Diso La Nzika - Kugulitsidwa kwa Msika wa Kamba mu mzinda wa Blantyre

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 8 ก.พ. 2025
  • #disolanzika#africa#malawi

ความคิดเห็น • 79

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 2 หลายเดือนก่อน +3

    Boma ngati liri ndi nzeru lisandutse msikawu shopping mall, awamangire anthuwa ma shop olongosoka ndi owoneka bwino, shopping mall ayipezere malo ena.
    Zimamvetsa chisoni ma vendor akupsa ndi dzuwa mmisewu koma amwenye ali ndi ufulu ndipo salola munthu kupanga malonda pakhonde la shop koma mukapita ku new york mukapenda ma vendor mma khonde a ma shop. Amalawi ndife ogona ndithu. Even ku Johannesburg boma linayika ma bench a ma vendor ndikuwapatsa malamulo.

  • @JamesMajamanda
    @JamesMajamanda หลายเดือนก่อน +1

    NZiko likutha ilii!!!!!!

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Kodi si iwe Malawi?

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Kutereko watenga ndalama kwa a mwenye

  • @martinkhozombah
    @martinkhozombah 2 หลายเดือนก่อน

    🎉Kudesa town ndizimasaka zanuzo, iyaaaa. BCC gulisan malowo

  • @EDGARMPIKAMEZO
    @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน +3

    Ine ndiri ndi maganizo Osiyana. A malawi tisiyanitse ufulu ndi chitukuko Cha dziko. Naperi it's part of urban, msika wa pa kamba sugwilizana ndi Area imene ija. Shopping mall ndi filling station ndi chitukuko chapamwamba. Pa kamba pamapindulira zidakwa, ma Hule ndi akuba. Kodi ma restaurant ake ati? Azimasakawo? Please a malawi tikamati Mizinda yathu itukuke ingatukuke bwanji?

    • @adamusaidih8570
      @adamusaidih8570 2 หลายเดือนก่อน

      Amwene mwangokula mulibe nzeru

    • @zayedmitawa8345
      @zayedmitawa8345 2 หลายเดือนก่อน

      Chitukuko sitibisa,momveka bwino anthuwa akuti nthawi yosamuka ikuchepa komanso kosamukira sanauzidwe.
      Zomanga shopping zilibe umboni ndimphekesera chabe.
      Udzifunse Mchifukwa chiani BCC siikulankhura zomveka pa izi?

    • @EDGARMPIKAMEZO
      @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน +1

      @@adamusaidih8570 anzeru ndinu komano ndingokupemphani muziyenda. Mu township simumakhala ma restaurant azisaka. Opanda mzeru ndi iwe ukufuna kumayala makala mu mkati mwa mzinda. Kumasuntha ndi dziko amwene.

    • @EDGARMPIKAMEZO
      @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน

      @@zayedmitawa8345 point ikhale yoti palibe njira yonveka bwino pa za relocation kapena compensation. Koma Malo Aja patha kuchitika Cha mzeru kuposa mmene palili panomo

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Iwe wa city council ndi galu

  • @AlexNjovu-j4z
    @AlexNjovu-j4z หลายเดือนก่อน

    Kodi mukuti amphawife titani?tilowerekuti?

  • @MikeSangano-b6x
    @MikeSangano-b6x 2 หลายเดือนก่อน

    The most important thing in life is human welfare. Mukati achoke ma vendor Mali atagulutsidwa it means sangabwererenso pamenepo coz pagulitsidwa. Amalawi tiyeni tidzikondana tokhatokha,Moyo pano walimba, ntchito kulembedwa sizikutheka pomwe katundu akukwera mtengo daily salary yomweija. Munthu uli ndi family penanso kumasamala makolo,achibale plus amasiye,ndiyeno akuthamangise pa malo a business zitha bwanji? Chitukuko cha filling station sichingasamale banja lako komanso zosowa zamunthu. Ngati kuli kotero,amange kaye msika wabwino woti mavenda apa Kamba asamukiremo pomwe akuyamba kumanga zama filling station zawozi. Boma lonyasa ngati ili sindinalionepo chibwadwireni. 2025 ilimukhonde,muzawafuna mukuwanzunzawa.God is watching you!!

  • @GodfreyWhayo-hh1dm
    @GodfreyWhayo-hh1dm หลายเดือนก่อน

    Tidapatsidwa ufulu odandaula ngati sitikukondweretsedwa ndi mmene mfundo Zina zikuyendera pakaendetsedwe ka dziko Koma tidziyamba taona mbali zonse .

