Limpopo FM yomweyo galu iwe Ntanyiwa kufotokoza za anthu 7 omwe anakamaliza a Chilima ndi anzawo

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 18 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 152

  • @giftwankhama9914
    @giftwankhama9914 4 หลายเดือนก่อน +16

    Stay safe comrade. May the God in heaven keep u safe my brother.u the only source of true information to us.

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 3 หลายเดือนก่อน +2

    Thanks alot comrade, May God protect u so that a Malawi tipitilize kuziwa zoona zenizeni

  • @BerthaKasambala-y5k
    @BerthaKasambala-y5k 4 หลายเดือนก่อน +11

    Kunena zowona paziko rapansi pano paribe chinsinsi sure nyimbo ikhare ya grace chinga ndizaurura tchimo rimazunza orichita sure 🥱🙆

  • @hajjdaud123
    @hajjdaud123 4 หลายเดือนก่อน +5

    ❤❤❤❤more fire 🔥🔥🔥 ndipo titemana serious muno oky mungoti pheee anthu amenewa asazayerekeze kubwera kumangochi serious azaona ngati akufuna kuti azalembe book la history lomkuzana anthu akumangochi 2024 yelekezani kubwera kuno , zimunezo kulilongwe komweko kwa anthu aganiza mwauchitsiluwo try to come here in Mangochi try

    • @Hudhayf
      @Hudhayf 4 หลายเดือนก่อน +2

      😂😂😂😂 Mangochi m'bomamo

  • @CharlesKajawa
    @CharlesKajawa 3 หลายเดือนก่อน +3

    Number one Limpopo FM more 🔥

  • @EdnahShantell
    @EdnahShantell 4 หลายเดือนก่อน +3

    From South Africa all i have is a protecton prayer for you my brother ,, may God protect you from these anacondas for not swallowing you Amen

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      Tikuziwa zisisi zambiritu mmm

  • @ProspaMitumba
    @ProspaMitumba 4 หลายเดือนก่อน +4

    watching from cape town limpopo no: 1

  • @WilliamKapungu
    @WilliamKapungu 4 หลายเดือนก่อน +5

    ❤❤❤❤ More fire comrade ntanyiwa

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka 4 หลายเดือนก่อน +7

    Mulungu salakwitsa kalikose adziwa yekha chochita nximu wanu uuse mumtendere bwana chilima

  • @jacquelinecunningham363
    @jacquelinecunningham363 4 หลายเดือนก่อน +12

    Limpopo 🎉🎉❤❤🔥🔥🔥🔥🔥💯

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 4 หลายเดือนก่อน +8

    Chakwerao osangomuombera bwanji watikwana kwambiliaaa

  • @eliasnyilongo4865
    @eliasnyilongo4865 4 หลายเดือนก่อน +7

    My redio in malawi

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 3 หลายเดือนก่อน +2

    Viva Limpopo FM ❤❤🔥🔥🔥🔥🔥

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti 4 หลายเดือนก่อน +5

    Following.... Limpopo 🔥 🔥 🔥

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 4 หลายเดือนก่อน +10

    Viva Limpopo FM

  • @JoyceChimphwika
    @JoyceChimphwika 3 หลายเดือนก่อน +2

    Ulosi wa grace chinga umandikumbusa kwambili chipani chamwadzi ichi mulungu achite nawo ndithu

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      Ndipo kwambiri tu mmm

  • @LawrenceMalinda
    @LawrenceMalinda 4 หลายเดือนก่อน +3

    This is true station

  • @ShyreenMbwana
    @ShyreenMbwana 4 หลายเดือนก่อน +5

    Chidanti Malunga wako uja amusankhadi kukhala VP monga umanenera dzulo lija

  • @BFWCPHIRI1978
    @BFWCPHIRI1978 3 หลายเดือนก่อน +1

    Watching from limpopo province in lephalale town

  • @MustapherDavie-su3nk
    @MustapherDavie-su3nk 4 หลายเดือนก่อน +9

    Tili pa mbuyo panu

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 3 หลายเดือนก่อน

    Limpopo is powerful massage 💪💪💪✊✊✊❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ModesterMkawa
    @ModesterMkawa 3 หลายเดือนก่อน +1

    More fire comrade kusatira ndi chidwi

  • @JamesKakhome
    @JamesKakhome 4 หลายเดือนก่อน +6

    Comrade mtanyiwa! Chamzelutu apa kunali kungotulusa zinthuso coz mukat mwatulusa olo report mudikilalo sangatuluseso n mukhoza kumacedwa conco then kaya nditsokaso akusowetsan sibas zizakhala kut mwatidikilisa pachabe umbon muli nawowoso mwapita nawo! Tulusan chabe zomwe muli nazozo mukucedwa mukucedwa

