Tangotsegulani kawundula olembetsa osati zomwe mukunena apa zoyesera. Maina omwe muyeserawo mutani nawo? Please ngati mukupita kuma church pangani chilungamo for the first time
Mwaonatu umunthu alinawo anthu aku Malawi kupulumutsa anthu pa ngozi,funso mkumati Kwa Mr chikangawa ndi achina yudasi munakanika bwanji kuwapulumutsa a vice president ndi anthu ena ???
Ku Malawi nkhani ya kuvuta kwa madxi musaname kuti ndi chifukwa cha kuchuluka kwa anthu ayi nkhani ndi kusakhala ndi chidwi cha atsogoleli aundina wamadzi South Africa ili ndi anthu kuposa malawi koma simungamve nkhani yovuta kwa madzi ngati malawi nkhani malawi aphungu kuzikundikira
Musalore anthu wotsutsa kuti ayeselele chifukwa akupwetekani futi samayeselera PA munthu ndee Amec ndi chakwela Ali PA ubale pobeal zisankho chonde a opposition Musalore kuyeselera ayi mapeto ake muputa mkhwiyo WA a Malawi wochuluka
Tangotsegulani kawundula olembetsa osati zomwe mukunena apa zoyesera. Maina omwe muyeserawo mutani nawo? Please ngati mukupita kuma church pangani chilungamo for the first time
Kodi kuyeselela masango ziyamba chaka chino ifetu sikuyamba kuvota sitinamvepo zoyeselela masango zitheka bwanji
Don't worry guys, next year kaboma aka kakuturuka basi 😂😂😂 and sikazabweranso
Tangotsegulani kawundula olembetsa osati zomwe mukunena apa zoyesera.
Maina omwe muyeserawo mutani nawo?
Please ngati mukupita kuma church pangani chilungamo for the first time
Kweshoni
Timenyanatu, from when? Why you didn't imform as before zakuvutani then muti timayesela zida fosek
Kod ayesela bwanji mmalo mongoyama..., zoyesazo ndie zitiso..,,, ndayamba kukaika guys
Mwaonatu umunthu alinawo anthu aku Malawi kupulumutsa anthu pa ngozi,funso mkumati Kwa Mr chikangawa ndi achina yudasi munakanika bwanji kuwapulumutsa a vice president ndi anthu ena ???
Zachison kwambiri anthu akumwa madzi okuda chocho 😢😢😢😢 I wish ndikanakhala othekela kuthandiza ndikawakumbila mjigo boma lipangepo kanthu please please zililiso
Born kalindo anachenjeza kale izi azipani zotsutsa boma musafatse moonjeza akuberani zisankho mutu uli gwaaa
Musalorere pliz...!!! Masankho sayeserera,, uku mkuba😢😢😢😢
Abrian banda komatu ngozi yathu ija alo modzi opolumuka anthu 9 awa adzathuwa bwanji anthu atatu kupulumuka modzi,plz tifusutsileni amw.
Nthawi yoyeselela machine azisankho tilibe sitingaipeze, plz aChakwela ndi abale anu mutha kuwayesa nde mutiuze
Kalembera oyesera zichani zakuba bas kuyambira liti zimenezi gati ntchito simuntha osagonena bwanji mafilim anu tawadziwa
Zisankho samayeselela akufuna abele
Chisankho sichimayeseledwa akufuna abele mavote, inu osusa musamale muzalila
Tiwonepo bwino apa zinayamba zachitikapo zimenezo chibwana ichi anthu akuvutika dziko muno ndye muzipanga masewera anuwo
Akayenderenso dera la Mulanje Pasani mmudzi mwa Nkwaira anthu akyenda mtunda wa 3 kilometres kuti apedze madzi akumwa, anthu akumagona pa chitsime kudikilira madzi. Mijigo inawonongeka pomwe inawuma madzi sakutuluka. Mapaipi amadzi awaterboard anachotsa ndi cholinga choti anthu adzilipira ndikuika mapaipi awo, koma mapaipi awowo sakugwiranso ntchito. Anthu akuvutika kowopsa zikumaphweka kwa munthu yemwe ali ndi njinga koma amene alibe akumwa madzi adzithaphwi.
