ZAYAMBA KUULULIKA TSOPANO / KWACHEMA KU MALAWI🙌🙌🙌🙌

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 15 พ.ค. 2024

ความคิดเห็น • 250

  • @user-ub1mw7ce5p
    @user-ub1mw7ce5p 15 วันที่ผ่านมา +8

    We need people like you in our country. The people guided by love, care, humanity, ❤❤❤❤❤. May Allah bless you sir, and the people who are with you.

  • @wilfredkazembe676
    @wilfredkazembe676 15 วันที่ผ่านมา +5

    Wow!! I like you guys first kumva amalawi akuyakhula chonchi public tatopadi amalawi tikusekedwa kwambiri tikamakhala mayiko eni wakewa good job guys

  • @MosesNdebele-kc2cp
    @MosesNdebele-kc2cp 15 วันที่ผ่านมา +10

    Zikomo Inu abungwe la CDED mulungu akuyendereni abwezedi. Anthu akufa ndi njala.awa utsogoleriu angogwelamo let's do it more fire

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 15 วันที่ผ่านมา +7

    Yeah! Apa ndiye anyera mapiko a Chakwera, saulukanso. Abweze ndalama za boma basi, asah!

  • @thomluciouss7360
    @thomluciouss7360 15 วันที่ผ่านมา +3

    Kkk I like the topic Malawians nowadays they are clever than before keep it up guys job well done

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 14 วันที่ผ่านมา +1

    This is type of people we need in our country

  • @user-ig5uf9pb3n
    @user-ig5uf9pb3n 14 วันที่ผ่านมา +1

    Much respect @ cded!
    Dese people works in iniquity, it's why dem nuh care about citizens
    Rastafari bless, Selassie I de first🤝

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o 15 วันที่ผ่านมา +1

    Thank u Mr Namiwa with ur true speaking

  • @DavidCainoiss
    @DavidCainoiss 15 วันที่ผ่านมา +9

    Zilikotu kkkkkk

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 15 วันที่ผ่านมา +2

    Amabungwe tithandizen chisankho chichitike ....may ..Abale osati september

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 15 วันที่ผ่านมา +2

    Chakwera ndiwamisala ngati Habakuku sinyangwe😂 , analonjeza kuti atakanika utsogoleri mu zaka ziwili he will resign pano chikukakamila

  • @MustapherLino
    @MustapherLino 15 วันที่ผ่านมา +1

    That's great message

  • @mcdonaldgerard9707
    @mcdonaldgerard9707 15 วันที่ผ่านมา +1

    Ndiye kuchepa nzelu kumeneko, tsiku lokumbukira kamuzu nkuikapo mau onyoza Mutharika, palibepo nzelu apa.

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 15 วันที่ผ่านมา +1

    Koma ndie anamukuwizadi mpakana kunali kuimba kuti achoke Chakwera achoke❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ iye alipompotu😂😂😂😂

    • @Pangolinimw
      @Pangolinimw 15 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 15 วันที่ผ่านมา

      @@Pangolinimw 😃😃😃😃😃😃😃😃Kunakomeramo mmmmmm ndipo akhaula zedi sanati campaign ikangotsegulidwa kukhala kumugenda koopsa ndiminyala sure 😃😃

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 15 วันที่ผ่านมา +1

    Kkkķkk good message ❤

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 15 วันที่ผ่านมา +5

    The DC must be a member of CDEDI also once is there,is going to be a fire🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 14 วันที่ผ่านมา

    Abwezedi ameneo chakwera ndi wawusilu ka amangopanga zinthu za uchisilu ngat kuti kamuzuyo pali cimene Malawi 🇲🇼 muno anapangapo

  • @PatrickChalimba
    @PatrickChalimba 15 วันที่ผ่านมา +1

    Uthenga wabwino ndithu ....koma angabwenze or kuyankhapo ???? Chifukwa kudzudzula Anthunu mukudzudzula but nothing changes

  • @SelemaniFred-rg9tt
    @SelemaniFred-rg9tt วันที่ผ่านมา

    Power the massage ❤

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk 14 วันที่ผ่านมา

    Powerful massage Namiwa!

