ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Azatipase mtendele ndi yesu yekha amene samasitha ngati munthu komanso sakhumudwisa Amen
MCP singasithe ndiyamagazi bas akufuna asataniki awo
bon 😊 i lov this man
Tiyenazon bg agaluwa atitopesa
Umakwana Kalindo
Mulindi nkhawa mutha munthu wazeru akaona Kuti ukubkwaipa amachoka okha welcome everyone to MCP boma ndilomweli
Zipani zaku mabanja zimenezo ndiye mukuonakuti angachite chani Mary chilima angotaya nthu anamuvotera ndindani masewera eti utsogoleri sukusika Mbale pabanjatu ai Koma dziko.Ndiye mukamati Mary chilima mukuona Ngati bank mkhonde dzikoli
❤❤❤ the ddccc❤❤❤
Amene mukunena kalindo ndiwe opusa kalindo amanena zowona .
Ati agula Dan luu 500 milion,chikhariren athu akudya chitezi mm
You see ndeakuyembekedzera kuti Mulungu akhale chete never
Marry chilima abweleso ndi boza la mamuna wake
Ananena Chakwera yekha ku conversation kuti mutsogoleri wogula anthu ndikuti utsogoleri mulibe ndichizete
Kalindo alibe chipan palibe ku zionesa kuti ndi wa dpp galu iwe
Kd or atamugula Danyo Daniyo ndi Mulungu ndamene atapangise kuti chakwela awineso chakwera akuchokatu pampando or atagula oyimba onse zikomo koma chakwera akumuchosa pampando ndi Mulungu osadera khawa
MCP ndi ma vampire 👹👺🦀🦞🐦🔥🐞
Kalindo wazionesa kut ndwe wa dpp
Dan Lu akukayimba zokupha chilima
Komanso ndalama ndi tsatana basi.a dan lu mpaka kulowa mcp😢😢komano adzavotera adad mopandanso kukayikira
The Dc 😊
iiiiii mcp ndilibe nawo mau
Azilima Ku mpoto bwanji sitidya chitedze
Winiko kkkk umphawi wavuta kwambiri
❤❤❤❤❤❤
Mkuchedwa ndzimenezo akalindo
Akalindo zilakhula zanu sizomanga or athu ena amakhalila kukuombelani m'manja koma zolakhula zanu ndizokhuza khondo wy?
Dan lu ndi ndani so mu ndale achoke kumene
Ngati ndichoncho zilibwinotu kt a mcp akachite manyazi akaone anthu mene akazazile ku nsonkhano wa dpp
Iwe ndiye wakamba iwe Malonda ndim'aso kumeneko MCP ingotumiza Wana chakwera sapita wakula ndipamene mudziwe Kuti MCP bomaaa ndilomweli gotani chimwendo oladi Musa akwana tambala Ali ndimoto pamutu wina akalira tiyeni konko tikakhomana DPP imadelera muona Ngati muliku mulanje kayiyambeni mudzadutsa Kuti simu Lilongwe tithana mukuchepela nyawu zathu konzekani tinyape alomwe pobwela kumeneko a police pumani tiombane Kaye apa
Kod ndwe was dpp
Nthawi yonseyi ngat mumadziwa kut Dan lu anamugula, munkalekeranji kunena asanalengeze kut walowa MCP? Ndie chifukwa chakuti lero walengeza yekha kut walowa MCP ndie muzikati aaa ai amugula! Aaa ndinunachitsiru. Ndipo zomwe mukuyankhula apazi ndizopanda nzeru, mesa a DPP-wo ndiamene akumayambitsa nsankho kumanena kut MCP isadzapiteso ku kumwera, zomwe a DPP-wo amayankhula ku phalombe zija, bwanj osadzudzula zimenezijazi ukukanena za MCP? Kod basi umafuna kuyambanitsa anthu dziko muno chifukwa chot ndiwe mulomwe wakumwera? Activi wanji okhala ndi mbali chonsecho umati siwe wandale? Mmutu mopanda nzerumo, anakuuza kut Mery Chilima amafuna u president ndindani? Simupindula kanthu baba ndipo muphulika 😅😅😅😅😅😂😂😂
Mcp ndalama zomwe Ali nazo ndi zogulira Anthu basi
Koma zodabwitsa kut mukupanga izi ndinu alomwe okhaokha bwanji chikukuwawani ndichani asiyeni azani apange mbali yawo kupusa basi kuzikonda
Kod wabwino ndiuti
Zoona zake zit
Akalindo ndinu openga inu dan Luu sanalakwitse azikayimbila chinkhalamba chija nindani wazelu angayime kukavotela fundudwa ngati imene ija
Nawe mutu mwakomo uli misala
Dani lu ndindani kape malawi wafika poyipa
Pantumbo pako ndi chikangawa wakoyo panyini pamako
Bambo Akonso Ndpo akavotero DPP iweyo ndkupusa kwakoko khala choncho
mmulibe agogo kod 😂
Mwakangalika ndikupanga zaziko lapasi,soka Kwa iye wobwelesa chokhumudwisa
Azatipase mtendele ndi yesu yekha amene samasitha ngati munthu komanso sakhumudwisa Amen
MCP singasithe ndiyamagazi bas akufuna asataniki awo
bon 😊 i lov this man
Tiyenazon bg agaluwa atitopesa
Umakwana Kalindo
Mulindi nkhawa mutha munthu wazeru akaona Kuti ukubkwaipa amachoka okha welcome everyone to MCP boma ndilomweli
Zipani zaku mabanja zimenezo ndiye mukuonakuti angachite chani Mary chilima angotaya nthu anamuvotera ndindani masewera eti utsogoleri sukusika Mbale pabanjatu ai Koma dziko.Ndiye mukamati Mary chilima mukuona Ngati bank mkhonde dzikoli
❤❤❤ the ddccc❤❤❤
Amene mukunena kalindo ndiwe opusa kalindo amanena zowona .