Kuyesela ku vote 😂😂😂😂 tikayesera PA ndani za ziiiiih
Zisiru dzosavazo zapangisa kare
Pasapezeke Malawi opita kukavota zoyeselelazi plizzzz anthu awa afuna atiputsitse amalawi chondeeeee
Ndiye ndege yanthu ija zinatheka bwanji kusapulumusa anthu 9 ajaa km achakwela😢😢😢😢😢😢😢😢 munamulakwila chilima
Kuyesako anthu adzikavotera ndani?
Mmalo moti igwe ndege ya chakwera 😂😂😂😂
Iwe mtali manja usamalize ndi maprogram akowo, unavapo kuti zoyetselera mavote
Zoyeserazo ayesele pa anthu 10 okha zinazo mzanong'onedza bondo
Ku Malawi nkhani ya kuvuta kwa madxi musaname kuti ndi chifukwa cha kuchuluka kwa anthu ayi nkhani ndi kusakhala ndi chidwi cha atsogoleli aundina wamadzi South Africa ili ndi anthu kuposa malawi koma simungamve nkhani yovuta kwa madzi ngati malawi nkhani malawi aphungu kuzikundikira
Mukutimwesa za boza
A mec samalani kayetsedwe ka chisankho posakondela mbali otherwise any mistake zizayambitsa nkhondo mu dziko lathu n you will be answerable!!!!!!
Ndili ndi Funso,Kodi mukakhala pa mupikisano ndiye wina akuyamba kutukwana,chimathandauza chani ???? Answer me please
First to comment ❤ Brian Banda moto 😊
Akufuna kuyesela kubela mavote agalu amenewa
Zakuchikangawa zija sizinakwanile?😢😢😢😢
Denge ya chakwela igwa liti Eish 😂😂😂
Pajatu bon ananena kale kuti kuyeselelako afuna abere anthuwa...zodabwitsatu zitsankho amayeselela???chonde amalawi umphawi watikwana osapitako kuzitsankho zoyeselela akavote onkha
Tipanga mademo mukapanga xibwana
Ndpo inagwa ndege ya iye chikangawa aMalawi akanasangalala..pano chili kwa papa kukamugwadira
Musamaletu mayi mpinganjira amalawi siwopusatu
😢😢Athu adakavutika madzi eeeeeh koma malawi
Ma vote sayesera
Chisankho sayesera kumeneko ndi kuba kodi ziyamba Chaka chino zimenezi Koma Bon kalindo akamayankhula musamazitenge Ngati ndiwamisala,,,,Koma Chalakwe
Iwe hule iwe ukangopanga masewela uzawona
Kodi mavotiso amayesereraso? Aaa koma ndiye kubatu uku eshiii ineso ndakayika ndithu
Bodza akufuna kubera
😂😂😂😂😂 kuti mudzaphatikize ndi mavote a mr chikangawa yooo
Mankhwala osavomelezeka alokod
Ango funa kubela mavoti
Ndipo sizinachitikepo kuyetselera mavote mu mbiri yathu muno malawi.
Kuyetselela zitsankho zimenezo ndizoona? Mmm kumalawi ndikovetsa chisoni
😂😂😂 makhwara kulibe muzipatara nde athu azitani ngati mukuligulitsa mankhwara afake vuto ndi utsogoleri ukungo baaa nde zili bwanji muzipatara
Koma Dpp idakhala zambiri osawapatsako mijigo mmaderawa.
