PHALOMBE BIG BOY LERO 26JUNE,,,,2024 TSIKU LINA WINA AZALIRA.....A MALAWI TIYENI TICHOTSE MANTHA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 30 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 168

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya 3 หลายเดือนก่อน +4

    Inu assemblies tabwerani muliwuze zoona dziko, kodi uyu mwati analidi m'busa? 😭😭😭😭😭😭😭😭Malawi waliratu

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 3 หลายเดือนก่อน +4

    Palibeso zoendetsa bwino kuno , achoke basi awa palibe chilimo awa

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 3 หลายเดือนก่อน +4

    Apapa mene mcp yafikapa ofunika tonse tidzuke tikaduduze chakwela ku state house kumweko azipita kwawo kukasiya mbuzi imeneyi isatitenge ngati ife a Malawi ndife anthu opusa ai

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 3 หลายเดือนก่อน +3

    Kuyankhula zanzeru aise ndipo chakwala sindikuonela kukondwa ndipo ufe ndithu pasana pamako

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie 3 หลายเดือนก่อน +2

    Watiphela chilima pano ma radio angokhala chete kuwopa ikukamba zowona ndi social media basi museke ma radio anuwo😊

  • @FloraMweza-u7y
    @FloraMweza-u7y 3 หลายเดือนก่อน +3

    Tatopa ndithu ndachakwera achoke

  • @DaudJulius-hz8uy
    @DaudJulius-hz8uy 3 หลายเดือนก่อน +3

    Amwene nthawi yomulangiza chakwera inali kale pano anytime is teatime osakhalanso za tsikulina mapeto ake atiphatonse galu amaneu akuenera kuchoka lero olo m'mawa pano

    • @WatsonNtchito
      @WatsonNtchito 3 หลายเดือนก่อน

      Mu m c p muli mbudzi zokhazokha za wathu

  • @RabecaMvula
    @RabecaMvula 3 หลายเดือนก่อน +3

    Go konko pa 10 pano tikaonesana konko

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 3 หลายเดือนก่อน +2

    Enough is Enough we're tired, on 10 July something is going to happen , Malawi viva let's unite together

  • @AubreymjBanda
    @AubreymjBanda 3 หลายเดือนก่อน +2

    Tell them my brother listen from Zambia

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 หลายเดือนก่อน +2

    Koma MCP nyasi zachipani agalu kwabasi

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 หลายเดือนก่อน +1

    Apolisi opusa samalani. Musiya ana Anu chifukwa chofuna tuteteza chigawenga komanso mbava yanuyo.
    Muli busy asilikali komanso apolisi kuteteza mbavazi.
    10 July ndilo tsiku mulisunge apolisi komanso asilikali.
    Palibe zopempha chilolezo

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 3 หลายเดือนก่อน +1

    Basi mr bon kalindo ankhale president wa ziko ndipo ndizomwe ndikuona aaaaa❤❤❤❤

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ukuneneska razarus must fall , Ine Kuno nanozgeka pa 10 July ,Lazarus gwenembe achoke

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 หลายเดือนก่อน +2

    Akutamika kumanga anzawo nthawi yawo ikubwera nawonso amagidwa kuba kupha agalu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 หลายเดือนก่อน +1

    Azakhumudwa tsiku Lina chakwera Born Kalindo Ali President Tidzabwedza

  • @SteveSamson-t9d
    @SteveSamson-t9d 3 หลายเดือนก่อน

    nsitingapange chifukwa manda kwambili tiyegalasi kuyamba kuthawa

  • @AlexNjanje
    @AlexNjanje 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kodii inuu ma big boy pa 10 sipanatalike pa 29 bwanji oloo pa 30 tikhozatu oloo lero lomwe tatopa nazo ifee

  • @Jasonnyatwa
    @Jasonnyatwa 3 หลายเดือนก่อน +1

    Mitimayathu ili Mwamba asiyeni pamene titachile mademopo opolisi tizaphana, kunkuyu zikhale ng'oma tizathana naye

