ZOMWE AYANKHULA ACHAKWERA DZUWA LIKUSWA MTENGO KU BLANTYRE 🙌🙌

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 13 พ.ค. 2024

ความคิดเห็น • 536

  • @stevenfrancism3638
    @stevenfrancism3638 21 วันที่ผ่านมา +7

    Amene sakufuna chakwela Ngati ine . Come here.akunamiza anthu uyu

  • @samsonmtumbati4855
    @samsonmtumbati4855 21 วันที่ผ่านมา +30

    Mr pule mukuzinamiza zoti mupitiliza chaka chamawa mukunama kwambiri pa ground sipalichoncho baba muzakhumudwa kwambiri

    • @user-px9gd6fc6w
      @user-px9gd6fc6w 21 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂😂😂

    • @charleslimbani8590
      @charleslimbani8590 21 วันที่ผ่านมา +1

      Koma na Dpp yokha zoti ingazalowensooo mmmm tikunamizanaaa

    • @user-nx7yz4qo8f
      @user-nx7yz4qo8f 21 วันที่ผ่านมา +1

      DPP boma chaka chamawa

    • @user-nx7yz4qo8f
      @user-nx7yz4qo8f 21 วันที่ผ่านมา

      DPP boma chaka chamawa

    • @user-rd2td7bg4c
      @user-rd2td7bg4c 21 วันที่ผ่านมา

      Dpp boma bas

  • @alfredbanda886
    @alfredbanda886 21 วันที่ผ่านมา +17

    Mbuziiiii Yakumwa Madzi Ometela Ndevu Galuuuuuuuuu Chikwanteleeeeee

    • @user-px9gd6fc6w
      @user-px9gd6fc6w 21 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂 really😂

  • @user-yy8pi8zl9l
    @user-yy8pi8zl9l 21 วันที่ผ่านมา +9

    Only God knows the 2025 leader... May God intervene

    • @LovelyAzaleaFlower-uc8vr
      @LovelyAzaleaFlower-uc8vr 21 วันที่ผ่านมา

      Yes God knows what will happen tomorrow....I dreamt that Peter will be president of MALAWI

  • @LovelyBlini-cu3iu
    @LovelyBlini-cu3iu 21 วันที่ผ่านมา +6

    Mlungu atimenyela nkhondo bwana ngati mkudalira kuba ziwani ichi ku mwamba kuli mlungu

  • @TrysonChimenya4-fm8nt
    @TrysonChimenya4-fm8nt 21 วันที่ผ่านมา +7

    Malawi tikapusa tipitilira kuvutikabe President wanji wosapanga regret
    Mukamakavotera MCP kawiri zanu izo, Kodi bwanji sakutiuza percentage ya zomwe atipangila out of Promises????????? Time to vote for president based on region will no longer help us ....... Ine ndiye ayi Chakwera, Chilima akagwere ndi anthu onama zedi
    Komanso what we should know this is political battle, sangabwere poyera nkumatiuza kuti eya 2025 tizaluza that's why even those small small parties are promising that they will win come 2025.
    Uku nkulira kwanga ndatha ine wanu amalawi anzanga

    • @LovelyAzaleaFlower-uc8vr
      @LovelyAzaleaFlower-uc8vr 21 วันที่ผ่านมา

      Ndipo you have said the truth anthu awawa mukut a MCP waaa God will give them a severe punishment

  • @samsonmtumbati4855
    @samsonmtumbati4855 21 วันที่ผ่านมา +15

    Boma la mcp limatinamiza kwambiri kamuzu palibe chomwe adachita mdziko la Malawi chimene tikudziwa ndikuba ndalama za Malawi makolo athu amakagona kutchire chifukwa kamuzu amafuna misonkho ndiye kuti chiyani lero

    • @berthamigodi6529
      @berthamigodi6529 21 วันที่ผ่านมา

      Ulibe manyazi komaso mwna umakomoka ma University, zipatara kkkkk Malawi tayani ndale

    • @FraserNamaona
      @FraserNamaona 20 วันที่ผ่านมา

      Zoti ma University or zipatalazo amangozinsintha mayina simukuziwa? Even Kamuzu stadium ija, bunda college kungonena zochepa anamanga ndi asamunda.