    • @ElizabethZiyadi
      @ElizabethZiyadi 4 หลายเดือนก่อน +1

      Umboni alibe awa chomwe akukanikira kutulutsa ndi chani?monse muja

    • @SufyaanAhmedChazama
      @SufyaanAhmedChazama 3 หลายเดือนก่อน

      Chabodza ichi

  • @BarnettWitness
    @BarnettWitness 4 หลายเดือนก่อน +3

    Ipanse Moto tiziwe zoona zen zen

  • @AliceGeorge-il6ig
    @AliceGeorge-il6ig 4 หลายเดือนก่อน +1

    Bravo bravo achimwene,be safe plz

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 4 หลายเดือนก่อน +3

    Limpopo ❤🔥🔥🔥

  • @LuciousKotamu-dh5uq
    @LuciousKotamu-dh5uq 3 หลายเดือนก่อน +1

    Keep on inform us good work

  • @francismlilima
    @francismlilima 3 หลายเดือนก่อน +2

    Koma mukuchulikitsa gagadiwa...go straight to the points

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 4 หลายเดือนก่อน +11

    We are great to have you comrades

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 4 หลายเดือนก่อน +5

    Magalimoto adutsa ku Lunzu?

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 4 หลายเดือนก่อน +2

    Magalimoto amene mukunenawo mungovutika amene aja ndi alendo ongudusa amachoka ku nacala port adusa ku Moçambique mpaka zimbabwe

  • @ElizahMadi
    @ElizahMadi 4 หลายเดือนก่อน +5

    More fire

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo 4 หลายเดือนก่อน +5

    Umunthu alibe mphamvu ya satana basi,ngati opemphera koma Satana weniweni ineso ndi mchewa koma awaso aonjeza

  • @emmanuelalbertbotolo
    @emmanuelalbertbotolo 4 หลายเดือนก่อน +1

    More fire Mr muthanyiwa

  • @jonas-xh4hz
    @jonas-xh4hz 4 หลายเดือนก่อน +4

    mumakwanira a mtanyiwa

  • @HalimaMussa-j6t
    @HalimaMussa-j6t 3 หลายเดือนก่อน

    Tili nyengo ya kalikonse tikaziw more 🔥

  • @PETERSINKADZIWA
    @PETERSINKADZIWA 4 หลายเดือนก่อน +4

    Emusipi Chipani Cha Nkhanza komanso chakupha

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro 3 หลายเดือนก่อน +1

    Mcp omse ndi amagazi manja agalu Eni Eni mbuzi za wanthu

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 4 หลายเดือนก่อน +6

    Mbuzi zawanrhu zukanika kulamulira dzko

  • @YatoRoy-kt4lh
    @YatoRoy-kt4lh 4 หลายเดือนก่อน +4

    2025 they will be no votes.
    Dziko lonse lapansi kukhala Climate Lockdown(NWO)
    mufufuze zimenezi

  • @DumisanPhiri
    @DumisanPhiri 4 หลายเดือนก่อน +3

    Koma mathelo a nkhani izi ndi Otani?

  • @ChawingaMwaseteza
    @ChawingaMwaseteza 4 หลายเดือนก่อน +4

    Wina aziphe kumene agalu amenewa sangatiphele adzibale athu motelo

  • @HamiltonChabwera-t7h
    @HamiltonChabwera-t7h 3 หลายเดือนก่อน

    Zimatrauza zachani? Ntanyiwa may god protect you

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 4 หลายเดือนก่อน +1

    Mo fire Limpopo FM

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda 4 หลายเดือนก่อน +1

    Alimi afodya asangalala chaka chino musanamizepo anthu pamenepo inu a Limpopo FM. Ifenso alimi achimanga tikusangalala panopa chafika kale 750 per kg osati za 150 zija tinkaona mmbuyo zija ali, zomathandiza alesi osalima, olima nkumangolira. Kazingokhalani kumeneko anthu osowa zochita inu.

