Mmmmmm inuso ndinu abodzaso bwanji nde ngat ndi DPP bwanji kubwela ma report a kugwa Kwa ndege ( sometimes you need to close your mouth and open your eyes )
Ineso ndili wosangalala kwambili zo tupere thawi yake maso kusongolo ndi adadi mulungu akudalisene moyo wako nose inshall allah tiyangidwa ziteka komaso mcp ekschoka boma xs bas mapa kare wosaziwonaso
🙏plz apm gwilanani manja atupele plz ombolani dzikoli mai p kaliati chotseni chekwera achihana plz atambo chonde amalawi azikhalira kuthawi moyenda coz uyu chakwera
Ndipo ngati zili Chocho mulungu adalise kwambili🙏🙏🙏🙏🙏
Chilima bwezi ali moyo achinkhla kuti ali ku Dpp Peter ali ndi umunthu
We want national unity of political parties. Thanks a lot
❤❤❤❤❤❤ tiyeni tiyendeleni limodzi UTM UDF AFORD and DPP Tiyeni tyendele limodzi
Ndipo mulungu atikomele m,tima abale tikungopepha kuti mulungu atichotsele zikhanilazi tatopa ndi chikangawa party
Mulungu wathu ndiwamoyo amamvatu kulira kwa Amalawi
Amen 🙏
@@GospelSoldiers-sr7np kulilakwiratu dzina la Mulungu bwana kundaletu kulibe uzimu chonde ganiza mwaulemu pamaso pambuye
Mukunya chakwera bomaaa ndiyekuti 50+1 Palibe chakwera saona satutumuka akuumbuzani sizoyesa
Game Changer I salute you Brother
Exactly this is president of malawi well respected man Dr Peter muthalika true man muthu osapha muthu olemekeza omoyo wamuthu
More 🔥🔥🔥💯 gwirizano
Gwirizano umenewo ulibwino kobas talila kokwanila iyaaaa
My vote
Ndipo uku ndiye kubwera Dpp apa yanyamuka waboma uyu
More fire more fire ❤❤❤❤❤❤❤
Zachamba basi mmesa ndi dpp ikungofuna kugwiritsa zipan zinazi by the end big problem will come
Bola MCP itachokabe Bas
@@EmmanuelNtago ukunamatu iweyo pitala walephera ngakhale kupanga hold convention kulephera kudzayankhula pomaliza chifukwa chokalamba ndie angayendetse dziko ameneyo
Ndakunyadirani.🎉❤🎉❤
Koma iwe game change ndiwe mbuzi yamunthu zaziii palibe chimene tikumvapo apo peter sitikumufuna bora anali munthu wina mukufuna tizayambeso kukhala pakhomo 6oclock chifukwa chwopa zigawenga zanuzo inuso ndinu munapha chilima mukunamizira mcp muganiza kuti sitikuziwa kuti panayenda ndale agalu inu
Mmmmmm inuso ndinu abodzaso bwanji nde ngat ndi DPP bwanji kubwela ma report a kugwa Kwa ndege ( sometimes you need to close your mouth and open your eyes )
My vote❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ DPP
Inde MCP yizipita kwawo even ,ppls party ,asale Okhla amcp ,atiphera chilima azipita azikavina gule
💙 My vote
Palibe chomwe mungawine anthu asankho inu ziko pano likuyenda bwino ,kusinthasintha ma president sikutithandiza chifukwa peter ndiwokalamba apanga chani
Apm my vote
My vote Dpo
Game changer ing'alure ❤
Dpp wooooooooooo
UDF DPP UTM AFORD kungotheka mcp izathera pomwepo ndithu 😂😂😂
