BRIAN BANDA KUWELENGA NKHANI

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 97

  • @SkabhuKabhu
    @SkabhuKabhu 2 หลายเดือนก่อน +8

    Kodi kuyeselela masango ziyamba chaka chino ifetu sikuyamba kuvota sitinamvepo zoyeselela masango zitheka bwanji

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 2 หลายเดือนก่อน +3

    Don't worry guys, next year kaboma aka kakuturuka basi 😂😂😂 and sikazabweranso

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 2 หลายเดือนก่อน +8

    Tangotsegulani kawundula olembetsa osati zomwe mukunena apa zoyesera.
    Maina omwe muyeserawo mutani nawo?
    Please ngati mukupita kuma church pangani chilungamo for the first time

    • @Sofi-p1v
      @Sofi-p1v 2 หลายเดือนก่อน +1

      Kweshoni

  • @NAKHWAIYANA
    @NAKHWAIYANA 2 หลายเดือนก่อน +1

    Timenyanatu, from when? Why you didn't imform as before zakuvutani then muti timayesela zida fosek

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 2 หลายเดือนก่อน +3

    Kod ayesela bwanji mmalo mongoyama..., zoyesazo ndie zitiso..,,, ndayamba kukaika guys

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo 2 หลายเดือนก่อน +5

    Mwaonatu umunthu alinawo anthu aku Malawi kupulumutsa anthu pa ngozi,funso mkumati Kwa Mr chikangawa ndi achina yudasi munakanika bwanji kuwapulumutsa a vice president ndi anthu ena ???

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 2 หลายเดือนก่อน +1

    Zachison kwambiri anthu akumwa madzi okuda chocho 😢😢😢😢 I wish ndikanakhala othekela kuthandiza ndikawakumbila mjigo boma lipangepo kanthu please please zililiso

  • @EllieMvoso
    @EllieMvoso 2 หลายเดือนก่อน +2

    Born kalindo anachenjeza kale izi azipani zotsutsa boma musafatse moonjeza akuberani zisankho mutu uli gwaaa

  • @kondwanisikatoleka7354
    @kondwanisikatoleka7354 2 หลายเดือนก่อน +5

    Musalorere pliz...!!! Masankho sayeserera,, uku mkuba😢😢😢😢

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 2 หลายเดือนก่อน

    Abrian banda komatu ngozi yathu ija alo modzi opolumuka anthu 9 awa adzathuwa bwanji anthu atatu kupulumuka modzi,plz tifusutsileni amw.

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 2 หลายเดือนก่อน +2

    Nthawi yoyeselela machine azisankho tilibe sitingaipeze, plz aChakwela ndi abale anu mutha kuwayesa nde mutiuze

  • @BwanaGD
    @BwanaGD 2 หลายเดือนก่อน +4

    Kalembera oyesera zichani zakuba bas kuyambira liti zimenezi gati ntchito simuntha osagonena bwanji mafilim anu tawadziwa

  • @DysonKamama-yh7hq
    @DysonKamama-yh7hq 2 หลายเดือนก่อน +3

    Zisankho samayeselela akufuna abele

  • @JohnWalekana-z2f
    @JohnWalekana-z2f 2 หลายเดือนก่อน +3

    Chisankho sichimayeseledwa akufuna abele mavote, inu osusa musamale muzalila

  • @ThokozaniBondo-em9fr
    @ThokozaniBondo-em9fr 2 หลายเดือนก่อน +2

    Tiwonepo bwino apa zinayamba zachitikapo zimenezo chibwana ichi anthu akuvutika dziko muno ndye muzipanga masewera anuwo

  • @SteveriaNyalugwe
    @SteveriaNyalugwe 2 หลายเดือนก่อน

    Akayenderenso dera la Mulanje Pasani mmudzi mwa Nkwaira anthu akyenda mtunda wa 3 kilometres kuti apedze madzi akumwa, anthu akumagona pa chitsime kudikilira madzi. Mijigo inawonongeka pomwe inawuma madzi sakutuluka. Mapaipi amadzi awaterboard anachotsa ndi cholinga choti anthu adzilipira ndikuika mapaipi awo, koma mapaipi awowo sakugwiranso ntchito. Anthu akuvutika kowopsa zikumaphweka kwa munthu yemwe ali ndi njinga koma amene alibe akumwa madzi adzithaphwi.

