Shehe uyuso wagagada ulariki wake mopanda mantha kusiya anthu akungoombera mmanja

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 5 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 156

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 5 วันที่ผ่านมา +16

    Tayesedwa ndi president wakhaza chakwera ndie timupempha Allah kuti atichosele chakwelayo ameen

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo 5 วันที่ผ่านมา +10

    Sheikhe ulaliki wanu siukugwilizana ndi ma aya omwe mumatulutsa pakamwa panu, uku ndikugulitsa mawu amulungu, ambuye akumvelen chison Ameen

    • @omardyman8083
      @omardyman8083 5 วันที่ผ่านมา

      Analandila ndalama nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto zachamba

    • @rasulmaulidi2224
      @rasulmaulidi2224 3 วันที่ผ่านมา

      zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu

  • @abdulhameed7808
    @abdulhameed7808 5 วันที่ผ่านมา +5

    Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.

  • @NenehMasanje
    @NenehMasanje 5 วันที่ผ่านมา +12

    Sheikh mwadya now ndrama

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา +3

    7:53 7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizanu
    Mayeselo aifa muyesa ife sitimaziwaaa,
    Nde imfazake zochita kumugwira munthu pakhosi mwadaladala , kumuombela mfuti mkamwa munthu ,kodi yinu mulankhulabwanj muli ndiwumunthuyinu ,aaa muzichotsela ulemu nokhatuyinu mwangotengana nonse odya ndalama zamagazibasi ,
    Afitiwo alimwetuuuu ati zikuyenda malawi wake utiyo amene mungamunamize lelo ,
    Azibusa muzichotsera ulemu nokha mwamva

  • @SulaimanaJames-b9v
    @SulaimanaJames-b9v 3 วันที่ผ่านมา

    Maa Shaa Allah
    May Allah bless this message and make it beneficial

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา +3

    Wadya nawo ndalama zamagazi iwee, usatinamize asilamufe pamodzi ndi amalawife, ifenso ndife asilamutu, mayesero ukunena apawa simayesero ochokeraxkwa ALLAH, awa ndimayesero ochokera kwa satana kudzela kwa chizukulu tudzi chake chotchedwa chakwela ndi boma less lake 😂😂😂😂😂

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 5 วันที่ผ่านมา +3

    Odya ndalama zamagazi ngati akumasowa zoyankhula zawo? Allah mukunenayo akuyendereni Sheik😢

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam 5 วันที่ผ่านมา +2

    Ameen sheikh Allah ahead u. From Cape Town centre

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา +3

    Chemoto alipomwepo anapha ALLAN WITIKA, anapha chilima kuchikangawa 😂😂😂😂

  • @SteveriaZimba-qs1id
    @SteveriaZimba-qs1id 5 วันที่ผ่านมา +1

    Amen and amen uthenga wamphavu ambuye alemekezeke ndipo akhululukire zochimwa zathu

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali 5 วันที่ผ่านมา +1

    Naam sheikh ma shaa Allah ulaliki wabwino ndithu ❤❤❤❤

  • @BrownMatonyola-xi3lb
    @BrownMatonyola-xi3lb 3 วันที่ผ่านมา

    Mwadya zingati
    Aliyese wanyambita ndalama zoti azizilise za imfa yachilima ndikupepha Yehovah Mulungu wathu amuonetse kiyama akumane ndi mavuto

  • @FebbieMaulidi
    @FebbieMaulidi 5 วันที่ผ่านมา +1

    God bless you sheik for unity message ❤

  • @SayidiIshmael
    @SayidiIshmael 3 วันที่ผ่านมา

    ❤Allah give you more life and imaan to defending this deen

  • @IshaaakKango
    @IshaaakKango 2 วันที่ผ่านมา

    Maashallah sheikh

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 15 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Aaaa sizomwezija Izi inu asheikh opanda manyazi ,
    Panja peni peni wadya ndalama Za Chikangawa uyu,
    Sali pachilungamo uyu

  • @muhmmadsarwer9527
    @muhmmadsarwer9527 4 วันที่ผ่านมา

    Ameen thuma ameen Allah tichotseleni President ameneyu..ndipo tipatseni mtsogoleri wabwino mdziko mwathu muno

