DALITSO KABAMBE CHIFUKWA CHANI ADATULUKA DPP.

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 38

  • @LovelyGalaxy-rb7yl
    @LovelyGalaxy-rb7yl หลายเดือนก่อน +7

    Ayende bwno mwana waukape Awona ngati akapeza upele ku UTM, KOMA AXIWE KUTI NDIMWANA PANDALE 😅😅😅

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj หลายเดือนก่อน +3

    ngani yankulla and yakt ankufunna nkumugulla ndi m c p nkoma saneena nkandu ankabambe

  • @user-lw4hw9ce4w
    @user-lw4hw9ce4w หลายเดือนก่อน +3

    APM akuzasosora aswiswiri onse awo achoke alibe meaning ku dpp

  • @ThomasChiwaya-qx9mf
    @ThomasChiwaya-qx9mf หลายเดือนก่อน +2

    Ine mau ambiri ndilibe kom Peter mulungu adalise amalaw tinaphuzir bas kut chikuni chachikulu chimasunga moto bas

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 หลายเดือนก่อน

    At this stage, we need to concentrate on National Interest and not political. Mavuto akula ku Malawi. Malawi must unite first to defeat MCP. That's top on the agenda. Politics ndi maudindo later.

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v หลายเดือนก่อน +1

    Kabambe wachita bwino akhale President wa UTM basi best wishes DK

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 หลายเดือนก่อน

    DPP my vote

  • @JayoneAmbitious
    @JayoneAmbitious หลายเดือนก่อน +1

    Kabambe apanga phuma peter anafunika awatenge akabambe kukhala vp wao after 2or 3 years akanapanga resin kuwasiila akabambeo km paokha sangawine

  • @lungisanishezi1023
    @lungisanishezi1023 5 วันที่ผ่านมา

    Pali ndale zoopsya dpp ndi a katundu,akudzaphatikizana dpp ndi utm

  • @OmegahThipa
    @OmegahThipa หลายเดือนก่อน

    Ngakhale anthu ambiri angayike maganizo awo motani, Ndichisankho chawo koma sikuti DPP ingagwedezeke palibe (APM 2025 boma akutenga

  • @gifttembo2306
    @gifttembo2306 หลายเดือนก่อน +1

    DPP ndiyochenjera akudziwa kuti utm ikhala pa mgwirizano ndi dpp and akufuna adzachithetse mphamvu chipani cha utm in the coming yrs. pomuika madalitso kabambe as vice president

  • @user-nj4ob8jw6y
    @user-nj4ob8jw6y หลายเดือนก่อน +1

    Mbabva iyiyi sidatuluke ku DPP, koma a Peter Mutharika amutuma kuti akayimile ku UTM cholinga ndichofuna kukatenga mabvoti a UTM kukapeleka ku DPP. Chonde a Malawi chenjerani

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 หลายเดือนก่อน

    Ameneyu ndi wandale. I don't believe he has left DPP. Why? Here is the reason: HE ENDORSED APM.

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p หลายเดือนก่อน +1

    Akufuna udindo wa uprezident

  • @adamu1287
    @adamu1287 หลายเดือนก่อน

    Komano kunena zoona kabambe simunthu wandale

  • @user-zo3bf3ec3g
    @user-zo3bf3ec3g หลายเดือนก่อน

    Muyendako bwino koko

  • @AndrewSimakweli
    @AndrewSimakweli หลายเดือนก่อน +1

    Akabambe si andale

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki หลายเดือนก่อน

    Sanalakwise Ali Malawi momuno kulikose kumene angalowele akatumikila amalawi

  • @user-dc7qq9yz3v
    @user-dc7qq9yz3v หลายเดือนก่อน

    Akamati mfulumila ndiumeneu

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly หลายเดือนก่อน

    Muononga dziko ndiinu amene achinyamata simuziwa chomwe mukuchita munasonkhana mu 2020 lero ndi izi mumazitenga ngat otsogola lero mukuzinzika

  • @user-hb2hr5oc9l
    @user-hb2hr5oc9l หลายเดือนก่อน

    vuto anthu ambili sakufuna kunthandiza Malawi Koma Kuba ndalama Za boma akakhala pa udindo

  • @bornface4786
    @bornface4786 หลายเดือนก่อน

    This is not a right time for the Kabambe to move we can he doesn't lo Malawi

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 หลายเดือนก่อน

    Kabambe anatuluka kalekale ku Dpp, the thing is iyeyu Ali ngati nankhumwa amafuna president komaso ndiwa phuma nde no wonder palibe move apa ndi APM koma iyeyu wafuna you can see ma meeting ambiri adpp samapitako.. Ayende bwino

  • @user-ml2vw1dc9c
    @user-ml2vw1dc9c หลายเดือนก่อน +2

    Achinyamata akutulula kamba koti APM sapeleka mpata kwachinyamata ndiye ataya chikhulupililo

  • @yasitafuphiri-nw2he
    @yasitafuphiri-nw2he หลายเดือนก่อน

    This is a plot for DPP 😢, APM will make him his running mate
    Kutuluka DPP ,kudzagwiranso ntchito ndi DPP yomweyo😮?? Pali nzeru apa??

  • @AntonyEdwinMuyila-ij4sx
    @AntonyEdwinMuyila-ij4sx หลายเดือนก่อน

    There is no future for the youth in Dpp.

  • @user-vl8uw8mc3u
    @user-vl8uw8mc3u หลายเดือนก่อน

    Kuthamangila udindo.saphulapo kanthu awa

  • @ChrisEnos-to5uv
    @ChrisEnos-to5uv หลายเดือนก่อน +1

    Uyu sanatuluke ku Dpp achita kumutuma

  • @user-bp1cu2rb4f
    @user-bp1cu2rb4f หลายเดือนก่อน

    Kape iwe:Palibe chomwe uli.Galubwakoooo.Kachipanda ka peter bwenzi ulingati ndani?

  • @user-bz4fs6gv8v
    @user-bz4fs6gv8v หลายเดือนก่อน

    Uyu amutuma serious

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj หลายเดือนก่อน

    Kuba bas ndizimene akufuna anthu kufinya mukaka ng'ombe yakuwanda kare

  • @JustineAdani
    @JustineAdani หลายเดือนก่อน +1

    y⁷

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di หลายเดือนก่อน

    MOTi ku UTM kulibe oti angaimile u president? Zikukhala bwanji?
    UTM say NO to Kabambe ( UTM presidency).

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o หลายเดือนก่อน

      Musavutike wakuuzani ndani zomwe mukunenazo

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o หลายเดือนก่อน

      Aliko kabambe akutaya nthawi uyo

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b หลายเดือนก่อน

    Let just Mary chilima stand guys to heal the heart s of Malawi

  • @user-nj4ob8jw6y
    @user-nj4ob8jw6y หลายเดือนก่อน

    Kabambe ndiwe mbabva wakuba. Udaba ndarama zambiri, zankhani nkhani. If u think that u r clever, Ukunama. U will never become president of UTM, never. Ndiwe mwana wa ng'ono pa ndale ku Malawi kuno.