BILLY MALATA WATULUKA MCP NDIPO WAIKHADZULA MOSAONA NKHOPE KUTI ANALI MABWANA AKE 25 JANUARY 2025

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 3 ก.พ. 2025

ความคิดเห็น • 136

  • @LalaKhan-t9q
    @LalaKhan-t9q 9 วันที่ผ่านมา +4

    Chilipo akufuna iwo awa
    Ben ndi billy
    Alipo akufuna amusake iwo.

  • @MapataMohammed
    @MapataMohammed 8 วันที่ผ่านมา +5

    Usatuluke ukhale komweko

    • @WarriorKB-l3i
      @WarriorKB-l3i 6 วันที่ผ่านมา

      Kkkkk wamuza boh

  • @cmsanyama200
    @cmsanyama200 9 วันที่ผ่านมา +3

    Ma original activisists nonse mwawaona ma fishermen akuwedzani mukawagonekera khosi atumidwatu awa.

    • @edwinearlkachiwala3070
      @edwinearlkachiwala3070 9 วันที่ผ่านมา

      Billy Billy bwanji unkhale I we president mwina ziyenda chifukwa muli ndi nzerutu a malata

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 9 วันที่ผ่านมา +2

    Kodi Billy Malata munalikuti? Nthawi yonseyi mumasapota Chakwera ndi MCP yake, ndipo mwalankhula bwino kwambiri. Si unatenge mbali.100%.

  • @juliussamson6212
    @juliussamson6212 9 วันที่ผ่านมา +2

    TAKE CARE DPP NDI BILE MALATA

  • @louisgolden
    @louisgolden 9 วันที่ผ่านมา +2

    Too rate 😂😂😂 bon kalindo more fire simunthu wamba ameneuja🔥🔥🔥🔥

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u 9 วันที่ผ่านมา +2

    Achina boma ndlomweli mutipeza ku DPP simunati

  • @juliussamson6212
    @juliussamson6212 9 วันที่ผ่านมา +2

    BIlE MALATA AFUNA KUSENDERA PAFUPI NDI ANTHU A DPP

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 6 วันที่ผ่านมา +2

    Mr Namzimkambe is talking but he is talking nonsense and rubbish this guy is real monster devil himself

  • @CharlesSungani-j8c
    @CharlesSungani-j8c 6 วันที่ผ่านมา +2

    Anthuwa apangana akufuna akole ntanyiwa

  • @KettieNathaya
    @KettieNathaya 6 วันที่ผ่านมา

    Zoona aBilly Malata mwabwera pamodzi ndi ife aMalawi osauka?zikomo kwambiri ❤❤❤

  • @HotMilla
    @HotMilla 5 วันที่ผ่านมา +1

    I've ndi galu kwabasi, kagwere uko

  • @MarySinjirani
    @MarySinjirani 6 วันที่ผ่านมา +2

    Takumvani che malata koma chonde zimenezo muka walangizeko apa banja pako zikomo

  • @AlexKaunda-w7l
    @AlexKaunda-w7l 6 วันที่ผ่านมา +2

    KALINDO .NTANYIWA.BAKILI TV .NDI ENA NONSE MUSACHIKHULUPILIRE CHIGALU ICHI ANA AMA HULE AMATELO

  • @MercyKziphondo
    @MercyKziphondo 8 วันที่ผ่านมา +2

    Athu awa osawakhulupilanso chifukwa ndamene amatoza amthu iyeyu malatayu,Beni logwe,munlow anthu amenewa ndagalu mchende awoso

  • @juliussamson6212
    @juliussamson6212 9 วันที่ผ่านมา +2

    MUSAPUSE AI BILE MALATA SANATULUKE MCP MUSACHITE MASEWERA AI NDICHIDA CHA MCP

    • @LoyceChipwaila
      @LoyceChipwaila 9 วันที่ผ่านมา

      Ineso nkuonaso choncho ngakhaleso Ben Longwe akukaikitsa zedii

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u 9 วันที่ผ่านมา +1

    Adziona kuti aphedwa limodzi koma ayituluke
    DDP yikuwina ndichifukwa wayinyowa kuti afela limodzi kufa kwa MCP ndikumeneko

  • @ChrisPhiri-s2p
    @ChrisPhiri-s2p 8 วันที่ผ่านมา +2

    Billy malata pantumbo pako ukunamidza ndani panya pako galu iweee do u think we ar stupid as u think

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 9 วันที่ผ่านมา +2

    ABilly Malata mwalnkhula bwinotu lero nthawi yonseyi munali kuti?

