Eeeh wachita kutembelera boma lonse andale onse Prophet Mbewe kuti awalange Mulungu

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 8 ก.ค. 2024

ความคิดเห็น • 99

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 15 วันที่ผ่านมา +8

    Ndimo mudzina la yesu mau Anu agwile ntchito pa andale okubawa mu dzina la yesu

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z 10 วันที่ผ่านมา +1

    Only Young president can do better... Coz they can do it in new model...NOT 60'S MODEL

  • @MussahIman-cw1cu
    @MussahIman-cw1cu 14 วันที่ผ่านมา +1

    U man of God continue to pray for those bad people to gate pushed from god

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 2 วันที่ผ่านมา

    Amen man of God. We are tired wth that thng we call chakwera

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 15 วันที่ผ่านมา +1

    Mau owoona mulungu atimenyele nkhondo ameeen

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 15 วันที่ผ่านมา +1

    Mulungu wamatembelelo kkkkk mwayamba zibwana ndimulungu ky pot ndi business yanu ndimulungu wanu

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 15 วันที่ผ่านมา +2

    Ndipo athu atizuzuza yawa sitizaiwala m, pakana kale kale mmm ndipo asatana

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 14 วันที่ผ่านมา

    Amen mau ishiii ziko lathuli ai zikomo akuluakulu kuntunda mavuto okhaokha bsi.

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo 2 วันที่ผ่านมา

    God bless you man of God

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 15 วันที่ผ่านมา +1

    Perfect said 👏 🙌

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 14 วันที่ผ่านมา

    Very bold.....the only Man of God that have told govt the truth

    • @TheresaKuluwemba
      @TheresaKuluwemba 13 วันที่ผ่านมา

      Koma ndipo! Koma nthawi ya APM azibusa ma prophet ansembe palipose kunali kuyakhula zoipa zaboma lija koma pano kuli ziii, palibe akukamba zoipa kapena zabwino za bomali uyuyu ekha basi, ayi zikomo

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 14 วันที่ผ่านมา

    Kodi chakwerayu tu bvuto ndi school komanso mtundu komwe akuchokera mmmmmmmm so shame walephera basi 2025 azipita !!

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 13 วันที่ผ่านมา

    Tiye prophet awawa mulungu awachose 2025 zikutiwawà .

  • @AlickBaton
    @AlickBaton 15 วันที่ผ่านมา +1

    This is 2023,, but only God knows

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 15 วันที่ผ่านมา

    Oooh yes tatopa ndi boma ili please azibusa lowereranipo ndithu timenyereni nkhondo Kuti kumwamba kuseguke tatopa ndikulira amalawi

  • @MafunaseKamoto
    @MafunaseKamoto 13 วันที่ผ่านมา

    Basi man of God ndalamazo andipatsira ine tikabweze komwe zinabedwa...kkkk

  • @kennedybanda
    @kennedybanda 15 วันที่ผ่านมา +1

    Matenda ake ena mwa iwo ndi misala.

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie 14 วันที่ผ่านมา

    Iwe usankhepo chimodzi pakati PA ubusa ndi Der wamva osamphatikinza za mulungu ndi Zadary 😂😂😂

  • @julietmussa5103
    @julietmussa5103 14 วันที่ผ่านมา

    Alavule ndalama zikenezo in Jesus Name

  • @PiscaDicksoni
    @PiscaDicksoni 15 วันที่ผ่านมา +1

    Amen man of God

  • @PaulKambuzi
    @PaulKambuzi 4 วันที่ผ่านมา

    amen aprophert power full

  • @user-xe5il4cg5d
    @user-xe5il4cg5d 15 วันที่ผ่านมา

    Amen prophet

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p 15 วันที่ผ่านมา

    Amen mudzina la yesu

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 15 วันที่ผ่านมา

    Nkhale Lili LA 2023 akuphempha ndi chimozi mozi tikuyembekezera amipingo ina tinve kunyasidwa kwanu Asilam tiye maduwa

