ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Munasowatu Mr Njawala.. Welcome back
Vw
Your welcome to Malawi 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 🇲🇼
Exactly mr njawala u ar true man osati uyu akumuti manganya
😂😂😂😂
Felix ndi more fire
APA NDAWONADI KUTI UTM INAKALU YAMPHAMVU.. Ndubwera konko bola osamphwekensaso..!! More fire 🔥 UTM
I'm following, Salam alaikum
Tell them ❤❤❤
More fire Njawala
Felix Njawala my man
Good speech Felix Njawala.
Madam kaliyati for President ❤❤❤
Please akulu akulu a UTM takhaliranani pansi pasakhale kugawanika mmachitidwe together we can, pasamapezeke Ena odzipatula, pakhale mtsogoleri yemwe adzibwsletsa umodzi ngati mmene SKC amachitila, SKC adali munthu odziwa zomwe akuchita komaso zokomera aliyese, kulibwino kukhalirana pansi kukambilana kusiyana mkumanenana ku groundMunthu olalata kwambiri samakhala ndi mphavu, kupita pa ground mkumakalankhula za awo ndi awo sizithandiza chipani koma kuwauza wanthu pomwe muli ndi komwe mukupita ndi zomwe mukufuna kukachita, pewani a Utiko okhala pazenera ooneka ngati Ali nanu koma mkati mwawo Ali kwina, samalani ndi anthu omwe akulowa posatengera mbiri yawo,
Elder my brother ndi zoona zedi mwayankhula and keep it up osaopa
Thanks brother
Powerful speech. 🔥🔥🔥🔥🔥
Njawala motooooooooo!!❤
Anthu ndiomwe amuphetsa Chilima chifukwa iyeyu saamafuna MCP
Njawala keep it up mulungu ankhale nawe
Kuchotsa mboraaaahhh imene ili MCP 😂😂😂😂😂😂
Chilima is still living through his people ❤
UTM on🔥🔥🔥🔥❤❤❤
Bomaw ilooo my vote
Utm more fire
Mudalitu limodzi lero muyikana poyera ok,oh!zikomo yenkhova poti inu nokha simukhumudwitsa
Mjawala ndimakunyadilani pamodzi mayi kaliyati ndi onse a utm mulandile ulemu wanu 2025 mavoto aku utm
Dr chilima wasiya chipatso ana afundo
Zoona. 🔥🔥🔥
I love u mr njawala
Words❤
Zikomo Felex njawara kumeneko ndiye kuyankhula tikuziwa zimakuwawani nafeso zimatiwawa
Zoona zoona Mr njawala auzeniiiii
Zoona zoona
Felix kumeneko ndiye kubwela
Njawala ,,Fredo ndi Kaliati tikulimba mtima
Moto kuti 🔥🔥
Tinkakuuzani ife kuti sapita kawiri, inu munkachita makani lero ndi izi
Chimene ndinapeza ine ndichakut Chilima uja was bigger than UTM itself.
❤❤❤ UTM 🔥
😂😂😂😂 awa palibe cha nzeru anganene ndakayikanso ngati ali ndi ma followers
UTM more fire.
❤❤ one love
Akumanga chakwera
Mkango ukafa,ana ake sangaleledwe ndi fisi tanthauzo monga ife ana autm kholo lathu mmene lidafera (SKC)mcp singatisunge ndiye tosefe itimenza.
Welco😊me❤❤
Koma mwanena miyambi yamphamvu Felex chilima adakuphuzisadi eti kkkk
Gwilanani manja a UTM ine vote yanga ndzakupatsan, manganya ndi oipa ndpo waonekelatu kuipa kwake sakudzwika mbali
MCP Chipani chankhaza kwambiri don't make alliance with them again.