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 5 วันที่ผ่านมา +1

    Mukufuna mutamike. M'nungu tam'nyekule ngulumbira une

  • @mosewallace9717
    @mosewallace9717 3 วันที่ผ่านมา

    mweye che kuntamba 🔥🔥

  • @kekeaufi9834
    @kekeaufi9834 5 วันที่ผ่านมา +2

    *WA ALYKUM SSALAAM WARAHAMATULLAHI WABARAKATUHU,,,,Inna lillah wa Inna ilayh rajoon*

  • @TWAIBAKBANIES
    @TWAIBAKBANIES 4 วันที่ผ่านมา

    Ma vesi ali apa zili kutali tali . Aaaaaaa koma akulu akulu sheikh mudziima pachilungamo komanso ma ves osamawakhitetsa ai

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson 5 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkkkkk wabodza ndiwe ma inovolopu yakutseka pakamwa ya chakwela, zikhale ndi kunkuyu 😂😂😂 waukape ndani sakudziwa.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา +1

    Sheikh awa salibwino akugulitsa mawu aMulungu ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa mutsiku lomaliza

  • @AndersonTsoyo
    @AndersonTsoyo 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    100% shehe uthenga omanganga dziko

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 2 วันที่ผ่านมา

    Ili ndiye gulu loyitana chakwela ku Eid atawapasa mbia makwacha mashehe adyera ichoooo!

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา +1

    Usatiipisile Islam yathu iwe wamva , bwanji sukuwalesa makafiir omwe ulinawo pomwepowo kuti azikha okonda anzawo?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา +2

    Mwapatsidwa ndalama

  • @Macsaidi
    @Macsaidi 5 วันที่ผ่านมา

    Komabe sitinganame pa chilungamo.
    Saulos Chilima anaphedwa ndi ndege ya boma la mcp

  • @omardyman8083
    @omardyman8083 5 วันที่ผ่านมา

    Ndine msilamunso koma sheikh uyu wapochelaapo nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto akatero anali ku state house

  • @MollenMponya
    @MollenMponya 2 วันที่ผ่านมา

    Awa ndye mau ochokwera kwa Mulungu osati Za Anja amaziyesa Okha opambana

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io 5 วันที่ผ่านมา

    Alhamudulillla sheih my Allah bless you all the time what's a sweet Message like 💋💗 this Marshall ( port Erizabeth SA missionvale

  • @johnarushamasese108
    @johnarushamasese108 5 วันที่ผ่านมา +1

    Ana usawi chemwalimu apochele silingwa

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 5 วันที่ผ่านมา

    God bless you Sheik all the time ❤❤❤❤❤

  • @juntoiman
    @juntoiman 4 วันที่ผ่านมา

    Mmmmm sheikh zoona malo molankhula chilungamo pamaso pa anthu muli busy kubisa choona.Pamenepotu padali anzanu koma lero alikyt

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr 5 วันที่ผ่านมา

    Nyasi zenizeni pamaso pamulungu chilungamo mukuchidziwa Shehe iwe. Wadya ndalama

  • @MafumuBanda
    @MafumuBanda 5 วันที่ผ่านมา

    Sheikh ilim yanu ndiyochepa mupite mukaphunzirenso, ngati mukuzitenga zinthu za Allah maso mmwamba eeeeee chilango chaukali chkupezani pompo mulipo asakutameni awowo andalewo ndizotsala , ifenso tinaphunzira kwambiri kuposa iweyo xxx

  • @AbouzaidahSayeed
    @AbouzaidahSayeed 5 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkk sheikh wasanjatu uyu 😅

  • @NuradinaAbrahima-rt9ip
    @NuradinaAbrahima-rt9ip 4 วันที่ผ่านมา

    No i was interested ndi ulaliki wanu Sheikh koma kumapetoko mwandionongela data yanga😭😭😭😭

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา +1

    Ine ndine Msilamu, uyu ndi sheikh wa chishiya uyu kafiir weniweni uyu,

    • @HusseinAdamLidezo
      @HusseinAdamLidezo 5 วันที่ผ่านมา +1

      Sheikhe wamanyi uyu mbuz

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา

      @@HusseinAdamLidezo zoona angamasinthanise chisilamu ndi ndalama?, bwanji sakulesa asatana anzakewa kuzunza ndikupha anthu mdziko muno ?