  • @beakab2378
    @beakab2378 9 วันที่ผ่านมา +2

    We can never trust you Malata. Ukalamkhule lero? Never!

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mwayamba liti kuzindikila zimenezo kkkkk MCP anthu mwayamba kuzindika sopano mubwelako nonse by June MCP kuzasala Chimwendo ndi chikangawa Vinyo watha😂😂😂😂

  • @Harrsoni
    @Harrsoni 7 วันที่ผ่านมา +1

    Mmmmmm amalawi tilibenanu zochita mr

  • @Mavisbunny346
    @Mavisbunny346 5 วันที่ผ่านมา +1

    Wabodza uyu watumidwa musamale naye ziripo zomwe akufuna achite. Lero zoona zimenezi koma bambo ameneyu umunthu alibe umunthu. Sindingakhulupirire munthu wachipongwe.

  • @Harrychokanda
    @Harrychokanda 6 วันที่ผ่านมา

    Mbambande bwana billy malata....apa mwabwela ndi more 🔥🔥🔥

  • @AaAa-qy9id
    @AaAa-qy9id 8 วันที่ผ่านมา +2

    khuluku iwe ukumiza ndani

  • @ClementMunyolowa
    @ClementMunyolowa 5 วันที่ผ่านมา

    Kuteroku mwakonza imeneyo cholinga wina akole koma mtanyiwa kapena bakili muluzi TV simunga wapusise walembam,madzi

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 6 วันที่ผ่านมา +3

    Kod mkutulo kapena malodza munatchukatu inu lero zakuwawan ai zikomo khalan komko anzanu amenyera ufulu atopa inu munalikt?

  • @MaxwellChiwaya-i8q
    @MaxwellChiwaya-i8q 6 วันที่ผ่านมา +2

    APM Mulungu wamumenyera nkhondo yekha

  • @BeatŕiceMfundenji
    @BeatŕiceMfundenji 6 วันที่ผ่านมา +2

    Achina ntanyiwa ndi anzanu samalira ndi Billy Malata ndi pusi pusi ameneyu njoka muwudzu

  • @JusticeKawilira
    @JusticeKawilira 6 วันที่ผ่านมา +1

    Chenjera nawoni anthu ngati awa ndidzopangana izi ngati kuli kumenyera ufulu asiyeni okha osawayandikira chonde chonde😳

  • @GiftHaward
    @GiftHaward 9 วันที่ผ่านมา +2

    Bon kalindo ananena Kuti 2025 tiona zinthu

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs 9 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkk malata pantumbopako oipa iwe

  • @WarriorKB-l3i
    @WarriorKB-l3i 6 วันที่ผ่านมา

    Gyz tikamanena kuti mavuto ali dziko munowa sawona mtundu kapena chipani koma ndi a tonse a malawi tikamanena billy amaona ngati ife amisala lero sizi? Gyz vuto si billy koma mcp chifukwa imalemba anthu ganyu azinena zabwino zaiwo pamene pa ground palibe chikuchitika nde anyamatawa ayitutumuka awona kuti akungotaya nthawi chifukwa dzikoli palibe chikuenda.Uwuwu ndi umboni oti mcp yagwa chifukwa zomwe walankhulazi ndi zina zimene mcp yalephela kuchita tsoka ndilo nthawi yawo yatha alibe nthawi yoti angakoze zinthu panopa adzingopakila atilephela a malawi uyu amadzitcha kuti mcp boy nde walankhula zolephela kulephela kwa makolo ake, kumvomeleza kuti makolo ake alephela ife sititekeseka voti ndi a dad 💙💙💙💙💙💙❤❤❤❤❤ boma la a malawi