  • @JoyceLiwonde
    @JoyceLiwonde 2 หลายเดือนก่อน

    Kuyesela ku vote 😂😂😂😂 tikayesera PA ndani za ziiiiih

  • @ManuelLifa-s9o
    @ManuelLifa-s9o 2 หลายเดือนก่อน

    Zisiru dzosavazo zapangisa kare

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz 2 หลายเดือนก่อน +2

    Pasapezeke Malawi opita kukavota zoyeselelazi plizzzz anthu awa afuna atiputsitse amalawi chondeeeee

  • @AishaChipande
    @AishaChipande 2 หลายเดือนก่อน +3

    Ndiye ndege yanthu ija zinatheka bwanji kusapulumusa anthu 9 ajaa km achakwela😢😢😢😢😢😢😢😢 munamulakwila chilima

  • @WilliamGama-w8m
    @WilliamGama-w8m 2 หลายเดือนก่อน

    Kuyesako anthu adzikavotera ndani?

  • @InnohLukah.1998
    @InnohLukah.1998 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mmalo moti igwe ndege ya chakwera 😂😂😂😂

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe mtali manja usamalize ndi maprogram akowo, unavapo kuti zoyetselera mavote

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl 2 หลายเดือนก่อน

    Zoyeserazo ayesele pa anthu 10 okha zinazo mzanong'onedza bondo

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 หลายเดือนก่อน +1

    Ku Malawi nkhani ya kuvuta kwa madxi musaname kuti ndi chifukwa cha kuchuluka kwa anthu ayi nkhani ndi kusakhala ndi chidwi cha atsogoleli aundina wamadzi South Africa ili ndi anthu kuposa malawi koma simungamve nkhani yovuta kwa madzi ngati malawi nkhani malawi aphungu kuzikundikira

  • @ShalifuMatola
    @ShalifuMatola 2 หลายเดือนก่อน

    Mukutimwesa za boza

  • @SaeedMaunde
    @SaeedMaunde 2 หลายเดือนก่อน

    A mec samalani kayetsedwe ka chisankho posakondela mbali otherwise any mistake zizayambitsa nkhondo mu dziko lathu n you will be answerable!!!!!!

  • @MathiasEgama
    @MathiasEgama 2 หลายเดือนก่อน

    Ndili ndi Funso,Kodi mukakhala pa mupikisano ndiye wina akuyamba kutukwana,chimathandauza chani ???? Answer me please

  • @SheenahMwalabu-iz3pr
    @SheenahMwalabu-iz3pr 2 หลายเดือนก่อน

    First to comment ❤ Brian Banda moto 😊

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 หลายเดือนก่อน

    Akufuna kuyesela kubela mavote agalu amenewa

  • @YusufuAnafi-e6v
    @YusufuAnafi-e6v 2 หลายเดือนก่อน +5

    Zakuchikangawa zija sizinakwanile?😢😢😢😢

  • @JoyceLiwonde
    @JoyceLiwonde 2 หลายเดือนก่อน

    Denge ya chakwela igwa liti Eish 😂😂😂

  • @MariaButao
    @MariaButao 2 หลายเดือนก่อน

    Pajatu bon ananena kale kuti kuyeselelako afuna abere anthuwa...zodabwitsatu zitsankho amayeselela???chonde amalawi umphawi watikwana osapitako kuzitsankho zoyeselela akavote onkha

  • @CassimMbalaka
    @CassimMbalaka 2 หลายเดือนก่อน

    Tipanga mademo mukapanga xibwana

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 2 หลายเดือนก่อน

    Ndpo inagwa ndege ya iye chikangawa aMalawi akanasangalala..pano chili kwa papa kukamugwadira

  • @FleasherIshmael
    @FleasherIshmael 2 หลายเดือนก่อน

    Musamaletu mayi mpinganjira amalawi siwopusatu

  • @JoyceLiwonde
    @JoyceLiwonde 2 หลายเดือนก่อน

    😢😢Athu adakavutika madzi eeeeeh koma malawi

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft 2 หลายเดือนก่อน

    Ma vote sayesera

  • @JamesDaud-jz7uq
    @JamesDaud-jz7uq 2 หลายเดือนก่อน

    Chisankho sayesera kumeneko ndi kuba kodi ziyamba Chaka chino zimenezi Koma Bon kalindo akamayankhula musamazitenge Ngati ndiwamisala,,,,Koma Chalakwe

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 2 หลายเดือนก่อน

    Iwe hule iwe ukangopanga masewela uzawona

  • @WillmotChiuimia-vr6ou
    @WillmotChiuimia-vr6ou 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi mavotiso amayesereraso? Aaa koma ndiye kubatu uku eshiii ineso ndakayika ndithu

  • @PatrickMtira
    @PatrickMtira 2 หลายเดือนก่อน

    Bodza akufuna kubera

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂 kuti mudzaphatikize ndi mavote a mr chikangawa yooo

  • @SteviePatrick-g2p
    @SteviePatrick-g2p 2 หลายเดือนก่อน

    Mankhwala osavomelezeka alokod

  • @JacquereenPereira
    @JacquereenPereira 2 หลายเดือนก่อน +2

    Ango funa kubela mavoti

  • @SifatiMoses
    @SifatiMoses 2 หลายเดือนก่อน

    Ndipo sizinachitikepo kuyetselera mavote mu mbiri yathu muno malawi.