  • @user-rd2td7bg4c
    @user-rd2td7bg4c 15 วันที่ผ่านมา +4

    Message the power❤❤

  • @PatrickChalimba
    @PatrickChalimba 15 วันที่ผ่านมา +2

    Tidziwa bwanj kut ndalama zabwenzedwa??? Nanga ngat sizibwemzedwa or kuyankhapo kanthu whats the next to benefit us

  • @PrinceThom-pe6ie
    @PrinceThom-pe6ie 15 วันที่ผ่านมา +2

    Tili ndi a malawi womwe akuvutika chifukwa cha umphawi ku Malawi ena akugona ndi njala ena akufa ndi njala wina ndikumatenga 90 million akuti kukumbikira galu wachabechabe kamuzu chigawenga chomwe chidapha ndi kuzunza makolo athu.

  • @JamesChiphole
    @JamesChiphole 15 วันที่ผ่านมา +5

    Chilungamo abweze sizikutikhudza

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 15 วันที่ผ่านมา

    More 🔥🔥🔥 we need people like you anthu akuvutika ndi njara ku mwalira kumene pomwe ndarama zikungowonongeka

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h 15 วันที่ผ่านมา +1

    Umakwana Mr Namiwa

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 15 วันที่ผ่านมา +4

    Inshort , Tonse alliance has come to finish MALAWl,
    Corruption is now on every where ,
    Corruption now is like culture & behavior of MCP.
    If MCP will continue to rules am sorry my fellow malawians , my brother's and sisters

    • @user-ol7ly5in2f
      @user-ol7ly5in2f 15 วันที่ผ่านมา

      Tikuyamikeni inu abungwe ndipo mupitilize

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 15 วันที่ผ่านมา +1

    True message ❤❤❤❤

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op 15 วันที่ผ่านมา +1

    Kuyakhula kwabwino kwambiri ❤

  • @user-do3qn6ux4r
    @user-do3qn6ux4r 15 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwerayi akulakwisa kwambiri sakuganizira zika zake chifukwa chani?

  • @ElizabethMajiga
    @ElizabethMajiga 14 วันที่ผ่านมา

    Asiye kupisila kumene mwayitha makotsana 🥳🥳🥳🥳🥳🥳

  • @PatrickMariko
    @PatrickMariko 14 วันที่ผ่านมา

    Good message

  • @LovenessJere-up6ie
    @LovenessJere-up6ie 15 วันที่ผ่านมา +3

    Abweze bas

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 15 วันที่ผ่านมา +6

    Good message Thanks

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u 15 วันที่ผ่านมา

    Inu mumayimiladi amalawi go ahead

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 15 วันที่ผ่านมา +1

    Komanso inuyo bola musalandle chibanzi abale

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 15 วันที่ผ่านมา

    Ndipo sindinaone muthu okuba ngati chakwera

  • @user-rd6zo8ry2d
    @user-rd6zo8ry2d 15 วันที่ผ่านมา +1

    Tidziwa bwanji kuti ndramayo yabwezedwa

  • @aggogokina8992
    @aggogokina8992 15 วันที่ผ่านมา

    Mau amphamvu ndi dangalira brother Namiwa Zikomo kwambiri polimba mtima ndikudzipeleka kwaulere potiimilira ife amalawi. Pali Bon Kalindo, Namiwa ndi journalist wa Bakili Muluzi TV ndi anthu ofunika kwambiri mdziko muno Mulungu adalitse anthu amenewa. Ndipo amalawi ambiri tikanakhala ngati anthu atatu amenewa malawi wathu atachoka mmisinga ya umphawi.

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 15 วันที่ผ่านมา

    Awo nde mau zoona zake,justice system ikukumeladi anthu andalama,mau mau

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u 15 วันที่ผ่านมา

    Panyapawo tilibe mtsogoleri
    Uyu ndi galu Lazarus Panyapako

  • @isaaczidana2914
    @isaaczidana2914 15 วันที่ผ่านมา +1

    Abungwe musafoke , abweze ndalama .

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y 15 วันที่ผ่านมา +1

    Ndakufila cded please mupitilise kuti yankhulali

  • @user-zy9ik7gq2t
    @user-zy9ik7gq2t 14 วันที่ผ่านมา

    Chakwera NDI fiti yopanda chisoni, Ambuye akukatheni ndithu iwe chilima zeze

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 15 วันที่ผ่านมา +1

    Mmmmh kunja kuno kuli Mulungu ,tiyakhulireni abale tikupsa ife ndi moto

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g 15 วันที่ผ่านมา +3

    Abweze chakwera ndalama zoonad big

  • @MadalitsoGeorge
    @MadalitsoGeorge 15 วันที่ผ่านมา +1

    Mabungwe ndi ofuniklad enawa monga CIDEDI.Chekis and balansi nzofunikadi

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi 15 วันที่ผ่านมา

    Good jobs guys

  • @user-ux5md4cy3d
    @user-ux5md4cy3d 15 วันที่ผ่านมา +1

    Awatu abwezadi ofunika kuwakakamira akanganya amenewa koma zomwe anangulitsa sung zo tiziwone atiwonjeza kwabili

  • @CharlesWyson-ue5fz
    @CharlesWyson-ue5fz 15 วันที่ผ่านมา +1

    power the message 💪

  • @ishmaeldama8906
    @ishmaeldama8906 15 วันที่ผ่านมา

    That's true, they must give it back, all the way from Johannesburg.