  • @Felie-p7l
    @Felie-p7l 9 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi bro ,munali kutiko thawi yosei mmene timavutikilamu ,mesa mumadyetsedwa mabazi ndiabwana anuwo

  • @AlexPhiri-in1re
    @AlexPhiri-in1re 9 วันที่ผ่านมา +2

    Ndiwaboza uyu osamum'vela

  • @MapataMohammed
    @MapataMohammed 8 วันที่ผ่านมา +2

    Pamtumbo pako Billy malata

  • @MphatsoChilangiza
    @MphatsoChilangiza 9 วันที่ผ่านมา +4

    A billy abilly abilly abilly pano mcp yaipa ayi khalani komweko ku mcp mwatidoda doda kenako nkumati mwathawamo kkkkkkkkkkk

  • @Gift-m4g
    @Gift-m4g 9 วันที่ผ่านมา +1

    Omwe akutukwanawa ndi aboma ndilomeli usadere khawa pitiliza

  • @dalitson3558
    @dalitson3558 5 วันที่ผ่านมา +1

    Person with no integrity, mulungu akungomenya nkhondo aliphe

  • @LukeMapukusa
    @LukeMapukusa 9 วันที่ผ่านมา +1

    😂😂😂😂 matchela awa ukodwa wekha msampha umenewo ufuna umukole Ntanyiwa ndi bakili muluzi tv wanya tikuponda tikakupeza wamva iwe billy 😂😂😂😂

    • @JustinWBanda
      @JustinWBanda 9 วันที่ผ่านมา

      Galu ameneyu kobasi akufuna amukole wina mosavuta aziti tili limozi kkkkkkk

  • @YasmeenYalabi-e8g
    @YasmeenYalabi-e8g 6 วันที่ผ่านมา +1

    Muli ngat njoka muudxu

  • @AyasiWhite-l6s
    @AyasiWhite-l6s 6 วันที่ผ่านมา +1

    Bodxa nkhumba imeneyi ikufuna kulimbana ndazake

  • @PatrickMangochi
    @PatrickMangochi 9 วันที่ผ่านมา +1

    Eni ake a Channel ichi ndi mbuli kwambiri, why are you lying kuti Malta watuluka Mcp? U may have more viewers but no subscribers

  • @MphatsoChilangiza
    @MphatsoChilangiza 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mesa inu a billy mumati muli mu boma momwemo mwaionera patali kuti azanu akatenga boma muzazuzika komano nthawi yatha mwachedwa bwana billy muzakhala oyamba kumangidwa tina kuikani kare kugulu la anthu oyamba kumangidwa tikasintha boma chonde musa tuluke Mcp bwelelani komweko abwana

  • @CharityChirwa-v8v
    @CharityChirwa-v8v 3 วันที่ผ่านมา

    Zaziiiiiiii nde ufuna kipudisa ndani

  • @JamesYassin-n7t
    @JamesYassin-n7t 9 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkk koma malata mwadya zaku mcp zatha apa mwaya kuukila ayi ambuye akuyendeleni

  • @fatsankapitikitsa
    @fatsankapitikitsa 8 วันที่ผ่านมา +2

    ayi chilipo apangana aw musamvele

  • @GreysonChilongo
    @GreysonChilongo 9 วันที่ผ่านมา +1

    Ben longwe ndimuzako Bill malata ndimwe agalu or dogs 🐕‍🦺🦮

  • @LuciusPatrick-f2c
    @LuciusPatrick-f2c 9 วันที่ผ่านมา +1

    Paja iwe pamutu pako sipamayenda bwino pakumumabe ngati pamwana ndi chifukwa chake sumaganiza bwino

  • @LukeshadrickShadrick
    @LukeshadrickShadrick 6 วันที่ผ่านมา +1

    Amalawi musqmumvere billy malata ndi wamisala komaso amutuma a mcp chikangawa

  • @lastonekaponya7675
    @lastonekaponya7675 9 วันที่ผ่านมา +1

    Udziwa kuti iweyo Ndiyimba kukalowa

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 8 วันที่ผ่านมา +1

    Malata chilipo akufuna atsusa kuti awone mavuto otsusa otsakhulipilila uyu ndigalu kwabasi

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 9 วันที่ผ่านมา +1

    Che billy malata mwatani sopano Kodi dziko likukhulupilireni bwanji?? Mesa inu ndi anyamata ojiya a chakwera?????

