AMENE ALOWE M'MALO MWA ACHILIMA KU UTM/ NKHANI

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 7 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 58

  • @BestonMakochera-qk4sz
    @BestonMakochera-qk4sz 12 วันที่ผ่านมา +2

    UTM president Tikufuna brian banda wisy man

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 12 วันที่ผ่านมา

    Chakwela asowe fiti yothelatu UTM ganizani mofasa musakonde ndalama kumbukani tsogoleli wanu chilima upangili omwe analinawo sitikufuna kuti kupita kwachilima ndizinalake lithe ayi mukuziwabwino zomwe amafuna chilima still I remember S K C ambuye sungani mizimuyawo 😭😭😭💔💔💔

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 12 วันที่ผ่านมา +3

    Chakwera pamtumbo pakę anaba ndalama za fertilizer asamatipusitse azipusitsa zitsiru zake zomwezo

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q 12 วันที่ผ่านมา +2

    Malawi is lacking good leadership that's why is the poorest country in the world.

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 9 วันที่ผ่านมา

    Chakwela satana wohipa ziko lamu nyeraaa

  • @user-xu9rh1lm8o
    @user-xu9rh1lm8o 12 วันที่ผ่านมา +3

    Asamango namidzila covid19

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza 12 วันที่ผ่านมา +2

    UTM,mapulezident awa mayi chirima, mwana wachilima , Brayani Banda UTM awa ndi mapulesident a malawi, mukawasiya awa chipani chapita ndimazi, kongo kabira analowa ali ndi 31 years mundinkhulupirire , yeremiya, davidi, anali ana kaliyati ankhale muzati wa UTM, BY BY

    • @saadisadie3125
      @saadisadie3125 12 วันที่ผ่านมา

      Ayi kabira analowa Ali ndi28

  • @DanielVictor-pi5fj
    @DanielVictor-pi5fj 12 วันที่ผ่านมา +1

    Tikufuna Timothy mtambo

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 11 วันที่ผ่านมา

    Fredo yomweyo

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 12 วันที่ผ่านมา +1

    Am still worried about Chilima, Chakwela Anapaga Zolakwa Kwambili, Sangamuphe Munthu Chonchija

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o 12 วันที่ผ่านมา +1

      Kwambiri ndipo ine zimandiwawa mpaka lero pano bwenzi chilima atatiyankhula zokhuza comvension imeneyi hmm😢

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 9 วันที่ผ่านมา

    Chakwela mbuzi yamuthu

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 12 วันที่ผ่านมา

    Big up brother man!!

  • @TiyanjaneLuka-e2l
    @TiyanjaneLuka-e2l 9 วันที่ผ่านมา

    😢😢😢😢Hey

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 12 วันที่ผ่านมา +3

    chakwera asanamizire zimenezo chakwera ndi chitsiru chamunthu chigawenga

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3q 11 วันที่ผ่านมา

    Mwakweza ferteleza tsopano mukuti tizigwilitsa ntchito manyowa ayi zikomo Bola la chakwera

  • @goodwilljeza8419
    @goodwilljeza8419 12 วันที่ผ่านมา +1

    Adah iweyo Bass limenero bwanji Koma?????

  • @user-ii2sh1mz3r
    @user-ii2sh1mz3r 12 วันที่ผ่านมา

    President Chakwera akanabwera ndi chipani china osati MCP , nichifukwa chake mbiri yakale ya MCP ikumukhuza, but instead of kutukwana a president let us pray for our country, kutukwana sikusintha zinthu guys,

  • @MisheckNtanbalika
    @MisheckNtanbalika 12 วันที่ผ่านมา

    Mukufuna kt azaimile chifukwa mukuziwa kt Ali ndi mphavu xokupha aliyese odana ndichipanichi

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa6267 12 วันที่ผ่านมา +3

    Wathamanga kukasiya ma pepela opikisana nawo pa udindo wapulezidenti chifukwa akudziwa kuti munthu yekhayo amene akanalimba mtima kuti apikisane naye wamupha kale (Chilima)changucho sichina koma kusangalala

  • @user-sd3cl2dq7v
    @user-sd3cl2dq7v 12 วันที่ผ่านมา

    Mwalephera kuyendetsa boma osanyengezela COVID 19

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 12 วันที่ผ่านมา

    Covid 19 mupaka liti bwanji simukufuna kuvomereza kuti mwalemphera

  • @user-sd3cl2dq7v
    @user-sd3cl2dq7v 12 วันที่ผ่านมา

    Mwalephera osanyeng ezela COVID 19

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h 12 วันที่ผ่านมา

    Chakwela akangokhala pamupando basi mcp yathela pomwepo ndithu galu uyo wakupha achoke

  • @MisheckNtanbalika
    @MisheckNtanbalika 12 วันที่ผ่านมา

    Komas osamanena kt covid 19 wasokoneza kd matendawo anagwela ife tokha komwe zinayambilako zithu zikuyenda bwanji

