Akuti Awamangatu chifukwa amafuna kupha munthu mungakhulupilira zimenezo? 😳

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 23 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 110

  • @JeremiahFalakeza-c1m
    @JeremiahFalakeza-c1m 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +7

    A malawi tidzuke tipepherere dziko lanthu makamaka 11:pm and 02:pm popephera timupephe Mulungu Atipulumutse.

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

      Zoonadi zimenezi popanda kudalira Ambuye tili madzi

    • @LeticiaKaferawanthu
      @LeticiaKaferawanthu 8 นาทีที่ผ่านมา

      Ndipoe.zoona

  • @IshmaelLosani-cs4cl
    @IshmaelLosani-cs4cl 30 นาทีที่ผ่านมา +1

    Osamatengera malamulo mmanja dikirani chilungamo chioneke 👏

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama 53 นาทีที่ผ่านมา +2

    Chilima analakwitsa yekha kuwinitsa mcp lelo akuvutitsa otsala

  • @HarrisonTembenu
    @HarrisonTembenu 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +4

    Chiwembu cha abambo ake asikono Ichi. Maganyatu ndi owukira nd mfitiso

  • @HalimaShafie-q9k
    @HalimaShafie-q9k ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Vuto apolice aku Malawi alowa mcp agalu okhaokha a mcp komaso chakwera mboloyao

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +5

    Apapa Malawi yense timayenera kupanga mademo a emergency

    • @ShamilahSaizi
      @ShamilahSaizi 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ndipo izi ndizoona

  • @Willardmakande-p2q
    @Willardmakande-p2q ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Amafuna kupha munthu koma opha SKC alikuti?

  • @JasonMailos
    @JasonMailos 43 นาทีที่ผ่านมา

    Ndiusi ameneyo manganya Ngati anapeleka chilima akalephele kumupeleka kaliyati

  • @edwinnyasulu2088
    @edwinnyasulu2088 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Thanks for the update

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

      Any time!🎉❤

  • @NicholasMackinnah
    @NicholasMackinnah 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Kodi mwayamba za one party system

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    MCP chifukwa chiyani ikumawatengela a Malawi kuntoso a kweni alakwanji koma

  • @BrandinaMphuka
    @BrandinaMphuka 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mmmmmh mayi kaliyati sanamvekepo ndi mbiri imeneyo zalowa ndale iziiii

  • @angelmwethewa8010
    @angelmwethewa8010 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Kodi zafika poti apolice kulesa anthu kuti asatenge ma placards?mpaka ma placards kusungidwa kuseli kwampando?ok

  • @BrianMamiwa-k8m
    @BrianMamiwa-k8m 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Eeee koma mcp a zoona ng'ona ndi ngona mcp sizasintha

  • @DavieKumbanga
    @DavieKumbanga ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mwaona inu ana amma 2000 zomwe munapanga? 1 million jobs ija ndiimenei

    • @HabrilMalaya
      @HabrilMalaya 25 นาทีที่ผ่านมา +1

      Vuto ndife 😂😂😂😂

  • @JudithKatungwe
    @JudithKatungwe 18 นาทีที่ผ่านมา

    Bola muzimanga umboni ulipo,,osati misonkho yathu ipitenso apa

  • @DysonChiumia
    @DysonChiumia 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Aah police yaku Malawi penapake💔

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 56 นาทีที่ผ่านมา

    Amalawi mizimu zukani,monga nzika ya chimalawi,yambaponi kutibula,mpolice aliyese ndi odelela kwambili.

  • @mrcool531
    @mrcool531 34 นาทีที่ผ่านมา

    Munthu wake ndani?

  • @RhodaPhiri-d6q
    @RhodaPhiri-d6q 2 นาทีที่ผ่านมา

    Aliyense wandale ndioipa bas ndipo ife ndiomwe timapanga zopusa kumataya nthawi yathu

  • @PaulPhiri-c5u
    @PaulPhiri-c5u ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma zoona zimenezi achakwera mbiri yanu isaonongeke chifukwa cha anthu anu oipa mtima chifukwa chipani cha mcp anthu akchita kunenakuti. Ndi chakhaza kwambiri pamene chafika aliyese akuopa kufikira pafupi

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Broh panopa ndpamene ndikumamva zoona.zake pitilizan kutiunikira koma after kulephera kumugwira wa Bakili Muluzi TV komas Ntanyiwa muone adzimanga aliyense apa angoyamba kumene

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 40 นาทีที่ผ่านมา

    Police yathu ikugwlisidwa ntchito ndiandale basi zitsiru zapolice

  • @BennettNjedza
    @BennettNjedza 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Apapa akuonjezera mkwiyo wa anthu

  • @AlexKamfosi
    @AlexKamfosi 48 นาทีที่ผ่านมา

    Zosezo. Ndizaboza. Akufunakupasa. Poizoni. Mapulaniawo. Alichocho. Pakufunika. Kuchitapokathu. Akweni tialuzaso. Ngati chilima bomaili. Liphaathu