  • @ChristopherUmari
    @ChristopherUmari 3 หลายเดือนก่อน

    Amalawi tiyeni tisaope apolice nawotso apolice wo sizikuwasangalatsa tiyeni tipange ngati kenya

  • @MajiduMakiyi
    @MajiduMakiyi 3 หลายเดือนก่อน +1

    Guys chakwela timuonese mwaziona ruto chimodzimodzi ndi chakwela akuziona ndi madolo chimunthu banda usamale

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 3 หลายเดือนก่อน

    Guys let stand for the truth ,chakwela must step down before 10 if not fire every timaoffce topusa ta mcp anthu amagazi mumanja nfiti kumampha anthu ofunilila anthu zambino

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 หลายเดือนก่อน

    If only we can deliberate over our national teasers philanthropically and patrioticallly other than provocative demonstrations,Malawi will achieve her blissful vision and missions for prosperity

  • @OweniMalokooweni-es9qx
    @OweniMalokooweni-es9qx 3 หลายเดือนก่อน

    🎉🎉🎉🎉 ndipo kwambili zikwanje pa 10 komo ku pramet

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kalu ameneyu analibe chilicose koma amalawi matha kukondamoyo tatiyeni tichangamuke ngat pa Mozambique

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 3 หลายเดือนก่อน

    Go malawi Goo!!achoke and analowela mademo mbavazi anaoipa chakwela

  • @GodfreyTSAMDOKA
    @GodfreyTSAMDOKA 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo mwalakhula moveka bwino president ndiomwe akuononga maiko ndithuditu tikuvuti kusauka chifukwa chama president wa

  • @GShaba-wm9uk
    @GShaba-wm9uk 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amade...Amade...yakukenya ichitike kumalawi kwathu kuno phaka chakwera anyere kaya kuzipha aziphe tilimbe naye tchinto azaluza kwaoko

  • @HusseinMoffatt-mi1fl
    @HusseinMoffatt-mi1fl 3 หลายเดือนก่อน +1

    Zoonadi chakwela waonjeza akupanga zamanyi ngati akuzuza buys a mkaziwake

  • @MasterJailos-kv5sd
    @MasterJailos-kv5sd 3 หลายเดือนก่อน

    Muzikapangira kupariyametiko

  • @AgnesMatola
    @AgnesMatola 3 หลายเดือนก่อน +1

    Tilikonko ku ma demo ko anthu amenewa atilowa Mchala kwabasi

  • @feliciajohn6041
    @feliciajohn6041 3 หลายเดือนก่อน

    Pa 10 gokoko more fire

  • @KizzFrank-g1v
    @KizzFrank-g1v 3 หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera achoke walephera, tili kusewu koko more fire

  • @EdwardSamuel-xj8qq
    @EdwardSamuel-xj8qq 3 หลายเดือนก่อน +1

    Wopha chilima aphedwesonaye,busa Wang,nombeyo

  • @joekamphulusa4767
    @joekamphulusa4767 3 หลายเดือนก่อน +1

    Makape a mcp 🚮🚮🚮

  • @KittyNdazi-bm1lh
    @KittyNdazi-bm1lh 3 หลายเดือนก่อน +1

    Zamveka we are tired I miss chilima for good analakwa chani?

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ndipo masoohenya abwino boni kalindo adzakhale plesdent wazuzika kwambili ndipo chakwela tikukhala ngati ku Malawi si kwathu njenje mulungu atithandize 😢😢

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 3 หลายเดือนก่อน +1

    Ine sindikupanga comment
    Koma boma likadzasintha,ngat anyani amenenewa simudzawamanga...tidzapanganso mademo kutanthauza kut it is a must kumanga aliyense anene akutizunza lero.....