  • @MuhammadSamson-yz1kl
    @MuhammadSamson-yz1kl 9 วันที่ผ่านมา +1

    Iwe Malata ngati ukufuna chikhululuko ukandilimire mmunda

  • @JuweriaMussa
    @JuweriaMussa 6 วันที่ผ่านมา +1

    Nyambo iyi mesa pompano amati ntanyiwa tuluka aaaaa osamuvela

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 6 วันที่ผ่านมา

    Akutuma " WAMKULU BVUMBWE OTANTHA PA TSEKERA" khalani komweko muthandizane kumwa Magazi ndi mikodzo yo Mukamaliza muzanena. Momwe umatumbwira iwe muja ndani angakukhukupirire Mphyodza Magazi ndi mikodzo iwe, Munthu wokupha.
    Kadyeni Dzilope kuchikangawa KO. Akutumaonso ndi Mbuzi ngati iweyo . Ndiwe m'bututu wa MCP omwe amawugwiritsa Ntchito kutayiramo madzi Onunkha Dzuwa likalowa,ukachokako MCP idzikatayira Kuti Madzi Onunkha Dzuwa likalowa? Khalani komweko muzigwiritsidwa Ntchito ngati ma Tissue a Ku Chimbuzi.

  • @PAULMABVUTO-r9d
    @PAULMABVUTO-r9d 9 วันที่ผ่านมา +1

    Tisachedwe mapwalako malati

  • @ELLENZAPS
    @ELLENZAPS 6 วันที่ผ่านมา

    Mwala oyendayenda supeza ndele I trust kalindo ntanyiwa ndi bakili ndi ena osasunthika Koma enanu shupt

  • @Siter-m6y
    @Siter-m6y 9 วันที่ผ่านมา +1

    Akunamatu ameneyi, amutumatu uyu

  • @Noel-y6t
    @Noel-y6t 9 วันที่ผ่านมา +1

    Kape iwe

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel 7 วันที่ผ่านมา +1

    Mwayamba kuthawako ku chikangawako

  • @MussaWilliam-q3l
    @MussaWilliam-q3l 9 วันที่ผ่านมา +1

    Galu iwe wayamba liti iyeyo akufuna kupusisa anthu mutuwake

  • @AaliyaKalembo
    @AaliyaKalembo 9 วันที่ผ่านมา +1

    Ndalama zatha mukatelo koma Amalawi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

    • @JustinWBanda
      @JustinWBanda 9 วันที่ผ่านมา

      Vinyo watha 😂😂😂😂😂

  • @besterlumbe4404
    @besterlumbe4404 9 วันที่ผ่านมา +1

    Mutu otupawo

  • @GreysonChilongo
    @GreysonChilongo 9 วันที่ผ่านมา +1

    Agalu Inu

  • @AdyasiMaulana
    @AdyasiMaulana 6 วันที่ผ่านมา +2

    iwe ndi mbuzi ya munthu ukuganiza kuti mbwelela zakozi azikuvela ndani ma activis anakwana iwe get out

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 6 วันที่ผ่านมา +1

    Kanyele uko iwee palibe amene angakumvele mbwekela zakozo, zimenezo uzikawauza akwanu and akwanu akenso opusa okhaokha ngat iwe coz ochenjera ngat ine pano sangamvele zopusa zakozo

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 9 วันที่ผ่านมา

    Tamia Ja akuyitanako usapiteko MCP Ndichakwela akufuna kukupha

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 9 วันที่ผ่านมา

    Malamgngizo abwino Mr Malata , though too late too ,nyengo yamala

  • @petertengani
    @petertengani 6 วันที่ผ่านมา

    Bodzatu lili, ndipo enanu ndithu tsiku lina mudzafera nazo ku tulo izi.
    Manyazi mulibe?.
    Tilipamoto.
    😆😆🤦🏽‍♂️❤️.

