FELIX NJAWALA WASAMBWANZA CHIPANI CHA MCP NDIPO WASIMIKIZADI KUTI ANATULUKA MU TONSE ALLIANCE

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 17 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 120

  • @violetpotani
    @violetpotani 2 หลายเดือนก่อน +14

    Munasowatu Mr Njawala.. Welcome back

  • @RafickOsama-k2r
    @RafickOsama-k2r 15 วันที่ผ่านมา

    Your welcome to Malawi 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 🇲🇼

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 2 หลายเดือนก่อน +11

    Exactly mr njawala u ar true man osati uyu akumuti manganya

    • @fannyzimba149
      @fannyzimba149 2 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂

  • @deniskondani1305
    @deniskondani1305 2 หลายเดือนก่อน

    Felix ndi more fire

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 2 หลายเดือนก่อน +3

    APA NDAWONADI KUTI UTM INAKALU YAMPHAMVU.. Ndubwera konko bola osamphwekensaso..!! More fire 🔥 UTM

  • @MuyaoComedies
    @MuyaoComedies 2 หลายเดือนก่อน +3

    I'm following, Salam alaikum

  • @BeatriceProfessor
    @BeatriceProfessor 2 หลายเดือนก่อน +1

    Tell them ❤❤❤

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 2 หลายเดือนก่อน

    More fire Njawala

  • @sesfikileshop7344
    @sesfikileshop7344 2 หลายเดือนก่อน

    Felix Njawala my man

  • @CarolynMtegha
    @CarolynMtegha 2 หลายเดือนก่อน

    Good speech Felix Njawala.

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 2 หลายเดือนก่อน +1

    Madam kaliyati for President ❤❤❤

  • @BrianNowa
    @BrianNowa 2 หลายเดือนก่อน +1

    Please akulu akulu a UTM takhaliranani pansi pasakhale kugawanika mmachitidwe together we can, pasamapezeke Ena odzipatula, pakhale mtsogoleri yemwe adzibwsletsa umodzi ngati mmene SKC amachitila, SKC adali munthu odziwa zomwe akuchita komaso zokomera aliyese, kulibwino kukhalirana pansi kukambilana kusiyana mkumanenana ku ground
    Munthu olalata kwambiri samakhala ndi mphavu, kupita pa ground mkumakalankhula za awo ndi awo sizithandiza chipani koma kuwauza wanthu pomwe muli ndi komwe mukupita ndi zomwe mukufuna kukachita, pewani a Utiko okhala pazenera ooneka ngati Ali nanu koma mkati mwawo Ali kwina, samalani ndi anthu omwe akulowa posatengera mbiri yawo,

  • @RodneySupply-tx3ul
    @RodneySupply-tx3ul 2 หลายเดือนก่อน +7

    Elder my brother ndi zoona zedi mwayankhula and keep it up osaopa

  • @modestamhango7737
    @modestamhango7737 2 หลายเดือนก่อน

    Powerful speech. 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 2 หลายเดือนก่อน +3

    Njawala motooooooooo!!❤

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 2 หลายเดือนก่อน +3

    Anthu ndiomwe amuphetsa Chilima chifukwa iyeyu saamafuna MCP

  • @FrancisMazamba
    @FrancisMazamba 2 หลายเดือนก่อน

    Njawala keep it up mulungu ankhale nawe

  • @AgnessKavalo
    @AgnessKavalo 2 หลายเดือนก่อน

    Kuchotsa mboraaaahhh imene ili MCP 😂😂😂😂😂😂

  • @doreendzimuuzani7180
    @doreendzimuuzani7180 2 หลายเดือนก่อน

    Chilima is still living through his people ❤

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 2 หลายเดือนก่อน

    UTM on🔥🔥🔥🔥❤❤❤

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 หลายเดือนก่อน

    Bomaw ilooo my vote

  • @CathyYobe
    @CathyYobe 2 หลายเดือนก่อน +1

    Utm more fire

  • @NazaniNoah
    @NazaniNoah 2 หลายเดือนก่อน

    Mudalitu limodzi lero muyikana poyera ok,oh!zikomo yenkhova poti inu nokha simukhumudwitsa

  • @EleniJames-rc3ot
    @EleniJames-rc3ot 2 หลายเดือนก่อน

    Mjawala ndimakunyadilani pamodzi mayi kaliyati ndi onse a utm mulandile ulemu wanu 2025 mavoto aku utm