Awa ndi adolo
Ndipo ndizoonadi abale mulungu ativa kulila kwathu ndithu
Kuswa kuswa basi. Emusipi No chance
Mwini wake wa miyambi anapita inuyo simungaikwanitse pangani fundo zenizeni
Uku ndiye kuyankhula osaopa.chiuzeni chilungamo chipani chakupha ndi chakupha basi fisi sasintha ndi fisi basi
🎉🎉🎉🎉🎉 yomweyoooo❤
Ndiye mwabweretsa Kabambe kuti akupititseni ku DPP😢
kuthana ndi ululu wa njuchi ndikuchotsa mbola
Chipani chapa FB😂
Inde inde ichotseni mbolayo
Inu a UTM musafooke chifukwa a MCP nawoso anayamba pang,ono pang,ono sanafikile kutenga boma inutso pachedwe pasachedwe muzalowa boma
😂😂😂😂😂 koma miyambi yabwino bwanjiii?❤❤
Nane ndaifila😂😂
Izi ndi zoona
Aaaa chilima kulibe pangani fundo zanu ajawala
Last kicks of the dying horse,umaliro wachipani
Uthenga ogwira mtima 🙏🙏
Wayakhula bwino tichose chakwela
Ndiye munalephera bwanji kumusitha chakwalawo poti mwati inu mumasitha
UTM in my blood
Mfundoles Udali kuti wabodza iwe
Sindimaganiza kut UTM yatha koma mmmmm❤❤
❤❤
Mwapilila
Kkkk awa angomataya nthawi kachipani aka plus ka aford sazalamulilapo boma ai
Guys chipanichi timachikonda koma stop zomangoti chilima chilimazi Mukumatiwawisa mtima
Kuyankhula chilingamo kulifela dziko mulungu akutetezele
Kd guys manganya ndiutiyo paja😢😢😮😮
Bambo a sikono😂😂😂
Mudyelatu dzina la malemu hahaha😅
Boza munali nose atose alliance mumanga nose musathawe inu a utm palibe chanzeru apo ife tikufuna Dpp ndiyimene inakwarisa zodya katatu inu alliance mwalowesa njala mziko nd umphawi oopya bon kalindo president wa Dpp
Mmm musova inu simumaona ndeu zimachitika zija hiyaaa fundo zanu ndi ziphwasula lembani zina ndani yemwe samaona kuti anthu sakugwirizana??
Jawala moto ku buuu
Kutuluka m'boma kupanga campaign kufuna kulowaso m'boma mukuzitendetsa bwanji kodi ana amasiye inu kufuna undunu kokhakokhako kkkkk nkhope zake zimenezo anjawala mukhale nduna yamalawi aaas pitani ku dpp komko mwaiwalaso muja dpp onazizira chilimamu kathetseni kachipani kothaithako
Tiyesetse kuzolowera kulankhula zodzetsa mtendere .
Koma ichi chikulakhula mr njawala
Za ziiiiiiiii
Wa ziiiii ndiiweyo
@@TemboHaswell 🤣🤣🤣🤣🤣
Alibe fundo uyu
Mukukamba zachitukuko mwapanga zotani inu anjawala zaziiiii!!
Chakwera wakoyo wapanga chani sikungopha Chilima basi
Awa ndachitsiru
Chitsiru ndiweyo nd Chakwera okupha Chilima uja
Ana inu mwachepa MCP boma mpaka mpaka 😂😂
Mwana Wa njoka iwe zachikale zimenezo anthu ake anapita ndi Kamuzu
Pja zimathera pa media pompa zosaopsa ana kulira ndi mkodzo
Pamtumbo panu inu achitsiru mulibe mzeru mkomweso apa
Wayankhula wakuva wava mulungu aliko ayankha ma pemphelo athu
Mawu
Uyu akukwanira pa utsogoleri
Ndipo kwambiri
Oh yes 😂😂😂😂, nthawi yakwana.
UTM moto
Osati 1995 yokha komaso amalawi ambili timakonda chilima
Ka background song kanuko kamasokoneza ma audio ambiri maguyz
Ndipo kwambiri kkk
MCP chipani cha Kupha aaa, Chakwera Criminal,usi Yudasi adagulisa Chilima aa, Chakwera wazi Wanda aa, Wanthu wopanda manyazi Ndi mzeru u fake pastor
Kodi muloza chiyani zimene mwapanga chitukuko chake chilikuti anjawala inu 😂😂😂😂😂😂
Ndalama boma lawapatsa zopangira?
Mmmmmmm inu umbuli chani utm yinalowapo m'boma kkkkkkkk uziganiza kawiri usananene
MBatata iwe choka apa ana ama 2000 sauzande inu sanagwinetu akufunika apiteso kwina akapangeso alayasi Ina zazi
@@SafariBvumbwe umbuli otengera kwa inu mmesa
Koma muli fundo umu
lozani zanu ife tiwone. 🤕
Mulungu. Ali. Ndi. Chidwi. Koma so. Akuyona
😂
Osafoka
Kodi Mr Njawala campaign yanu izikhala ya Chilima???? Pangani ndale za smart.Musiyeni Chilima apume mumntendere
You cannot fulfil the idea of someone... chilima was best but not you maguy
Munasowatu Mr Njawala.. Welcome back
Vw
Your welcome to Malawi 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 🇲🇼
Exactly mr njawala u ar true man osati uyu akumuti manganya
😂😂😂😂
Felix ndi more fire
APA NDAWONADI KUTI UTM INAKALU YAMPHAMVU.. Ndubwera konko bola osamphwekensaso..!! More fire 🔥 UTM
I'm following, Salam alaikum
Tell them ❤❤❤
More fire Njawala
Felix Njawala my man
Good speech Felix Njawala.