  • @MaikNkhoma
    @MaikNkhoma หลายเดือนก่อน

    Makape inu

  • @EsterJackson-v4g
    @EsterJackson-v4g 3 หลายเดือนก่อน

    Go deeper 😢

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 3 หลายเดือนก่อน +1

    Zamaphunzirozi ndiku Malawi konkuno maiko ena amasankha munthu ngakhale osapita ku sukulu chifukwa utsogoleri si maphunziro ayi koma luntha kuchokera kwa Yehova. Za maphunziro izi ndi dyera komanso kuponderedza anthu anzeru za chilengedwe

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 3 หลายเดือนก่อน +1

    Uku ndiye kuswa kwenikweni😂😂

  • @cjaylucky
    @cjaylucky 3 หลายเดือนก่อน +1

    NO PAIN NO GAIN AWUZE BIG BOY BON KALINDO ONE DAY ITS ONE DAY AZAKALA PHULUMUS INSHA ALLAH

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 3 หลายเดือนก่อน +1

    Well spoken my brother amene akukhalilabe kumbuyo chakwera ndi boma lakeli ndimfiti yothelathu

  • @HarrisonKalonga-k7p
    @HarrisonKalonga-k7p 3 หลายเดือนก่อน +1

    Tikwapulanamo mmenemo soon

  • @TressLuka
    @TressLuka 3 หลายเดือนก่อน +2

    Game on 😢😢😢😢

  • @adamusaidih8570
    @adamusaidih8570 3 หลายเดือนก่อน +1

    Amenewo ndiye mau chakwela ndimbuzi yamuthu

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 หลายเดือนก่อน +1

    Gwenembe anapha m, bale wake Chilima zachisoni ndithu😭😭😭

    • @LeendaDeborah2005
      @LeendaDeborah2005 3 หลายเดือนก่อน

      Sikusinja ndi yemwe adapha gwenembe. Komabe nzachisoni kuti Chilima azitchedwa kuti malemu 😢😢😢

    • @mayomayo-uf9hu
      @mayomayo-uf9hu 3 หลายเดือนก่อน

      ndipo mzoopsa guys

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi titakhala five million angatikwanise

  • @AgathaJerard
    @AgathaJerard 3 หลายเดือนก่อน +1

    Kutelokotu chilungamo chimapweteka akuyendela iweso akumange 😂😂😂😂😂

    • @ceciliakayira7891
      @ceciliakayira7891 3 หลายเดือนก่อน

      Tikuona ndi maso athu zonse zomwe zikuchitika. Kuteroko akutitseka pakamwa by kumangana

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 หลายเดือนก่อน

    Malawi muno mukukhala ngati tilibe zipani zotsusa angokhala phwiiiii kudikira kuti Born kalindo aziwamenyera campain thats not true this is time for you to rise takumbukirani momwe ankachitira a mcp ma demo amapanga daily.

  • @Mahamudu-q6b
    @Mahamudu-q6b 3 หลายเดือนก่อน +1

    Yes🤞🤞🤞🇿🇦💪🏾💪🏾💪🏾💪🏾

  • @innocentnjoka7014
    @innocentnjoka7014 3 หลายเดือนก่อน +1

    Truth have spoken

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 3 หลายเดือนก่อน

      Truth have spoken😂😂😂

  • @RabecaMvula
    @RabecaMvula 3 หลายเดือนก่อน +1

    Awuzeni zowona Antalya again amenewa

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 3 หลายเดือนก่อน

    Komaso wamisarayodi ankhaledi mpampando aramuliledi

  • @PharrohmagawaZimba230
    @PharrohmagawaZimba230 3 หลายเดือนก่อน +1

    Anthu mumafika potopa kkkkkkkkkkkkkkkkk

  • @WatsonNtchito
    @WatsonNtchito 3 หลายเดือนก่อน +1

    This is only the action!

  • @ReginaNyilenda-ug1lf
    @ReginaNyilenda-ug1lf 3 หลายเดือนก่อน

    We coming from deference country we are ready to do!!!!!! Mr chakwela please step down we are tried with u!!!!!!!

