KANGAUDE---29/10/2023...ku mulanje anthu okwiya aika mtembo pakhomo la munthu...on @mibawatv

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 90

  • @pioireneuvictorpio1391
    @pioireneuvictorpio1391 10 หลายเดือนก่อน +3

    Akulu akuluwo ndiwolakwitsa chifukwa sanawauzei koti akayike maliro ndipo athuwo ndiwosalakwai pakutengera ndimene akufotokozeramo,

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr 10 หลายเดือนก่อน +5

    Kuyambira aTA ndi mafumu enawo ndi achinyengo manda sazaza amadula minda yomwe yadzungulira mandawo pang'ono pang'ono ndiponso nkhati ndalama inasonkhedwa ndikukagula munda chirungamo chinachitika koma kwanako anakana mukukana kwawo amafuna chichitike chani ? Zomwe anakafuna ndizomwe zachitikadzo asamusepo nyumbayo akamange kumandako akunkha panyo mayiro ndiyosalakwa ndipo ndianthu abwino .😂😂😂😂😂😂

    • @josephkuseke4166
      @josephkuseke4166 10 หลายเดือนก่อน

      Mandawo ndi family osati ammudzi

  • @AronLuka-ue5hl
    @AronLuka-ue5hl 10 หลายเดือนก่อน +4

    Nkhani ndayimvesela bwino bwino apa olakwa ndi Group ndi TA anthu awo palibe chimene alakwa

  • @jacquelinewasili-eh3uv
    @jacquelinewasili-eh3uv 10 หลายเดือนก่อน +2

    Mukuyesetsa Mibawa creativity that dazzles indeed.keep it up kutibweretsera nkhani zodabwitsazi.

  • @user-dd8sk4wp4t
    @user-dd8sk4wp4t 10 หลายเดือนก่อน +4

    Malaw ngti atafike December ndakaika

    • @user-og1nx7en7j
      @user-og1nx7en7j 10 หลายเดือนก่อน

      Malawi akutha mu November muuuu!!!!!

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 10 หลายเดือนก่อน

      Malodza zomwe sitinadzione tukalamba pano 🙆‍♀️🙆‍♀️

    • @BealiniaLangultone-jk5nj
      @BealiniaLangultone-jk5nj 10 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 10 หลายเดือนก่อน +3

    😅😅😅😅😂😂koma anthu akuyenda okwiyatu

  • @blandinabonaventure
    @blandinabonaventure 10 หลายเดือนก่อน +4

    Khani ya maliro ndiovuta llibe bwana kma mamfumu ndiolakwa apa utsogoleri wavuta apa

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 10 หลายเดือนก่อน

    Aaaaa kangaude uli bho

  • @TriciaDeborah
    @TriciaDeborah หลายเดือนก่อน

    Mwakumana nazotu bwino mungamenyedwe

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 10 หลายเดือนก่อน +2

    Eeeee amfumu a mayero ndi nkhani Zina ndi ufumu zosagwilizana eeeee phuma 2 much

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 3 หลายเดือนก่อน

    Awaso ufumu wawo okanika za mowa bas

  • @MtenjeHassan
    @MtenjeHassan 10 หลายเดือนก่อน +3

    Umwa chani Abel Zulanga ❤❤ iweyo ndi one asy

  • @mustafahaji2599
    @mustafahaji2599 10 หลายเดือนก่อน +2

    Amayero akuyakhura ndiphuma

  • @PikeypapucildeRamilo
    @PikeypapucildeRamilo 10 หลายเดือนก่อน +1

    Malawi on flre

  • @user-zz5ww7mv8v
    @user-zz5ww7mv8v 10 หลายเดือนก่อน +1

    Por favor boa noite meus caros irmãos do programa kangaude simplesmente eu respondo pelo nome de Eusencio sidadao mosambicano.venho por esta:agradecer a Deus nos vossos programas.por favor pesso o vosso contacto eu quero conversar convosco me ajudem

  • @user-nx2su4yr1l
    @user-nx2su4yr1l 10 หลายเดือนก่อน +2

    Komat kufotokoza Kuli apa pa mfumu a mayelo eshi zovuta kunvesesat.