  • @SamuelJoseGaviteni
    @SamuelJoseGaviteni 2 หลายเดือนก่อน +6

    Dr chilima wasiya chipatso ana afundo

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 2 หลายเดือนก่อน +2

    I love u mr njawala

  • @jahmanmakwinja-ef7zn
    @jahmanmakwinja-ef7zn 2 หลายเดือนก่อน

    Words❤

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 หลายเดือนก่อน

    Zikomo Felex njawara kumeneko ndiye kuyankhula tikuziwa zimakuwawani nafeso zimatiwawa

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 หลายเดือนก่อน +2

    Zoona zoona Mr njawala auzeniiiii

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 หลายเดือนก่อน

    Zoona zoona

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 หลายเดือนก่อน +5

    Felix kumeneko ndiye kubwela

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 2 หลายเดือนก่อน +1

    Njawala ,,Fredo ndi Kaliati tikulimba mtima

  • @DynessMsiska
    @DynessMsiska 2 หลายเดือนก่อน

    Moto kuti 🔥🔥

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu 2 หลายเดือนก่อน +1

    Tinkakuuzani ife kuti sapita kawiri, inu munkachita makani lero ndi izi

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 2 หลายเดือนก่อน

    Chimene ndinapeza ine ndichakut Chilima uja was bigger than UTM itself.

  • @DENSONZULU
    @DENSONZULU 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤❤ UTM 🔥

  • @nelsonkajawo5176
    @nelsonkajawo5176 2 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂 awa palibe cha nzeru anganene ndakayikanso ngati ali ndi ma followers

  • @ewn-mc6jv
    @ewn-mc6jv 2 หลายเดือนก่อน +1

    UTM more fire.

  • @AlexSamalan
    @AlexSamalan 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤ one love

  • @MakawaBenjamin
    @MakawaBenjamin 2 หลายเดือนก่อน

    Akumanga chakwera

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 หลายเดือนก่อน

    Mkango ukafa,ana ake sangaleledwe ndi fisi tanthauzo monga ife ana autm kholo lathu mmene lidafera (SKC)mcp singatisunge ndiye tosefe itimenza.

  • @FatimaLuwembe
    @FatimaLuwembe 2 หลายเดือนก่อน

    Welco😊me❤❤

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 หลายเดือนก่อน

    Koma mwanena miyambi yamphamvu Felex chilima adakuphuzisadi eti kkkk

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 2 หลายเดือนก่อน

    Gwilanani manja a UTM ine vote yanga ndzakupatsan, manganya ndi oipa ndpo waonekelatu kuipa kwake sakudzwika mbali

  • @AustinMhone-r3s
    @AustinMhone-r3s 2 หลายเดือนก่อน

    MCP Chipani chankhaza kwambiri don't make alliance with them again.

  • @StalloneButao
    @StalloneButao 2 หลายเดือนก่อน

    Awa ndi adolo

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 2 หลายเดือนก่อน +3

    Ndipo ndizoonadi abale mulungu ativa kulila kwathu ndithu

  • @PETERSINKADZIWA
    @PETERSINKADZIWA 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kuswa kuswa basi. Emusipi No chance

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 2 หลายเดือนก่อน

    Mwini wake wa miyambi anapita inuyo simungaikwanitse pangani fundo zenizeni

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 2 หลายเดือนก่อน

    Uku ndiye kuyankhula osaopa.chiuzeni chilungamo chipani chakupha ndi chakupha basi fisi sasintha ndi fisi basi

  • @GraceLobart
    @GraceLobart 2 หลายเดือนก่อน

    🎉🎉🎉🎉🎉 yomweyoooo❤

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga1781 2 หลายเดือนก่อน

    Ndiye mwabweretsa Kabambe kuti akupititseni ku DPP😢

  • @brownodalla
    @brownodalla 2 หลายเดือนก่อน

    kuthana ndi ululu wa njuchi ndikuchotsa mbola

  • @aggiemlotha1208
    @aggiemlotha1208 2 หลายเดือนก่อน +2

    Chipani chapa FB😂

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 หลายเดือนก่อน

    Inde inde ichotseni mbolayo

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 หลายเดือนก่อน

    Inu a UTM musafooke chifukwa a MCP nawoso anayamba pang,ono pang,ono sanafikile kutenga boma inutso pachedwe pasachedwe muzalowa boma