Madam kaliyati for President ❤❤❤
Please akulu akulu a UTM takhaliranani pansi pasakhale kugawanika mmachitidwe together we can, pasamapezeke Ena odzipatula, pakhale mtsogoleri yemwe adzibwsletsa umodzi ngati mmene SKC amachitila, SKC adali munthu odziwa zomwe akuchita komaso zokomera aliyese, kulibwino kukhalirana pansi kukambilana kusiyana mkumanenana ku ground
Munthu olalata kwambiri samakhala ndi mphavu, kupita pa ground mkumakalankhula za awo ndi awo sizithandiza chipani koma kuwauza wanthu pomwe muli ndi komwe mukupita ndi zomwe mukufuna kukachita, pewani a Utiko okhala pazenera ooneka ngati Ali nanu koma mkati mwawo Ali kwina, samalani ndi anthu omwe akulowa posatengera mbiri yawo,
Elder my brother ndi zoona zedi mwayankhula and keep it up osaopa
Thanks brother
Powerful speech. 🔥🔥🔥🔥🔥
Njawala motooooooooo!!❤
Anthu ndiomwe amuphetsa Chilima chifukwa iyeyu saamafuna MCP
Njawala keep it up mulungu ankhale nawe
Kuchotsa mboraaaahhh imene ili MCP 😂😂😂😂😂😂
Chilima is still living through his people ❤
UTM on🔥🔥🔥🔥❤❤❤
Bomaw ilooo my vote
Utm more fire
Mudalitu limodzi lero muyikana poyera ok,oh!zikomo yenkhova poti inu nokha simukhumudwitsa
Mjawala ndimakunyadilani pamodzi mayi kaliyati ndi onse a utm mulandile ulemu wanu 2025 mavoto aku utm
Dr chilima wasiya chipatso ana afundo
Zoona. 🔥🔥🔥
I love u mr njawala
Words❤
Zikomo Felex njawara kumeneko ndiye kuyankhula tikuziwa zimakuwawani nafeso zimatiwawa
Zoona zoona Mr njawala auzeniiiii
Zoona zoona
Felix kumeneko ndiye kubwela
Njawala ,,Fredo ndi Kaliati tikulimba mtima
Moto kuti 🔥🔥
Tinkakuuzani ife kuti sapita kawiri, inu munkachita makani lero ndi izi
Chimene ndinapeza ine ndichakut Chilima uja was bigger than UTM itself.
❤❤❤ UTM 🔥
😂😂😂😂 awa palibe cha nzeru anganene ndakayikanso ngati ali ndi ma followers
UTM more fire.
❤❤ one love
Akumanga chakwera
Mkango ukafa,ana ake sangaleledwe ndi fisi tanthauzo monga ife ana autm kholo lathu mmene lidafera (SKC)mcp singatisunge ndiye tosefe itimenza.
Welco😊me❤❤
Koma mwanena miyambi yamphamvu Felex chilima adakuphuzisadi eti kkkk
Gwilanani manja a UTM ine vote yanga ndzakupatsan, manganya ndi oipa ndpo waonekelatu kuipa kwake sakudzwika mbali
MCP Chipani chankhaza kwambiri don't make alliance with them again.