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 10 หลายเดือนก่อน

    Malawi wa lero malodza eni eni aliyense akupanga zomwe akufuna🙌🙌🙌

  • @blandinabonaventure
    @blandinabonaventure 10 หลายเดือนก่อน +2

    Amayiro samayenera kukhala mfumu nda mphuma

    • @miccah81
      @miccah81 10 หลายเดือนก่อน

      Kwabasi, muli phuma la nyooooo

  • @user-hs5xv6bk2f
    @user-hs5xv6bk2f 10 หลายเดือนก่อน +2

    Kkkkk mbado wachakwela tiona zovuta kwabasi ngati pulezidenti akupanga chinyengo ndiye bwanji mfumu

  • @miccah81
    @miccah81 10 หลายเดือนก่อน +1

    Anthuwa ndiolusadi komaso phuma 🙌😅😂

  • @semusiliva4106
    @semusiliva4106 10 หลายเดือนก่อน +1

    Khaniyi njayikuludi .

  • @PatrickMbewe-cz6tn
    @PatrickMbewe-cz6tn 5 หลายเดือนก่อน

    🤝

  • @SamsonChitezi
    @SamsonChitezi 10 หลายเดือนก่อน +1

    Paribe fundo achose mariro pakho mkutitukwanisa alomwefe

  • @mtisungegondwe2043
    @mtisungegondwe2043 4 หลายเดือนก่อน

    Anthu si anthu😂😂😂

  • @khadjahmustafa8273
    @khadjahmustafa8273 10 หลายเดือนก่อน +1

    Nchifukwa chaketu ife tinaukana ufumuwo nkungoupatsa kea ena asaaaa kuphetsa izi. Nzachibwana aaaaaa

  • @user-dy5ho4qn6k
    @user-dy5ho4qn6k 10 หลายเดือนก่อน

    Big up abel💪

  • @HopePhiri-r7q
    @HopePhiri-r7q 10 หลายเดือนก่อน +1

    Kumalawi adha

  • @MichaelKalua-mc8ty
    @MichaelKalua-mc8ty 9 หลายเดือนก่อน

    Ukakhala ndi ndalama ndimavuto pa malawi ishiiiiiii

  • @egreymkumba-tj5ji
    @egreymkumba-tj5ji 9 หลายเดือนก่อน +1

    Amfumu a mayelo mutu wanu sumagwila

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 10 หลายเดือนก่อน

    But in Ghana, Angola, South Africa and Botswana there are other cultures which bury their beloved ones within their yards some in Ghana bury a person in a house and the bedroom a person died from. The bedroom used which the corpse has passed that's where they dig a hole to bury the person including the children of the person if the bedroom has been big enough and every year they put wreath as well as marble stone where the grave is after a year, i think even some Nigerian cultures like the Philippines. Ghana they can keep the body of their beloved ones inparticular for more than two to three years depending on the agreement of the children of the dead person.

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v 10 หลายเดือนก่อน +2

    All this is because of poor leadership in Malawi starting from the President. This was a very simple problem.

    • @Clyne_Phiri_265
      @Clyne_Phiri_265 10 หลายเดือนก่อน +1

      Would you make a connection between the two?

    • @victorbanda9039
      @victorbanda9039 10 หลายเดือนก่อน +1

      Ndale mwafika nazo pauchitsiru zikugwirizana bwanji ndi poor leadership

    • @gesinasutherland9241
      @gesinasutherland9241 10 หลายเดือนก่อน

      kufuna kuwoneka anzeru😂😂😂boma ndi Maliro zikufana chani?busy kunyoza boma pa ziiii...mburi za Ku Malawi..😂😂 penzani chonyezela boma...si za ndale iziii..more fire kangaude..

