Bwana Ku Army Anyamata Anu Ndi Okwiya Kwambiri - Bon Kalindo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 16 ต.ค. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo alleges that all is not well within the Malawi Military Establishment, as junior officers are reportedly unhappy with the reduction of their benefits and remunerations.
    Ku Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo wati zinthu sizili bwino mu gulu la asitikali a Malawi, kamba koti akuluakulu achichepere sakukondwera ndi kuchepetsedwa kwa mapindu ndi malipiro awo.
    #malawi

ความคิดเห็น • 32

  • @BishopMaxwell
    @BishopMaxwell 2 หลายเดือนก่อน

    M, dani wamkulu ww MCP ndi Mr bakili muluzi tv ❤❤amene uja ndi shasha kuposa akalindo

  • @Richardbanda-hg6pt
    @Richardbanda-hg6pt 2 หลายเดือนก่อน

    Mr❤kalindo may God bless u all the time in Yesaya41v10,Yesaya54v17,fear not this is Democracy thank u very for reminding the oppositions

  • @AufiThera
    @AufiThera 2 หลายเดือนก่อน

    The DC 💪 always with you 💗

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 หลายเดือนก่อน

    The DC president wa anthu osawuka 💪✊❤

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 2 หลายเดือนก่อน

    A kalindo za MDF zilekani Waka ndivizeleza chomene is better iwe ngati ukaya command wa MDF panji ngati viwawa vya muno mu malawi ngati kulinje oloso ngati Dr chilima Andafwe Akalindo chiuta akutumbikani

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 2 หลายเดือนก่อน

    Ndalama adula kumalipiro a Asirikali wo akufuna akagulire zida zokaphera Anthu Ku Chikangawa. Mukutchukatu Chikangawa boys, Kuba Za Amalawi ndi kupha . Anthu opanda Chisoni Komanso opanda manyazi ⚒️👹👹

  • @HassanTmasuku
    @HassanTmasuku 2 หลายเดือนก่อน +1

    Athanenazo aku army ulemu kwambiri bwana chigawa sanafunetu chibwana nthawi ya kamuzu

    • @zubairsantoschifomboti3604
      @zubairsantoschifomboti3604 2 หลายเดือนก่อน

      That's only commander we hard our history genaral manken chigawa he was true lead who sacrifice to us malawians to deal with pioneer

  • @Dellingsmunthali
    @Dellingsmunthali 2 หลายเดือนก่อน

    Ati asaaa

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 หลายเดือนก่อน

    ASILIKALIOTU AKUYENERA AZIONE CHIFUKWA NDI ZITSIRU ZA ANTHU KWAMBIRI MENE CHAKWERA AKUCHITIRA PANO WAONONGERA DZIKO AKUBERA NDALAMA ZA BOMA ZOMSEZO ASILIKALI AKUNGOTI NDWIIIII AKANAKHALA MAIKO ENA ATAMUKHAZIKA KALE CHAKWERA PANSI KOMA AWA AMAOMBERA MANJA CHIKANGAWA , NDIYE LERO NDI IZII AKUWALOWERANSO KU BARACKS KUMAKAWAPHA MALO MOONETSA NKWIYO.ALI CHETE AZIONA

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 2 หลายเดือนก่อน

    Mumayesa abon kalindo koma anthuwa samava,akhapanaso kubaracks ko kkkkkk

  • @savinapili7185
    @savinapili7185 2 หลายเดือนก่อน

    akalindo kuyesesa ndiye mukuyesesa kulangiza koma mmmmm chakwela ndi galu ndithu

  • @GreenBadani
    @GreenBadani 2 หลายเดือนก่อน

    👍💪💞🇿🇦

  • @Sarahmuskambo
    @Sarahmuskambo 2 หลายเดือนก่อน

    Masalimo 118:17:18

  • @AbdullahaziziAmoswalala
    @AbdullahaziziAmoswalala 2 หลายเดือนก่อน

    😢mavuto alipo ndithu

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 2 หลายเดือนก่อน

    The DC 🎉🎉🎉

  • @PatrickMulangala-os4by
    @PatrickMulangala-os4by 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ingoyambika bas

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 2 หลายเดือนก่อน

    Inde bwana zoonadi

  • @Sarahmuskambo
    @Sarahmuskambo 2 หลายเดือนก่อน

    Yesaya 54:17

  • @IreenChilingulo
    @IreenChilingulo 2 หลายเดือนก่อน

    Mwina chifukwa analanda futi kona aadula kkkk

  • @AufiThera
    @AufiThera 2 หลายเดือนก่อน +1

    Anthuwa Nd a nonsense km

  • @georgelupiya1313
    @georgelupiya1313 2 หลายเดือนก่อน

    za ziiiii

  • @Uladimbwana-fr9ev
    @Uladimbwana-fr9ev 2 หลายเดือนก่อน

    Akuti charakwe😂😂😂😂😂😂

  • @SackinaMachemba
    @SackinaMachemba 2 หลายเดือนก่อน

    Chonena ndiribe

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkk ayambilatso yokakamidza anthu kuti adzipeleka mphatso mowawumilidza iiii koma sidzatheka basi oo

  • @MussaAsibambo
    @MussaAsibambo 2 หลายเดือนก่อน

    DC sazatheka😂😂😂😂😂

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o 2 หลายเดือนก่อน

    Bwana wathu🎉🎉

  • @james-zd2nz
    @james-zd2nz 2 หลายเดือนก่อน +1

    The Dddddddd Ccccccccccc

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 2 หลายเดือนก่อน

    Aaaa chakwela olephela uyu chisilu ndi MCP yakeyo atadzuza amalawi

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 2 หลายเดือนก่อน

    You are lying,