  • @EdenNgulube
    @EdenNgulube 2 หลายเดือนก่อน

    Kuyetselela zitsankho zimenezo ndizoona? Mmm kumalawi ndikovetsa chisoni

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂 makhwara kulibe muzipatara nde athu azitani ngati mukuligulitsa mankhwara afake vuto ndi utsogoleri ukungo baaa nde zili bwanji muzipatara

  • @PatrickcDecembers
    @PatrickcDecembers 2 หลายเดือนก่อน +2

    Koma Dpp idakhala zambiri osawapatsako mijigo mmaderawa.

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 2 หลายเดือนก่อน

    Koma ma camera tameyesetsani ku times uko

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 2 หลายเดือนก่อน

    Boba liziyesesa anthu akumudzi akuvutika

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 2 หลายเดือนก่อน +1

    a mec osadzalora kupanga chibwana kut wina akuguleni AYI
    otherwise tizavotaso kawili

  • @Paul-q2p
    @Paul-q2p 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kuyeselela mutsalole akuba awo

  • @emmanuelchimela4656
    @emmanuelchimela4656 2 หลายเดือนก่อน

    Anthu asalole izi pakuti ife makani wina azichita kulawila

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 2 หลายเดือนก่อน

    anthu awa akufuna kubela koma sayezera kuno kumalawi zibwana zimenezo muwona anthu apite kumeneko ndi mbunzi kwabasi ndipo kuyesera uku kubera munja chaka chamawa munthamanga inu ameke

  • @MatthewsJanuary
    @MatthewsJanuary 2 หลายเดือนก่อน

    Ngati kuli kuyeserera yesani anthu 100 okha,osatizimene mukunama apazi

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 2 หลายเดือนก่อน

    NDIPO NAWO AZIPANI ZOTSUTSA AKANGOYEREKEZA KUVOMEREZA ZOYESERERAZO PAMENEPO NDI PAMENE ATATHERE AWA ASANAMIZE A MALAWI ZISANKHO SITIMAYESERA KUYAMBIRA KALE ZITHEKABWANJI LERO NDI LERO CHONDE INU OSUSA BOMA MUSAVOMEREZE ZIMENEZO MUKANGOVOMERA MWALUZIRATU 2025 ISANAFIKE

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 2 หลายเดือนก่อน

    Aziyesera zichani chibwana chimenecho osangoyesera iwo okha mma ofesimo bwanji mpaka kuyesera malo 100 aaaaaaa

  • @moosamlembe3939
    @moosamlembe3939 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi basi malawi atsegulira ngozi za ndege?😢😢😢😢😢😢

  • @PanganoChilambe
    @PanganoChilambe 2 หลายเดือนก่อน

    Sure mungakambe muyesa machine ameki muziyakhula ngati enanso anapita kusukulu osamakamba ngati muuza ana akalasi wani kuti nonse mwakhonza mwamva

  • @Giftphirih-p3r
    @Giftphirih-p3r 2 หลายเดือนก่อน

    Kuyeselera eti ai zikomo

  • @luckymalata3387
    @luckymalata3387 2 หลายเดือนก่อน

    Kwa nsundwe kulibe mazi timamwa apazithaphwi

  • @GeoegeGRSHala
    @GeoegeGRSHala 2 หลายเดือนก่อน

    Mwachita makora kupanga test pankhani yachisankho than Kuti mukozgane naamadam tepex

  • @MosesMkandawi-e2v
    @MosesMkandawi-e2v 2 หลายเดือนก่อน

    Zonsezi zikudikila Peter muthalila osati gwape uyu alipoyu ayi uyu kwake ndi Kuba
    Basi demon

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 2 หลายเดือนก่อน

    Amayi Ntalimanja zomatiyesa ife ayi

  • @JeanfatsanJere
    @JeanfatsanJere 2 หลายเดือนก่อน

    Palibe zimenezo muziyeserela chani anthu inuyo musalore izi zisachitike akufuna zitheke zomwe anakoza a MCP

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 2 หลายเดือนก่อน

    Zisankho mpaka kuyetsera kae mmm kubera mavoti uku.