    • @user-jn9tz3li3v
      @user-jn9tz3li3v 10 หลายเดือนก่อน

      @@victorbanda9039 you will understand when you go back to school.

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj 10 หลายเดือนก่อน +1

    Alomwe ndi makape

  • @user-nx9tj5ho2c
    @user-nx9tj5ho2c 10 หลายเดือนก่อน +2

    Malawi on fire 🔥🔥🔥🚒

  • @khadjahmustafa8273
    @khadjahmustafa8273 10 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkkkkk koma iwe wamibawq iweee adzakukanganirana ndithu kkkkkkkkk koma ndaseka mpaka ntola nkhani kusowa omumvera

  • @langsonmndalanga
    @langsonmndalanga 10 หลายเดือนก่อน +1

    Amaudindo mmziwe mulungu 😢😢

    • @blandinabonaventure
      @blandinabonaventure 10 หลายเดือนก่อน

      Koma abale zoipa Mulungu amudziwedi

  • @user-md5uv2cg6i
    @user-md5uv2cg6i 10 หลายเดือนก่อน +1

    Dyela amalawi kafuneni ntchito iya

  • @GiftChadika-he7nd
    @GiftChadika-he7nd 10 หลายเดือนก่อน

    Inuyo ngati uli umphawi mmm nyamata iwe ndimaona ngat ulankhura zanzelu naweso ulibe nzeru ngat kuli kusauka yamban kugwira ntchito nanga milandu ya manda mmmmm

  • @lillahnmahuzahshabah5883
    @lillahnmahuzahshabah5883 10 หลายเดือนก่อน +1

    Mafumu akumalawi kudyera 😂

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 10 หลายเดือนก่อน

    Ambuye atithandize 😢😢

  • @gladyschisomo4324
    @gladyschisomo4324 10 หลายเดือนก่อน

    Unakumanana nazotu Abel kugugudidwa pachifuwa anatsala pang'ono kukumenya 😂😂😂😂😂

  • @austinvincent1264
    @austinvincent1264 10 หลายเดือนก่อน

    Iyiy nkhani inali ya simple koma chinyengo dyela

  • @user-hs6sh3xz1f
    @user-hs6sh3xz1f 10 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk afumu ati ndizivomela ene kkk

  • @freedommuyaka8597
    @freedommuyaka8597 10 หลายเดือนก่อน

    Zichitika mmasiku osiriza ndithu timva ndi kuona zinthu nthawi yakumapetoyi ndithu this is just a beginning

    • @JOHNSANGWALI-ox8mu
      @JOHNSANGWALI-ox8mu 10 หลายเดือนก่อน

      Not masiku osiliza blo zikoli lilipo mpaka kalekale

  • @user-ne1kt6hx5w
    @user-ne1kt6hx5w 10 หลายเดือนก่อน

    Mafumu dyera eishhh

  • @AnnettieChimwala
    @AnnettieChimwala 5 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 kumalawi nkokoma

  • @user-yj1nu6ij8m
    @user-yj1nu6ij8m 5 หลายเดือนก่อน +1

    Abel my vote 😂

  • @user-md5uv2cg6i
    @user-md5uv2cg6i 10 หลายเดือนก่อน +1

    Tizingo otchana izo zimatha malo

  • @anafiidie9058
    @anafiidie9058 10 หลายเดือนก่อน

    Mafumu anji olephera kulongosola nkhani bwinobwino

  • @marymuhahara791
    @marymuhahara791 10 หลายเดือนก่อน

    Next interview kwa a group a Dzenje plz tiwaone

  • @user-ip6pt3rw7f
    @user-ip6pt3rw7f 10 หลายเดือนก่อน

    kulakwa anyamataw sanalakwe kanthu olakwa ndi mafum

  • @josephkuseke4166
    @josephkuseke4166 10 หลายเดือนก่อน

    Manda si a mmudzi manda ndi banja. Dzenje tinakupezani

  • @user-br4xo5hc1f
    @user-br4xo5hc1f 9 หลายเดือนก่อน

    Akulu awa sakukwanitsa kufotokoza

  • @user-ks6fj4uk4i
    @user-ks6fj4uk4i 10 หลายเดือนก่อน

    A group zawavuta ndithu

  • @user-ws4ue7tf6j
    @user-ws4ue7tf6j 10 หลายเดือนก่อน

    Dyela rakulapo apa chinyengo amalawi nawoso police mulibe chilungamo bwanji kod?