Kokolilikoyo adzipita nthawi yake idapita ndi mtsamunda mzake uja samatha chichewa kamuzu ..inu sinthawi ya makhadi ayi chikangawa next year azikayimba ng.oma kudambwe zikhare /chimwendo adzikavina
My vote Dppppppppppppppppppppppppppppp
Yes
💪💪💪💪💯 kwayaka moto🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤❤❤❤❤
Chakwera nambala wani,kulalika nambala wani,umbava nambala wani,chigololo nambala wani I, Chikangawa forest Chakwera woyeeeee wakupha wakupha aa
Compliments Malawi
Dppppppppp woyeeeeeeeeeee
❤❤
DPP woyeeeee, Peter mutharika woyeeeee
Gemucheja udziweichi utm sikupanga naozagwilizano umeneo chilima adatiphanyila phanje tikupita kuchisankho tokha zimenezo udziuza audf omweo
Kma simungawine
Aaa akudziwa ndi Mulungu zowinazo koma ife gogoyu ayi sitikupanga nawo
@@AishaChibwana-b8oineso ndikudana ndi gogoyo coz sangalole kut pule akhale wa utm amakakamila pampando ife tikufuna president wa utm basi
Guys gwilanani manja bas tigwese athu akuphawa ambuye azikudalisan
❤ exactly kulakhura kwabwino respect
More fire morefire😊
This is so amazing
Massive alliance ever
🙏🙏🙏🙏🍊🍊
Mulungu amakonda munthu wodzichepetsa, Mulungu lowereraniponi ndithu musalore satana apambane, tichitireni chifundo anthu talapa tinasankha molephera ti khululukireni Mulungu tithandizeni kutisankhira Atsogoleri amene adzawombole dziko lathu la malawi
Congratulations Mr game changer
UTM and AFFORD musamadzaliretu mtsogolo muno ayi kumatulutsa tizizungu twanu takuti GENTLEMANS AGREEMENT. Chifukwatu a Lomwe onsewa akuti tiombere dziko kuti akunena zoona ayi AKUTHAUZA KUTI BWERANI MUTIOMBOLE KU OPPOSITION KUNO KULIBE MIGODI NGATI MMENE ANAYANKHULIRIRA CHAPONDA CHIFUKWA AKUTI MIGODI ILI MBOMA.
ADAD 2025
Enanu museguka mimba ndinthu kkk chikangawo achoke basi
Tikunyadirani ifeeeeee
Atuluseni mcp apiteso kuholiday
A UDF ndiye anatha kale kale alibe kolowera.
Ndipo mukagwirizane zoti report la ndege lituke osainva
Gwirizanani guys muchose chipani chakupha .udf,aford ,utm ndi dpp chonde gwirizanani.Apm wakula kale adzakusiyiran .chachikulu mwachosa chipani chamagazi kuti malawi awomboledwe
Tazikonda ife zimenez alemekezeke mbuye shiver
ADAD OMWEWOOOOO!!! KUMENEKO NDIYE KUBERAAÀA!!! I INENSO NDIKAKHALA NAWO KONKOOOOOO!!!!
Ineso ndili wosangalala kwambili zo tupere thawi yake maso kusongolo ndi adadi mulungu akudalisene moyo wako nose inshall allah tiyangidwa ziteka komaso mcp ekschoka boma xs bas mapa kare wosaziwonaso
A Malawi takhalani serious peter mene wakalambila paja akhalenso nsogoleli ,munthu wafika stage yoziyipsira yekha angakhale nsogoleri
MCP 2025,Bomaaaaaaa!
Mulungu adalitse Malawi.
Ok tanva❤
Umatimilila aise pitiliza kutiuza ase more fire peter
Ubwino Wake chisankho nchamuntina mwaekha
Zipani ziphatikizana potengera kuchuluka kwa mavoti omwe wotsogola adzapeze. Kwapafupi kuphatikizanso zoluza zonse pamoza kapena otsogola ndi ena oluza. 17th September, 2025 will devide Winners from losers.