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 2 หลายเดือนก่อน +1

    Accept development

  • @EDGARMPIKAMEZO
    @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน +2

    Pa kamba patafika shopping mall, ma modern restaurants ndi filling station. Patha kupezeka mwai wa mbiri wa ntchito kwa a Malawi ambiri kuposa omwe akupeza phindu pano. Maganizo anga

    • @SliviaJosephy
      @SliviaJosephy 2 หลายเดือนก่อน

      Inu ntchito amalembana okhaohka mutsavutike kuti anthu akhodza kugwira ntchito

    • @EDGARMPIKAMEZO
      @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน

      @Slivia Awiri atatu amapezeka abale athu

    • @zayedmitawa8345
      @zayedmitawa8345 2 หลายเดือนก่อน

      Maganizo a shopping mall ndi abwino koma pali vuto mpoti BCC siikutsindika zomanga shopping mall komanso siikufuna kukambilana ndiochita malonda munsikao.

    • @AlexNjovu-j4z
      @AlexNjovu-j4z หลายเดือนก่อน

      Think about poor people

    • @EDGARMPIKAMEZO
      @EDGARMPIKAMEZO หลายเดือนก่อน

      @AlexNjovu-j4z come out of that mentality. Those poor will get employed. We should not put it that some are poor, rather all of us we deserve better living. All we need is to force our government to set proper measures on business policies between locals and foreigners. We need not to pay equal tax on equal business with foreigners.

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf 2 หลายเดือนก่อน +2

    Abale athuwa sakudana ndi chitukuko, koma dandaulo limveke. Nthawi ili yachabe. Apatseni 5 years notice kudzanso alternatives.

    • @Crysis25
      @Crysis25 2 หลายเดือนก่อน

      @@lastonmasoatenganji-bs5gf 😅😅😅malo ndi a khonsolo not awo..chikuvutani kumvetsetsa ndi chan kod?? . Umunthu ukatichulukila sittitukukapo apa

  • @JosephyKambalu
    @JosephyKambalu 2 หลายเดือนก่อน

    Msika is under district council not government. School ijaso pena imathandiza kudziwa omudandaulila.

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Zonsezi ndi chimwendo Banda. Ndi woipa kwambili

  • @SalatiKiddie
    @SalatiKiddie 2 หลายเดือนก่อน +2

    Osatopa osawopa osafoeoka

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Usi ndi galu

  • @Crysis25
    @Crysis25 2 หลายเดือนก่อน +1

    Thats wat we call development...pena timakakamila zopanda tsogolo

    • @zayedmitawa8345
      @zayedmitawa8345 2 หลายเดือนก่อน

      Development sabisa.Kuwafotokozera anthu momveka bwino zimachepetsa mikwiyo.
      Zikuoneka kuti malowa agulitsidwa pa zifukwa Zina osati kumanga shopping mall.

    • @Crysis25
      @Crysis25 2 หลายเดือนก่อน

      @zayed munakamva zomwe ceo wa bt anayankhila b4 kutiyankha

  • @cvali2653
    @cvali2653 2 หลายเดือนก่อน +1

    To be honest ,nsika uwuwu sumapanga ndalama ndipo kuikapo shopping mall and filling station zithandiza kwambiri,this area anthu omwe amabwera apa ndiozadya ndikumwa mowa

    • @zayedmitawa8345
      @zayedmitawa8345 2 หลายเดือนก่อน

      Kodi shopping mall ndi filling station zimathandiza ndani?
      Msikau ulipo mpaka pano chifukwa umathandiza anthu ozungulira.
      Council ya Blantyre yagulitsa malowa pa zifukwa zina.
      Chitukuko siukambila kuseri

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Munthuyi ndi oipa kwambili akukonda makobili kwambili

  • @SamuelKhumbiwa
    @SamuelKhumbiwa 2 หลายเดือนก่อน

    Khani yomanga mnsika pliz ndiyofunuka,ma new models akufunika kt mzinda .ndi ma toun zizioneka bwino.kma pakufunika ndondomeko kt anthu ali mmenemu apasidwe Malo ena ,kupanda kutero simunthana nawo chifkwa ndi m'badwa ndi mzika zamalo ao.nthaka ya amalawi ndiya wo kma ulemu ndi ndondomeko zikhalepo.