    • @priscillamangata4023
      @priscillamangata4023 4 หลายเดือนก่อน

      150 mukuinenayo and imagula feteleza 18000 matumba awili zingafanane ndipano 200000 matumba awili

    • @LucianoKapepuza-sy9wx
      @LucianoKapepuza-sy9wx 3 หลายเดือนก่อน

      Are u a member if MCP or are u from central region u show your evil and dirty mind here better no comment if u not interested with him

    • @LucianoKapepuza-sy9wx
      @LucianoKapepuza-sy9wx 3 หลายเดือนก่อน

      Its not home of debates

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 4 หลายเดือนก่อน +2

    We are very angry we want to given us good information,we are not joking, Chakwera,Chakwera, Becareful., you will flee and Leave Malawi One Day,zida wagula zija ndi zathu tizazi tenga zonse tiku ziwa Chakwera Ufa ngati Nazombe Malawi uyu ndiwa sopano Siwa Kale munapha uja Chirima ndiye Anali bwana wanu,siku limodzi ma ofesi a MCP aza pshya tsiku ndi limodzi Osati Ndi chipani,Gulu la anyamata liku konzeka wenatu Alípo secret soldiers Malawi an there's is outside, Asirikari mukama gwiri sidwa ntchito Ndi MCP zizakuvutani yang'anirani Amalawi,Os militar não tenho partido, tem dereito para defender população ouviu Malawiano Malawiano não pode deixar Chakwera para vingar cidadão malawiano quidado Chakwera

  • @christopherchikankhen
    @christopherchikankhen 4 หลายเดือนก่อน +5

    Limpopo Yayamba Kunamiza Anthu, Munatiuza Kuti A Chidanti Malunga Ndiomwe Adasankhidwa Ukhala Wachiwiri.

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge 3 หลายเดือนก่อน

    Big up bro✊✊✊✊✊🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo 3 หลายเดือนก่อน

    Big up mtanyiwa ❤❤
    Live from south Africa Durban Pietermaritzburg

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda 4 หลายเดือนก่อน +1

    Katundu akudula chifukwa cha kugwa kwa Kwacha yathu. Kwacha yathu ikugwa pafupipafupi chifukwa chosowa forex, forex ikusowa chifukwa chochepa kwa export; amalawi tachulutsa ma import osati export. Amalawi tiyeni tilimbikire kugwira ntchito zomwe zitha kutibweretsera katundu yemwe titha kutumiza mayiko akunja kuti forex ilowemo yambiri muno.

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip 4 หลายเดือนก่อน

    Am watching you from Lusaka zambia

  • @paulinekayuni1621
    @paulinekayuni1621 3 หลายเดือนก่อน +1

    Vuto ndiloti report yanuyi sikhala official zomwe zikuoneka zabodzazo ndizomwe zizamveke makutu a anthu ambiri. Koma tingopemphera ngati zanuzi zili chilungamo zizakhale official and anapanga azazengedwe mlandu

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda 4 หลายเดือนก่อน +1

    Munthu akuyankhula za achewayu wangoonetseratu umbuli waku wonse kuti za democracy sazidziwa. Democracy imabwera ndi ma condition ake. Boma lingapereke ku ma company angati ndi ufulu wa pa malonda omwe ulipowu? Muli ma company angati m'Malawi muno kuti boma lingakwanitse kuperekako ndalama? Taganizirani za fetereza wotsika mtengo momwe zikuyendera, akupindula ndi amphawi kapena anthu andalama? Zomwe zikuchitika ndi fetereza ndi zomwe zikhoza kuchitikanso ndi sopo kaya ndi sugar kaya ndi mafuta ophikira. Omwe ali ndi ndalama zambiri akhoza kumakangozikokololako zonse nkumagulitsa ku amphawiwo modulabe.

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 4 หลายเดือนก่อน +1

    Its better kumakamba zinthu ndi umboni coz pamawa uzayankha brother

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      La 40likwana one day is one day

  • @WilliamKapungu
    @WilliamKapungu 4 หลายเดือนก่อน +3

    Amfumu akabudula 😂😂😂😂 muziti Chan? 😂😂😂😂

  • @RichardMphopheya
    @RichardMphopheya 4 หลายเดือนก่อน +1

    more fire limpopo

  • @ProspaMitumba
    @ProspaMitumba 4 หลายเดือนก่อน +3

    kkkkkkk ooooh ndodo itulukedi basi

  • @TryceMagombo-sh7kb
    @TryceMagombo-sh7kb 3 หลายเดือนก่อน

    Big up big more and more imfo

  • @KeltonKapanda
    @KeltonKapanda 3 หลายเดือนก่อน

    May God keep you safe comred

  • @JulietKamanga-2
    @JulietKamanga-2 3 หลายเดือนก่อน

    Ndipo ndimsona Ngati fm'yi ndiyakujonitu🤣🤣🤣🤣pa Malawi ayi ndithu

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ndichifukwa chiyani osangomuchoseratu pompano chakwerayo? Apatu zikuonesakuti before 2025 kukhala kutafa anthu ambiri chakwera salibwinoyi

