Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting. Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
munthu amene amadana ndikalindo ndifiti kwambiri Kalindo amatiimirila ife amalawi
Kuyakhula mwatchutchu bon ❤
The DC mwana oopsaaa kwambiri gwilan ntchito boss
💔💔💔
Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting.
Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
Kuyankhura molikonda zdiko mowakonda a Malawi mulungu apitilize kupatani mphavu Komaso madalitso ochuluka
The dc ..mwana owopsa kwambiri 🤣🤣
Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
Munthu uyu amenyela nkhondo Malawi it's up to you Malawians kukhala mene mulili olo kutengapo step
Nkhaniyo ndiyowona
Mr pangolin tatulutsireni ndodo ija achinagwenembewa
❤❤❤❤ The DC nthawi zonse kuima pa chilungamo. Ndipo chilungamotu sichimawopsa stand with u all the time
I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi.
Powerful massenge fadah ❤❤
Chakwela ndi mbutuma yamunthu ndi gulu lake
Ndipo message ya apolice ndi iyi mukazagopezeka mukutenga bali ya chakwera uzazima sitikuchedza pa 10 ok we need change our Malawi 🇲🇼
❤❤❤❤❤ DC
Za ma hca zo ndee eeeeh zavuta zedi
Ulemu wanu Malume ❤
Panopa ine ndikupanga biziness koma profit ndiyaying'ono kwambiri. Mutu wanga wayima.
Oletsa zoyankhula zanu munthu wamkulu,ameneyo ndiye kuti ndi mfiti.mulungu akudalitseni bwana
Good Messnge my Bon Kalindo
Mashing opangila mashin anzake D. C NUFF RESPECT TO YOU MUMATIIMILIRA 💯💯💯
Umakwana
That's true Mr. D.C
Olo uyankhule mbwelera, timamukondabe The DC.
Anabwelatu pa shop yanga ndi nfuti akuti kuzatolela ndalamaya nsongo kkkk mpaka mfuti tiziwopa zomwezi?
Kalindo...The Great Man....winawe osangochoka bwanji
The Dc 👹👹👹👹
Boma lokuba kwambri
Nanga munthu oti anachita kukatengedwa ku Church angaziwe kulamulira dziko? Ndinkona amangolembana mbutuma zokha zokha
Mmakwana boss mn
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
Vuto lovotela mulimi ndi kupanga president ndi limenelo munthu wakukakasiya ndikukukhala president manthongo Ali tho azasukusula liti
Akuluwa akufuna kusochelesa anthu iwowa akudana ndikusakhara pa udindotu
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
The DC!!!!
Munthu wamkulu zedi, the DC
Good massage boss
Ife2 tikudikila ndodo ituluke
Yes!kodi izatuluka liti ndodo
Boma la anthu opusa ma savage
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
Nde nkhani zake
The DC chimwana cholimba mtima kwa osauka more 🔥🔥 Mr Kalindo Tell them😅😅
The DC mwana woooopsa kwambiri
Indeed it's bullshit a MRA the DC ayankhula
A opposition afasa ngati Chilima
Ndipo inu a China pharaoh amenewa Sali bwino mulungu wa Israel awayendele
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
The DC. Chimwana choopsa kwambiri ..ine buzines wanga anaduka kale kale.
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
The DC mwana olimba mtima
Assani,keti
Wi love you ❤❤ bon kalindo
Proud of DC
D c ❤️❤️❤️❤️❤️
Munthu ukuzitama wekha iwe ndiwe chitsiru chenchen
Iwetu akupasazo ukabweza
Chitsiru ndi wagule akulephela kuyendesa dzikoli, kwacha kumangogwa siku ndi siku
❤❤❤❤❤ great full story poor DC
Dangerous child ❤
The DC
Audio iyi yandikhudza kwambiri.
Morning the DC
❤❤❤ The Dc
Mwana owopsa kwambili
Akudziwana onsewatu
Powerful!!!!
Powerful 👊
Amalawi tiyeni tikhale maso osalola zimenezo zoonadi ndikuba poyera
Timakunyadiran bg
💪💪💪💪💪 Bon K
Timam'konda Dc,,,iwanawe ušamalimbane ndi Dc
Kod ma track ndi zida zoopya zomwe zinalowa m'muziko mwanthu zija zikuzatani! Kapena boma linagula zida zankhondo za M.D.F? Tatifufuzileni mr kalindo please! Otherwise chakwela atha kutigulisapo apa!!
🔥🔥🔥
Wenawe ngati wadya ndalama za eni tuluka usamanvele apa ife ndi bon ❤ wagwana nayo pita ukabweze ndalamazo cos apa walephela 😂😂😂😂😂😂
Amutuma kuti azasunzumile kuno Ha😅😅😅😅😅😂😂😂😂wanya nayo wadya ndalama zaulele
Ndipo Ine andikhomela pa shop akut ndisokhele 80
❤❤❤❤❤
D.C ukhalise umatiimilila kwambil
❤❤❤❤karido
Mcp boma lakuba kwambiri.
Auzeni chilungamu
❤❤
Nde mwati Yosefe anali wa number chani? Nanga Benjamin? Pilizi chonde!
Joseph wa 11 Benjamin 12 walakwitsa pati munthu
Anganga
📌
A DPP ADYA BANZI NDIIIIITHu!!?
The DC umakwans
Tingopita ku cort basi
Dc
Mumakwana kunena dzoona the dc
Ndili pambuyo pako bon kalindo the D.C
Rest in peace Redson Munlo 😢😢😢😢😢.
We love you the DC
Boni kalindo watha basi
Iwe usamalimakimbane ndi DC ukutaya thawi
I stopped listening to this nonsense frm coz I don't see any profit
Who told you to listen get out
Iwe ndiwe chitsulu osangatuka bwanji ndani akukukamiza kuti uzimvela zomwe akunena bon kalindo musiyeni akutokota za nzelu zothandiza ife iwe unalandila ndalama kuti uzifowola anthu choka galu
The DC
Timakunyadiran bg