Ati agula Dan luu 500 milion,chikhariren athu akudya chitezi mm
You see ndeakuyembekedzera kuti Mulungu akhale chete never
Marry chilima abweleso ndi boza la mamuna wake
Ananena Chakwera yekha ku conversation kuti mutsogoleri wogula anthu ndikuti utsogoleri mulibe ndichizete
Kalindo alibe chipan palibe ku zionesa kuti ndi wa dpp galu iwe
Kd or atamugula Danyo Daniyo ndi Mulungu ndamene atapangise kuti chakwela awineso chakwera akuchokatu pampando or atagula oyimba onse zikomo koma chakwera akumuchosa pampando ndi Mulungu osadera khawa
MCP ndi ma vampire 👹👺🦀🦞🐦🔥🐞
Kalindo wazionesa kut ndwe wa dpp
Dan Lu akukayimba zokupha chilima
Komanso ndalama ndi tsatana basi.a dan lu mpaka kulowa mcp😢😢komano adzavotera adad mopandanso kukayikira
The Dc 😊
iiiiii mcp ndilibe nawo mau
Azilima Ku mpoto bwanji sitidya chitedze
Winiko kkkk umphawi wavuta kwambiri
❤❤❤❤❤❤
Mkuchedwa ndzimenezo akalindo
Akalindo zilakhula zanu sizomanga or athu ena amakhalila kukuombelani m'manja koma zolakhula zanu ndizokhuza khondo wy?
Dan lu ndi ndani so mu ndale achoke kumene
Ngati ndichoncho zilibwinotu kt a mcp akachite manyazi akaone anthu mene akazazile ku nsonkhano wa dpp
Iwe ndiye wakamba iwe Malonda ndim'aso kumeneko MCP ingotumiza Wana chakwera sapita wakula ndipamene mudziwe Kuti MCP bomaaa ndilomweli gotani chimwendo oladi Musa akwana tambala Ali ndimoto pamutu wina akalira tiyeni konko tikakhomana DPP imadelera muona Ngati muliku mulanje kayiyambeni mudzadutsa Kuti simu Lilongwe tithana mukuchepela nyawu zathu konzekani tinyape alomwe pobwela kumeneko a police pumani tiombane Kaye apa
Kod ndwe was dpp
Nthawi yonseyi ngat mumadziwa kut Dan lu anamugula, munkalekeranji kunena asanalengeze kut walowa MCP? Ndie chifukwa chakuti lero walengeza yekha kut walowa MCP ndie muzikati aaa ai amugula! Aaa ndinunachitsiru. Ndipo zomwe mukuyankhula apazi ndizopanda nzeru, mesa a DPP-wo ndiamene akumayambitsa nsankho kumanena kut MCP isadzapiteso ku kumwera, zomwe a DPP-wo amayankhula ku phalombe zija, bwanj osadzudzula zimenezijazi ukukanena za MCP? Kod basi umafuna kuyambanitsa anthu dziko muno chifukwa chot ndiwe mulomwe wakumwera? Activi wanji okhala ndi mbali chonsecho umati siwe wandale? Mmutu mopanda nzerumo, anakuuza kut Mery Chilima amafuna u president ndindani? Simupindula kanthu baba ndipo muphulika 😅😅😅😅😅😂😂😂
Mcp ndalama zomwe Ali nazo ndi zogulira Anthu basi
Koma zodabwitsa kut mukupanga izi ndinu alomwe okhaokha bwanji chikukuwawani ndichani asiyeni azani apange mbali yawo kupusa basi kuzikonda
Kod wabwino ndiuti
Zoona zake zit
Akalindo ndinu openga inu dan Luu sanalakwitse azikayimbila chinkhalamba chija nindani wazelu angayime kukavotela fundudwa ngati imene ija
Nawe mutu mwakomo uli misala
Dani lu ndindani kape malawi wafika poyipa
Pantumbo pako ndi chikangawa wakoyo panyini pamako
Bambo Akonso Ndpo akavotero DPP iweyo ndkupusa kwakoko khala choncho
mmulibe agogo kod 😂
Mwakangalika ndikupanga zaziko lapasi,soka Kwa iye wobwelesa chokhumudwisa