Asilikaliwo amene akufalitsa bodzawo ndi a bodza ngati enanu bwanji sakupita ku court kukanena umboni wawo anthu mwazolowera ku pachika mayina a anthu apa cholinga wina ayipe inu mukome mukolola zomwezo bwanji osatchulako makolo anu mukunena anthu ena muferatu momwemo mu bodzamo ndiye pali phindu lanji zikuwoneka kuti ena 8 aja si anthu koma chilima basi kudafatu anthu enieni kunja kuno alikuti kili ziiii amapita kumanda nanga inu ndi ine mudzapita kuti kwa anthu andale kapena kumanda kumaganiza 😅😅😅😅😅 awa
Apite ku khoti for what? Timapereka umboni popanda mulandu? Ku khothi siku polisi tu tizidziwa zimenezo! Pakuyenera pakhale mulandu ndiye iyeyo nkukakhala mboni
@@DaeyangSonon ndiye siyani kulankhula zopanda umboni akutumani a ndale eti mukhalila yomweyio munthu anafa basi mwatsala inu ndi ine dzimvereni chisoni nanga bwanji asakatsegula mulanduwo mukungubwebweta pasi ngozi ya ndege mumayidziwa inu paja mkuyamba ku Malawi kuno eti ndiye ngoziyi yangokumaba ndi mbuli zomwe
Tathokodza potiudza koma usanapite machende ako bwanji unalolera kuti chilima afe chotelo iwe pokhala nsilikari nyini yamako and u chakwera nyini yamako😢😢😢😢 RIP Chilima
Wapha Kenako mkumayankhula za Mkutu apapa mapazi ndithu,,infact whats his name?? Killing VP just for 10 mita mmmmm it's a shame,,ndalama yot olo mansion sungamalize 😢
MA CADET MULI PA CHINTCHITO CHA SATANA MDYEREKEZI KWAMBIRI KOMA DPP CAN'T WIN BECAUSE OF PLANET CRASH OF VP. WE ARE STILL RECALL WHAT EVIL WORKS DPP HAS DONE TO INNOCENT BLOOD OF ALBINISM. GOVERNMENT VEHICLES WERE MISUSED TO AS POLITICAL PROPERTIES TO KILL THE OPPONENTS. SHAME ON YOU CADETS.
Boza ili, paja nvula ikagwa kuchuluka zoliralira, nanga ndege inachita kutela kapena kuphulisidwa? Mesa inagwa kusowa choyakhura eti amalawi tili ndi khwiyo pa ifa ya anthu amene aja ndiye osamatiuza boza ngati limeneri.
Simunati mutuluka mizimu ya anthu amene Aja ikudzuzani zedi ndipo muulurana wat is 10 million after all ndalama malo moyendesera dziko mukupangira uchigawenga inu agalu kwambiri.
Mulungu wanthu sazagona tulo mpaka mwazi wa anthu omwe anafa pa ndegeyi utaonesa Chilungamo Romand Catholic Les prayers so hard mpaka Mulungu atationesa choona
Jusas Iskariot anatumidwa ndi satana kukapha Yesu Christu osachimwa ndiye iwenso ndi mmodzi wa satanic wapha SKC ndi anthu ena mundege. Ndiwe munthu wovetsa chisoni ukuyenera kulapa machimo ako
Ambuye landilani mizimu ya abalewa amene mwawayitana kubwera Kwa Inu chitilani chifundo midzimu Yao pamozi ndi vice president Chilima Mulungu wamphamvuzonse landilani mizimu
Bwanji wangotchula kuti ukupezekera ku zomba Barack while ku zomba kuli air wing kuli cobbe kulinso changalume and rank number Yako sunatiuze and why sunanene early because iweyo izizi ndekuti unazidziwa zisanachitike nde utha kuwauza anthu za Zina zimenene zikufuna zitadziwidwa kuti zili pati and zinaenda bwanji anatenga ndi ndani mafuso ngati amenewa utha kuyankha?
