ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Penapake gayz mulungu timamulakwila izi vuto nditokha Malawi achina kalindo akhazula kuchikamwa paka kutopa so don't blame god please 😢😢😢😢😢😢😢
Mulungu izizi zoziyanba dalazi Koma akulu akulu tiyeni Pena tizikhala serious Anthu ambiri alankhyladi ndikutopa kunikira ndikutopa nsiyeni Mulungu
Lack of philanthropy and genuine patriotism in Malawi has brainwashed divers leaders into thinking in very negative and limited terms.
Mbaleme iwe wabodza nanga mchifukwa chiyani anthu mukungomanga?
We are cursed as a nation
Gwetsaso kwacha
Kkkkkk pamenepo ndipamene mungadziwe kuti mcp onse ndi anthu oononga ndipo kulibe Utsogoleri.
Mulungu atithandize
AAA mavito ku Malawi ochita kwakozawo
IMF must go
Kunkuyu ndiye palibe zomwe amayankhula bas oyankhulana zake zomunyengelela chakwela kut aziwoneka kut ali mbali yake kubisa chilungamo kut ziko lamalawi bwana sili kuyenda bwino bas kumangokwakopa ndimaboza alibe zelu kunkuyu
After mutamwanza ndalama zankhaninkhani....
Guys tiyeni tidzuke mwa mphamvu coz izizi zitiwonongera Malawi wanthu
Dzuka wekha iweyo zitilipirira fee Ana zimenezo
Tsogolo logwetsaso kwacha layamba kunukhila a Malawi tili pamavuto akulu
We are not crc as country 😭
Corrupt minister
Mulungu atithandiza
Penapake gayz mulungu timamulakwila izi vuto nditokha Malawi achina kalindo akhazula kuchikamwa paka kutopa so don't blame god please 😢😢😢😢😢😢😢
Mulungu izizi zoziyanba dalazi Koma akulu akulu tiyeni Pena tizikhala serious
Anthu ambiri alankhyladi ndikutopa kunikira ndikutopa nsiyeni Mulungu
Lack of philanthropy and genuine patriotism in Malawi has brainwashed divers leaders into thinking in very negative and limited terms.
Mbaleme iwe wabodza nanga mchifukwa chiyani anthu mukungomanga?
We are cursed as a nation
Gwetsaso kwacha
Kkkkkk pamenepo ndipamene mungadziwe kuti mcp onse ndi anthu oononga ndipo kulibe Utsogoleri.
Mulungu atithandize
AAA mavito ku Malawi ochita kwakozawo
IMF must go
Kunkuyu ndiye palibe zomwe amayankhula bas oyankhulana zake zomunyengelela chakwela kut aziwoneka kut ali mbali yake kubisa chilungamo kut ziko lamalawi bwana sili kuyenda bwino bas kumangokwakopa ndimaboza alibe zelu kunkuyu
After mutamwanza ndalama zankhaninkhani....
Guys tiyeni tidzuke mwa mphamvu coz izizi zitiwonongera Malawi wanthu
Dzuka wekha iweyo zitilipirira fee Ana zimenezo
Tsogolo logwetsaso kwacha layamba kunukhila a Malawi tili pamavuto akulu
We are not crc as country 😭
Corrupt minister
Mulungu atithandiza