Alliance ndiyimeneyo tiyen tipange koma peter asakhaletu president nayeso ngwatsakho peter mmmmm bola utm
Chakwela adulidwa 2025😂😂😂😂galu wa pusident 😂😂😂
Zomwe timayembekeza ndi zomwezo tiyeni amalawi tikavote mwaunyinji tikachose nyasi izi zamagazi
More fire🎉
Ndipo Akapanga zachibwana game chang'r mwamalize akutinyasa kwabasi a mcp tikukhala mosamasuka ife muziko mwathu
Mwachita bwino kuphatikizana tikumenyeren limodzi
Tikuwonga kukhala pamoza vipani vyose vya kususka boma ivyo mukorerana mu unenesko ise nase TIKORERERANA NAVYO kwa THUNTHU----mu UMODZI MULI MPHAMVU
Tithokoze atsogoleri onse amane mwachita mngwirizano umenewo tiyeni tichose achakwera ife timagwira ntchito ndi manja athu osat kudalira ngongore
Ndipo takondwa ,atiwombole mu Ng,anjo ya moto, MCP olo yipange Makani yipta kwawo ndithu
Kutereko sudalime ndi khobwe yenwe kumati dpp ikuombole ukuona ngt adzakupatsa ndalama
Nde atasogolele gululi ndindani poti peter zintchito zake tinaziona kale mwina muyikepo atupere ndi amene asogole
Ali ndimoyo oziwa mavuto amalawi mulungu azimudalitsa Dr Peter muthalika
My vooooooote
Zikomo big man ulemu
Pangani ngwirizano plz😭😭😭 plz
Mgwirizano uwu ndiomwe ungachonse chipani chamagazi chakupha cha mcp.
Thwerenyenye ❤
Tiomboleni pa moto uwu wa MCP chifukwa tikupsa ndithu
Please tiyeni titelo abale chikangawa chakwera watitopesa abale
Zilibwino kwambiri tatopa tinakhuta nsima ndi kale tinamwa tea ndi kale
chipani cha chakwera chaka cha 2025 apitaso kumbwe kukavinidwa
❤🔥🔥🔥🔥
Zitsiru angale a afford ngati angapange mugwilizano ndi a galu awa a DPP
Apita mwaganiza bwino pangani uchamuna sinthani dziko
Koma apitawo pulizi alliance yi asakhaletu president 😂😂😂😂😂😂😂😂
If it like this atleast malawi will be restored from those nfwit
💥💥💥💥
Koma zinazi zaziiii ndiye mukuganiza kutsina mutsogoleri ndiko kusintha ziko palibe chimene mukulankhura ndipo kungoti azipani zinawo ndiwo nzeru alibe nanga konivechoni yanu ndiye enawa akapangaku chani zaziii amalawi ake ati naweso iwe tatiye uko ukuti chakupha nayesa iweyo ndiwe wadura anthu ziwaro malubino mwatha azimayi kuchosa mabele anthu kwapopa magazi zaziiii kuphako siyani ndipo dpp ndiyo yinawomba theki muluzi kuti chipani cha udf chithe kumanga bakili muluzi ndiye mutiwuza chani njoka ndinjoka singasinthe mawanga wanachosedwa peter palibe chimene anali kuchita pamene inuyo ndinu mulindimagazi ngamalubino mumalawi muno zaziiii
So if you said That kusintha president that can not change anything so why DPP munayi chosa m'boma???
Exactly white man
Tikuyamika kwambiri fundo yimeneyi, MCP yichoke basi a Malawi sitikuifuna.
Nkhululu
Ngat zili chomwechi zilibwino mcp isuthepo eish tapanga zithu amalawi
MCP Isegulatu m'mimba apa. 😂😂
A utm plz musalole kut pule akhale adadie muononga chipani akulawo awo ngat zilizimenezo pule achokere ku utm basi muzingowalowetsa azanu pampando zoona inu a utm ayi
Tikufuna mgwirizano ndi zipani zimezo zingati Khalre bwino kwambiri
Mcp iwezeka chaka chamawa amvanyekwe
Amenewo akulalatayo wadya ndalama ameneyo moti polalata kwakeko ndalama zikulowa pamenepo,,a Malawi chenjelani
Zathapo basi
Chonde pangani zomwezo zamugwirizano tatopa ndi MCP palibe chomwe yikupanga zinangobwera kuzangowononga
Valema wanthu na chikangawa ngeyingafumapo waka mwahuno
Mumantha bro timakudyadilani