The greatest ever president to rule Malawi 🇲🇼. He was a man of great intelligence and wisdom, a God fearing man and a man of great love for his people and his country. He died for the flag of Malawi 🇲🇼
Munayesesa kupanga control zinthu kukana kubvomeleza zinthu zoipa that's y Malawi amabvutika koma munthu ndi munthu kubvuta kunvesesa amatilowa kamba ka thandizo lawo for this moment i would like to say thank you for your strong my president will remember you all time RIP
Koma president ngati uyu tizamupezanso, Koma mbuzi ilipanoyi ati chakwera
This one was truly gifted to rule this country... may his soul continue resting in eternal peace.... we miss your love
BINGU the legend
Great man, we still miss you boss.
The best presedent we had in Malawi still remember u Mr Presedent u showed us that Malawians can also export 😍
Kulakwa ndi umuthu kukhululuka ndi mulungu we miss you bingu
This issue was extremely, extremely, extremely deep
In him was the spirit to set Malawi free from the bondage of internal slavery.
good leader that we will never have again in Malawi
Abingu mwatisila nkhondo Kuno chakwera wa chipani cha MCP akutipha amalawi
Wise man Bingu
The greatest ever president to rule Malawi 🇲🇼. He was a man of great intelligence and wisdom, a God fearing man and a man of great love for his people and his country. He died for the flag of Malawi 🇲🇼
Great man ever
Which Bible did the president read which says "to err is human, to forgive is divin."?
Sitizapezanso mtsogoleri oposa uyu oohhh BINGUUUU
Amenewoo timati wakulu akakhale ku paladaiiizo kumwambako
Bingu was a President wawa. He was a president yet some disgruntled Malawians betrayed him
We Miss u a lot Bingu 😭
He was really a good leader
He was a Patriot
May your soul keep resting in Gods love....i miss you and i cry everyday...you were the best Dad.....
Awa adali abwana awa......much respect
Great presdent ever..... Continue resting in peace
i miss this moment
Zinangowona kuvuta, kuti Bambowa anaticia
Munayesesa kupanga control zinthu kukana kubvomeleza zinthu zoipa that's y Malawi amabvutika koma munthu ndi munthu kubvuta kunvesesa amatilowa kamba ka thandizo lawo for this moment i would like to say thank you for your strong my president will remember you all time RIP
Bingu may your soul continue resting in peace
Dzimu wanu uziwutsa muntendele bwana
Bingu munthalira once said.
Awa ndiye anali akatundu osati zilipo lerozi zingovomera zilizonse zonyasa
Sipazapezekaso ngati uyu amalawi tonaluza musogoleli waluntha kwambiri osati achina bakili anangiwononga Malawi basi kumusiya paumoto pano ndi izi daily kulira
Iwe ndiye unali dolo
Great leader
Everyone miss you rest in peace
RIP Bingu
I miss you sir...RiP
Malawins are still mouning
We loose Good God fearing leader may your soul rest everlasting peace
MYSRIP
Best ward let president
Nyasi zimenezidi kumalawi sizikufunika
Munthu uyuyu analidi wanzeru
good
Ause muntendere munthu wankulu, udayesetsa mbali yako
RIP
Adali akatundu moris Tayali mangochi
Zoona
hehehe
zoona.Munthu wanzeru
The best presedent we had in Malawi still remember u Mr Presedent u showed us that Malawians can also export 😍