokoneze zinthu

  • @PreciousKARINGANIZA
    @PreciousKARINGANIZA หลายเดือนก่อน

    Anampereka zake chifukwa chofuna mpando

  • @Shire9627
    @Shire9627 หลายเดือนก่อน

    Malawians timadana ndi chilungamo🤣🤣🤣

  • @MayiSwale
    @MayiSwale หลายเดือนก่อน

    Chanzeru ndi chani??? Zaziiii

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera หลายเดือนก่อน

    Malamulowo anaphwanya kake akadangopitiriza panafutsa kale masiku 10 asadasakhe

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp หลายเดือนก่อน

    Sachamba

  • @janemsiska3345
    @janemsiska3345 หลายเดือนก่อน

    Mukwonago video yatsiku amalengeza maliro manganese amasekelera

  • @RonaldGama-gz9ug
    @RonaldGama-gz9ug หลายเดือนก่อน

    Eya akuyenera kutenga komweko ndi chifukwa chofuna kuwapusitsa

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e หลายเดือนก่อน

    Utsi nd wa mcp inu a utm mukapusa mugulitsa chipan😮

  • @NefassiNefitarZaqueioZaqueio
    @NefassiNefitarZaqueioZaqueio หลายเดือนก่อน +1

    Kutukwana kwanu kwanveka dziko lonse mulungu walola kuti mutukwane koma mudzayankha mwapadera .Dziyanganileni nokha onyoza inu.

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 หลายเดือนก่อน

    Inuyoso nanu aaàa manganyayu anapha nawo Chilima galu wamunthu uyu kakuwoneka mumask ka manganyaka kanachenjela udyo