  • @MoosaChirwa
    @MoosaChirwa 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi kuyeselerako osamapanga nokhanokha ogwira Ku MEC konko bwanji mukufuna kuyesa dziko lose game yanji musewera Kodi

  • @JonathanMunthali-n3c
    @JonathanMunthali-n3c 2 หลายเดือนก่อน

    Ukhuluku basi dziko lapansi nkoyamba kumva zoyesera utambwali

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 2 หลายเดือนก่อน

    Imeneso nde yiti,,,,kod zoyesedwa zabwera ndindani??? Zachanba akufuna kubwera agalu amenewa

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 2 หลายเดือนก่อน

    Paja chakwera ngwa satanic mmene zayambira kugwa ndegee zizingogwa basi. Chifukwa analowetsa kale ziwanda mdziko..chibusa choipa

  • @Ertyvhk
    @Ertyvhk 2 หลายเดือนก่อน

    Zisankho zinayamba zayesedwa ? Izitu zofuna kusamalanazo izi

  • @EllahEllah-hu7hi
    @EllahEllah-hu7hi 2 หลายเดือนก่อน

    Koma plz chikangawa party wat au trying to play,,tangotulutsani report iyaaa

  • @ZekezekeNjala
    @ZekezekeNjala 2 หลายเดือนก่อน

    Mundegemo amomaona ngati munali manganya

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 2 หลายเดือนก่อน

    Zinayambaso zachitika kuti zoyesera zisankho apposition osalora zopusazo akufuna kubera agalu awa

  • @alexmkolongo3089
    @alexmkolongo3089 2 หลายเดือนก่อน

    Koma kuba kwake zakuti zomayesela machine fodya et

  • @JosephyMakunganya
    @JosephyMakunganya 2 หลายเดือนก่อน

    Dpp ikapusa ayibela mavoti for sure

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy 2 หลายเดือนก่อน

    Anthu amaba koma or wakubayo yekha adzadabwa kut sakuwinabe 😂😂😂

  • @LasieMolebatsi
    @LasieMolebatsi 2 หลายเดือนก่อน

    Ife zimenezo ayi

  • @Yoxym
    @Yoxym 2 หลายเดือนก่อน

    Koma kumwera kuno why😭😭😭😭😭🇲🇼anthu akuchita kumwa madzi apachitsime koma boma kungoti zii ayi mutifuna nthawi yamavoti

    • @SteveriaNyalugwe
      @SteveriaNyalugwe 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo zaka zammbuyomu madzi samkavuta kwambiri koma litalowa boma ili linasintha mapaipi kuwapatsa mpata a waterboard akuti cholinga anthu akumudzi asamangomwa madzi aulere adzilipira pakutha pamwezi. Lero anthu akuvutika kowopsa chifukwa cha zimenezo. Akanachotsa zimapaipi zawozo ndikubwenzeretsa zakale zomwezo bwenzi anthu asakuvutika ayi

  • @JosephyMakunganya
    @JosephyMakunganya 2 หลายเดือนก่อน

    Chakwera paja he says Alowaso Boma ,Why he has confidence????

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 2 หลายเดือนก่อน

    Chikangawa mashende yake

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 2 หลายเดือนก่อน

    Iya mwasitha kuti chani sizinachitikepo izo mukunenaizo ayi mukufuna kuti akawina pita muzamuphe ayi mwarephera

  • @WinerdShadreck
    @WinerdShadreck 2 หลายเดือนก่อน

    Zisankho amayeserera???? Kuba masana

    • @EugeniaNgoyi
      @EugeniaNgoyi 2 หลายเดือนก่อน +2

      Zija ankanena born kalindo zija zoti abweretsa machine anew cholinga chaka chamawa azizati ena anavota kale. Agalu amenewa

  • @CardoJustin
    @CardoJustin 2 หลายเดือนก่อน

    Sizithekha masankho sayeserera mwauponda

  • @MaryJefry
    @MaryJefry 2 หลายเดือนก่อน

    Masankho amaeseredwa?zakuba basi

  • @MosesMkandawi-e2v
    @MosesMkandawi-e2v 2 หลายเดือนก่อน

    Musalore anthu wotsutsa kuti ayeselele chifukwa akupwetekani futi samayeselera PA munthu ndee Amec ndi chakwela Ali PA ubale pobeal zisankho chonde a opposition Musalore kuyeselera ayi mapeto ake muputa mkhwiyo WA a Malawi wochuluka

  • @KalipentalaJamu
    @KalipentalaJamu 2 หลายเดือนก่อน

    Osalola ayi

  • @phillkaunda5623
    @phillkaunda5623 2 หลายเดือนก่อน

    This is a lie. The new already how to say to the citizens

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam 2 หลายเดือนก่อน

    Izi za testing ndizachamba kwambili wy a position alora zimenezi guy's aamcp azapweteka zipani zina akufuna kubera awa

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 2 หลายเดือนก่อน +2

    No Tpex please

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 2 หลายเดือนก่อน

    Tangotsegulani kawundula olembetsa osati zomwe mukunena apa zoyesera.
    Maina omwe muyeserawo mutani nawo?
    Please ngati mukupita kuma church pangani chilungamo for the first time