  • @PATRICKTHlMZY
    @PATRICKTHlMZY 24 นาทีที่ผ่านมา

    Kmaso sizikufunika kupephela kma kupita kukagona kupolice

  • @EvasonThupilifana
    @EvasonThupilifana 8 นาทีที่ผ่านมา

    Ine ndine wakumudzi ndimafuna boma limeneli litandimanga a police angazaone polekela sure

  • @Peter-w7h
    @Peter-w7h 40 นาทีที่ผ่านมา

    Zopusa basi kwacha mumango ngwesa basi pangani zoyendesa ziko mmmm

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Amafuna kuphaa muthu kutiko kapena zalowa kundale. Muthu wake ndani , palowa ndale apapa sizonamizana. Ayiwala kuti ndamene analowetsa boma

  • @MarthaBalakasi
    @MarthaBalakasi 10 นาทีที่ผ่านมา

    Boma ndilomweli tingositha president ndi apolice

  • @AndersonBishop-i2t
    @AndersonBishop-i2t ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chikalayayo ndi wawusilu walandila ndalama km kungoluza onsewo azakhala ma lova azawonas tizalemba ntchito ena nosenu a mcp mpakana ndi ma judge omweso ntchito yawo izawathla kmaso azamangidwa ndi awusilu mesa ndi Andale amene apolicewo

  • @JoaquimNasiyaya
    @JoaquimNasiyaya ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Vuto apolice aku Malawi amakhala Ngati Siaku Malawi

  • @MikeMpapasaJeremia
    @MikeMpapasaJeremia 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Akufuna tibweleleso ku one party system. Akukanika bwanj kunena mulandu wenewen omwe amangila mmmmm

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Muli busy kumanga anthu malo moti mukhale busy kusaka njira yomwe mungapezere mafuta dziko. Mcp ndiyochitisa manyazi poganiza koma chalakwe amaganiza ngati mwanadi ndithu, zina umangoona waziyambadi.

    • @PidoMaganga
      @PidoMaganga ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ndye mwati chalakwe kkkkk

  • @ShukuraniTonex
    @ShukuraniTonex 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Akupanga zopusa kwambiri anthuwa

  • @PATRICKTHlMZY
    @PATRICKTHlMZY 26 นาทีที่ผ่านมา

    Kmatu aboma akuyesa zida

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zachamba chikangawa chakwera garu 😮

  • @PaulPhiri-c5u
    @PaulPhiri-c5u ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma mulungu akuchitileni chifundo pa nkhaza mkuchitila anthu zikutikhuza kwambiri zimene zikuchitika mziko mwathu muno ngat mtsogoleri kulibe zoona chitanipo kanthu achakwera

  • @EdsonGeorgeViagem
    @EdsonGeorgeViagem ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mbava zosowa pogwila

  • @BridgetKondowe-j4f
    @BridgetKondowe-j4f ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Maro Moti azirimbana ndi dzikori kuti Kodi dzikori rikuyenda bwanji koma akurimbana nd chirima amene amumangayo ndi skc Muzimu wakhe uwuse mumutendere

  • @SHAIBUSALIMU-l1o
    @SHAIBUSALIMU-l1o ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Izitu zomwe zikuchitikazi ndi khaza kwa amayi chifukwa chani koma ziko mukuliwona ngati ndilanu

  • @michaelkallyz2425
    @michaelkallyz2425 12 นาทีที่ผ่านมา

    Malo mosaka Mafuta mwayamba kusaka Anthu😄

  • @ChimwemwePhiso
    @ChimwemwePhiso 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganya Manganya Manganya manganya

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A polisi musayiwale kuti mnzanu waphedwa ndi MCP yomweyo

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Apha chilima ndi witika muwamanga liti?

  • @chemandotamwale
    @chemandotamwale 38 นาทีที่ผ่านมา

    Sizachilendo m c p kupanga nkhanza

  • @HafizahHarack-bn3bf
    @HafizahHarack-bn3bf 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Police yakumalawi is very useless amumanga bwanji muthu mulibe umboni wina uliwonnse, this is proper gander srious.

  • @johnlameck8366
    @johnlameck8366 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Munthu wake uti yemwe akuti amafuna kumumpha mmmm

  • @BrianMamiwa-k8m
    @BrianMamiwa-k8m 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Apapa akanamangidwa wa mcp akanawalola kuti amuone m,balewao koma pot ndiosusa alibe ufulu

  • @FlynessWinga
    @FlynessWinga ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iiiii koma ndale

  • @GeorgeFrank-k1q
    @GeorgeFrank-k1q ชั่วโมงที่ผ่านมา

    mbuye menyeleni nkhondo,malawi okoma uja waonongeka,ivani kulira kwathu

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    nkulu wina wake akuti quarter chani kaya sangapiteko muona

