Bwana Ku Army Anyamata Anu Ndi Okwiya Kwambiri - Bon Kalindo
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 16 ต.ค. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo alleges that all is not well within the Malawi Military Establishment, as junior officers are reportedly unhappy with the reduction of their benefits and remunerations.
Ku Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo wati zinthu sizili bwino mu gulu la asitikali a Malawi, kamba koti akuluakulu achichepere sakukondwera ndi kuchepetsedwa kwa mapindu ndi malipiro awo.
#malawi
M, dani wamkulu ww MCP ndi Mr bakili muluzi tv ❤❤amene uja ndi shasha kuposa akalindo
Mr❤kalindo may God bless u all the time in Yesaya41v10,Yesaya54v17,fear not this is Democracy thank u very for reminding the oppositions
The DC 💪 always with you 💗
The DC president wa anthu osawuka 💪✊❤
A kalindo za MDF zilekani Waka ndivizeleza chomene is better iwe ngati ukaya command wa MDF panji ngati viwawa vya muno mu malawi ngati kulinje oloso ngati Dr chilima Andafwe Akalindo chiuta akutumbikani
Ndalama adula kumalipiro a Asirikali wo akufuna akagulire zida zokaphera Anthu Ku Chikangawa. Mukutchukatu Chikangawa boys, Kuba Za Amalawi ndi kupha . Anthu opanda Chisoni Komanso opanda manyazi ⚒️👹👹
Athanenazo aku army ulemu kwambiri bwana chigawa sanafunetu chibwana nthawi ya kamuzu
That's only commander we hard our history genaral manken chigawa he was true lead who sacrifice to us malawians to deal with pioneer
Ati asaaa
ASILIKALIOTU AKUYENERA AZIONE CHIFUKWA NDI ZITSIRU ZA ANTHU KWAMBIRI MENE CHAKWERA AKUCHITIRA PANO WAONONGERA DZIKO AKUBERA NDALAMA ZA BOMA ZOMSEZO ASILIKALI AKUNGOTI NDWIIIII AKANAKHALA MAIKO ENA ATAMUKHAZIKA KALE CHAKWERA PANSI KOMA AWA AMAOMBERA MANJA CHIKANGAWA , NDIYE LERO NDI IZII AKUWALOWERANSO KU BARACKS KUMAKAWAPHA MALO MOONETSA NKWIYO.ALI CHETE AZIONA
Mumayesa abon kalindo koma anthuwa samava,akhapanaso kubaracks ko kkkkkk
akalindo kuyesesa ndiye mukuyesesa kulangiza koma mmmmm chakwela ndi galu ndithu
👍💪💞🇿🇦
Masalimo 118:17:18
😢mavuto alipo ndithu
The DC 🎉🎉🎉
Ingoyambika bas
Eti esh kk
Inde bwana zoonadi
Yesaya 54:17
Mwina chifukwa analanda futi kona aadula kkkk
Anthuwa Nd a nonsense km
za ziiiii
Akuti charakwe😂😂😂😂😂😂
Chonena ndiribe
Kkkk ayambilatso yokakamidza anthu kuti adzipeleka mphatso mowawumilidza iiii koma sidzatheka basi oo
DC sazatheka😂😂😂😂😂
Bwana wathu🎉🎉
The Dddddddd Ccccccccccc
Aaaa chakwela olephela uyu chisilu ndi MCP yakeyo atadzuza amalawi
You are lying,
Mmmm