  • @trickermussa472
    @trickermussa472 4 วันที่ผ่านมา

    Kukangotinyasisila deen yathu mbuzi ya shaikh

  • @marvelousmadzimure1811
    @marvelousmadzimure1811 3 วันที่ผ่านมา

    Masha Allah ❤❤❤

  • @Sasha-g3z
    @Sasha-g3z 4 วันที่ผ่านมา

    Bas allah awadalotse ndi ulaliki wawow

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 3 วันที่ผ่านมา

    Msilamu wolakira zau Mulungu osati enewa .Akuti ngati munthu wa mulungu walalika osanyoza president akuti ndiye sadziwa kulalikira. Shame

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 5 วันที่ผ่านมา +1

    Soka kwaiye akupindisa chilungamo popeza akuziyandikisa matako ake kumoto

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา

    Zikhale ng'oma akuwombelanso mmanja pamfundoless zomwe wanena, kodi unamulesa kuti asamaphe ma ruandaniz and Burundians komanso amalawi?.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 15 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Inu nde muletsa zoipazooo suyu muyamikira mfiti ,wakuba, musatinyase

  • @Musa-cz1nm
    @Musa-cz1nm 5 วันที่ผ่านมา

    Ma shaallah ma shaallah ma shaallah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา

    Izo mzoona zoti tiziphunzisana zabwino ndikulesana zoyipa, funso kwa iweyo shehe ndiloti;
    Kodi zoipa zomwe akuchita chakwelayo wamulesa?
    Kupha kumene akupha aboma anthu kumalawi kuno wawalesa aboma ako awusiluwo ?,

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo วันที่ผ่านมา

    Thanks shelk potipatsa ulaliki wabwnowu

  • @KasundaAbbasi
    @KasundaAbbasi 5 วันที่ผ่านมา

    Ngakhale mawu akewo akupepuka zoyakhula zakeso kumalemelera abusa aja

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 5 วันที่ผ่านมา

    Mzimu wa Chilima ukunyetseni nonse amene mukugawa ma yellow band ndi inu amene mukudya ma bans

  • @AminahMussah
    @AminahMussah 5 วันที่ผ่านมา +3

    sheikh zamanyazitu iziii kufuna kuoneka wabwino pamanso pa pule mwadya zingat

    • @JUSTINChigamba
      @JUSTINChigamba 4 วันที่ผ่านมา

      Ndipo inu zosayenda

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 5 วันที่ผ่านมา

    Chemoto akhale Kunkuyu😅😅😅😅

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา

    Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani
    Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya ,
    Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali
    Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva

  • @FarhaazbashaMdoka
    @FarhaazbashaMdoka 3 วันที่ผ่านมา

    Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏

    • @FarhaazbashaMdoka
      @FarhaazbashaMdoka 3 วันที่ผ่านมา

      Koma ndalamazi guyz tisamale nazo

  • @udkconsultancy5567
    @udkconsultancy5567 5 วันที่ผ่านมา

    POWERFUL

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 5 วันที่ผ่านมา

    SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI

  • @Ishmael376
    @Ishmael376 5 วันที่ผ่านมา

    Komati choti muziwe kulankhula boA pamaso pamulungu pomwe chilungamo mukuziwa muziwe kuti akakuwochani

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z 5 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwela akusapoter Israel shehe wa mabi

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael 5 วันที่ผ่านมา

    Naam ena akwiya chifukwa mwayakhula zosephana ndizomwe Iwo akufuna

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 5 วันที่ผ่านมา

    Awaso nawo aaaaaa zaziiii mazidyani wosatipusitsa

  • @emilynthite6545
    @emilynthite6545 5 วันที่ผ่านมา +1

    Apasidwa ndarama alaliki adyela

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja 5 วันที่ผ่านมา

    Akutuma Kodi sheikh wachinyengo iwe nde akupasa zingati ?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา

    7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizaunu

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o 5 วันที่ผ่านมา

    Sheikh apatu nanu mwanama kwambiri 😂😂😂😂😂😂

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn 5 วันที่ผ่านมา

    Mashala

  • @ChristianMtambalika
    @ChristianMtambalika 5 วันที่ผ่านมา

    Anthu muzinena chirungamo osamabisala mukaona omunenayo kuti alipopo mamizimu anthu akuvutika pqmene iweyo ukufunq kukomesera president umenewo moyo oyipa ngati uli sogoleri wapingo ndiwe waboza liuze chirungamo dziko

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 5 วันที่ผ่านมา

    Walykum ssalam wakahmatul llah wabaraktu

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od 5 วันที่ผ่านมา

    Kmatu musamapange zindu kut akutamen shehe Allah wanji angasangalale ulaliki zimayi sisi kunja osamvala pango 😢😢😢 dini ulindo bas inarilah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา

    Moses kumkuyu akukuwombela mmanja pamfundoless zakozo, kodi unamulesa kuti asamaphe anthu ngati mmene anaphela ALLAN WITIKA uja?