Uyu akuyenera kutengedwa ndi akubanja akalongosole bwino ...chifukwa ali nawo mu gulu lakupha
Asilikaliwo amene akufalitsa bodzawo ndi a bodza ngati enanu bwanji sakupita ku court kukanena umboni wawo anthu mwazolowera ku pachika mayina a anthu apa cholinga wina ayipe inu mukome mukolola zomwezo bwanji osatchulako makolo anu mukunena anthu ena muferatu momwemo mu bodzamo ndiye pali phindu lanji zikuwoneka kuti ena 8 aja si anthu koma chilima basi kudafatu anthu enieni kunja kuno alikuti kili ziiii amapita kumanda nanga inu ndi ine mudzapita kuti kwa anthu andale kapena kumanda kumaganiza 😅😅😅😅😅 awa
Apite ku khoti for what? Timapereka umboni popanda mulandu? Ku khothi siku polisi tu tizidziwa zimenezo! Pakuyenera pakhale mulandu ndiye iyeyo nkukakhala mboni
@@DaeyangSonon ndiye siyani kulankhula zopanda umboni akutumani a ndale eti mukhalila yomweyio munthu anafa basi mwatsala inu ndi ine dzimvereni chisoni nanga bwanji asakatsegula mulanduwo mukungubwebweta pasi ngozi ya ndege mumayidziwa inu paja mkuyamba ku Malawi kuno eti ndiye ngoziyi yangokumaba ndi mbuli zomwe
ndipo apite akamange palibe zoti akunama ndizoona zinachitikadi
Eshiiii mulungu amakondwera ndi munthu ovomera tchimo lake inutu mwayamba bwino ingomalizani Kuti anthu tidziwe chowonadi
Tathokodza potiudza koma usanapite machende ako bwanji unalolera kuti chilima afe chotelo iwe pokhala nsilikari nyini yamako and u chakwera nyini yamako😢😢😢😢 RIP Chilima
Eeeee bosss
Ndaika muzimu wa malemu Chilima manja wa Mai maria. Proud katorika / Lusaka Zambia
Nzelu mulibe Mai maria atan
Inusotu ndinu abodza Inu, msilikali wake wakuti? Dzitchuleni dzina ndi unit yanu, msilikali ophunzitsidwa bwino angapange zimenezo ukukamba mlayiya iwe, umawudziwa uskali iwe?
Ali bado,akuyesa kwambirii
Mulungu amakanda munthu onena chilungamo iwe msilikali mulungu akukhululukile pazimenezi koma tikuthokoza ponena chilungamo usasiye pitabe chitsogolo oipa aoneke pa mbalambanda 😂😂😂😂😂
Tell us where is blackbox?
Only JAH knows....everyone shall get paid according to works he has done🔥
Udye ndalamayo usaope usachite matha nyani iwe unatani kuulura zisanachitike mwana wanjoka iwe
Iwe tiye uko vyaboza
Fake news
Example kenya , anthu aku kenya anasiya kupembeza boma lakuba ,
Ife amalaw wachuluka ndi umbuli .
Ndpo sukunama I don't kod mdziko mwathu mchan chnachtka ife tisakuchidziwa kut tiziona zinthu zikungochtka mosakhala bwno mkumangozisiila choncho bas
Pitani ku TIMES TV on live interview ndi Brian Banda amwene
Three mukanene
Bwerani poyera basi osaopa chilungamo chioneke 😭😭😭😭😭😭 ineyo
Ndiwa kk umudzi koma ndikumamva kuwawa ok Allah🤲🤲🤲 protect marawi prize
Limenelo ndi bodza lochita kupeka. Iweyo bewanji upite ku Police nkukaperekela umboni umenewo. Chimene ukuopa nchani? Wasowa chonena!
Olo zimakhala zoona sangamusiyesiye atanena komano ndioipa yekha atinanalandira ndalama
Kkkk kma zitakhala kut ndizoona police yake ya a yolamu
Bola kungoisunga mkhaniyo
Koma munalakwa kwambili munapha muthu ofunika kusiya zitsilu komaso ndale zophana zinatha kale kale kupusa kumeneko adzakuvoteleni ndi Amanu😢😢
Kabwezeni ndalama zo pemphelani pemphero lolapa lonsweka tima mulungu akukhululukirani mupite poyela kukabweza ndalamazo 😂😂😂😂😂
Eyaaa.apangedizomwezo
Malankhulidwe anu zikuonetsa kuti ngakhale 8 simunafike, mumagwira ngati ndani ku airport?