  • @joebrown1158
    @joebrown1158 7 วันที่ผ่านมา

    Attention to all freedom fighters! please don't listen to or not even to dare to do your things openly with this dog

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 6 วันที่ผ่านมา

    Iwe namachende iwee don't take us for granted, tinakutuluka kalekale limodzi ndi satana mzako ben longwe, munlo etc , ana anjoka asatana okudya manyi inuu, otimenyela nkhondo ife kuno kumalawi ndi ntanyiwa, bakili muluzi tv, bon kalindo, masautso banda, etc

  • @TysonMwenye
    @TysonMwenye 9 วันที่ผ่านมา

    Njira imene wadutsayi MALATA uchedwa nayo peza ina chifukwa ife amalawi ndife ooopsaaa kwambriii takuwelenga kale zofuna zako pati.Ndiwe kape sungakwanitse kuyandikilana KALINDO, NTANYIWA or BMTV.

  • @Costance-nf7ue
    @Costance-nf7ue 5 วันที่ผ่านมา

    Abilly malata inu mukufuna chani chiwa no da iwe tiye uko

  • @MarkoGangire
    @MarkoGangire 9 วันที่ผ่านมา +1

    Apm mwapepetura anthu awa

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 6 วันที่ผ่านมา

    Malata ukunena chilungamo 😂😂😂😂😂😂 ana onse otaika bweran ndthu😂

  • @mabvutomichaelpanagona1949
    @mabvutomichaelpanagona1949 6 วันที่ผ่านมา

    Iwetu usatipusitse billy malata mzeru zako tikuzidziwa ukufuna udzikamba zodzudzula boma akutuma ndi a MCP, cholinga chakuti ufukirane ndi mtanyiwa,wa bakili muluzi TV ndi enaose amene amadzudzula boma, nomse odzudzula boma musachimvele chitsiru chimenechi, kodi billy malata tanena zoona ukufuna kufotoza chiyani mau ako akupepuka sakulemelela, alibe weti, tsopano ine ndikuuze izi ndukutuma kuti upite kwa amene anakutumawo ukawauze kuti mzeru zathu zija azidziwa kuti ukufuna uyandikirane ndi amene amadzudzula boma amalawi adziwa akuti ndikagwele uko kutali mwana wa satana.

  • @ShayibuJames-f5q
    @ShayibuJames-f5q 9 วันที่ผ่านมา +1

    akunama akufuna wina wake amupeze mosavuta

    • @VioletSinthulo
      @VioletSinthulo 9 วันที่ผ่านมา +1

      Nane ndikuganiza chomcho akuona ngati gulu la mtanyiwa ndikalindo limuyandikila

    • @RuthChimangeni
      @RuthChimangeni 9 วันที่ผ่านมา

      Wachepa ameneyu

  • @MaxwellChiwaya-i8q
    @MaxwellChiwaya-i8q 6 วันที่ผ่านมา +1

    Iwe malata usapusitse amalawi

  • @StevenGJohn
    @StevenGJohn 6 วันที่ผ่านมา

    Inu suja munkasapota MCP ndi Chakwera ? lero ndiye mwatani komano mwachita bwino popeza mwazindikira

  • @InnocentKandaya
    @InnocentKandaya 9 วันที่ผ่านมา +1

    Awona kut boma sikuwapasa ndalama😂😂😂

  • @CharlesSungani-j8c
    @CharlesSungani-j8c 6 วันที่ผ่านมา

    Achitsilu inu mukuona ngati ungatipusise mwapangana yofoyila 😂😂😂 😮ngoooooo

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 8 วันที่ผ่านมา

    Yesani ulimi kaye, sizikumveka mfundo mulibe mbwelela zokhazokha

  • @pauljosephmakaula6835
    @pauljosephmakaula6835 6 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂 7 branches of government?????