  • @user-zf7xk8fk5s
    @user-zf7xk8fk5s 5 วันที่ผ่านมา +1

    Km Inu sheikh ndinu opanda nzeru apurezident akunyoza chisilam kms amakokomezera nkhondo ku Palestine kut adziwapha asilam zoon Inu kumaim pagulu kwacemera

    • @user-zf7xk8fk5s
      @user-zf7xk8fk5s 5 วันที่ผ่านมา

      Ndipo panop asilam akumalaw akuchititsa manyaz chisilam chifukwa chokonda ndalam mmmm zomvetsa chison

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon 5 วันที่ผ่านมา

      Ndipo sheih uyu watinamizapo wadya nao ndalama za pule malawi sadzathekayi

    • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
      @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา

      Alibenzeru uyu

  • @user-fm7yg5yc2c
    @user-fm7yg5yc2c 5 วันที่ผ่านมา

    Walaikum salaam warahmatullah wabarakatuh... Innalillah wainna illaih rajiun

  • @AliSinoya
    @AliSinoya 4 วันที่ผ่านมา

    Sheikh uyu manyakwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 5 วันที่ผ่านมา

    Shehee wadya chamba chanji chakwera Mutu Ngati gwafa😂

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 3 วันที่ผ่านมา

    Mashallah

  • @user-qs7xw4ph7z
    @user-qs7xw4ph7z 4 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi 5 วันที่ผ่านมา

    Chakwera anapha chilima😊

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh 5 วันที่ผ่านมา

    Live from Gaza city

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv 5 วันที่ผ่านมา

    Palibe amene angakutameni yinu bodza zidyani ndalamazo msilamu weni weni akuonani Kuti mwanama akulu ndinu adyela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 5 วันที่ผ่านมา

    Achina chimoto ndi a MCP ndiwe shehe😂

  • @moosakananji1879
    @moosakananji1879 5 วันที่ผ่านมา

    Sheikh awa Malo ngt awa kumafunika Sheikh ayyub azipita kumeneku not awa

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 5 วันที่ผ่านมา

    Ndiye ulaliki otaninso uwu, mukulalikila ngati simukumva kuwawa bwanji, odya banzi sasowa.

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y 5 วันที่ผ่านมา +1

    Ndalama Za mcp zikuyakhula

  • @bisweckchimphamba8497
    @bisweckchimphamba8497 5 วันที่ผ่านมา

    Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope

  • @abbasdamsonamini4888
    @abbasdamsonamini4888 4 วันที่ผ่านมา

    Naam Ameen thumma Ameen

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p 5 วันที่ผ่านมา

    Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 5 วันที่ผ่านมา

    Ameen

  • @shadrackdrums3536
    @shadrackdrums3536 5 วันที่ผ่านมา

    Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t 4 วันที่ผ่านมา

    Chemoto ndinu mwandila ma unforp

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 5 วันที่ผ่านมา

    Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 5 วันที่ผ่านมา

    Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 5 วันที่ผ่านมา

    Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir

  • @JumaMboneka
    @JumaMboneka 4 วันที่ผ่านมา

    Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi 5 วันที่ผ่านมา

    Awapasa ndalama 😮 awa

  • @NchocitoTuaibo
    @NchocitoTuaibo 5 วันที่ผ่านมา

    Naam sheh

  • @JamesRoben-dy7bx
    @JamesRoben-dy7bx 5 วันที่ผ่านมา

    Uyu anadya kale ndalama uyu komaso ndi wa mcp uyu

  • @abdulllahanubieimran06comanubi
    @abdulllahanubieimran06comanubi 5 วันที่ผ่านมา

    Jazackah alla

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 2 วันที่ผ่านมา

    Shehe my foot 😅😅😅

  • @EmanuelPaul-io2hk
    @EmanuelPaul-io2hk 3 วันที่ผ่านมา

    Shehe akufuna chuma chamagazichi eti?