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      Ndipo kwambiri tu mmm

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro 3 หลายเดือนก่อน +1

    Usiyo chiwembu chomwe anafera chilima uja akuchiziwa

  • @Sirmax-p3e
    @Sirmax-p3e 3 หลายเดือนก่อน

    Keep on

  • @MODESTERNGWENY
    @MODESTERNGWENY 3 หลายเดือนก่อน

    Iimpopo 🔥🔥🔥🤝

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 4 หลายเดือนก่อน

    Limpopo iweyo umakwanila ndipo mulungu azikudalisani ndikupasani moyo wautali

  • @PatriciaIron
    @PatriciaIron 4 หลายเดือนก่อน +3

    Sanati amusankha chidanti koma amati ndizomwe akukambirana ndye nzosadabwitsa kuti ayitembenuza pamenepo

    • @ElizabethZiyadi
      @ElizabethZiyadi 4 หลายเดือนก่อน +1

      Mmmm anati amusakha osabakira mveraninso mwina simunamve bwino

    • @KennethChagunda-gn8kg
      @KennethChagunda-gn8kg 4 หลายเดือนก่อน +1

      Ndykt iyeyu amatiuza zopanda umbon

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      Anaisintha game

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      ​@@KennethChagunda-gn8kgkoma zimaphelezera akulu sikuti amanama ayi

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu 4 หลายเดือนก่อน +4

    🔥🔥🔥🔥 Limpopo umakwana

    • @oathbilliot
      @oathbilliot 4 หลายเดือนก่อน +1

      ❤❤❤❤Limpopo

  • @CheMass-05
    @CheMass-05 4 หลายเดือนก่อน +3

    🔥🔥🔥🔥

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 4 หลายเดือนก่อน +8

    Ndizisiru chakwera watha basi South Africa

  • @Phiricostina
    @Phiricostina หลายเดือนก่อน

    Antanyiwatu mmaitha ndipo inuyo anakoza kusekakokhakotu chikangawa angosegula mmimba mot akufunika thazi ORS chifukwa afakasegula michere itha muthupi

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 3 หลายเดือนก่อน

    Koma tilimba chaka chino kapena Tipange zaku kenya kuti mudziwe kuti anthu tili ndi mphavu

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 4 หลายเดือนก่อน +4

    Bwanji ya nzungu wamathanyula sunafune kuti tiyikepo maganidzo

    • @IssacMateyo
      @IssacMateyo 4 หลายเดือนก่อน +1

      Sangave samadikila kuti amuuzeko ena kkkk

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 3 หลายเดือนก่อน

      Ife tupanga kaye za ifa ya Malawi nzathu, akanakhala Chakwera wafa ifa yotere ifeso sitikanakhala chete tikanafuna chilungamo chioneke

  • @justinanyirenda6899
    @justinanyirenda6899 3 หลายเดือนก่อน

    Tikudikira report ndi ma audio mukunenawo

  • @ChipiliroLungu
    @ChipiliroLungu 3 หลายเดือนก่อน

    Ase some you talk truth ,koma zina zikuoneka kt mmmmm ndizonama ngati kuli chaka chimene alimi asangalala ndi fodya nde ndi chinochi ase zafodya usafinamize mwina zinazotu

  • @OwamThoko
    @OwamThoko 4 หลายเดือนก่อน +1

    Zero ya bwino pofuna kukamiza chakwera kuti asiye anthu onse Malawi asiye lupita muzintchito dzeko lonse mabungwe ,aboma,amwenye asilikali,apolisi,mabusi,matekesi,mbc,wina aliyese,magurd ,capita muzintchito,palibee kanthu muvutike koma mawa muzasangala,dzeko lonse liyime paka achoke.mukuina bwanji amalawi

    • @OwamThoko
      @OwamThoko 4 หลายเดือนก่อน +1

      Yah mzeru yabwino,achoke basi ameneyu,

  • @partmaulidiPatrick
    @partmaulidiPatrick 4 หลายเดือนก่อน +3

    Adahinuyo makwana

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc 3 หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera evil 😈

  • @GiftFrancesco
    @GiftFrancesco 4 หลายเดือนก่อน

    Limpopo number one

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 4 หลายเดือนก่อน

    Kagwedwe ka ndege tilibenazo ntchito , kubedwa kwa black box yamu ndege izo tilibenazo ntchito ,
    Mufunilanji umboni wina chonsecho tikudziwa kuti chakwela ndi nduna zake ndizomwe zinapanga plani yogwetsa ndege yomwe inapha anthu 9 kuphatikizamo V'P Claus chilima .