MUZIDZIWA MULUNGU.. ZITICHEDWERSA IZO. MUBWERETSE UMBONI MWACHANGU... TIMVE # YANUYO. YA ZOMBA. PRAISE GOD
Thanks for providing us you service
Eeee akulu akulu, ai bora.... tinkangova komaso kuwelenga KUT MCP ndiyakupha koma ai ndithu
Uchitsilu mukananena anthu asanafe ndinu m'Modzi mwakuphawo
Wapha Kenako mkumayankhula za Mkutu apapa mapazi ndithu,,infact whats his name?? Killing VP just for 10 mita mmmmm it's a shame,,ndalama yot olo mansion sungamalize 😢
Akulu zopanda nzeru izi.
MA CADET MULI PA CHINTCHITO CHA SATANA MDYEREKEZI KWAMBIRI KOMA DPP CAN'T WIN BECAUSE OF PLANET CRASH OF VP.
WE ARE STILL RECALL WHAT EVIL WORKS DPP HAS DONE TO INNOCENT BLOOD OF ALBINISM.
GOVERNMENT VEHICLES WERE MISUSED TO AS POLITICAL PROPERTIES TO KILL THE OPPONENTS.
SHAME ON YOU CADETS.
Zopanda ntchito tonse timaziwa kuti tidzafa koma sitikuziwa mmene tingazafere
Zaboza ngat nkazi wako ndiwopemphera uma chitiranji zimenezo
Amalawife ndife mbuli , tikudikila john chilembwe azatimenyelenso ufulu
Ambuye akuyendere mwapaderadera kuti unene zoona zokhazokha.
Stop taking weed +Ambuye ntengeni Bro
Looking for 1M viewers
Eish desperation is real
Kkkk msilikalli opusa wapha nawo
Waboza kulankhula ngati wakurundi bwerani poyera kuti mumangidwe munthu oyipa iwe kumakapanga chiwembu
mukusowa zochita mmene mumvekeramu mungakhale ten million kulira ndi umphawi
Ndiwe chitsilu kwabas bwanji sukwatchula anzakowo nanga
Bodza ili, simsilikali uyu. Bodzatu silisowa kwa munthu wanzeru. Mvetsetsani zomwe akunena.
1. Sakunena kuti ndege inagwa bwanji
2. Asilikaliwo anadziwa bwanji kuti ndege igwera pano
3. Akuti ndege itagwa inaphulisidwa. Ndege ingaphulisidwe koma osayaka?
Mfundo zokhazi ndizokwanira kupeza kuti munthuyu ndiwabodza. Mbuli ndi zitsiru zokha ndizomwe zitakhulupirire pakuti bodza limakoma mkhutu la chitsiru.
Sakupita kukhoti ndimaumboni awowa bwanji
Why is the government busy ku anga a Kaluw kusiya athu ngati a wawa why
iweyotu ukunama ndipo palibepo chikumveka panfundo zakozo usanamize ndipo usasokoneze anthu ndi bodza lakolo
Boza ili, paja nvula ikagwa kuchuluka zoliralira, nanga ndege inachita kutela kapena kuphulisidwa? Mesa inagwa kusowa choyakhura eti amalawi tili ndi khwiyo pa ifa ya anthu amene aja ndiye osamatiuza boza ngati limeneri.
Zowona ndiye ndiziti malume?
@mishecksipolo71 mukavele yomwe watumiza lero mukhulupilila kuti ndiwaboza apa anati ndimusilikali anali kuchikangawa lero akuti anajambula dege ndiyeyo ku airport amalawi tiyeni tiseguke chonde anthu azikusewelesani chochi koma ambuye amukhululukile sakuziwa chomwe akupanga
Zikundimvekela ngati zaboza mukufuna kungotipusisapo
Asilikari mukutani mukurephsra ntchito yanu nanga zinthu zikuonon geka mukungoyanganira
Vuto mumandira ndarama basi zoteteza anthu mwayiwara anzanu asilikari akunja akanachitapo kanthu
1993 pa Operation Bwezani panari General Manken Chigawanbwenzi izi kulibeko anali olimba mtima komanso okhurupirka kt agwira ntchito kuteteza anthu a dzimo lza Malawi osati chipani
Simunati mutuluka mizimu ya anthu amene Aja ikudzuzani zedi ndipo muulurana wat is 10 million after all ndalama malo moyendesera dziko mukupangira uchigawenga inu agalu kwambiri.