Koma ma camera tameyesetsani ku times uko
Boba liziyesesa anthu akumudzi akuvutika
a mec osadzalora kupanga chibwana kut wina akuguleni AYI
otherwise tizavotaso kawili
Kuyeselela mutsalole akuba awo
Anthu asalole izi pakuti ife makani wina azichita kulawila
anthu awa akufuna kubela koma sayezera kuno kumalawi zibwana zimenezo muwona anthu apite kumeneko ndi mbunzi kwabasi ndipo kuyesera uku kubera munja chaka chamawa munthamanga inu ameke
Ngati kuli kuyeserera yesani anthu 100 okha,osatizimene mukunama apazi
NDIPO NAWO AZIPANI ZOTSUTSA AKANGOYEREKEZA KUVOMEREZA ZOYESERERAZO PAMENEPO NDI PAMENE ATATHERE AWA ASANAMIZE A MALAWI ZISANKHO SITIMAYESERA KUYAMBIRA KALE ZITHEKABWANJI LERO NDI LERO CHONDE INU OSUSA BOMA MUSAVOMEREZE ZIMENEZO MUKANGOVOMERA MWALUZIRATU 2025 ISANAFIKE
Aziyesera zichani chibwana chimenecho osangoyesera iwo okha mma ofesimo bwanji mpaka kuyesera malo 100 aaaaaaa
Kodi basi malawi atsegulira ngozi za ndege?😢😢😢😢😢😢
Sure mungakambe muyesa machine ameki muziyakhula ngati enanso anapita kusukulu osamakamba ngati muuza ana akalasi wani kuti nonse mwakhonza mwamva
Kuyeselera eti ai zikomo
Kwa nsundwe kulibe mazi timamwa apazithaphwi
Mwachita makora kupanga test pankhani yachisankho than Kuti mukozgane naamadam tepex
Zonsezi zikudikila Peter muthalila osati gwape uyu alipoyu ayi uyu kwake ndi Kuba
Basi demon
Amayi Ntalimanja zomatiyesa ife ayi
Palibe zimenezo muziyeserela chani anthu inuyo musalore izi zisachitike akufuna zitheke zomwe anakoza a MCP
Zisankho mpaka kuyetsera kae mmm kubera mavoti uku.
Kodi kuyeselerako osamapanga nokhanokha ogwira Ku MEC konko bwanji mukufuna kuyesa dziko lose game yanji musewera Kodi
Ukhuluku basi dziko lapansi nkoyamba kumva zoyesera utambwali
Imeneso nde yiti,,,,kod zoyesedwa zabwera ndindani??? Zachanba akufuna kubwera agalu amenewa
Paja chakwera ngwa satanic mmene zayambira kugwa ndegee zizingogwa basi. Chifukwa analowetsa kale ziwanda mdziko..chibusa choipa
Zisankho zinayamba zayesedwa ? Izitu zofuna kusamalanazo izi
Koma plz chikangawa party wat au trying to play,,tangotulutsani report iyaaa
Mundegemo amomaona ngati munali manganya
Zinayambaso zachitika kuti zoyesera zisankho apposition osalora zopusazo akufuna kubera agalu awa
Koma kuba kwake zakuti zomayesela machine fodya et
Dpp ikapusa ayibela mavoti for sure
Anthu amaba koma or wakubayo yekha adzadabwa kut sakuwinabe 😂😂😂
Ife zimenezo ayi
Koma kumwera kuno why😭😭😭😭😭🇲🇼anthu akuchita kumwa madzi apachitsime koma boma kungoti zii ayi mutifuna nthawi yamavoti
Ndipo zaka zammbuyomu madzi samkavuta kwambiri koma litalowa boma ili linasintha mapaipi kuwapatsa mpata a waterboard akuti cholinga anthu akumudzi asamangomwa madzi aulere adzilipira pakutha pamwezi. Lero anthu akuvutika kowopsa chifukwa cha zimenezo. Akanachotsa zimapaipi zawozo ndikubwenzeretsa zakale zomwezo bwenzi anthu asakuvutika ayi
Chakwera paja he says Alowaso Boma ,Why he has confidence????
Chikangawa mashende yake
Iya mwasitha kuti chani sizinachitikepo izo mukunenaizo ayi mukufuna kuti akawina pita muzamuphe ayi mwarephera
Zisankho amayeserera???? Kuba masana
Zija ankanena born kalindo zija zoti abweretsa machine anew cholinga chaka chamawa azizati ena anavota kale. Agalu amenewa
Sizithekha masankho sayeserera mwauponda
Masankho amaeseredwa?zakuba basi
Musalore anthu wotsutsa kuti ayeselele chifukwa akupwetekani futi samayeselera PA munthu ndee Amec ndi chakwela Ali PA ubale pobeal zisankho chonde a opposition Musalore kuyeselera ayi mapeto ake muputa mkhwiyo WA a Malawi wochuluka
Osalola ayi
This is a lie. The new already how to say to the citizens
Izi za testing ndizachamba kwambili wy a position alora zimenezi guy's aamcp azapweteka zipani zina akufuna kubera awa
No Tpex please
Tangotsegulani kawundula olembetsa osati zomwe mukunena apa zoyesera.
Maina omwe muyeserawo mutani nawo?
Please ngati mukupita kuma church pangani chilungamo for the first time