BON KALINDO WANG'ALULA AZIBUSA __5 February 2025

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 9 ก.พ. 2025

ความคิดเห็น • 46

  • @chimwemwenkute3839
    @chimwemwenkute3839 5 วันที่ผ่านมา +4

    I always support you just because you stand for the truth may God always be with you the DCCCCCCCCCCCCCC from mulanje southern Africaaaaaaaa malawi

  • @JosephMpokosa
    @JosephMpokosa 4 วันที่ผ่านมา

    😂😂 Chilungamo chimamveka Pena ngati mwano kkkk

  • @ShukulaniMthipera
    @ShukulaniMthipera 4 วันที่ผ่านมา

    Makwana Mr DCCCCC ulemu wanu

  • @mathewshauya
    @mathewshauya 5 วันที่ผ่านมา +1

    Azibusa anakulodzani ndani koma?? Mene Malawi waonongekelamu kumalambila munthu zoona a ccap? Zooona

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 5 วันที่ผ่านมา +1

    CCAP ndi amfiti Bon kalindo avala zoyera koma mkati mwa mtima ali akuda 🎉🎉🎉

  • @BertherMatiya
    @BertherMatiya 3 วันที่ผ่านมา

    Chilungamo chiyende ngati madzi

  • @DysonYohaneChingwalu
    @DysonYohaneChingwalu 4 วันที่ผ่านมา

    iwetu nde adakoza

  • @SaidiMilinje
    @SaidiMilinje 4 วันที่ผ่านมา

    Mumakwana big

  • @GreysonLimula
    @GreysonLimula 4 วันที่ผ่านมา

    Mitumbo yawo azibusa a nkhoma synod machende awo kutigulitsa ife kamba ka 10 million

  • @Dellingsmunthali
    @Dellingsmunthali 4 วันที่ผ่านมา

    Azibusa adyera akakowa awapasa nthumbwana basi akut bwana zilibwino azibusa a ccap adyera omasangarara anthu akuvutika

  • @RuthOsman-m6x
    @RuthOsman-m6x 3 วันที่ผ่านมา

    Thana nawoni mu tea Estate muli nkhanza aoneseni afisi amenewo

  • @BernardChikopa
    @BernardChikopa 5 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi azibusa bvuto lanu ndi chani,,,makamaka aaaa mbuye akuyendereni,,,thawi yokhala limodzi ndi apulezdent.yatha inuyo simukuona mene awonongera zithu muno Malawi nde mumakatani kumeneko....ntengo ukakhota ngakhale utakula simungaungole awa ndi anthu oyipa,,azibusa opanda masophenya...

    • @DanielGanizani-h8r
      @DanielGanizani-h8r 5 วันที่ผ่านมา +1

      Azibusa aCCAP koma ndi chani,ndine wa ccap koma mukutichitisa manyazi kwambiri ndinu mimbulu eti ija amanena Ambuye wathu Yesu eti?dyelanitu Moto ukukuyembekezani posachedwa,mulibe manyazi poyenda ndizina la ubusa mukutchulidwalo?mulibe mantha ndi Mulungu chifukwa chani?asatanic inu ,mundilakwisaso ,Mulungu alowe ndi nkwapulo munyumba ya m'busa aliyense mwalowa ndalama ya mwaziyi,mdzina la Yesu

  • @JustinMakoka
    @JustinMakoka 4 วันที่ผ่านมา

    Apa ndiye akunyazisa mipingo anthuwa palibe kukhulupilira opemphera Maka mazibusa onse

  • @chisomochawinga4905
    @chisomochawinga4905 5 วันที่ผ่านมา +2

    Ndiwe kape

  • @kennedychinguwo1640
    @kennedychinguwo1640 5 วันที่ผ่านมา

    Komano pa nkhani yobera anthu muma kampani,kuzunza powagwiritsa ntchito anthu mwakalavuala gaga ndi kuwapatsa malipiro ochepa,zakhala zikuchitika kwa nthawi yayitali ndipo maulamuliro onse akuyenera kudzudzulidwa posapangapo kanthu.
    All the past regimes have to take the blame.All the governments have never taken any company accountable when the citizens are being exploited by their companies.And surprisingly most of these companies are depended by govt

  • @Kamwachale
    @Kamwachale 4 วันที่ผ่านมา

    Let the opposition register all fertilizer beneficiaries and find out from each if he or she received all two bags of fertilizer if not then all who were responsible to be accountable otherwise this is theft.