    • @DeveliousMasinja
      @DeveliousMasinja 20 วันที่ผ่านมา

      Tiziti Bingu uja adali ozungulira mutu akamati Kamuzu adapanga zinthu zambiri??

    • @wisdom20mkango49
      @wisdom20mkango49 20 วันที่ผ่านมา

      Iwe ngodwala bwanji..... don't include kamuzu mukhani yako...he is the only guy that did good for Malawians ukafunse agogo ako...osati mbuzi zako Za dpp zo😂😂😂😂😂4get guys dpp will never come back muulamuliro

    • @bernardnyirenda7639
      @bernardnyirenda7639 19 วันที่ผ่านมา

      K​@@wisdom20mkango49

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 21 วันที่ผ่านมา +8

    Chakwera ndi mbuzi yamuthu inu mwapanga chani mu 4 yrs ??? Ai lekani kunamiza amalawi

  • @ThokohKalonga-je9rx
    @ThokohKalonga-je9rx 21 วันที่ผ่านมา +10

    Kodi chifukwa chani amalawi timangopusisidwa apapa wbwera uyu ku blanttyre mukuombela manja ngati akupanga zinthu why!?

    • @user-zg7iw8kq4r
      @user-zg7iw8kq4r 20 วันที่ผ่านมา

      Vuto dzikoli mbuli zachuluka

    • @user-oo1sx7fb4v
      @user-oo1sx7fb4v 20 วันที่ผ่านมา

      Ndalama

    • @charleslimbani8590
      @charleslimbani8590 20 วันที่ผ่านมา

      Ndiye muziwe kuti zokonda za inuyo c zokonda za awooo.....ngati inuyo mumakonda Dpp musayembekeze kuti awo akondanso Dpp ayiiii .....ngati mmaombera mmanja Peter ...panopa ena akuombera mmanja chakwera.....ngati mwagona ndi njara pa khomo panu musayembekezere kuti kwa Neba nakonso agona ndi njara .....umo ndi momwe moyo umakharira ......simungawapange anthu onse kuti akonde Dpp ......koma wanzeru amakwera Timu imene ikusogora pa ground nthawi zambiri yoluza .........

  • @AliSalimu-wl3vi
    @AliSalimu-wl3vi 21 วันที่ผ่านมา +10

    Koma guys kod ku state house ku amasuta chamba eti nanga boza limeneli bwanji

    • @babranzima8120
      @babranzima8120 21 วันที่ผ่านมา +1

      Akuzinamiza amenewo

    • @LovelyAzaleaFlower-uc8vr
      @LovelyAzaleaFlower-uc8vr 21 วันที่ผ่านมา

      MCP ikuzinamiza Peter is already chosen to be president of MALAWI

    • @CliveNdalama
      @CliveNdalama 20 วันที่ผ่านมา

      😂😂😂😂

  • @user-gk3bb8dx1m
    @user-gk3bb8dx1m 21 วันที่ผ่านมา +12

    Apm my vote

    • @user-nj4ob8jw6y
      @user-nj4ob8jw6y 20 วันที่ผ่านมา

      Your president is another Bola Tinubu of Malawi, sorry he has pasted his sell by date, u can even ask Namalomba.

    • @EmmanuelChiweza
      @EmmanuelChiweza 19 วันที่ผ่านมา

      Chabwino

  • @user-vh1cq5gs5u
    @user-vh1cq5gs5u 21 วันที่ผ่านมา +3

    Koma mmene akumuyang'anira Anthu ake amene wabwera nawo kuchoka ku lilongwekowo akuwawona chifukwa akumuysuysatu zoti akhoza kuwinaso

  • @user-xv5pr3ji6w
    @user-xv5pr3ji6w 21 วันที่ผ่านมา +4

    Inu nde ayi ndithu za ziiii!!