  • @ENOKMAKONDI
    @ENOKMAKONDI 2 หลายเดือนก่อน

    This action is encouraging kuti anthu azilowa ndi Malonda nkati mwa town apezeka kuti akukagulisa Malonda pa nandos kandodo etc kenako a city azitengaso galimoto kumakalanda Malonda omweyo kumakadya makwawo are you trying to kill poor malawians

  • @JamesKalasa-s6s
    @JamesKalasa-s6s หลายเดือนก่อน

    Blantyre ikufunika ma building abwino,chokani kasakeni kwina malo amange zooneka

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 2 หลายเดือนก่อน

    Koma Council posakhala transparent pa nkhani ngati iyi nchiani?
    Ngatidi akufuna kumanga shopping mall mwai umapelekedwa Kwa nzika kukhala ndi mashop awo mkatimo ndipo iyi ndi nkhani yabwino.
    Koma ngati kuli kupha Kwa nsikawu at least apange relocate ma vendors apititse kwina kudzera mkufotokozerana.
    Apa a council plus Boma akubisala mawa adzayambe kugwiritsa ntchito a police kuthamangitsa anthu ndi teargas.
    Mchifukwa ninji boma la Malawi silikhala ndi chidwi ndi nzika zake.Mzika zimaesetsa kuzipezera zokha zochita zomwe Boma limapindula nazo misonkho koma boma lomwero likafuna chinthu pa anthuwa limagwiritsa ntchito mphanvu osati kukambilana.
    This nonsense must stop.
    Wakawaka in Lilongwe, you're next!!!!

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Iwe wa bcc ndiwe chitsilu ndipo galu

  • @chesterdimba0209
    @chesterdimba0209 2 หลายเดือนก่อน

    The govt should be non profit business allow its citizens to conduct business

  • @Maxielyies
    @Maxielyies 2 หลายเดือนก่อน

    Ma senior a Blantyre city council ndi makape akatero apeza mwenye kuti amugulitse

  • @ChrissieMakombe
    @ChrissieMakombe หลายเดือนก่อน

    Kulakwa anthu azipanga chani asachoke

  • @MemoryMsuku-ex9pt
    @MemoryMsuku-ex9pt หลายเดือนก่อน

    Inu fatsani ngati kuli kukuchotsani akupangirani ndondomeko yabwino . Musachuluke nzeru . Dziko lizioneka bwino

  • @chancyblack6384
    @chancyblack6384 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ayi tikufuna chitukuko amangebas akupasani pena

  • @RaheemNgoma-pk1ev
    @RaheemNgoma-pk1ev 2 หลายเดือนก่อน +1

    Osachoka ndipo osaopa

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Chakwera asakuzunzeni ayi

  • @YusufuKaifa-r2y
    @YusufuKaifa-r2y 2 หลายเดือนก่อน +1

    Osachoka akamange kwawo kwa zimayi awo zachibwana

  • @AngellahKaukonde-z7l
    @AngellahKaukonde-z7l 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo asachoke nsika umene uja umathandiza Maka ukakhala ku chipatala kuja

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 2 หลายเดือนก่อน +2

    MCP kubesa mavoti....

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 2 หลายเดือนก่อน +1

      Amwenye ali ndi malo opangira malonda mwa ufulu, ayini ake adziko akupsa ndi dzuwa mmbali mwa misewu, amalawi ndife ogona.

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 2 หลายเดือนก่อน +1

    Shopping Mall basi .pitani ku mukakhala kwa Manje inu basi

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 หลายเดือนก่อน

    INU CHITUKUKO CHA CHIYANI BOMA ILIRI NDI LAKUBA LIKUKONDA KILANDA MALO NDIYE NGATI SINUSAMALA IZIZI ZIKUVUTANI ANTHU AKWAKAMBA MYSAVONEREZE AYI A CITY NAWONSO MUWAKUNTHE ZIMENEZO MUWAUZE AZIKAPANGA KU LILONGWE KWAOKO OSATI BLANTYRE ASATIONE KUPUSA OSACHIMA AKAFUNA NDEU IBADWE ZAUTSIRU INU AMENE MUKUIKIRA KUMBUYO KUTI MUKUFUNA CHITUKUKO BOMA LIKUKANIKA KUKUGULIRANI FETLIZER MAFUTA KUDOWA NDIYE MUKUONA NGATI ANGAMANGE NSIKA WA KAMBA? BOMA ILI NDI LAMANYI KUTEROKO ALIPO AMENE AKUFUNA KUGULA MALOWO WAMBOMA MUNDIKHULUPIRIRA

  • @BakhePaliso-h8h
    @BakhePaliso-h8h 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mmmmm komano anthu akuchipatala azizagula kut zinthu zawo

  • @SamuelKhumbiwa
    @SamuelKhumbiwa 2 หลายเดือนก่อน

    Khani iyi ndiyosekesa kalata yopanda siginecha so why?ndichifkwa chani sanasayinile umeneo ndiye utambwali,Blantyre city ilipo chifukwa Cha wanthu ,popanda wanthu city kulibe,Inu acity musamalakhule kt Malo ndi anu ,munawatenga kt?