  • @Dorah-zl9uf
    @Dorah-zl9uf 15 วันที่ผ่านมา

    Amen may God bunish them

  • @user-gj8td8pc4d
    @user-gj8td8pc4d 14 วันที่ผ่านมา

    Names nkukhala mommo mundalemo.😂😂

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 14 วันที่ผ่านมา

    May God restore our country

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 14 วันที่ผ่านมา

    Amen zikomo🙏❤️💖

  • @BrianZenengeya
    @BrianZenengeya 15 วันที่ผ่านมา

    Yes 100% truth

  • @michaelsakala8884
    @michaelsakala8884 15 วันที่ผ่านมา +1

    100% true

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j 15 วันที่ผ่านมา

    Mulungu akuwonesa ukulu wake sopano mzimu wa Chilima Uli pakati pa Malawi

  • @yowasschitsosa5348
    @yowasschitsosa5348 14 วันที่ผ่านมา

    Kkkkkk zamanyazi a prophet m'malo molalika zamulungu mwayamba ndale

    • @TiyanjaneMkwate-we8gu
      @TiyanjaneMkwate-we8gu 14 วันที่ผ่านมา

      Udzimu umaenda bwino anthu akamakhala umoyo wabwino, kuvutika ndi kupemphera siziyenderan, away akuzuzula nchitidwe omwe andale athu oipawa amapanga pozunza aMalawi kuti zao ziyende, ndikupempheranso kwa Mulungu kuti ndalama akubazo zithere kugula ma kidneys, zaoneneni nkhalamba momwe zikuzunzikira kumiziku yet they were promised alot for them to win.

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie 14 วันที่ผ่านมา

    Koma pamenepo ine kukhosi mweee😂😂😂

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 15 วันที่ผ่านมา

    Ameeeeeeeeeeeeeeen

  • @user-po7zs9zd7u
    @user-po7zs9zd7u 14 วันที่ผ่านมา

    Amen amen amen amen 🙏🙏🙏❤️❤️❤️

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 15 วันที่ผ่านมา +1

    Gen Z is watching

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 12 วันที่ผ่านมา

    Kkkkk 2023 izi Aaaa

  • @user-hg2cw1om1p
    @user-hg2cw1om1p 15 วันที่ผ่านมา

    ❤❤

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v 14 วันที่ผ่านมา

    Osaopa mbewe chilungamo Nena boma lotopesa ili ipondeni mbewe yomweyo

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 15 วันที่ผ่านมา

    Ifenso tikupemphera mwachinsinsi ndipo mapemphero athu akutheka. MCP mthawi yanu yatha kale. Ndipo MCP yatheratu. Mark my words.

  • @user-xe5lb4uf3n
    @user-xe5lb4uf3n 11 วันที่ผ่านมา

    Walankhula munthu wa Mulungu

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 14 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 15 วันที่ผ่านมา

    Paja adanena zoti akantheni

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb 15 วันที่ผ่านมา

    Amen amen

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i 15 วันที่ผ่านมา +1

    Izizi ndizakalekale,Kodi chifukwa chani mumabweretsa zinthu zoti ndi zakale?

    • @alicechinyama4155
      @alicechinyama4155 15 วันที่ผ่านมา

      Zakale lake liti

    • @user-si7po9sd5i
      @user-si7po9sd5i 15 วันที่ผ่านมา

      @@alicechinyama4155 I saw it in 2023, but maybe you didn't see it then

    • @user-si7po9sd5i
      @user-si7po9sd5i 15 วันที่ผ่านมา

      The msg was powerful though

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 15 วันที่ผ่านมา

    Ameen

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 15 วันที่ผ่านมา +1

    Tell dem men💯

  • @DorrahBanda
    @DorrahBanda 14 วันที่ผ่านมา

    Amen❤❤

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 14 วันที่ผ่านมา

    Ameen 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-fb6kh2dk1y
    @user-fb6kh2dk1y 14 วันที่ผ่านมา

    we are after message not chaka chakacho sungani inu

  • @AminAbbass-xc4qk
    @AminAbbass-xc4qk 15 วันที่ผ่านมา

    🎉🎉🎉🎉🎉

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 15 วันที่ผ่านมา

    May God also punish fake prophets

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r 15 วันที่ผ่านมา

    Anzanuso asanarowe mboma anaringat auzimu ngat inu km anasintha mawanga amarawi osangot amen zirizonse ngat simuziwa mawu bwanji munthu wowopa chauta sankhara busy ndizandare chifukwa kundare kuribe kuopa murungu baibo rimat muthange mwafuna ufumu wake ndipo zonse zizakusatani auzeni zaufumu wakumwamba osat zazikozo ayi panopa amarawi asavoteraso azibusawa ayi asibusa nomwenu ndinu amene mwawononga zikori mawonekedwe achipembezo km mphwnvu yake munaikana kare pezani njira zina zosakira ndarama akuru

