ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Koma Pena Mulungu zimene amapanga eeeh zodabwitsa ndithu🙌🙌
Zonadi
Ndi chissomo ca ambuye!❤
Haleluya mulungudiodabwisa
Ndinakumana naye mnyamata ameyu ku Lilongwe and andipemphandi chithazo, but malingana ndi mmene amaonekeradi ndinakana poti kunja unaopsa uku, umati ndikuthandidza munthu nati akupwyeteke
Kofi bwanji osangofotokoza za mmene unabwerela kudziko kuno ukungobwerezabwereza zoti ufiti kulibe,ife tikufikilira za mmene iwe unafikira kukhomo kwamakolo ako ukungoti kumalawi ufiti kulibe mobwerezabwereza
Amen and amen
Ndipo inu ziko iri anthu achuma awa mlungu azawarange ngati chakwera uzarangidwa unamupha chirima osarakwa
Iwe ndwe wachamb wav chilima nd ngzi chab kapen ulindiumbon chakwela alibe vuto km iwe
akumanga ulinawo uboni
Zoonadi zimenezo kusalima zinachhika pano pakana pano adabeleka mwana
Abelu zuranga I like him the the way he is doing his job
Alihamudulillah
Government must change this law ,it's the poor always fill the pain 😢😢
Yehova amayika njira popanda njira.Ambuye mulemekezeke amen
Ukanafotokoza bwinobwinooo zammene unabwelera kuno kudziko kuno osamangofotokoza zaufitizo iyayi kambani zakubwera kwanu anthu titolepo fundo yogwilika chifukwa chochulutsa zotankhulayankhula anthu sangakukhulupilire
Praise God ❤
Nkhani iyi ndi yoona kumene zathu wina adamwalira kuno ku South Africa koma adakapezeka ku Malawi ali moyo pano akufotokoza chilichose
Abel thank you for what you’re doing. Tadziwa zambiri zikuchitika,
Zabwino zonse Willy!!
Wamaboza nyamatayo aaaaaa
Wabodza ndiweyo kaya palibepo chimene chikukukhudzapo kaya iweyo kwako ndikuvela basi
Fiti iweyo usatipusitsepo apa
Wabodza bwanji umbon oseu
Amen and Amen
Mulimekeze Yehova dzikoli likupita kuti tilikumapeto
Zoonadi anthu awa akufanana koma akafukule mandamo DN a
Yooooo zithu zake
Kwa mulungu wamoyo kulibe chobisika,, mulungu apitize kugwila ntchito yake
Abele wakumana nazotu apa chilungamo munthuyo akufotokoza
Nyamatayi akundionekera ochenjera kwambir, watumidwa ameneyi... iyaaa
Ineso akundibowa mmalo mofotikoza zamabweredwe ake akungokimbikira zakuti kumalawi ufiti kulibe mmene wayambilaa akubowaso kobasi
Tingawapeze bwanji
Eish
Last days
Km Ambuye atichitire chifundo
Koma Pena Mulungu zimene amapanga eeeh zodabwitsa ndithu🙌🙌
Zonadi
Ndi chissomo ca ambuye!❤
Haleluya mulungudiodabwisa
Ndinakumana naye mnyamata ameyu ku Lilongwe and andipemphandi chithazo, but malingana ndi mmene amaonekeradi ndinakana poti kunja unaopsa uku, umati ndikuthandidza munthu nati akupwyeteke
Kofi bwanji osangofotokoza za mmene unabwerela kudziko kuno ukungobwerezabwereza zoti ufiti kulibe,ife tikufikilira za mmene iwe unafikira kukhomo kwamakolo ako ukungoti kumalawi ufiti kulibe mobwerezabwereza
Amen and amen
Ndipo inu ziko iri anthu achuma awa mlungu azawarange ngati chakwera uzarangidwa unamupha chirima osarakwa
Iwe ndwe wachamb wav chilima nd ngzi chab kapen ulindiumbon chakwela alibe vuto km iwe
akumanga ulinawo uboni
Zoonadi zimenezo kusalima zinachhika pano pakana pano adabeleka mwana
Abelu zuranga I like him the the way he is doing his job
Alihamudulillah
Government must change this law ,it's the poor always fill the pain 😢😢
Yehova amayika njira popanda njira.Ambuye mulemekezeke amen
Ukanafotokoza bwinobwinooo zammene unabwelera kuno kudziko kuno osamangofotokoza zaufitizo iyayi kambani zakubwera kwanu anthu titolepo fundo yogwilika chifukwa chochulutsa zotankhulayankhula anthu sangakukhulupilire
Praise God ❤
Nkhani iyi ndi yoona kumene zathu wina adamwalira kuno ku South Africa koma adakapezeka ku Malawi ali moyo pano akufotokoza chilichose
Abel thank you for what you’re doing. Tadziwa zambiri zikuchitika,
Zabwino zonse Willy!!
Wamaboza nyamatayo aaaaaa
Wabodza ndiweyo kaya palibepo chimene chikukukhudzapo kaya iweyo kwako ndikuvela basi
Fiti iweyo usatipusitsepo apa
Wabodza bwanji umbon oseu
Amen and Amen
Mulimekeze Yehova dzikoli likupita kuti tilikumapeto
Zoonadi anthu awa akufanana koma akafukule mandamo DN a
Yooooo zithu zake
Kwa mulungu wamoyo kulibe chobisika,, mulungu apitize kugwila ntchito yake
Abele wakumana nazotu apa chilungamo munthuyo akufotokoza
Nyamatayi akundionekera ochenjera kwambir, watumidwa ameneyi... iyaaa
Ineso akundibowa mmalo mofotikoza zamabweredwe ake akungokimbikira zakuti kumalawi ufiti kulibe mmene wayambilaa akubowaso kobasi
Tingawapeze bwanji
Eish
Last days
Km Ambuye atichitire chifundo