  • @VincentChikondano
    @VincentChikondano 21 วันที่ผ่านมา +1

    Stadium sinadzadze or half nde simungadabwe?

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 21 วันที่ผ่านมา +5

    Kodi mukulota kapena kubwebweta? Nayensotu Kamuzu wanuyo ankatelo

  • @geoffreykankhomba
    @geoffreykankhomba 19 วันที่ผ่านมา

    Ovota ndi anthufe kulankhula uku its like ma vote muli nawo mnyumba mwanu ,sitinaiwale ñjala ,kukwera kwa zinthu kubvuta kwa chakudya ,kukwera kwa chimanga mpaka 60 000 zomwe sizinachitikepo mu History ya Malawi ,ziwani kuti anthu ada nanu kukhosi kuyambira ku primary school mpaka ku collage ,ma civil servants ndi Ena onse ,aphunzitsi ndi ena onse ,kufikira munthu wakumuzi sakufunanso kumva dzina la tonse alliance and MCP tionana September 2025 ndipamene mudzaziwe kuti Amalawi anatopa nanu

  • @elizamaster2168
    @elizamaster2168 21 วันที่ผ่านมา +2

    Achakwela musamathe mawu kumbukilani kt ovota ndife Malawi amene tikukumana nd mazuto muulamulilo wanuwu

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 21 วันที่ผ่านมา +3

    Apule kuyesera kubayibitsa anthu ku Kamuzu Stadium, eti anthu kumangoyang'ana osabwezera kkkkkk! Koma m'Malawi anakonza ndithu.

    • @JackMvura-ik2td
      @JackMvura-ik2td 21 วันที่ผ่านมา

      Sanje akulu ndinu afiti eti mumadya matewera kwanu eti demeti or pitala angafike gulu limeneli mbuzi

  • @louischitete1076
    @louischitete1076 20 วันที่ผ่านมา +1

    Chakwela my vote kulibe opikisana naye uyo ndi owina basi

    • @JonathanDube-vc5qp
      @JonathanDube-vc5qp 17 วันที่ผ่านมา

      I support, chakwera is going to win❤

  • @IshmealSaidi-kw6pd
    @IshmealSaidi-kw6pd 21 วันที่ผ่านมา +1

    Zaziiiiiiii president osadziwa chimene akuyankhula

  • @user-rl8xs2kf1o
    @user-rl8xs2kf1o 21 วันที่ผ่านมา +3

    Kodi Ali ku kapeni 😂 ayiwala zomwe apitira mbuzi za anthu

    • @user-cq1wv9nq4y
      @user-cq1wv9nq4y 21 วันที่ผ่านมา

      Aaaaa ine mmene ndanvera ma speech awo kumeneku nduona kuti uyu unali mnsonkhano wa ndale wa mcp not mwambo okumbukila Kamuzu asamatinamizepo apa olo aja akuti achimwendo aja kulakhula kwanji kumenekuja ati akutchula Peter Munthalika ati sangatenge boma aaaaa zugwirizana chani ndi mwambo okumbukila malemu Kamuzu??? Eeeee koma guys ku Malawi mmm ayi zikomo

  • @Malawinews1
    @Malawinews1 21 วันที่ผ่านมา +4

    Cant you memorize the script and present as you not just reading...

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 21 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi Mnyamata woganiza bhooo basi amuchita tame????

  • @ElvisSpesho
    @ElvisSpesho 20 วันที่ผ่านมา

    Makamaka chisilamAchakwera amadana nacho limodzi nd anthu akulilongwe,bas zingo khala zamutundu,tsopano msilam ndye ali paliponse,azichemwali anu onse anakwatiwapo ndi msilamu tili ndi anatu mwa kabudulamu, kuphiri la njudz,kwamasumba,ndye nkhondoyo ife tingo ona kucheedwa,kt tikuonetsen

  • @MwambakuluKamwambasa
    @MwambakuluKamwambasa 21 วันที่ผ่านมา

    Am a boy who belong to both two sides Lomwe and Chemwa because my dad from kasungu in Santhe and mom in thyolo Thomas .u like it or not .am a solution.