  • @MarkManyowa
    @MarkManyowa 15 วันที่ผ่านมา

    Amen 😂😂😂

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 15 วันที่ผ่านมา

    Iweso ndiwa bodza mulungu wake UTI

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 14 วันที่ผ่านมา

    Tell them

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 15 วันที่ผ่านมา

    Iweee ukubwera anthuwo ndizako

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf 14 วันที่ผ่านมา

    Fire abusa

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 15 วันที่ผ่านมา

    Amen😂

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe7448 15 วันที่ผ่านมา

    😮😮😮😮😂😂😂😂😂

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 15 วันที่ผ่านมา

    Yes boma ili ndi lolephera koma zoti uyu ndi fake prophet sizisintha.

  • @kingsleyhopematchaya5184
    @kingsleyhopematchaya5184 15 วันที่ผ่านมา

    Simulungu mbewe ndipo tsogolo la muthu sangalidziwe ndindani amewneyu tikusauka chifukwa cha kuba kwa dpp

  • @curtisewilliams8784
    @curtisewilliams8784 15 วันที่ผ่านมา

    Cant you see that, the video was recorded in 2023? bloggers be serious

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 15 วันที่ผ่านมา

    Zakale izi akulu

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula731 15 วันที่ผ่านมา

    Aaaa m'busa wanji olowerera zadziko?? Ufumu wamulungu siuli wadziko lapansi baba, onvera awawa palibe chomwe akutsata

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 15 วันที่ผ่านมา

      Chitsiru iwe mchifukwa chake mwapha chilima

    • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
      @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 14 วันที่ผ่านมา

      NDE ZOTI DZIKO LAPANSI NDI LA ANTHU OIPA ANANENA NDANI,,MULUNGU SANGAOPE KUYANKHULA ZANDALE CHIFUKWA IYEYO NDE MWINI MPHAVU

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 14 วันที่ผ่านมา

      Ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 14 วันที่ผ่านมา

      @@CHIFUNDOCHINA-lp9lg ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi chifundo

    • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
      @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 11 วันที่ผ่านมา

      ASE UTSOGOLERI WACHIPEMBEZO NDI WOYAMBA KUPOSA U PRESIDENT,,DZIKO LAPANSI LIMADUNIKA LIZIYENDERA MALAMULO AMULUNGU,,TIKAWASIRA ASATANA KUT ALAMULIRE ANTHU AMULUNGU SIYIGWIRA

  • @user-nr8oq4tr1i
    @user-nr8oq4tr1i 15 วันที่ผ่านมา

    Fake prophet, yang'ana za Mulungu, waisted time

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 15 วันที่ผ่านมา

    Wabodzi

  • @TimothyNkhutembaChirwa
    @TimothyNkhutembaChirwa 15 วันที่ผ่านมา

    Amen pastor

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 15 วันที่ผ่านมา

    Amen ❤

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 3 วันที่ผ่านมา

    God bless you man of God

  • @MaryJefry
    @MaryJefry 15 วันที่ผ่านมา

    Amen prophet

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo 2 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @user-pn6ic9yr1t
    @user-pn6ic9yr1t 13 วันที่ผ่านมา

    Amen amen

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah 15 วันที่ผ่านมา

    Ameen

  • @ellenMakoloma
    @ellenMakoloma 11 วันที่ผ่านมา

    Amen prophet

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef 14 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @malitajere1609
    @malitajere1609 14 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @user-nv7qt1yp7g
    @user-nv7qt1yp7g 14 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 15 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 15 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 15 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @user-no2sn1fo1h
    @user-no2sn1fo1h 15 วันที่ผ่านมา

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 15 วันที่ผ่านมา

    Amen