Chomwe mukuopa kut umbon ngat umenewu kukapereka poyera mukuopa andare coz aliyese Ali ndi mantha
Mulungu wanthu sazagona tulo mpaka mwazi wa anthu omwe anafa pa ndegeyi utaonesa Chilungamo Romand Catholic Les prayers so hard mpaka Mulungu atationesa choona
Mulungu salephela tidziwa zonse pompano mu ukulu wake alibe othandizana naye
Komano ngati ukunama iweyo kufuna kuipitsa mbiri ya anzako ,ndikukutembelera komanso kulengeza matenda oopsa ndipo udzazuzika ndi 3:23 nthenda yofa ziwalo,ndipo sipapita zaka zimenezi zikuchitikila by fire by force,,, komano ngati ukunena zoona ambuye akudalitse ndikukutetezera 3:23 3:23
Kampeni silikaliyu ku zomba umboni wokwanila uwu
Ngati ukufuna kukhululukilidwa,bwerani poyera.
Kupusa kwako galu iwe mxiiiii😢
Ng'alula iwe😭
10 mita kupha munthu za Bodza ngat izi 😂😂
Amalawi chakwela ndindani kuti azunze malawi nde silikaliwe pita ukasume live pulumutsa malawi
BOMA Linapha CHILIMA full Stop 🛑 .
Koma zovesa chisoni kwambiri kumpha anthu wosalakwa chifukwa chandalama Koma ndi zoonadi Kuti pamene pamphedwa munthu osalakwa mulungu amaulula zitsitsi. Zobisika 🙆🙆🙆🙆💔💔💔😭😭😭😭
Jusas Iskariot anatumidwa ndi satana kukapha Yesu Christu osachimwa ndiye iwenso ndi mmodzi wa satanic wapha SKC ndi anthu ena mundege. Ndiwe munthu wovetsa chisoni ukuyenera kulapa machimo ako
Sunanene dzina lako bwanji kodi maliro mukuona ngati chithu choseweretsa kod atakhala bambo ako ungakambe zopusa kumanama ngati ukudziwa kathu uli jufuna kusikoneza athu iwe ngati unapha ndiwe osapita ku police kukadzipereka uzilakhula zophwisa apa malilo mukuyesa zoseweretsa kod
Alakhulayo panyepake
Nde iweso uli mugulu lokuphalo
Tell us more about the death of chilima, wat else dd u c?
Ndikuzimva mwabodza
Komanso munthu uyu Pena kumumvesa ngati akunamatu chifukwa akanadzichula dzina
10million mungagule moyo wa munthu mulungu akukanthen nonse asasiyeko or modzi
Nde osangozitchula dzina ngat mukunena zoona bwanj. Ndege yoti inaphulitsidwa ingawoneke chonchija? Komaso ndege yoti inatela inganyenyeka chonchija? Campaign yabwanj kod tiyiwone chaka chinoyi mwati
Inuyo ngt mukunena zoona tazitchulani dzina koma zomangoyakhulazi aaa zosakhulupililika
Mm mm only God knows everything,continue rest in peace SKC
Mulungu akuddalitse chifukwa chonana chilungamo
Ambuye landilani mizimu ya abalewa amene mwawayitana kubwera Kwa Inu chitilani chifundo midzimu Yao pamozi ndi vice president Chilima Mulungu wamphamvuzonse landilani mizimu
Komat zombesa cisoni zinachitikazo ndithu kumupha munthu osarakwa bwanji
Wabodza uyu, palibe chilungamo pamenepi
Ngati mukufuna kutchuka muneneee
True this is nosense
AM PASTOR CHRIS PLEASE BROTHER GIVE THEM BACK THEIR MONEY,
Exactly esh
A mukanazitchula dzina ndikanakhulupila koma simunaziulule . Coz olo ine ndithanso kupanha audio yanga kunena kuti ndinali mmodzi owamakizitsa pamene kunalibe
Mukungofuna mupitilize kumatiliza tisiyeni mitimai ibweletemo
😅😅😅😅😅 bas mukakhuta uko muzipanga ma audio abodza aaaa tsek mbuzi dzawana
We wish you well🙏
Ndiwe mbuzi chitsiru iweyo ndichifukwa chiyani unalandila ndalama chosecho unali ndimaganizo okana ndiye kuti iweso unapha chifukwa iweyo ukanalorela ufe Koma achilima apulumuke
Galu wachabe chabe uyu iwe umakatani kuchikangawa kuchoka ku Zomba? Bwanji osanena nthawi yomwe ija anthu tikusowa Mtengo ogwira? Ukamanama chonchi ukupempha tsoka kwa mulungu
Ngati mukunena zoona kuti ndi nsilikali mukuyenera kukanena ku malo oyenera. Komaso munena bwanji kuti amalawi tisamale pomwe inu amene mumayang'anira za security of people mukupanga zimenezo? Kodi mesa olo anthu atapanga protest ndinu nomwe mutawapange chipongwe chifukwa cholandira ndalama
Ichi chawoneka kuti ndichaboza apa akuti ndimusilikali analikuchikangawa lero akuti amagwira ku air amajambula nthaawi yonyamuka ambuye akukhululikile ndithu
Tiutseni soona sandege live in the sauth Africa estan 😢😢
Thank you so much for replying me your welcome
Tell me all story from you soon side please I am Malawian
sanamalize ataiphulisamo anatani anene zonsetu mesa anakipo
Bwanji wangotchula kuti ukupezekera ku zomba Barack while ku zomba kuli air wing kuli cobbe kulinso changalume and rank number Yako sunatiuze and why sunanene early because iweyo izizi ndekuti unazidziwa zisanachitike nde utha kuwauza anthu za Zina zimenene zikufuna zitadziwidwa kuti zili pati and zinaenda bwanji anatenga ndi ndani mafuso ngati amenewa utha kuyankha?
