At this stage, we need to concentrate on National Interest and not political. Mavuto akula ku Malawi. Malawi must unite first to defeat MCP. That's top on the agenda. Politics ndi maudindo later.
DPP ndiyochenjera akudziwa kuti utm ikhala pa mgwirizano ndi dpp and akufuna adzachithetse mphamvu chipani cha utm in the coming yrs. pomuika madalitso kabambe as vice president
Mbabva iyiyi sidatuluke ku DPP, koma a Peter Mutharika amutuma kuti akayimile ku UTM cholinga ndichofuna kukatenga mabvoti a UTM kukapeleka ku DPP. Chonde a Malawi chenjerani
Kabambe anatuluka kalekale ku Dpp, the thing is iyeyu Ali ngati nankhumwa amafuna president komaso ndiwa phuma nde no wonder palibe move apa ndi APM koma iyeyu wafuna you can see ma meeting ambiri adpp samapitako.. Ayende bwino
Kabambe ndiwe mbabva wakuba. Udaba ndarama zambiri, zankhani nkhani. If u think that u r clever, Ukunama. U will never become president of UTM, never. Ndiwe mwana wa ng'ono pa ndale ku Malawi kuno.
Ayende bwno mwana waukape Awona ngati akapeza upele ku UTM, KOMA AXIWE KUTI NDIMWANA PANDALE 😅😅😅
ngani yankulla and yakt ankufunna nkumugulla ndi m c p nkoma saneena nkandu ankabambe
APM akuzasosora aswiswiri onse awo achoke alibe meaning ku dpp
Ine mau ambiri ndilibe kom Peter mulungu adalise amalaw tinaphuzir bas kut chikuni chachikulu chimasunga moto bas
At this stage, we need to concentrate on National Interest and not political. Mavuto akula ku Malawi. Malawi must unite first to defeat MCP. That's top on the agenda. Politics ndi maudindo later.
Kabambe wachita bwino akhale President wa UTM basi best wishes DK
DPP my vote
Kabambe apanga phuma peter anafunika awatenge akabambe kukhala vp wao after 2or 3 years akanapanga resin kuwasiila akabambeo km paokha sangawine
Pali ndale zoopsya dpp ndi a katundu,akudzaphatikizana dpp ndi utm
Ngakhale anthu ambiri angayike maganizo awo motani, Ndichisankho chawo koma sikuti DPP ingagwedezeke palibe (APM 2025 boma akutenga
DPP ndiyochenjera akudziwa kuti utm ikhala pa mgwirizano ndi dpp and akufuna adzachithetse mphamvu chipani cha utm in the coming yrs. pomuika madalitso kabambe as vice president
Mbabva iyiyi sidatuluke ku DPP, koma a Peter Mutharika amutuma kuti akayimile ku UTM cholinga ndichofuna kukatenga mabvoti a UTM kukapeleka ku DPP. Chonde a Malawi chenjerani
Ameneyu ndi wandale. I don't believe he has left DPP. Why? Here is the reason: HE ENDORSED APM.
Akufuna udindo wa uprezident
Komano kunena zoona kabambe simunthu wandale
Muyendako bwino koko
Akabambe si andale
Sanalakwise Ali Malawi momuno kulikose kumene angalowele akatumikila amalawi
Akamati mfulumila ndiumeneu
Muononga dziko ndiinu amene achinyamata simuziwa chomwe mukuchita munasonkhana mu 2020 lero ndi izi mumazitenga ngat otsogola lero mukuzinzika
vuto anthu ambili sakufuna kunthandiza Malawi Koma Kuba ndalama Za boma akakhala pa udindo
This is not a right time for the Kabambe to move we can he doesn't lo Malawi
Kabambe anatuluka kalekale ku Dpp, the thing is iyeyu Ali ngati nankhumwa amafuna president komaso ndiwa phuma nde no wonder palibe move apa ndi APM koma iyeyu wafuna you can see ma meeting ambiri adpp samapitako.. Ayende bwino
Achinyamata akutulula kamba koti APM sapeleka mpata kwachinyamata ndiye ataya chikhulupililo
This is a plot for DPP 😢, APM will make him his running mate
Kutuluka DPP ,kudzagwiranso ntchito ndi DPP yomweyo😮?? Pali nzeru apa??
There is no future for the youth in Dpp.
Kuthamangila udindo.saphulapo kanthu awa
Uyu sanatuluke ku Dpp achita kumutuma
Kape iwe:Palibe chomwe uli.Galubwakoooo.Kachipanda ka peter bwenzi ulingati ndani?
Uyu amutuma serious
Kuba bas ndizimene akufuna anthu kufinya mukaka ng'ombe yakuwanda kare
y⁷
MOTi ku UTM kulibe oti angaimile u president? Zikukhala bwanji?
UTM say NO to Kabambe ( UTM presidency).
Musavutike wakuuzani ndani zomwe mukunenazo
Aliko kabambe akutaya nthawi uyo
Let just Mary chilima stand guys to heal the heart s of Malawi
Kabambe ndiwe mbabva wakuba. Udaba ndarama zambiri, zankhani nkhani. If u think that u r clever, Ukunama. U will never become president of UTM, never. Ndiwe mwana wa ng'ono pa ndale ku Malawi kuno.