  • @EthelKubalasa
    @EthelKubalasa ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kungowonjezela mkwiyo kwa aMalawi. Ma plan anu sayenda MCP

  • @wisdomchilanga723
    @wisdomchilanga723 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A police opusa awa

  • @McDonardMapala
    @McDonardMapala ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mukuwopa chan titulusilen munthuwanthu

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Amalawi ufulu wathu tinaugulitsa povota nthawi ijayi mmmmm

    • @HabrilMalaya
      @HabrilMalaya 24 นาทีที่ผ่านมา

      Tichilape😂😂😂😂😢

  • @FlorenceBanda-w5s
    @FlorenceBanda-w5s 55 นาทีที่ผ่านมา

    Zarowa ndare izi

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama 51 นาทีที่ผ่านมา

    Yakuphandiyakupha mcp anapha chilima kasambala Mia

  • @Agness-ic9tl
    @Agness-ic9tl 44 นาทีที่ผ่านมา

    Tumizani mafuta anthu akufa sanafike kuchipatala muwasaka anthu kuti atani

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Amafuna kupha Muthu koma chakwela anapha mumugwila lit

  • @AbdulMalik-o7n1q
    @AbdulMalik-o7n1q ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manganya usi ndiwe mfiti ndi chingawayo

  • @JaphetSakala-u5j
    @JaphetSakala-u5j 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Magalimoto asilikali ose aja amapita uku

  • @SamukLungu
    @SamukLungu 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Apangisa zosezi ndi manganya ndi chikangawa

  • @DavidFyson
    @DavidFyson 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zoopsa

  • @GamaChifundo
    @GamaChifundo 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Wathilila mchenga mpunga

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ma plan amanganya awa

  • @michaelkallyz2425
    @michaelkallyz2425 12 นาทีที่ผ่านมา

    Boma ndilomwelii😁

  • @FrancisChikazunga
    @FrancisChikazunga 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Umboni mulinawo

  • @JohnmarkNazombe-hi9xd
    @JohnmarkNazombe-hi9xd 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    UTSI ALIKUTI?????

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Manyazi akuwagwira apolice akuwaletselanji ma poster a, ikasaka mafuta kumene

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Eti amwene mafuta Akusowa akusaka anthu

  • @patriciajangaza675
    @patriciajangaza675 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zonsezi ndi manganya tikamati ngoyipa bamboyu mwaonatu

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chipani cha nkhanza osamakasaka mafuta bwanji

  • @DanielJuwawo-s5n
    @DanielJuwawo-s5n 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Apolice akumalaw ndiofoira kwambiri

  • @LeonardJere-r5y
    @LeonardJere-r5y ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kod moyo umeneu nduyekut ufulu wathetsad chikangawayu

  • @JuliusMtalika
    @JuliusMtalika 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iiiiii koma boma ili ayi ndithu

  • @HarrySteven-d6e
    @HarrySteven-d6e 57 นาทีที่ผ่านมา

    Yesaya 54v17

  • @CorneliusSande
    @CorneliusSande 28 นาทีที่ผ่านมา

    Mumtima ndi muthumba salowana

  • @PeterJere-ot5mg
    @PeterJere-ot5mg 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    amafuna kupha ndani?

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Kayasotu sakunena

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Malo mokasisa mafuta aja amati alingambwi ngambwi aja koma satana alipantchti

  • @KentWilliam-r2v
    @KentWilliam-r2v 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mcp ndye chipani choyipa ichi

  • @NelsonKasanga-b6q
    @NelsonKasanga-b6q 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tiyeni mahdemo

  • @MaxwellKapalamula
    @MaxwellKapalamula 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mcp chidure avomere kulephera

  • @MaxwellKapalamula
    @MaxwellKapalamula 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Malo mokasa mafuta, mukumanga anthu

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Munthu amafuna kupha yo Ali kutiko poyamba anena kuti chakwera tsopano tiva zoti tsopano

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Sakumutchuladitu

  • @WhyteSmart
    @WhyteSmart 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A police omvetsa chisoni kwambili

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      @@WhyteSmart Heavy

  • @Sofi-p1v
    @Sofi-p1v 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Komatu bambo a sikono longosokani

  • @ChirwaSanama
    @ChirwaSanama 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zovesachison mcp mbuzzi

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Aaaa koma police yaku malawi

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Zaukape man

  • @ChimwemweNthenda
    @ChimwemweNthenda 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma mcp amuziwe yesu

  • @EmilyKanyika
    @EmilyKanyika 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iiiiiiiiiiii koma machimo

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    amafuna kupha munthu kuti

    • @MalawianCamera
      @MalawianCamera  2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      @@alexsumani6823 kayaso man😂

  • @YamieManda
    @YamieManda 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kodi peter sanamange jese ndi sungama mwazionalero agwepe inu

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga 27 นาทีที่ผ่านมา

      Takasambeni uko uli mbuu apa ngt unagona paphulusa mwana wa njoka iwe