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 2 หลายเดือนก่อน +2

    😂😂😂😂😂 koma miyambi yabwino bwanjiii?❤❤

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c 2 หลายเดือนก่อน

      Nane ndaifila😂😂

  • @violetkamvanthupi2443
    @violetkamvanthupi2443 2 หลายเดือนก่อน

    Izi ndi zoona

  • @TanazioUziyele
    @TanazioUziyele 2 หลายเดือนก่อน +2

    Aaaa chilima kulibe pangani fundo zanu ajawala

  • @MacfelsonMunthali
    @MacfelsonMunthali 2 หลายเดือนก่อน

    Last kicks of the dying horse,umaliro wachipani

  • @elsontmsukwa4356
    @elsontmsukwa4356 2 หลายเดือนก่อน +1

    Uthenga ogwira mtima 🙏🙏

  • @Chikumbuso-l5m
    @Chikumbuso-l5m 2 หลายเดือนก่อน

    Wayakhula bwino tichose chakwela

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 หลายเดือนก่อน

    Ndiye munalephera bwanji kumusitha chakwalawo poti mwati inu mumasitha

  • @FelistasNkasalaMakumbo
    @FelistasNkasalaMakumbo 2 หลายเดือนก่อน +1

    UTM in my blood

  • @MaryChipeta-y4l
    @MaryChipeta-y4l 2 หลายเดือนก่อน

    Mfundoles Udali kuti wabodza iwe

  • @ShurahbilMakiyi
    @ShurahbilMakiyi 2 หลายเดือนก่อน

    Sindimaganiza kut UTM yatha koma mmmmm❤❤

  • @SamzyTimechisaleh
    @SamzyTimechisaleh 2 หลายเดือนก่อน

    ❤❤

  • @AnaLourencokan
    @AnaLourencokan หลายเดือนก่อน

    Mwapilila

  • @MpapiParadise
    @MpapiParadise 2 หลายเดือนก่อน

    Kkkk awa angomataya nthawi kachipani aka plus ka aford sazalamulilapo boma ai

  • @peterchiutsi
    @peterchiutsi 2 หลายเดือนก่อน

    Guys chipanichi timachikonda koma stop zomangoti chilima chilimazi Mukumatiwawisa mtima

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 หลายเดือนก่อน +4

    Kuyankhula chilingamo kulifela dziko mulungu akutetezele

  • @IsaacAmiyele
    @IsaacAmiyele 2 หลายเดือนก่อน

    Kd guys manganya ndiutiyo paja😢😢😮😮

    • @RebeccaNvenya
      @RebeccaNvenya 2 หลายเดือนก่อน

      Bambo a sikono😂😂😂

  • @elvisnjoka8428
    @elvisnjoka8428 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mudyelatu dzina la malemu hahaha😅

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj 2 หลายเดือนก่อน +1

    Boza munali nose atose alliance mumanga nose musathawe inu a utm palibe chanzeru apo ife tikufuna Dpp ndiyimene inakwarisa zodya katatu inu alliance mwalowesa njala mziko nd umphawi oopya bon kalindo president wa Dpp

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 หลายเดือนก่อน

      Mmm musova inu simumaona ndeu zimachitika zija hiyaaa fundo zanu ndi ziphwasula lembani zina ndani yemwe samaona kuti anthu sakugwirizana??

  • @MartinMajola
    @MartinMajola 10 วันที่ผ่านมา

    Jawala moto ku buuu

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 2 หลายเดือนก่อน

    Kutuluka m'boma kupanga campaign kufuna kulowaso m'boma mukuzitendetsa bwanji kodi ana amasiye inu kufuna undunu kokhakokhako kkkkk nkhope zake zimenezo anjawala mukhale nduna yamalawi aaas pitani ku dpp komko mwaiwalaso muja dpp onazizira chilimamu kathetseni kachipani kothaithako

  • @AlexanderYovatiKhumalo
    @AlexanderYovatiKhumalo 2 หลายเดือนก่อน +2

    Tiyesetse kuzolowera kulankhula zodzetsa mtendere .

  • @SafariBvumbwe
    @SafariBvumbwe 2 หลายเดือนก่อน

    Koma ichi chikulakhula mr njawala

  • @PatrickFicklem
    @PatrickFicklem 2 หลายเดือนก่อน +1

    Za ziiiiiiiii

    • @TemboHaswell
      @TemboHaswell 2 หลายเดือนก่อน

      Wa ziiiii ndiiweyo

    • @PatrickFicklem
      @PatrickFicklem 2 หลายเดือนก่อน

      @@TemboHaswell 🤣🤣🤣🤣🤣

  • @zutamgala
    @zutamgala 2 หลายเดือนก่อน +2

    Alibe fundo uyu

  • @TanazioUziyele
    @TanazioUziyele 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mukukamba zachitukuko mwapanga zotani inu anjawala zaziiiii!!