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 4 หลายเดือนก่อน +2

    Lelo akuluwa zolakhula khalangati zasowa

    • @KennethChagunda-gn8kg
      @KennethChagunda-gn8kg 4 หลายเดือนก่อน

      Ndiwa bodza inu munthu uyu. Kd iyeyu akudziwa bwanji zonsezi munthu ali ku SA??

  • @EmmanuelPhaundi
    @EmmanuelPhaundi 3 หลายเดือนก่อน

    Idonyole

  • @ElizabethZiyadi
    @ElizabethZiyadi 4 หลายเดือนก่อน +2

    Iwe osatulutsa lako lowonalo bwanji?hahaha mabodza awa

  • @CathyYassimin
    @CathyYassimin 4 หลายเดือนก่อน +1

    Kumatu muli phwete achimwene

  • @ElizabethZiyadi
    @ElizabethZiyadi 4 หลายเดือนก่อน +3

    Hahaha wailesi yabodza iyi dzulo imatiuza bodza kuti vice president ndi chidanti malunga lero alengeza kuti ndi manganya hahaha ndinkana social media sindimaikhulupirira

  • @AllanKasalu
    @AllanKasalu 4 หลายเดือนก่อน

    comrade Ntanyiwa woyeeeeeeeeeeeeeee

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko 3 หลายเดือนก่อน

    Asilikali aku Malawi amasunga mwambo,uyu ndiwabodza simsilikali!

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 4 หลายเดือนก่อน +1

    awa ndachisilu sanena zobveka amakonda bodza uzanamiza alomwe azako

  • @AhmedKjuma
    @AhmedKjuma 4 หลายเดือนก่อน +1

    ❤❤😂😂😂 Koma kuthawadi

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 4 หลายเดือนก่อน

    Prophet mbeweyo Ndie ayiso aaaaaaaa athu opephela siawa akutiliza apawa

  • @EmmanuelMakadali
    @EmmanuelMakadali 3 หลายเดือนก่อน

    Umatha iweyo

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko 3 หลายเดือนก่อน

    Inu ndabodza,anthu akumayakhula bwanji sakuwamanga?

  • @lloydmushali-dw2td
    @lloydmushali-dw2td 4 หลายเดือนก่อน

    Limpopo FM❤❤

  • @Emmanuelisraelsimbi
    @Emmanuelisraelsimbi 4 หลายเดือนก่อน +2

    Why unati kut chidanti ndi amene akhale vice president lero tu ndi Usi

    • @KennethChagunda-gn8kg
      @KennethChagunda-gn8kg 4 หลายเดือนก่อน

      Uyuyu ndiwa bodza akulu akungofuna kumatipatsa uthenga wabodza

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 3 หลายเดือนก่อน

      Anaisintha game kkk

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 4 หลายเดือนก่อน

    Ndiye akugwesa kwachayo ndindani mesa ndichisilu chanucho

  • @ChristopherNikola
    @ChristopherNikola 4 หลายเดือนก่อน +2

    Zilengwalengwadi eee

  • @THOCCOChimbali
    @THOCCOChimbali 3 หลายเดือนก่อน

    Mbambande

  • @ZelipaMalanda
    @ZelipaMalanda 4 หลายเดือนก่อน

    Wokhulupirira mabodza a Limpopo mutu wake sugwira. Ndani adatuma anyamata achipani kukafufuza za ndege? Muzichita manyazi ndi propaganda yanu makape inu.

  • @AlihIbrahim-w6n
    @AlihIbrahim-w6n 3 หลายเดือนก่อน

    Vutoso la inu ndi la propaganda,,,
    Zikanakhala kuti mumangotiuza nkhani kuti tinve tidziwe mmene zinthu zikuyendela
    Koma mumapangaso campaign kuti anthu anvotele yemwe inu mukumufuna this is no sense

  • @asayileernestsapao
    @asayileernestsapao 4 หลายเดือนก่อน +2

    Ndayamba kukukayikilani

  • @HamiltonChabwera-t7h
    @HamiltonChabwera-t7h 3 หลายเดือนก่อน

    Koma mchewayo wabwera kuzakhala