  • @JamesDaud-jz7uq
    @JamesDaud-jz7uq 3 หลายเดือนก่อน

    Big up phalombe boy, dziko la Malawi is for every one, Chakwera akutidzolowera heavy,akuona Ngati Ali Ku church what he knows is stealing and killing

  • @ceciliakayira7891
    @ceciliakayira7891 3 หลายเดือนก่อน

    Kenya yayambitsa kutiphunzitsa kulimba mtima

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera walephela komaso kupha kwa Chilima anapanga zolakwika and I hurt Chakwera with passion because of the death of Chilima.

  • @DicksonKaunda-o9v
    @DicksonKaunda-o9v 3 หลายเดือนก่อน

    I support u to put someone who is suffering now to be our future President like bon kalindo

  • @BerthaKasambala-y5k
    @BerthaKasambala-y5k 3 หลายเดือนก่อน

    Muwoneseni kenya kenya bas kkkkkkk anzanutu anaikidwa ku mzuzu ku zorozoro uko nthawi ya bingu marawi itakungana mpaka masiku atatu asirikari nkat kuchoka nthawi imene ija sindina woneposo mademo anzeru

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 หลายเดือนก่อน

    Tiyeni nafe tilionese bomali amalawi maiko anzanthu zinthu zikumasitha chifukwa satsekelera boma boma liziopa anthu not anthu aziopa boma ndichifukwa chake amatizuza

  • @evansjohn7766
    @evansjohn7766 3 หลายเดือนก่อน

    5:43 mantha to much a Malawi,kkkkkkk......simukwanisa anzanu amachita mademo mowirikisa inuyo mungathe?aaaaaa......koma pakamwa basi

  • @FlorenceDouglas-x5c
    @FlorenceDouglas-x5c 3 หลายเดือนก่อน

    Mwa chakwera mulibemo usongoleli ,kupha ,kuba ,

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 หลายเดือนก่อน

    RAZARO wadzilonda tamuuzeni watizolowera kwambiri tiyeni ku nseu basi

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 หลายเดือนก่อน

    Mau mau audzeni Big boy ndipo ndakodwa Nanu kwambiri tiyeni tipange zomwedzo Indeeeee opusa anaimba Ng'oma ochenjera navina azaziona ndithu Bola kuotcha nyumba yawo akuona ngati Malawi ndi amao ndi achagogo awo Big boy Moto kuti Buuuuuu🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 หลายเดือนก่อน

    Tili konko tipange zomwe zachitika ku Kenya a malawi tisapuse anthuwa atitola!!

  • @OssmanAbubaker-st7pu
    @OssmanAbubaker-st7pu 3 หลายเดือนก่อน

    Tatopa tatopa chakwera out ndi gululanu muchoke

  • @RegistermoseskashonKashon
    @RegistermoseskashonKashon 3 หลายเดือนก่อน

    Iwe galubwako mpaka pampando born kalindoyo chitsilu iwe wava

  • @Kilocssreaction
    @Kilocssreaction 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂 ipase moto

  • @MarciaNetonMagulinho-dq3fi
    @MarciaNetonMagulinho-dq3fi 3 หลายเดือนก่อน

    Koma nde anthu mwatopadi tsopano ndakuwonan ee koma zinthu sizili bwino mkomwe ayi kkkkk😂😂😂😂😂

  • @FlorenceDouglas-x5c
    @FlorenceDouglas-x5c 3 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂 siku lina pa mpando wa u presedent pa zakhala muthu wamisa ,,,

  • @StellahMsodoka
    @StellahMsodoka 3 หลายเดือนก่อน

    Iwe u president ungakukhale tayimilani tikuvotereni

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 3 หลายเดือนก่อน

    Chakusuzga ntchivichi iwe ?

