Zose izi ndi manganya ndi chikangawa chakwela ponyelela pa manganya ndi chakwela Mama kaliyati worry not mulungu aliko kumwamba Manganya ndichakwela ndi manyi aanthu alangika posachedwa apa UTM 🔥🔥🔥🔥🔥🔥moto moto🔥🔥🔥🔥🔥mutuluka mayi wanga
Cosiyasi & conscious are different. Can you try to read these before recording. I noted yesterday you were say mp is still investigating. It's malawi police (MP) en u need to say it in presentation even if it has been abbreviated 😢 in writing
Za bodza izi! Mai kaliyati Alibe foni pano mafoni awo Ali mmanja mwapolice, akupanga post ndi amene atenga maphone amai kaliyatiwo osati mai kaliyati wake up guys, akupitiliza kumupezera zinyau kt ampeze zifukwa nanga bwanji sakupanga VN kt timve mai awo amai kaliyatiwo. Manganya ndaamene akulemba izi ku Facebook kwa mai kaliyati satana manganya ndi gulu lake la chikangawa 😅😅😅
Akweni more fire more fire ❤❤❤ I love masten Monday mukupita ku nyumba
ambuye akudariseni mam ndipo ndikukupephererani kuti mukhare mwambuye akutetezeni pamene mkudutsa mnthawi zamayesero amen
Akweni what a courageous.woman you are ! Bravo.❤
May God see mai kaliati through and give her victory.
That's really mother's love, n your children will continue to fight n praying for you on the outside.
We pray for you mum
God will take care of you mama😍😍😍
My Strong woman with wisdom
Olo ndima ukulele bwanji kunja kumanga basi
God is watching from a distance
It is well
We need strong mom like u we are together with u ❤
We love you madam Patricia kaliat God be with you
Noble woman God protect you naba
Your courage even transform me we will win indeed
You can create a page and employ the manager ..
Yesoooooo mum we are 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
This party's vision was to work with the youths, n us the youth we are awake n ready to transform our country
God will take care for u Mama
Allah bless u akweni
Chipululu simofera, mulungu simunthu
Zose izi ndi manganya ndi chikangawa chakwela ponyelela pa manganya ndi chakwela
Mama kaliyati worry not mulungu aliko kumwamba
Manganya ndichakwela ndi manyi aanthu alangika posachedwa apa UTM 🔥🔥🔥🔥🔥🔥moto moto🔥🔥🔥🔥🔥mutuluka mayi wanga
God is there
Expect this to happen mom poti muyenda mapazi a SKC zomwe amaziona SKC muziona ndipo pamenepo nchiyambi chabe,but zabwino zili kuseri kwa lawi lawiko inuyo Mulungu ali nanu akumenyerani nkhondo Yehova anthuwo sakuziwa zoti alumenyerani campaign
Cosiyasi & conscious are different. Can you try to read these before recording. I noted yesterday you were say mp is still investigating. It's malawi police (MP) en u need to say it in presentation even if it has been abbreviated 😢 in writing
Osaopa .osafooka .osaopa..viva akweni
Amen
Be strong woman
Zingatheke bwanji kupanga Post zithu oti munthu analandidwa phone ndiye mukutiuza kuti akupanga post zinthu ndi apolice amene alindi phone yawowo. Amalawitu penapa munawoneka ngati mituyanu simagwila ntchito bwinobwino .nomwenu mumatiuzakuti analandidwa phone pano mukutiuza kuti akupanga post zinthu which is which
Iweyo ndiwabodza phon ayitenga kuti ukuwona ngati ose ndiopoyi aliposo anzelu akudziwa kt kunena bodza phon amalanda ofuna kuwaffuza apolcewo atiwuze
Be strong mama
The way I know this is the to the presidency
Akweni more fire moto kuto buuuuuuu❤
Nthawi zambiri mu ground ma players amalimbana ndi player yekhayo amene ali chiopsezo. Simukudziwa chimene mukulimbana nacho, ndinu mafana enieni
Mayi mwapanga history yanu muzizayankhula nsogolomo
Dziko lomwe lasowa usogoleri wochokera kwa Mulungu zimakhal choncho munthu sungasiye kutumikira Mulungu kenako kuyamba zadziko lapansi Mulungu tithandizeni Ambuye chonde
Za bodza izi! Mai kaliyati Alibe foni pano mafoni awo Ali mmanja mwapolice, akupanga post ndi amene atenga maphone amai kaliyatiwo osati mai kaliyati wake up guys, akupitiliza kumupezera zinyau kt ampeze zifukwa nanga bwanji sakupanga VN kt timve mai awo amai kaliyatiwo. Manganya ndaamene akulemba izi ku Facebook kwa mai kaliyati satana manganya ndi gulu lake la chikangawa 😅😅😅
Kunja kumaçha basi
Only God has the final say on this matter
Koma mesa akut awalanda ma 4n awo nde akulembera 4n yandani
Ndiwe waboza ukulemba ndiweyo munthu analandidwa phone azilemba bwanji uzipusisa ena
Izii ndiye zaziiiiiiiiiii makosana mwasowa zopanga post😂
Akweni akuyidziwa zofooka za mcp ,paja a mcp tu mitu yawo siyimagwira ntchito chilichonse amapanga ndi mkwiyo nkhanza that's why azikhalila yomweyo
❤❤❤❤❤
Mulungu akuthandizeni mama
Gys andale amsmanga mzandale izi
Chemwali mulungu akuyang'anireni
Ndiye zikutheka bwanji poti maphone anamulanda komweko
Mcp yapenga nanu mukatuluka mung'alura zonse
Maloto Munthu odzikonda wa mtundu ujawu ofuna zawo zokha ziziyenda mkumati mudzatenga BOMA ayi tili Mmalawi momwemuno bola osadzakomoka
Osaopa osafoka ambuye Ali pambuyo panu
How come, using a phone in a cell? This case is going no where kuzikola kwenikweni uku,cheap propaganda
Muzipusisa anthu opusa amene skukufusayo ndichitsilu
Amadya ekha apa wayamba kupindula
Amakuopani zitsiru izi
Munthu analandidwa zotheka bwanji?
Akuipanga post ndiwe yemwe most iweyo pakufunika Kumanga chifukwa ukugwirisa ntchito FB yamwini . kaliyatiyo alibe phone pakalipano munthu alamangidwa phone tima landa
Simumati anamulanda foni....😂
Kodi inuo mukt chani nanu????
Mumati alandidwa phone ndie awapasa? Ok page ndi yaodi
Kom
?
Wa pho
Eee mama golidi amaenela mung'anjo to be purified mudutsa my pa u president po
Osawopa,osa
God will take care of you mama😍😍😍
We need strong mom like u we are together with u ❤