ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
The guy talking after him messes the whole interest of listening to mbewe.asachite Ngati Ali mtchalichi
David Mbewe akuyenera u president osati ngati Chakwela wakupha vice wake coz of udindo
Inunso mukufuna kuzapeza experience pa dziko la malawi ngati Chakwera😂😂😂
Uyu ali mbalume waenela kukhala president guys❤❤
Who new chakwera would be like now? My fellow malawians, if u come to politics in the name of God, u will never make it. Vote as u wish time will tell, no truth in politics what they want is money
My hope ineyo guys Mr mbewe God bless you Sir palibeso wina
My vote on you Dr.
Tatopa ndi mabusa chakwela adabwelaso ngati mgelo koma lero ndi chilombo cha mitu 9 ndiye ngati muli abusa pitani ku church
Exactly chilungamo chenicheni azibusawa tisawakhulupilire amangofuna kuba azipitad ku church
Ambewe omwewo kuti wawawawawaaaaa
Ameneo akuma comentayo asiye anthu tomzvera speaker
We don't need this government again mcp is going now chikangawa walephera kuyendedza dziko la Malawi nonsense 🙄 government 🙄 😒
We need standing together tisalekelele
😂uyu size yake ndi fredo pa njawala sagafike
Mfundotu apa palibe olo zitatani sangawine ndipo sadziwina
I like achimwene akuyankha pa mic po
Kodi unali nsonkhano wa home cell yanji
Koma Ndale zimachepetsa Kaganizidwe! All 18 and Malawians adzilembetsa opanda ID, masanje credible electro-process
Amatiyo yes pansana pake koma Mbeweyo ali bho
Iwe ukumayika dzimawu dzako dzokometserawe kakhale komaliza akaka kupanga zimenezi, ulendo wina udzawaleke ambewewo adzayankhule okha popanda wina osokosera.
Ndpo ndiye akusokoneza bwanj
@@McdonaldSairo mwene, akundinyansatu kobasi uyuyu kkkk
😅😅😅😅 inuyo boss ndi one Mr mbewe
Mmm lnemani zomwe mudzapenge osati kuweluza azanu
Kodi muli ku church kapena ku nsokhano??😂😂😂😂 A mbewe muuzeni commenter wanuyo asiye kut zizikoma than akupangazo😂 akasiyamo mwina muvoteledwa ndithu
mesa inu ambewe ndinu aneneri bwanji osatiuza kut mulungu wakuyankhulani nkhani za ngozi ya ndege
Pamenepo🤣
😂😂😂😂😂😂
Malawi manvuto sa dzatha basi kuyambira mcp,dpp,utm,or udf sikuonapo apa amene angapulumutse mmawawiambewenso ndiye ayi
abewa nanuso 😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Komaso anthu omwe ali mayiko akunja apezeleni yoti nawoso atha kuvota or alikunja komweko ife tikamava ndi momwe dziko likundela zimatiwawa kwambili timafuna boma ili likudzuza kwambili katundu wadhula kwambili ka ndalama komwe timatuzila abale athu sizikutheka kamba kodula zinthu mu dziko lathu
Chipanichi tachikonda kma iwe ukumatsatizira mawu ambewe usiye kundale ndikuchurch usiyanitse usapangeso
Iyaaaa ukuyesa kumpingo kwako et,mpakana okometsera? Zankutu
Kkkkkkkkkk kmaa iwee
Powerful
Kuyankhula mophuza kkkkkk
Uyu akulankhula mosatana ndi ambeweyu akundisokoneza kuti mdimvele bwino bwino
Alowetsa church akulu ameneo koma zopanda plan zomwe wanenazo
Anthu osiya za mulungu kuyamba ndale pali nzeru ?
Palibe nzeru akulu akufuna kuba basi
Kkkkkk makwana bwana😅
Zaziiii
Akuyesa ali pa guwa.
Aaaaa inu mukuikira mang'ombe mwayesa muli mu church? Tamusiyeni President ayankhule opanda mang'ombe anuwo.😅
Koma inu etini
Akuti zimzimveka mwauzimu kkkkk
Kumsonkhonso mpaka omasulila ngati kuchurch
Wayesa ali pa guwa kkkkkk
Koma inu mulimba mtima mungawine 50+ 1 koma ndale pena mmm
Kkkkkkkkkk
Za ziiiiii
Koma uyu wabwera
Zoonadi Mr Mbewe timasuleni ife Amalawi musingazamotozi tikuvutika Malawi 🇲🇼 waonongeka
Ndisaikepo comment kma 😅😅😅
The guy talking after him messes the whole interest of listening to mbewe.asachite Ngati Ali mtchalichi
David Mbewe akuyenera u president osati ngati Chakwela wakupha vice wake coz of udindo
Inunso mukufuna kuzapeza experience pa dziko la malawi ngati Chakwera😂😂😂
Uyu ali mbalume waenela kukhala president guys❤❤
Who new chakwera would be like now? My fellow malawians, if u come to politics in the name of God, u will never make it. Vote as u wish time will tell, no truth in politics what they want is money
My hope ineyo guys Mr mbewe God bless you Sir palibeso wina
My vote on you Dr.
