ZOMWE ZACHITIKA KU MALAWI

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 28 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 20

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 2 หลายเดือนก่อน +3

    Penapake gayz mulungu timamulakwila izi vuto nditokha Malawi achina kalindo akhazula kuchikamwa paka kutopa so don't blame god please 😢😢😢😢😢😢😢

    • @KingDavedNkhata
      @KingDavedNkhata 2 หลายเดือนก่อน

      Mulungu izizi zoziyanba dalazi Koma akulu akulu tiyeni Pena tizikhala serious
      Anthu ambiri alankhyladi ndikutopa kunikira ndikutopa nsiyeni Mulungu

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 2 หลายเดือนก่อน

    Lack of philanthropy and genuine patriotism in Malawi has brainwashed divers leaders into thinking in very negative and limited terms.

  • @Blessings-b7h
    @Blessings-b7h 2 หลายเดือนก่อน

    Mbaleme iwe wabodza nanga mchifukwa chiyani anthu mukungomanga?

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo6251 2 หลายเดือนก่อน +1

    We are cursed as a nation

  • @AlickjoiceMatchipisa
    @AlickjoiceMatchipisa 2 หลายเดือนก่อน

    Gwetsaso kwacha

  • @Blessings-b7h
    @Blessings-b7h 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkk pamenepo ndipamene mungadziwe kuti mcp onse ndi anthu oononga ndipo kulibe Utsogoleri.

  • @MabvutoSembo
    @MabvutoSembo 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mulungu atithandize

  • @JasonMailos
    @JasonMailos 2 หลายเดือนก่อน

    AAA mavito ku Malawi ochita kwakozawo

  • @AndrewjemesJemes
    @AndrewjemesJemes 2 หลายเดือนก่อน

    IMF must go

  • @YaqoobStandwell
    @YaqoobStandwell 2 หลายเดือนก่อน

    Kunkuyu ndiye palibe zomwe amayankhula bas oyankhulana zake zomunyengelela chakwela kut aziwoneka kut ali mbali yake kubisa chilungamo kut ziko lamalawi bwana sili kuyenda bwino bas kumangokwakopa ndimaboza alibe zelu kunkuyu

  • @josephgabriel5941
    @josephgabriel5941 2 หลายเดือนก่อน +1

    After mutamwanza ndalama zankhaninkhani....

  • @yotamumahomed1313
    @yotamumahomed1313 2 หลายเดือนก่อน

    Guys tiyeni tidzuke mwa mphamvu coz izizi zitiwonongera Malawi wanthu

  • @RobertGalatiya
    @RobertGalatiya 2 หลายเดือนก่อน +1

    Tsogolo logwetsaso kwacha layamba kunukhila a Malawi tili pamavuto akulu

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 หลายเดือนก่อน +1

    We are not crc as country 😭

  • @onesterabayo1871
    @onesterabayo1871 2 หลายเดือนก่อน

    Corrupt minister

  • @MussaZakeyu
    @MussaZakeyu 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mulungu atithandiza