  • @marykaunga-cm1dd
    @marykaunga-cm1dd 10 หลายเดือนก่อน

    Kumalawi mkokoma😂😂

  • @austinvincent1264
    @austinvincent1264 10 หลายเดือนก่อน +1

    Mfumu mayero zikuoneka kut ali ndukali mpake kufotokoza

  • @alicehananiya
    @alicehananiya 10 หลายเดือนก่อน

    Mfumu maelo ndi mbumba yanu mupeze Munda wanu ukhale Manda zooka malilo Minda ya anthu enazo ayi

  • @jamesngalande4345
    @jamesngalande4345 10 หลายเดือนก่อน

    Vuto lakula apa ndi umphawi ndikusowa chochita

  • @user-cg7ud2vq8k
    @user-cg7ud2vq8k 9 หลายเดือนก่อน

    Malawi tikapuma kumwamba😂😂😂😂

  • @KeneMike
    @KeneMike 10 หลายเดือนก่อน

    🎉😂

  • @charleskalajira380
    @charleskalajira380 10 หลายเดือนก่อน +1

    Big up Abel

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft 10 หลายเดือนก่อน

    A group ndi a TA onse ndi adyera

  • @anniewhite3497
    @anniewhite3497 10 หลายเดือนก่อน

    Gwirinzano unavuta apa😢

  • @user-md5uv2cg6i
    @user-md5uv2cg6i 10 หลายเดือนก่อน +1

    In Malawi know good leadership sense all of them theyre dogs😂😂

  • @khadibasilli4897
    @khadibasilli4897 10 หลายเดือนก่อน

    Cecilia, m

  • @highcallingglobalministries
    @highcallingglobalministries 10 หลายเดือนก่อน

    WACHIBWIBWI NAYESO KKKK

  • @mwanaishababes9630
    @mwanaishababes9630 10 หลายเดือนก่อน

    Poti tamva mbali imodzi

  • @mwanaishababes9630
    @mwanaishababes9630 10 หลายเดือนก่อน

    Ku Malawi kupuma kulibe

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 10 หลายเดือนก่อน

    Kkkkkkkk

  • @aaronmakuta911
    @aaronmakuta911 10 หลายเดือนก่อน +1

    Mwini nyumba akanangofukula ndiku yasa moto basi chichitike chichitike

    • @semusiliva4106
      @semusiliva4106 10 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂

    • @user-ks6fj4uk4i
      @user-ks6fj4uk4i 10 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂. Ineso ndikanatero

  • @ChikondiBanda-r4h
    @ChikondiBanda-r4h 23 วันที่ผ่านมา

    Banda samazaza

  • @MercyMulenga-pc3ow
    @MercyMulenga-pc3ow 3 หลายเดือนก่อน

    So bad

  • @khadjahmustafa8273
    @khadjahmustafa8273 10 หลายเดือนก่อน +1

    Nchifukwa chaketu ife tinaukana ufumuwo nkungoupatsa kea ena asaaaa kuphetsa izi. Nzachibwana aaaaaa

  • @JaffaSaidi-db6ic
    @JaffaSaidi-db6ic 10 หลายเดือนก่อน

    So bad

  • @khadjahmustafa8273
    @khadjahmustafa8273 10 หลายเดือนก่อน +1

    Nchifukwa chaketu ife tinaukana ufumuwo nkungoupatsa kea ena asaaaa kuphetsa izi. Nzachibwana aaaaaa