Awa ndi adolo
Ndipo ndizoonadi abale mulungu ativa kulila kwathu ndithu
Kuswa kuswa basi. Emusipi No chance
Mwini wake wa miyambi anapita inuyo simungaikwanitse pangani fundo zenizeni
Uku ndiye kuyankhula osaopa.chiuzeni chilungamo chipani chakupha ndi chakupha basi fisi sasintha ndi fisi basi
🎉🎉🎉🎉🎉 yomweyoooo❤
Ndiye mwabweretsa Kabambe kuti akupititseni ku DPP😢
kuthana ndi ululu wa njuchi ndikuchotsa mbola
Chipani chapa FB😂
Inde inde ichotseni mbolayo
Inu a UTM musafooke chifukwa a MCP nawoso anayamba pang,ono pang,ono sanafikile kutenga boma inutso pachedwe pasachedwe muzalowa boma
😂😂😂😂😂 koma miyambi yabwino bwanjiii?❤❤
Nane ndaifila😂😂
Izi ndi zoona
Aaaa chilima kulibe pangani fundo zanu ajawala
Last kicks of the dying horse,umaliro wachipani
Uthenga ogwira mtima 🙏🙏
Wayakhula bwino tichose chakwela
Ndiye munalephera bwanji kumusitha chakwalawo poti mwati inu mumasitha
UTM in my blood
Mfundoles Udali kuti wabodza iwe
Sindimaganiza kut UTM yatha koma mmmmm❤❤
❤❤
Mwapilila
Kkkk awa angomataya nthawi kachipani aka plus ka aford sazalamulilapo boma ai
Guys chipanichi timachikonda koma stop zomangoti chilima chilimazi Mukumatiwawisa mtima
Kuyankhula chilingamo kulifela dziko mulungu akutetezele
Kd guys manganya ndiutiyo paja😢😢😮😮
Bambo a sikono😂😂😂
Mudyelatu dzina la malemu hahaha😅
Boza munali nose atose alliance mumanga nose musathawe inu a utm palibe chanzeru apo ife tikufuna Dpp ndiyimene inakwarisa zodya katatu inu alliance mwalowesa njala mziko nd umphawi oopya bon kalindo president wa Dpp
Mmm musova inu simumaona ndeu zimachitika zija hiyaaa fundo zanu ndi ziphwasula lembani zina ndani yemwe samaona kuti anthu sakugwirizana??
Jawala moto ku buuu
Kutuluka m'boma kupanga campaign kufuna kulowaso m'boma mukuzitendetsa bwanji kodi ana amasiye inu kufuna undunu kokhakokhako kkkkk nkhope zake zimenezo anjawala mukhale nduna yamalawi aaas pitani ku dpp komko mwaiwalaso muja dpp onazizira chilimamu kathetseni kachipani kothaithako
Tiyesetse kuzolowera kulankhula zodzetsa mtendere .
Koma ichi chikulakhula mr njawala
Za ziiiiiiiii
Wa ziiiii ndiiweyo
@@TemboHaswell 🤣🤣🤣🤣🤣
Alibe fundo uyu
Mukukamba zachitukuko mwapanga zotani inu anjawala zaziiiii!!
Chakwera wakoyo wapanga chani sikungopha Chilima basi
Awa ndachitsiru
Chitsiru ndiweyo nd Chakwera okupha Chilima uja
Ana inu mwachepa MCP boma mpaka mpaka 😂😂
Mwana Wa njoka iwe zachikale zimenezo anthu ake anapita ndi Kamuzu
Pja zimathera pa media pompa zosaopsa ana kulira ndi mkodzo
Pamtumbo panu inu achitsiru mulibe mzeru mkomweso apa
Wayankhula wakuva wava mulungu aliko ayankha ma pemphelo athu
Mawu
Uyu akukwanira pa utsogoleri
Ndipo kwambiri
Oh yes 😂😂😂😂, nthawi yakwana.
UTM moto
Osati 1995 yokha komaso amalawi ambili timakonda chilima
Ka background song kanuko kamasokoneza ma audio ambiri maguyz
Ndipo kwambiri kkk
MCP chipani cha Kupha aaa, Chakwera Criminal,usi Yudasi adagulisa Chilima aa, Chakwera wazi Wanda aa, Wanthu wopanda manyazi Ndi mzeru u fake pastor
Kodi muloza chiyani zimene mwapanga chitukuko chake chilikuti anjawala inu 😂😂😂😂😂😂
Ndalama boma lawapatsa zopangira?
Mmmmmmm inu umbuli chani utm yinalowapo m'boma kkkkkkkk uziganiza kawiri usananene
MBatata iwe choka apa ana ama 2000 sauzande inu sanagwinetu akufunika apiteso kwina akapangeso alayasi Ina zazi
@@SafariBvumbwe umbuli otengera kwa inu mmesa
Koma muli fundo umu
lozani zanu ife tiwone. 🤕
Mulungu. Ali. Ndi. Chidwi. Koma so. Akuyona
😂
Osafoka
Kodi Mr Njawala campaign yanu izikhala ya Chilima???? Pangani ndale za smart.Musiyeni Chilima apume mumntendere
You cannot fulfil the idea of someone... chilima was best but not you maguy
Bomaw ilooo my vote