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Iwe chimwendo wasala pang'ono kuphwa

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 2 หลายเดือนก่อน

    Musalore akufuna musowe zochita anthu oipa awa, kongeresi iyo ikufuna anthu aku Blantyre avutike

  • @TonykalicheloKalichelo
    @TonykalicheloKalichelo 2 หลายเดือนก่อน

    Abale athu kozekan bs boma ili siligonjatu paja azabwera usiku kuzachosa zimenezo

  • @ThaboyEst
    @ThaboyEst 2 หลายเดือนก่อน

    Inde chokani pabwere town pachuluka afiti kwa kamba kkkk achokepo basi

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3di 2 หลายเดือนก่อน

    Chipani cha mcp sichisamalila osauka as a lankhule mozembazemba apa tilongosola zonse 2025 kovota muziwona

  • @MikeKameta
    @MikeKameta 2 หลายเดือนก่อน

    Ati wagula ndi faizo matama basi ndi ndalama

  • @RencoMandah-vd2yp
    @RencoMandah-vd2yp 2 หลายเดือนก่อน

    Osamangakaye wenela bus deport bwanji instead kumalimbana ndi misika yamuma location

  • @JamJam-n4k
    @JamJam-n4k หลายเดือนก่อน

    Kuthana kuthana basi

  • @AmbiaTrust
    @AmbiaTrust 2 หลายเดือนก่อน

    Chokanu panenepo malondi abima akupatsan chipepeso

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Anthunu musalole zopusazo

  • @KampilaAllie
    @KampilaAllie 2 หลายเดือนก่อน +1

    Chilungamo ndichofunika kuwaudza anthu mcp why your doing this to Malawians

  • @faithkamlongera5128
    @faithkamlongera5128 2 หลายเดือนก่อน

    Koma tiyeni tlikinde dziko akamanga shopping Mall paonekabwino tauni idzisintha matemba tidzikagulabe kuseli kwa shopping Mall,, pano pa queens hospital padadzadza ma hawker palibenso amapita kwa kamba kukagula zinthu

    • @zayedmitawa8345
      @zayedmitawa8345 2 หลายเดือนก่อน

      Sakufuna kumanga shopping mall nchake anthuwa akuti sachoka.
      Malowa Council yagulitsa pazifukwa zina.
      Council iyenera ipeze malo kwina ikaike anthuwa

  • @YowelichipapaYowelichipapa
    @YowelichipapaYowelichipapa หลายเดือนก่อน

    Kutha kwa 60yeas aste caso anali kuti? kuti athu awauze kuti achoke zaka zino

  • @MikeKameta
    @MikeKameta 2 หลายเดือนก่อน

    Komatu

  • @valentinokaundama7902
    @valentinokaundama7902 2 หลายเดือนก่อน +1

    Koma if its redevelopment and malowo si amunthu, i dont see any problem, we need standard things, enawo akhoza kukayala panyumba pawo, or apeze pena akayambise okha

  • @KampilaAllie
    @KampilaAllie 2 หลายเดือนก่อน +1

    Funso mkumati kuyambila litiro kuona malowo ndi akulu ? This government its too much corruption ndeno akagulitsa malowo what is your benefit you will get ?

  • @EDGARMPIKAMEZO
    @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน

    Abale a Malawi anzanga ngati timafuna dziko lathu kutukuka ngati Maiko ena, tidzakwanitsa bwanji kutero ngati pano tikukana shopping mall mu urban? Kaya akumanga ndi a Mwenye kaya ndani koma tidziwe kuti zikumangidwa mu dziko lathu, ndipo olembedwa ntchito pamenepo ndi abale athunso

    • @ChikaNation-g8j
      @ChikaNation-g8j 2 หลายเดือนก่อน +1

      Kuchoka ndizotheka kma situation ku Malawi sikuli bho powachotsa pamafunika ndondomeko yoyenela at least kuwapititsa malo ena

    • @EDGARMPIKAMEZO
      @EDGARMPIKAMEZO 2 หลายเดือนก่อน

      @@ChikaNation-g8j ndizoona

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani 2 หลายเดือนก่อน

      Ma comment onse iweyo wabaya osat nzeru zozaza soda mutu​@@ChikaNation-g8j

  • @ChrisyMbewe
    @ChrisyMbewe หลายเดือนก่อน

    Ndipo.musachokedi.khaza.bas

  • @LonexWataya
    @LonexWataya หลายเดือนก่อน

    Anthunu gwirizanani musachoke

  • @KampilaAllie
    @KampilaAllie 2 หลายเดือนก่อน

    Chilungamo ndichofunika kuwaudza anthu mcp why your doing this to Malawians