  • @MartinKapito
    @MartinKapito 5 วันที่ผ่านมา

    Auncle bon kalindo mulungu aonjedzere masiku anu popanda inu amalawi titha. Ndibu yemwe mumatidzindikiritsa ndi kutiunira

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 5 วันที่ผ่านมา

    Inuyo the DC ndiwakulu❤

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 5 วันที่ผ่านมา +1

    Zitsiru za abusa

  • @juliussamson6212
    @juliussamson6212 5 วันที่ผ่านมา

    MAZIMBUSA NONSE MUNALANDILA NDALAMA ZOTI MUZIWUZA ANTHU MA CHURCH INUYO KAYA MUKUDAMBA MACHIMO YA CHAKWERA NDIPO MUKAYANKHA PAMASO PA MULUNGU CHIFUKWA CHAKWERAYO ANASANKHA KUPHA CHILIMA MALO MOFUNA KUPITILIZA UDINDO NOKHA INU MUZIFUSE KUTI CHIFUKWA CHIYANI SATANAYI AKUTIPATSA NDALAMA IZI KODI TSGWILA NTCHITO YOTANI KOMA CHIFUKWA CHOFUNA KUTI CHAKWERA ASAKALANGIKE YEKHA PAMENE AKUGAWILANI NDALAMA YACHIPHIMBA MASO KUTI MUSAWONE PATALI NOSE INU MWALANDILA NDALAMA MWAMVOMERA KUTI MUNAPHA NAWO MR CHILIMA AMEN MU JESUS NAME AMEN

  • @YassinzaoZao
    @YassinzaoZao 5 วันที่ผ่านมา

    The DC katundu zenizeni azibusa aminewa ndi mbuzi kwambiri

  • @AbrahamLLoyd-xb2xc
    @AbrahamLLoyd-xb2xc 5 วันที่ผ่านมา

    Powerful message

  • @MosesChinyamula-b3g
    @MosesChinyamula-b3g 5 วันที่ผ่านมา

    This is the truth ❤

  • @VictorMateyu
    @VictorMateyu 5 วันที่ผ่านมา

    YOU DESERVE RESPECT

  • @ManuelMagombo-m2u
    @ManuelMagombo-m2u 5 วันที่ผ่านมา

    A Nkhoma synod anthu awo akumva bwino boma ili. Ndi chifukwa anapita kukafunila Chakwera zabwino.

  • @OscarDavidBanda
    @OscarDavidBanda 5 วันที่ผ่านมา

    Kuyankhula mopanda mantha

  • @cyplusmsunje5483
    @cyplusmsunje5483 5 วันที่ผ่านมา

    DC munabwera kuzaimilira malawi

  • @WellingsChiona
    @WellingsChiona 5 วันที่ผ่านมา

    Kalindo iweso ndi mbuli kwambiri .Chiyambire sunagawepo chimanga .keep on shouting

    • @codeoflife1398
      @codeoflife1398 5 วันที่ผ่านมา

      Azigawa chimanga cha chani nanu inu....mutu okhotawo

    • @JudithKatungwe
      @JudithKatungwe 4 วันที่ผ่านมา +1

      😂😂😂😂😂😂😂

  • @OscarKathumba
    @OscarKathumba 5 วันที่ผ่านมา

    Dpp never again ndipo ulira zeni zeni, uli ndi zaka zina 5 ,ukulakhula zopusa zakozo

    • @samdiverson9733
      @samdiverson9733 5 วันที่ผ่านมา +2

      Ulila ndiweyo pulpet wa chabe chabe

    • @PiterDeleza
      @PiterDeleza 5 วันที่ผ่านมา +2

      Wopusa ndiiweyotu chifukwa ukuyikila kumbuyo zopusa.

    • @fridaylestar
      @fridaylestar 5 วันที่ผ่านมา +2

      Bola inuyo zilibwino zikukuyenderani komatu akuyankhualazi ndizowona anthu akuvutika, nkhani si DDP nkhani si MCP or UTM nkhani ndi a Malawi akuvutika ndipo zintbu sizikuyenda mu dziko lathu lino.

    • @codeoflife1398
      @codeoflife1398 5 วันที่ผ่านมา

      I think ndiwe osabala.

    • @samdiverson9733
      @samdiverson9733 5 วันที่ผ่านมา

      @@codeoflife1398 mpaka mwapeza chipangizo zoyezera kusabeleka kwa anzanu tikumana September 🤣