Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 9 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b 21 วันที่ผ่านมา +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 21 วันที่ผ่านมา +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @EversDman
    @EversDman 20 วันที่ผ่านมา

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane 14 วันที่ผ่านมา

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya 20 วันที่ผ่านมา

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri 20 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 21 วันที่ผ่านมา +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g 20 วันที่ผ่านมา

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t 20 วันที่ผ่านมา

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu 21 วันที่ผ่านมา

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 20 วันที่ผ่านมา

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @AffickChaona
    @AffickChaona 17 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤❤❤

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 20 วันที่ผ่านมา

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael 21 วันที่ผ่านมา

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 20 วันที่ผ่านมา

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy 20 วันที่ผ่านมา

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d 21 วันที่ผ่านมา

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w 21 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l 20 วันที่ผ่านมา

    Awa ndie mawu

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 21 วันที่ผ่านมา

    Big up bro

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j 20 วันที่ผ่านมา

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 21 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 20 วันที่ผ่านมา

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg 21 วันที่ผ่านมา

    The DC 🔥

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 20 วันที่ผ่านมา

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 21 วันที่ผ่านมา

    Ambuye akudalitsen

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq 21 วันที่ผ่านมา

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie 20 วันที่ผ่านมา

    Motor 💥 kalindoooo

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x 19 วันที่ผ่านมา

    Zoona amwene

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js 20 วันที่ผ่านมา

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula 20 วันที่ผ่านมา

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg 21 วันที่ผ่านมา +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 20 วันที่ผ่านมา

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 20 วันที่ผ่านมา +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 20 วันที่ผ่านมา

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q 20 วันที่ผ่านมา

    Dc

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd 20 วันที่ผ่านมา

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x 21 วันที่ผ่านมา +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 21 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi 21 วันที่ผ่านมา

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @SmartMoles
    @SmartMoles 20 วันที่ผ่านมา

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 20 วันที่ผ่านมา

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton 20 วันที่ผ่านมา

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j 21 วันที่ผ่านมา

    Awuzeni

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 20 วันที่ผ่านมา

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 21 วันที่ผ่านมา

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m 20 วันที่ผ่านมา

    Ai zikomo 🥱

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa 20 วันที่ผ่านมา

    Dzelu zachepa kkkk

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 21 วันที่ผ่านมา

    Kalindo samaopa😂😂

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu 21 วันที่ผ่านมา

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v 20 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 20 วันที่ผ่านมา

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 20 วันที่ผ่านมา

    Ati kutitola kapena chani

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l 20 วันที่ผ่านมา

    Mumatiyimilila

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 21 วันที่ผ่านมา

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f 20 วันที่ผ่านมา

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr 20 วันที่ผ่านมา

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 21 วันที่ผ่านมา

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f 21 วันที่ผ่านมา

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 17 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k 21 วันที่ผ่านมา

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 21 วันที่ผ่านมา

    Bigiliman naweni

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 21 วันที่ผ่านมา

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do 21 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @AaronLitete
    @AaronLitete 20 วันที่ผ่านมา

    Kkkkk boma lopusa

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b 21 วันที่ผ่านมา

    😅😅😅😅

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 20 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 20 วันที่ผ่านมา

    😂😂 kung'alulatu

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i 21 วันที่ผ่านมา

    K.K😂

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k 20 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera 19 วันที่ผ่านมา

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro 20 วันที่ผ่านมา

    😂🤣😂🤣

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o 21 วันที่ผ่านมา

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @GiftKulture
    @GiftKulture 20 วันที่ผ่านมา

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j 21 วันที่ผ่านมา +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri 20 วันที่ผ่านมา

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 20 วันที่ผ่านมา

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 20 วันที่ผ่านมา

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n 21 วันที่ผ่านมา +1

    😂😂😂😂😂😂

    • @MadalitsoManyozo
      @MadalitsoManyozo 21 วันที่ผ่านมา +1

      😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 21 วันที่ผ่านมา

    😂😂😂😂😂