  • @VictorMbewe-n1m
    @VictorMbewe-n1m 9 วันที่ผ่านมา

    Kodi kwatani Ku MCP kwanuko Ben longwe naye akutukwana mufuna mutauze Kuti Chan ifetu wathu ndi bon kalindo ndi ntanyiwa

  • @SamukLungu
    @SamukLungu 6 วันที่ผ่านมา

    Anamumana ndarama amene ndiye waying,arura

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 9 วันที่ผ่านมา

    Billy malata pamtumbo pako uzipusitsa zitsiru zimzako za mcp ndiwe munthu oipa kwambiri umuuzeso chakwera kuti pamtumbo pake

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 9 วันที่ผ่านมา

    A Billy Malata mwalankhulatu bwino lero.Abale munalikuti Abale nthawi yonseyi

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 9 วันที่ผ่านมา

    Namachende iwe malata ndi iwe benlongwe mapulani anu tawadziwa mukufuna adpp kuti mwakole chonde born kalindo ndi onse omenyela maufulu pls musamale ndi Ben logwe ndi biley malata Pali chimene akufuna anamachende amenewa

    • @MagieJames
      @MagieJames 9 วันที่ผ่านมา

      Iweyo umakhala ntwi yosaka ntanyika atakupma amcp iweyo ukuzembera ndani ife wathu nd kalindo bakiri muluz tv bwana ntanyiwa ntwi yonsei unali. KT galu umayenda nd chikangawa party

  • @JustinWBanda
    @JustinWBanda 9 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkk amwene ka koma uyu siomukhulupilila for now ndi zake Ben longwe alipo akumuzembelela atalephela njila zao zose 😂😂😂😂😂

  • @richardmahata5523
    @richardmahata5523 6 วันที่ผ่านมา +1

    Iwe ulibe mzeru oyenda ndi lupanga adzafa ndi Lupanga iweyo wasala pang'ono or Mfundo zako is useless and mfundo less

  • @MakupeWekha
    @MakupeWekha 9 วันที่ผ่านมา +1

    Tilibe nawe ntchito iwe

  • @steavejafali
    @steavejafali 9 วันที่ผ่านมา

    Lero limenero mukuyakhula zimenezo inu ausilu abilly zopusa

  • @McDonaldLucious
    @McDonaldLucious 8 วันที่ผ่านมา

    Adad chonde galu uyu okugwa khunyu uyu musamulandile ndi mbale wake ben Longwe agaluwa adikire kukalowa ndi chikangawa asathawe lero akhale komweko ndipo afere komweko chonde adad tikakukondani ife ana anu

  • @RelaxCool-dp9jn
    @RelaxCool-dp9jn 6 วันที่ผ่านมา

    Akunama ameneyu akufuna kupala maboza muzipani mwina azikhala ngati sali ku mcp koma alikomwekobe

  • @OdalaBanda-i9c
    @OdalaBanda-i9c 6 วันที่ผ่านมา

    Bwana malata apapa nde mwafika tilipambuyo panu

  • @Harrychokanda
    @Harrychokanda 6 วันที่ผ่านมา

    Ma passport a fake ..... chikangawa govt

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 9 วันที่ผ่านมา

    Billy mapazi ako

  • @InnocentKavalo
    @InnocentKavalo 9 วันที่ผ่านมา

    Mwezi onweuno mumanyoza ntanyiwa ndi wa bmz kut iwowo ndi opoila pano mwabwelaso mukunyoza mcp ife tiziti chani?

    • @lyiemanganjira9708
      @lyiemanganjira9708 9 วันที่ผ่านมา +1

      Awa atumidwa awa musankhulupilire

  • @PatrickBastion
    @PatrickBastion 9 วันที่ผ่านมา

    Wa chifufu uyu osamutengela😂😂😂😂😂😂😊