Palakwika chani apa.uthenga ndi uthenga ukupita kwa aliyense.koma lmasulirani mukuona ngati ngwa a Chakwera uthengawu.Mumudziwe Yesu ithink.Uthenga wa mu bible umapita kwa anthufe.osati uyo kapena uyu koma kwa ife anthu .chotero mmafunika maso auzimu kuti muzindikure.Chakwera mukulimbana nayeyu muchedwa naye. Zake zilibwino ohoooo.
Pachilungamo palibe Mantha 💪💪💪 kufera mbendela iyiiih 👉👉🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Powerful preaching
Nthawi yabwino ndiyomweyi kulapa ndikusiya zonyasa..Mulungu atitsekule maso ndi makutu kuti tione nyengo tili.
Abusa opanda banzi mukamwa amenewa
Palakwika chani apa.uthenga ndi uthenga ukupita kwa aliyense.koma lmasulirani mukuona ngati ngwa a Chakwera uthengawu.Mumudziwe Yesu ithink.Uthenga wa mu bible umapita kwa anthufe.osati uyo kapena uyu koma kwa ife anthu .chotero mmafunika maso auzimu kuti muzindikure.Chakwera mukulimbana nayeyu muchedwa naye. Zake zilibwino ohoooo.
Chakwela makutu giwogontha mukungotaya nthawi yanu mukuganiza kuti angasinthe ndikumuthawa amene panopa ndi bwenzi lake lapamtima Satana.
Amalalikira iweyo ndi dziwanda zakozo, umudziwe yes.
What a word!
What a bold messenger
I agree with you 100% my sister
Kuziyamba zoti siungazimalize
Powerful preacher
Powerful Amen
May God be praised
Utùmki wamphamvu ❤
Very powerful 🙏🏽
Abusa alalika bwino akumva wamva otsamva akwiya mutima
Uthenga wa mulungu ukafikile onse dziko lapansi.
Uthenga kunva mkumanva osasiya Kuba ndi kupha anthu osarakwa
Abusa zikomo,,koma anva awa
Mkanadziwa simkanapitako 😅
Ena mwaomverawo alephela
Hell is real