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 3 หลายเดือนก่อน

    😅😅😅😅😅😂😂😂🎉yomweyo galu iwe Gwenembe out go go go go

  • @HassanJameskananjie
    @HassanJameskananjie 3 หลายเดือนก่อน

    What are we waiting for here let's go guys

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 3 หลายเดือนก่อน

    Enough is enough now we don't want shit

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 หลายเดือนก่อน

    Malawi ndikumuziwa ine sangapange mademo ngat a ku Kenya

  • @CiprianoBindissone
    @CiprianoBindissone 3 หลายเดือนก่อน

    Akulu akulu ndidziko lonse Izi dzikoli lingotha

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 3 หลายเดือนก่อน

    Enough is Enough we're tired

  • @SymonPaul-s8h
    @SymonPaul-s8h 3 หลายเดือนก่อน

    Tiyen Tiyen tonse bas ulemu watha!!!!..

  • @GiftSoko-i3s
    @GiftSoko-i3s 3 หลายเดือนก่อน

    Mbava yamunthu uyu mumati mumati Chakwela utu mufiti

  • @ChristopherNikola
    @ChristopherNikola 3 หลายเดือนก่อน

    Komadi tikugonadi bwanji tiyeni tidzuke guyz

  • @AubreyThipa-zc6vs
    @AubreyThipa-zc6vs 3 หลายเดือนก่อน

    Boma lathapo kale ili president angokhala chifukwa cha mphavu ya constitution uyu, pa 10 Pano timuyendera

    • @MasterBlack-r2n
      @MasterBlack-r2n 3 หลายเดือนก่อน

      Amalawi tiyen tizuke pamene Kenya yatizindikilisa kupanga zinthu nkulimba mtima. freedom is coming ... Koma mmaso mwanga ndikuona nkhondo kumalawi. 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @lyiemax
    @lyiemax 3 หลายเดือนก่อน

    Powerful speech Big Boy

  • @GabiBanda-r3o
    @GabiBanda-r3o 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwera ndiwakupha kutumbu kwake

  • @MelvinVanRooyen
    @MelvinVanRooyen 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwela fiti went weni achoke bac watibela mokwana

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 หลายเดือนก่อน

    Agalu inu

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 หลายเดือนก่อน

    Chitsiru chen Chen za zii tikuziwa ndiwe ntumiki wa dpp koma enafe sitilola zautsiru uzipangira kwako komweko ku lomwe belt

  • @MAFUNSOMOLESI
    @MAFUNSOMOLESI 3 หลายเดือนก่อน

    Go ahead my boss I love you so much

  • @PhillipNyaugwe
    @PhillipNyaugwe 3 หลายเดือนก่อน

    Thyolo mulaje phalombe zomba chikwawa sanje blatantly chilazulo usakapagiseko sokhano chakwela uziwezimenezo uzafa uli ndi achitetezo tili pano ku school timaliza pomwepano

    • @MosesNyalugwe-ll8hh
      @MosesNyalugwe-ll8hh 3 หลายเดือนก่อน

      Ndipo live kuno ku chikwawa sitimamufuna kuyambra kare

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie 3 หลายเดือนก่อน

    Tulobasi amalawi ku wopa ku police

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 หลายเดือนก่อน

    Chitsiru Cha dpp iwe ndipo wauponda peter wakoyo sazabwerelaso boma anakalamba

    • @JustinGosten
      @JustinGosten 3 หลายเดือนก่อน

      Iwe ndiwopusa kwambiri ukuwona ngat anthu akukodwera mmoyo uno

  • @janemsiska3345
    @janemsiska3345 3 หลายเดือนก่อน

    Chifukwa chake amawakuwa pauwiri wawo

  • @SydneyMwale-u9w
    @SydneyMwale-u9w 3 หลายเดือนก่อน

    Ulendo ulikodi konko.
    Komanso aonadi

  • @EdwardSamuel-xj8qq
    @EdwardSamuel-xj8qq 3 หลายเดือนก่อน

    Bon kalindo yemweyo osaopa osatopa

  • @AlickJam
    @AlickJam 3 หลายเดือนก่อน

    My malawi

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz 3 หลายเดือนก่อน

    Chakwela tikuonesa