  • @user-jb5hr4rz2s
    @user-jb5hr4rz2s 15 วันที่ผ่านมา +1

    Thanks CED keep it

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5o 15 วันที่ผ่านมา +1

    Pongofunika Ku muchotsa ndi mademo chakwerayo osamangoyanganila ndalama zikubedwa chonchi waoononga dziko olo osamulipila malipiro Ake Kuti aone kuti

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 9 วันที่ผ่านมา

    90 million yachepatu check

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 15 วันที่ผ่านมา +2

    Well done acdedi kuyishosha tiyeni tizuke tonse

  • @VailetnyirendaShamah
    @VailetnyirendaShamah 15 วันที่ผ่านมา +1

    Amangidwe ka aaaa chitsilu chamunthu

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 15 วันที่ผ่านมา +1

    Boma Lili ndi chipha mtima ili iiiihhhh aliyese mtima uli ziiii no action taken koma tikuziwa ndithu kuti chuma sichikuyenda bwino.

  • @GiftNazira
    @GiftNazira 15 วันที่ผ่านมา +1

    Banja lawo likusqngalala chifukwa chandalama imeneyo wakuba

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 15 วันที่ผ่านมา

    Eya mbuzi imeneyo ibweze mamuna osatha kugula nsalu kuchuluka nzelu mbuzi ya kukasiya

  • @patesnkajenda4258
    @patesnkajenda4258 15 วันที่ผ่านมา +1

    More fire guy's 👍

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 15 วันที่ผ่านมา +1

    Auzeni amvetse bola musalandire mabanzi poti alipotu mabanziwo

  • @AshrafAshim
    @AshrafAshim 15 วันที่ผ่านมา +2

    Chilungamo kaa . Abweze ameneyo

  • @MarkoMkundiza
    @MarkoMkundiza 15 วันที่ผ่านมา +1

    Ambweze zimbanvazi

  • @user-bo1kt3nq6j
    @user-bo1kt3nq6j 15 วันที่ผ่านมา +1

    Osamusekelela abweze kwakwera

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 15 วันที่ผ่านมา +1

    Ndakunyadirani kobasi abungwe, mupitilize ku imilira a malawi ambuye akupasani nzeru zochuluka

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 15 วันที่ผ่านมา +1

    Achakwera nndichabosadi ndipo ndarama abwese

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609 15 วันที่ผ่านมา +2

    Aamenewa ndalama abweze kumeneku ndikupha Amalawi

  • @EnetChiomba
    @EnetChiomba 2 วันที่ผ่านมา

    Much appreciate

  • @user-lj7si9qy6w
    @user-lj7si9qy6w 15 วันที่ผ่านมา +1

    Koma malawi wabvunda . Tsiku lina tidzamenyana tokha tokha ayamba kumenyana ndi Andale okha okha

  • @user-ws9sy7pp3w
    @user-ws9sy7pp3w 15 วันที่ผ่านมา

    Fire 🔥 mabomba !!!!!!!💪🔥

  • @susantembo2076
    @susantembo2076 14 วันที่ผ่านมา

    Mwasowa chonena

  • @AllanChabwela
    @AllanChabwela 15 วันที่ผ่านมา

    Abweze iyah...

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 15 วันที่ผ่านมา +1

    Koma ladzalo iii mbusa uyu ndi oononga osakadza okupha akapume ameneyu mmutu mwake mulibe nzeru mbiri yadziko lamalawi mulibe mtsogoleri opanda nzeru ngati ladzaro cakwera

  • @user-oq7hi3hd4p
    @user-oq7hi3hd4p 15 วันที่ผ่านมา +1

    No doubt Abalalika.