  • @MkandawireKennedye
    @MkandawireKennedye 12 วันที่ผ่านมา

    Zaboza zimenezo kugwa kwa kwacha nanga. Zautsilu bas

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc 12 วันที่ผ่านมา

    Covid 19 mpaka liti kod akuba inu

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 11 วันที่ผ่านมา

    Hahaha covid

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g 12 วันที่ผ่านมา

    Patumbo pake chakweyo nyelo wake

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z 12 วันที่ผ่านมา

    Mmene anayambila za covid Muja mpaka liti

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 12 วันที่ผ่านมา +2

    Pongopha Chilima uja basi, Chakwera waluza, Chakwera must go

  • @user-em1qi8kj9h
    @user-em1qi8kj9h 12 วันที่ผ่านมา

    Inu mudzikhala ndi manyazi ponena za covid....palibe anthu opasa manyazi ngati inu every statement of economics development....koma mukafuna Kuba ndalamazo Palibe za covid anthu onyansa mitima

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 12 วันที่ผ่านมา

    MCP ndiyakupha

  • @user-nb8wg3fh4u
    @user-nb8wg3fh4u 12 วันที่ผ่านมา

    Patumbo pako chakwela

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f 12 วันที่ผ่านมา

    Utm uchitsiru mmmm

  • @HarryKandani
    @HarryKandani 12 วันที่ผ่านมา

    Blaming covid 19 mpaka pano? Abusa aku bagamoyo alibe nzeru za usogoleri

  • @phillipphiri2119
    @phillipphiri2119 9 วันที่ผ่านมา

    Next time go straight to the point,Tizionera Zama parish Mmalo mwa za UTM

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza 12 วันที่ผ่านมา

    UTM BALIBE MUGWILIZANO MAONA NONKHA AYIMASO AZANU AJA MAYI CHIRIMA KAPENA MWANA WACHIRIMA AYIME AMENE AGWILE NCHITO NDINU MAMUZUNGULILA KABILA 31 ANALOWA UPULESIDENT MUWINO MUSAKAYIKE MUKAPHONYA APO BRAYANI BANDA, MUKASIYA AWA CHIPANI MALUZA.

    • @user-ti9yk4eg2l
      @user-ti9yk4eg2l 11 วันที่ผ่านมา

      Mayi chilima ayime basi atha kuwina

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 12 วันที่ผ่านมา

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣

  • @user-kg5lf6bd1g
    @user-kg5lf6bd1g 12 วันที่ผ่านมา +1

    Mapwala abambo ake chakwelayo

  • @user-fh3dn8kt2j
    @user-fh3dn8kt2j 12 วันที่ผ่านมา

    MCP moto kuti buu patsogolo ndi Chakwera olo mutukwane zopanda phindu izo mutopa nokha

    • @user-ww9rj2wx8d
      @user-ww9rj2wx8d 12 วันที่ผ่านมา

      Za ziiiii basi

    • @user-vh3gq2tp2l
      @user-vh3gq2tp2l 12 วันที่ผ่านมา

      Misala etiii

    • @user-fh3dn8kt2j
      @user-fh3dn8kt2j 12 วันที่ผ่านมา

      Mukhaulatu inuyo ndipo simunatiii MCP mpakampaka

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 12 วันที่ผ่านมา

    I wish Timothy Ntambo alowe UTM party to mlowamumalo a later president SCK

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 12 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkk koma MCP kovid Wake uti shame on you anthu adayamba bwino kuvala buluku ndiye abwelerenso kupampaz 😂😂 you are not serious bullshit

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7q 12 วันที่ผ่านมา

    A MCP chimene chikwalimbitsa mtima ndichani?

    • @brainsmkumbwa6267
      @brainsmkumbwa6267 12 วันที่ผ่านมา

      M.C.P kudzungulira mutu ndikuzabela ma vote ndi zimene zikuwalimbitsa mtima

    • @user-xx4jb9se3z
      @user-xx4jb9se3z 12 วันที่ผ่านมา

      Kkķkk kupha kuba ndi nkhaza bro zomwe zikuwalimbitsa kulimba mtima ndipo mcp sidzawinanso

    • @user-xx4jb9se3z
      @user-xx4jb9se3z 12 วันที่ผ่านมา +1

      Kkķkk kupha kuba ndi nkhaza bro zomwe zikuwalimbitsa kulimba mtima ndipo mcp sidzawinanso

    • @EllahChikwatu
      @EllahChikwatu 12 วันที่ผ่านมา

      Ndpo inu zikudabwisatu

    • @user-xx4jb9se3z
      @user-xx4jb9se3z 12 วันที่ผ่านมา

      2025 ambuye MULUNGU akukasesa ku state house

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel 12 วันที่ผ่านมา

    Kovidi inali ku malawi kokha katangale ndi amenewakura mboma