Kumalawi tilibe omenyela ufulu waanthu ayi, tili ndi ma hippocrates basi anthira kuwiri monga redson munlo, timosi mtambo, ben longwe , gift trampez, just mention a few, ndikutyipa maina awo ndi ma small letters coz dey don't deserve our respect
koma yemwe anganyodze kalindo kuti siomenyera Ufulu.ameneyo ndi mfiti komaso ndi mdani wa kalindo ...Why I'm saying that. kalindo wamangidwa 15 times mu ulamuliro wa ch mcp.
Kumalawi tilibe omenyela ufulu waanthu ayi, tili ndi ma hippocrates basi anthira kuwiri monga redson munlo, timosi mtambo, ben longwe , gift trampez, just mention a few, ndikutyipa maina awo ndi ma small letters coz dey don't deserve our respect
Boooni kalindo number one basi palibeso
Wamisala anaona nkhondo
Only BONI KALINDO ndiye amayimila amalawi basi
Bon kalindo is the only true and trusted activist in Malawi and not manyaka ngati awawa
Peter Muthalika called this group, a Terrorism group and now I come to my senses that it was true. A traitor shame on you Mtambo.
Kalindo ndiamene amamenyera ufulu amalawi mtambo amkangofuna udindo
I like Bon kalindoo the Bc bola naye asazasitheeee
KU MALAWI KULIBE OMENYERA UFULU🎉😂
Uyu ndiamene atiwonongera malawi kwambiri, munthu oipa uyu
Ntambo si mmalawi so we all knows about that bwanjiso Pano sakuzuzula MCP pantumbo pake ndithu
Ku Malawi kulibe omenyera ufulu amangofuni kuwonekera patsogoro ngati chilungamo kwinaku matumba awo akukhuta... Tamuoneni manganya anazachuka pa tikufelanji koma pano bwanji mmmmm
Chitsilu cha munthu Mtambo, galu wachabe chabe.
Bon kalindo ndi wa chipani dpp ndipo nthawi zonse amangokakamiza kuti chakwela atule pansi udindo. Kwa ife anthu timangomuthandiza kupeza zomwe akufuna basi
Inuyo amene mudzintcha omenyela ufulu mudzidziganizila nokha coz mukupweteketsa anthu
Kupusa basi kumakhala ngat omenyera ufulu koma ali achipani,antambowa nde ulemu unatheratu....anthu alibe nawo ntchito
😂 apa aa❤ atipanga tabwa basi 😂my Malawi 🎉 anafa.asala andale wokha.
Nice 👍 more more
Kalindo number one
Omenyela ufulu amalawi yemwe alipo kumalawi ndi boni kalindo basi palibenso wina kaya enanu mukuona bwanji
awa a HRDC amafuna zawo ziwayendere afiti.
Zilimo zakatanngale koma kuyankhula kwake sayankhula ngati kalindo amadana ndi achakwela chifukwa choti anawamana udindo koma awa ankapeleka ulemu kwa mtsogoleli
Mau mbale wanga ndimene inenso ndimaonera ndi kjmva
Amangofuna aziti namiza kutipepelesa amakhala akuzimenyela khondo okha athuwa
Bora mutambo sanalowe zipani Ngati kalindo anali wa DPP atuluka alowa UTM atuluka chisisi chake anawanama udindo sopano Kuti ndiwomenyera yoooo
Vuto chifukwa cha u mphawi,they always act pofuna kudzithandiza okha
Zoona
Ndikape ameneyo
koma yemwe anganyodze kalindo kuti siomenyera Ufulu.ameneyo ndi mfiti komaso ndi mdani wa kalindo ...Why I'm saying that. kalindo wamangidwa 15 times mu ulamuliro wa ch
mcp.
Ndipo zoona
Mtambo amapanga zasogolo lake basi
Ntambo wamisala
Mtambo watha ngat makatani😂😂😂 bolaso bon kalindo
Panyapako ufuna akunkhendani pantumbopo funsolakolo kafunse amako tchanel chakocholankulazozizila
Iwenso pa mtumbo Pa makoo pa Gazi
Bon kalindo ndi amene akumenyera ufulu a dpp chifukwa Ali ndi nkwiyo pot sanamusankhe unduna
😂😂😂mwayiwalakale kuti anachita kunena yekha kuti zimamuwawa coz adamanidwa udindo??😂😂
Munadya kageyeni
Mtambo chitsilu cha munthu
Tikukuonani
Useless people anthu oipa mxeuii
It's possible that he is still receiving his monthly salary who knows what this government is a joke
Amtambo anali wanthu imebyeead uffulu akabwela pamseu ananena zifujwa zomwe azipangila mademo not akalindo kunabwe bweta ngati agalu
You are too slow.