Tatopa ndi mabusa chakwela adabwelaso ngati mgelo koma lero ndi chilombo cha mitu 9 ndiye ngati muli abusa pitani ku church
Exactly chilungamo chenicheni azibusawa tisawakhulupilire amangofuna kuba azipitad ku church
Ambewe omwewo kuti wawawawawaaaaa
Ameneo akuma comentayo asiye anthu tomzvera speaker
We don't need this government again mcp is going now chikangawa walephera kuyendedza dziko la Malawi nonsense 🙄 government 🙄 😒
We need standing together tisalekelele
😂uyu size yake ndi fredo pa njawala sagafike
Mfundotu apa palibe olo zitatani sangawine ndipo sadziwina
I like achimwene akuyankha pa mic po
Kodi unali nsonkhano wa home cell yanji
Koma Ndale zimachepetsa Kaganizidwe! All 18 and Malawians adzilembetsa opanda ID, masanje credible electro-process
Amatiyo yes pansana pake koma Mbeweyo ali bho
Iwe ukumayika dzimawu dzako dzokometserawe kakhale komaliza akaka kupanga zimenezi, ulendo wina udzawaleke ambewewo adzayankhule okha popanda wina osokosera.
Ndpo ndiye akusokoneza bwanj
@@McdonaldSairo mwene, akundinyansatu kobasi uyuyu kkkk
😅😅😅😅 inuyo boss ndi one Mr mbewe
Mmm lnemani zomwe mudzapenge osati kuweluza azanu
Kodi muli ku church kapena ku nsokhano??😂😂😂😂 A mbewe muuzeni commenter wanuyo asiye kut zizikoma than akupangazo😂 akasiyamo mwina muvoteledwa ndithu
mesa inu ambewe ndinu aneneri bwanji osatiuza kut mulungu wakuyankhulani nkhani za ngozi ya ndege
Pamenepo🤣
😂😂😂😂😂😂
Malawi manvuto sa dzatha basi kuyambira mcp,dpp,utm,or udf sikuonapo apa amene angapulumutse mmawawiambewenso ndiye ayi
abewa nanuso 😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Komaso anthu omwe ali mayiko akunja apezeleni yoti nawoso atha kuvota or alikunja komweko ife tikamava ndi momwe dziko likundela zimatiwawa kwambili timafuna boma ili likudzuza kwambili katundu wadhula kwambili ka ndalama komwe timatuzila abale athu sizikutheka kamba kodula zinthu mu dziko lathu
Chipanichi tachikonda kma iwe ukumatsatizira mawu ambewe usiye kundale ndikuchurch usiyanitse usapangeso
Iyaaaa ukuyesa kumpingo kwako et,mpakana okometsera? Zankutu
Kkkkkkkkkk kmaa iwee
Powerful
Kuyankhula mophuza kkkkkk
Uyu akulankhula mosatana ndi ambeweyu akundisokoneza kuti mdimvele bwino bwino
Alowetsa church akulu ameneo koma zopanda plan zomwe wanenazo
Anthu osiya za mulungu kuyamba ndale pali nzeru ?
Palibe nzeru akulu akufuna kuba basi
Kkkkkk makwana bwana😅
Zaziiii
Akuyesa ali pa guwa.
Aaaaa inu mukuikira mang'ombe mwayesa muli mu church? Tamusiyeni President ayankhule opanda mang'ombe anuwo.😅
Koma inu etini
Akuti zimzimveka mwauzimu kkkkk
Kumsonkhonso mpaka omasulila ngati kuchurch
Wayesa ali pa guwa kkkkkk
Koma inu mulimba mtima mungawine 50+ 1 koma ndale pena mmm
Kkkkkkkkkk
Za ziiiiii
Koma uyu wabwera
Zoonadi Mr Mbewe timasuleni ife Amalawi musingazamotozi tikuvutika Malawi 🇲🇼 waonongeka
Ndisaikepo comment kma 😅😅😅