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 15 วันที่ผ่านมา +1

    Tiyeni nayoni Nyauyi popha nyani sayang'ana nkhope ndie kulili nyau, tiyeni nayoni yatidzudza koopsa tatopa nayo ifee

  • @ThomasChiwaya-qx9mf
    @ThomasChiwaya-qx9mf 15 วันที่ผ่านมา

    Chakwera atiyakhe bas ndanena ndanena bas sindikubweza maganizo

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 15 วันที่ผ่านมา +1

    Abweze basi .Mbava chakwera ndichilima

  • @ChimwemweMagombobanda
    @ChimwemweMagombobanda 15 วันที่ผ่านมา +1

    Msonkhano umeneuja kunayenela kupita aliyense ngakhale osusa boma

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 15 วันที่ผ่านมา +1

    Abweze ndandama zamalawi tikagulile manthwala

  • @MasiyeDayton
    @MasiyeDayton 15 วันที่ผ่านมา +1

    Abwezedi ndalamaso mawa mukacha chakwera akusolowela

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 15 วันที่ผ่านมา +1

    NRB silibwino anthu akumalembetsa 200 patsiku sakutithandza akachali

  • @GiftChinji
    @GiftChinji 15 วันที่ผ่านมา

    Zuzuluni pofunika kudzudzula chilungamo chiyende ngati madzi tiphudzile

  • @KaipaEmanuel
    @KaipaEmanuel 14 วันที่ผ่านมา

    Mmmmm azathuwa awonjeza

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 15 วันที่ผ่านมา

    Abweze ndigalu kwambili nyani😢😢😢

  • @GodfreyWhayo-hh1dm
    @GodfreyWhayo-hh1dm 14 วันที่ผ่านมา

    Malawi will never be the same . Politicians wake up . Don't take us for granted .

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u 15 วันที่ผ่านมา

    Mumutenge bon kalindo muzithandizana naye there for it will be fire

  • @user-vn8zz1cw1t
    @user-vn8zz1cw1t 15 วันที่ผ่านมา

    Anthuwotu abweze amalawife tikuvutika Koma bambochakwera simunthuothandiza komawokupha

  • @ophlexmkondowe8107
    @ophlexmkondowe8107 15 วันที่ผ่านมา +1

    Amafuna apikisane ndi APM njamba rally

  • @vitumbikokamanga5869
    @vitumbikokamanga5869 15 วันที่ผ่านมา +1

    Abweze basi sitifuna kutinamiza ife

  • @user-pw1kl3vo5d
    @user-pw1kl3vo5d 15 วันที่ผ่านมา +1

    Tikukuvani bwino Kuno ku mosco amenewa bweze

  • @GeorgeKatundu-or1uf
    @GeorgeKatundu-or1uf 15 วันที่ผ่านมา +1

    Abweze chisiru cha president

  • @MustafaLikaomba
    @MustafaLikaomba 15 วันที่ผ่านมา

    Utsogoleli wausilu uwu wamamina mmutu

  • @AusmanBenthu
    @AusmanBenthu 15 วันที่ผ่านมา +1

    Akudya ndalama zathu chifukwa chakuti sakuopa aliyense

  • @Joydee1999
    @Joydee1999 15 วันที่ผ่านมา +1

    😂 good move and don't show them mercy

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 15 วันที่ผ่านมา +1

      😂😂😂😂😂

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 15 วันที่ผ่านมา +1

      😂😂😂😂😂Popha nyani sayang'ana nkhope ndie what more Nyau😂😂😂

  • @JONESNKOSI
    @JONESNKOSI 15 วันที่ผ่านมา

    bring it on lads!

  • @KaipaEmanuel
    @KaipaEmanuel 14 วันที่ผ่านมา

    Udzagotha bwanji mwambou

  • @user-wx5on7fx9p
    @user-wx5on7fx9p 15 วันที่ผ่านมา

    Mau kma awa🙏🙏🙏🙏

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 15 วันที่ผ่านมา

    Koma munalikuti poturuka lero? 👏👏 napokhapa mwakambila leromu ndititsegula mmaso a malawi mmmmmh ambuye akudalitseni ndikanakonda mma radio athu atamamverako izi juti mwina amalawi angasinthe maganizo posadzachivotelanso chilazalochi ndipo ndatopa nkumuona ine m'busa, mbava ameneyu

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z 15 วันที่ผ่านมา +1

    NO PAIN NO GAIN ABWEZE BAS

  • @GeorgeKatundu-or1uf
    @GeorgeKatundu-or1uf 15 วันที่ผ่านมา +1

    President chakwera akuwonga kwambiri zinthu mumalawi.
    Ndichisiru kwambiri