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน

      Chakwera wakoyo wapanga chani sikungopha Chilima basi

  • @samuelkachimphula7278
    @samuelkachimphula7278 2 หลายเดือนก่อน +1

    Awa ndachitsiru

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน +1

      Chitsiru ndiweyo nd Chakwera okupha Chilima uja

  • @EmmanuelChirwa-z3n
    @EmmanuelChirwa-z3n 2 หลายเดือนก่อน

    Ana inu mwachepa MCP boma mpaka mpaka 😂😂

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 หลายเดือนก่อน

      Mwana Wa njoka iwe zachikale zimenezo anthu ake anapita ndi Kamuzu

  • @kingsleyChisenga-i8g
    @kingsleyChisenga-i8g 2 หลายเดือนก่อน +1

    Pja zimathera pa media pompa zosaopsa ana kulira ndi mkodzo

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 หลายเดือนก่อน

      Pamtumbo panu inu achitsiru mulibe mzeru mkomweso apa

  • @WitnessPhiri-zr9uf
    @WitnessPhiri-zr9uf 2 หลายเดือนก่อน

    Wayankhula wakuva wava mulungu aliko ayankha ma pemphelo athu

  • @ElsonNsowoya
    @ElsonNsowoya 2 หลายเดือนก่อน

    Mawu

  • @patricksamson4852
    @patricksamson4852 2 หลายเดือนก่อน +1

    Uyu akukwanira pa utsogoleri

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 2 หลายเดือนก่อน

    Oh yes 😂😂😂😂, nthawi yakwana.

  • @ShillahChisi
    @ShillahChisi 2 หลายเดือนก่อน

    UTM moto

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 2 หลายเดือนก่อน +5

    Osati 1995 yokha komaso amalawi ambili timakonda chilima

    • @princemajonanga9026
      @princemajonanga9026 2 หลายเดือนก่อน

      Ka background song kanuko kamasokoneza ma audio ambiri maguyz

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo kwambiri kkk

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 2 หลายเดือนก่อน

    MCP chipani cha Kupha aaa, Chakwera Criminal,usi Yudasi adagulisa Chilima aa, Chakwera wazi Wanda aa, Wanthu wopanda manyazi Ndi mzeru u fake pastor

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi muloza chiyani zimene mwapanga chitukuko chake chilikuti anjawala inu 😂😂😂😂😂😂

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 2 หลายเดือนก่อน +1

      Ndalama boma lawapatsa zopangira?

    • @SafariBvumbwe
      @SafariBvumbwe 2 หลายเดือนก่อน +1

      Mmmmmmm inu umbuli chani utm yinalowapo m'boma kkkkkkkk uziganiza kawiri usananene

    • @IssacMateyo
      @IssacMateyo 2 หลายเดือนก่อน

      MBatata iwe choka apa ana ama 2000 sauzande inu sanagwinetu akufunika apiteso kwina akapangeso alayasi Ina zazi

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 2 หลายเดือนก่อน

      @@SafariBvumbwe umbuli otengera kwa inu mmesa

  • @HopesonButao
    @HopesonButao 2 หลายเดือนก่อน

    Koma muli fundo umu

  • @blessingsmangulama8442
    @blessingsmangulama8442 2 หลายเดือนก่อน +1

    lozani zanu ife tiwone. 🤕

  • @tracybennie7783
    @tracybennie7783 2 หลายเดือนก่อน

    Mulungu. Ali. Ndi. Chidwi. Koma so. Akuyona

  • @SophieLupiya
    @SophieLupiya หลายเดือนก่อน

    😂

  • @SamuelJoseGaviteni
    @SamuelJoseGaviteni 2 หลายเดือนก่อน

    Osafoka

  • @FranksonKennethChipande
    @FranksonKennethChipande 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi Mr Njawala campaign yanu izikhala ya Chilima???? Pangani ndale za smart.Musiyeni Chilima apume mumntendere

  • @aggiemlotha1208
    @aggiemlotha1208 2 หลายเดือนก่อน

    You cannot fulfil the idea of someone... chilima was best but not you maguy

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 หลายเดือนก่อน

    Bomaw ilooo my vote