UTM,mapulezident awa mayi chirima, mwana wachilima , Brayani Banda UTM awa ndi mapulesident a malawi, mukawasiya awa chipani chapita ndimazi, kongo kabira analowa ali ndi 31 years mundinkhulupirire , yeremiya, davidi, anali ana kaliyati ankhale muzati wa UTM, BY BY
President Chakwera akanabwera ndi chipani china osati MCP , nichifukwa chake mbiri yakale ya MCP ikumukhuza, but instead of kutukwana a president let us pray for our country, kutukwana sikusintha zinthu guys,
Inu mudzikhala ndi manyazi ponena za covid....palibe anthu opasa manyazi ngati inu every statement of economics development....koma mukafuna Kuba ndalamazo Palibe za covid anthu onyansa mitima
UTM president Tikufuna brian banda wisy man
Chakwela asowe fiti yothelatu UTM ganizani mofasa musakonde ndalama kumbukani tsogoleli wanu chilima upangili omwe analinawo sitikufuna kuti kupita kwachilima ndizinalake lithe ayi mukuziwabwino zomwe amafuna chilima still I remember S K C ambuye sungani mizimuyawo 😭😭😭💔💔💔
Chakwera pamtumbo pakę anaba ndalama za fertilizer asamatipusitse azipusitsa zitsiru zake zomwezo
Malawi is lacking good leadership that's why is the poorest country in the world.
Chakwela satana wohipa ziko lamu nyeraaa
Asamango namidzila covid19
UTM,mapulezident awa mayi chirima, mwana wachilima , Brayani Banda UTM awa ndi mapulesident a malawi, mukawasiya awa chipani chapita ndimazi, kongo kabira analowa ali ndi 31 years mundinkhulupirire , yeremiya, davidi, anali ana kaliyati ankhale muzati wa UTM, BY BY
Ayi kabira analowa Ali ndi28
Tikufuna Timothy mtambo
Fredo yomweyo
Am still worried about Chilima, Chakwela Anapaga Zolakwa Kwambili, Sangamuphe Munthu Chonchija
Kwambiri ndipo ine zimandiwawa mpaka lero pano bwenzi chilima atatiyankhula zokhuza comvension imeneyi hmm😢
Chakwela mbuzi yamuthu
Big up brother man!!
😢😢😢😢Hey
chakwera asanamizire zimenezo chakwera ndi chitsiru chamunthu chigawenga
Mwakweza ferteleza tsopano mukuti tizigwilitsa ntchito manyowa ayi zikomo Bola la chakwera
Adah iweyo Bass limenero bwanji Koma?????
President Chakwera akanabwera ndi chipani china osati MCP , nichifukwa chake mbiri yakale ya MCP ikumukhuza, but instead of kutukwana a president let us pray for our country, kutukwana sikusintha zinthu guys,
Mukufuna kt azaimile chifukwa mukuziwa kt Ali ndi mphavu xokupha aliyese odana ndichipanichi
Wathamanga kukasiya ma pepela opikisana nawo pa udindo wapulezidenti chifukwa akudziwa kuti munthu yekhayo amene akanalimba mtima kuti apikisane naye wamupha kale (Chilima)changucho sichina koma kusangalala
Mwalephera kuyendetsa boma osanyengezela COVID 19
Covid 19 mupaka liti bwanji simukufuna kuvomereza kuti mwalemphera
Mwalephera osanyeng ezela COVID 19
Chakwela akangokhala pamupando basi mcp yathela pomwepo ndithu galu uyo wakupha achoke
Komas osamanena kt covid 19 wasokoneza kd matendawo anagwela ife tokha komwe zinayambilako zithu zikuyenda bwanji
Zaboza zimenezo kugwa kwa kwacha nanga. Zautsilu bas
Covid 19 mpaka liti kod akuba inu
Hahaha covid
Patumbo pake chakweyo nyelo wake
Mmene anayambila za covid Muja mpaka liti
Pongopha Chilima uja basi, Chakwera waluza, Chakwera must go
Inu mudzikhala ndi manyazi ponena za covid....palibe anthu opasa manyazi ngati inu every statement of economics development....koma mukafuna Kuba ndalamazo Palibe za covid anthu onyansa mitima
MCP ndiyakupha
Patumbo pako chakwela
Utm uchitsiru mmmm
Blaming covid 19 mpaka pano? Abusa aku bagamoyo alibe nzeru za usogoleri
Next time go straight to the point,Tizionera Zama parish Mmalo mwa za UTM
UTM BALIBE MUGWILIZANO MAONA NONKHA AYIMASO AZANU AJA MAYI CHIRIMA KAPENA MWANA WACHIRIMA AYIME AMENE AGWILE NCHITO NDINU MAMUZUNGULILA KABILA 31 ANALOWA UPULESIDENT MUWINO MUSAKAYIKE MUKAPHONYA APO BRAYANI BANDA, MUKASIYA AWA CHIPANI MALUZA.
Mayi chilima ayime basi atha kuwina
🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Mapwala abambo ake chakwelayo
MCP moto kuti buu patsogolo ndi Chakwera olo mutukwane zopanda phindu izo mutopa nokha
Za ziiiii basi
Misala etiii
Mukhaulatu inuyo ndipo simunatiii MCP mpakampaka
I wish Timothy Ntambo alowe UTM party to mlowamumalo a later president SCK
Kkkkkk koma MCP kovid Wake uti shame on you anthu adayamba bwino kuvala buluku ndiye abwelerenso kupampaz 😂😂 you are not serious bullshit
A MCP chimene chikwalimbitsa mtima ndichani?
M.C.P kudzungulira mutu ndikuzabela ma vote ndi zimene zikuwalimbitsa mtima
Kkķkk kupha kuba ndi nkhaza bro zomwe zikuwalimbitsa kulimba mtima ndipo mcp sidzawinanso
Kkķkk kupha kuba ndi nkhaza bro zomwe zikuwalimbitsa kulimba mtima ndipo mcp sidzawinanso
Ndpo inu zikudabwisatu
2025 ambuye MULUNGU akukasesa ku state house
Kovidi inali ku malawi kokha katangale ndi amenewakura mboma