Ngati mukunena zoona amwene ndinu opusa coz munakanika kupulumutsa miyoyo ya anthu ngati Inu nsilikali, panthawi imeneyo munkayang'ana za ndalama not moyo wamunthu.mukudziwa kuti infa za anthu amenewa zinatiwawa motani?idyani ndalamayo mpaka masiku a moyo wanu isadzathe
Iwe ndichitsilu opusa ngati ukunena zoona pita poyera kuti anthu aziwe, komaso bwanji osanena anthu asanafe ndiwe galu
Tabwelani poyela2 nanga mukulekelanj kuwulula?
Chakwera munthu wakupha uyo izi zayenera kuyamba ndinu bomwe asilikali.Mukusekelera zinthu zopusa kupha anthu amtundu wanu womwe mkwiyo wa Mulungu ukukanthani ndithu,Muuzane inuyo asilikali muyambe kukantha Lazaroyo ndi akubanja ake onse
Ndiwe chitsiru kwambiri mene umalandila ndalama kuti ukachitse dzimu wa azako umati iwe ndiokhalitsa dziko lino Ambuye akukatheni bambo ngati zomwe munena zili zoona ndipo muthadi
Munalakwisa kupha ose komanso ndiwe chisilu
Koditu ndizoziwika kale kuti chakwela anapha chilima
Zikomo kwambili chifukwa Cha kuzipeleka kwanu pofuna kulapa chimo lomwe munalomwamo chifukwa Cha anthu ena mulungu akuyang'anileni ndi kukutetezani kuti oyipayo asatengeko gawo pa inu
Chomwe ndingaphembe amalawi azanga tiyeni tiyime njiii ngati azathu aku Kenya tichose mbuzi imeneyi
Wow
Following 🙏
Mudatani kumuthawitsa osamupha inu asilikali zovetsa chisoni😂😂😂😂
NDIWE MUNTHU OPANDA CHIKONDI BWANJI SUNADZIWITSE NTHAWI YOMWEYO KUTI ANTHU APULUMUTSE MIYOYO YA ANTHU? KOMANSO IWEYO ULI NDI UMBONI OKWANIRA BWANJI OSAYITANA MABANJA OFEDWA NDIKUWAUZAKUTI TIYENI KU COURT NDIRI NDI UMBONI? MUNAPHANAWO CHIRIMA NDI ANZAKE,BAMBO MLANDU MULINAWO
Aaa 10 mita kandalama kochepachepa, kupha president kumafunika ma 50 mita
Uyu azakhala mboni 2025 likachoka boma lilipoli
Wa Dpp iwe
Nawe camba chakukwana, tinzakhulupilira ukapita ku khoti kukasuma mlandu wakupha, udye ndalama yo, ukananena time yomwe amakokedwayo😂 ndie kut iweso akanakupha, ndie ndipamene tikananziwa kut wafa bwanji pomwe ndege munakwela athu 9, iweo kukhala WA ten, zaziiiii
Vuto Kodi president ngati sakupanga zabwino osapanga Kuti achoke bwanji pa mpando
Koma Chakwera why? Achewa ndithu ndinu oipa ndawonela Chakwera koma mulungu akukantheni tikuona ndithu
Mabodza oyambanitsawa mumapindula Chani?
Ambuye akusamalireni ndipo akutetezeni