Ena ananyoza Mulungu ku Los Angeles posachedwapa ku LA Palasede, few hours later kunabuka moto oopsa.....I hope mwapanga follow. Guys tikakhuta ndibwino tizingodikira kugeya koma osati kuyambana ndi Mulungu
dzina lake ndi yehova sasitha, ndiyemweyo dzulo, lero mawa tiyeni timulemekeze mulungu chifukwa ndamene analora kuti iwe ndi ine tipezeke pano padziko lapansi
Powerful message
Almighty God is is only one and only powerful one ❤we worship God and the world creator is only God almty God super power is one and only one Ameen
History is the best teacher
Glory be to God
Mulungu ndi Mulungu ❤
Ena ananyoza Mulungu ku Los Angeles posachedwapa ku LA Palasede, few hours later kunabuka moto oopsa.....I hope mwapanga follow. Guys tikakhuta ndibwino tizingodikira kugeya koma osati kuyambana ndi Mulungu
Good and educative content. God bless you for spreading HIS Greatness
Mulungu amafuna ulemu wake wake guys
God bless you brother ❤❤
Let God be God 🎉🎉
Good beginning keep it up bro 🙏
Tancro Neves adati
"Ngati ndingakwanise Ma votes 2000 even Mulungu sangandichonse pa mpando"
GOD IS OMNIPOTENT
God is power for everything
God is gud
Mulungu si Habakuku🙏
Mulungu sioseweresa timuope Mulungu
Ameneyo ndiye mulungu akamufunse hellode anasandukaka mphutsi mwa masekanzi inu mukuti mulungu saphamunthunu musamale adzakuwonetsani
Zinsisi nza Yehova
Zoona mulungu sAnyozeka
Your good guy
Mulungu safuna zachibwana
🙏 God
Don't play with God,
God for bit
Powerful
Jesus is a king
Osamaseweletsa Mulungu
👍👍👍
Zoona God can not be mocked
Mulungu siwosewera naye
Part 2 ifunika boss
Pharaoh ndigulu lake mmmm
Amen
mulungu alemekezeke lero mpaka muyaya
Muzivele nokha
Mulungu siwosewelesa
Mulungu sapha anthu achimwene,imakhala thawi
Inuyo munyozeni tione ngati muzidikirabe nthawi yakufa onani america ,zomwe waona .nanga last time ku Brazil kunachitika zotani atanyoza mulungu
God is the creator the owner
Mulungu ndi wamkuludi
Ok
Do not Mock God
History is the teacher ❤
And those who killed Jesus did not die kkkkk
God is powerful
Akafuse nebukadinezara nayeso anaziona
dzina lake ndi yehova sasitha, ndiyemweyo dzulo, lero mawa tiyeni timulemekeze mulungu chifukwa ndamene analora kuti iwe ndi ine tipezeke pano padziko lapansi
God is not James
Amen
Amen
Amen
Amen
Amen