  • @LamseyLazarous-dl5qd
    @LamseyLazarous-dl5qd 21 วันที่ผ่านมา +6

    Anthu akeso ndiwomwewa anali zulo ku DPP

  • @user-vh1cq5gs5u
    @user-vh1cq5gs5u 21 วันที่ผ่านมา +3

    Koma ukudalira chani galu wamunthu iwe zakudya ukunenazo waziwona kuti ukuwona ngati Anthu angakwanise kugula fertilizer pa ntengo was 108,000 kwacha? mbava, mbala, chiphe munthu oyipa ngati njala

  • @user-nl5rq9to2s
    @user-nl5rq9to2s 21 วันที่ผ่านมา +3

    mwayambilatu kulila pack and go

  • @mussahkachere2332
    @mussahkachere2332 21 วันที่ผ่านมา +2

    Kom amalawi nd anthu onvesa chison kwambil 😂😂😂..anthu tikuvutika km still kuiimbila mmanja zinthu zopanda sogolo..

    • @preciousthafungaunje6631
      @preciousthafungaunje6631 21 วันที่ผ่านมา

      Osaiwala kut amalawi Fe Tu tangofuma kumudyela munthu kma awa antha

    • @Eric-gb9ms
      @Eric-gb9ms 21 วันที่ผ่านมา +1

      Eti makamaka azimayi chosecho usiku azikagona nd njala

    • @Hastings-on9is
      @Hastings-on9is 21 วันที่ผ่านมา

      Sindikuziwa kut anthufe timaganiza Chan,, mpaka kululutira garu ija koma😢

  • @AjeliMw
    @AjeliMw 21 วันที่ผ่านมา +1

    😂🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣😂😂😂😂 mawu ake ndi onvetsa chisoni kwambiri 🤣 apule 🙌🙌🙌🙌

  • @MacdonaldMushaya
    @MacdonaldMushaya 21 วันที่ผ่านมา

    Ndiye anachoseranji ma office ku Blantyre kuunjika ku Lilongwe? Waziwa liti kuti Blantyre ndi Malawinso? Wadabwa chani Lazalo, Nyanja Nyanja ua Zana?

  • @yassinmpangiwa
    @yassinmpangiwa 21 วันที่ผ่านมา +3

    Apm my vote 😂😂

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc 19 วันที่ผ่านมา +1

    God knows what comes next

  • @PatrickHennry
    @PatrickHennry 20 วันที่ผ่านมา

    Ana amahule inu mulibe ulemu kufatsa kutenga phone yako kumalembaa zotukwana zeru mulibe.
    Mau mwawava kuti sachoka ndipo siichokadi
    Yanga vote M C P

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o 21 วันที่ผ่านมา +1

    Paja peter anayamba kunzikonzera chifukwa chokalamba

    • @user-on5qq9tg1y
      @user-on5qq9tg1y 21 วันที่ผ่านมา

      Inunso ndi achisilu nso bwanji

  • @davidmalasa9912
    @davidmalasa9912 17 วันที่ผ่านมา

    Kamuzu sadamange stedium iyi ndi sir geofry cobby

  • @giftjamali8204
    @giftjamali8204 20 วันที่ผ่านมา

    Muthu ukamati nkazi uyu ndimukwatila umakhapa kuti madongosolo onse ofunikira manja wapanga Apure akukunaminzani pls konzani nyumba yanu yokapumila

  • @spargomw
    @spargomw 21 วันที่ผ่านมา

    Kwasonkhana zipani 9😂😂😂😂 Peter dzana lija aliyekha koma kunali chiguluuuuuuu❤❤❤❤❤

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 21 วันที่ผ่านมา +7

    Kufuna osafuna iwe utuluka galu

  • @user-pf5er7gc9s
    @user-pf5er7gc9s 21 วันที่ผ่านมา +1

    Ndikufuna passport yanga mkulu zonamizana apa ai. Zinazo mukumanga kumalawi komwekuno?

  • @Betty-fe9ql
    @Betty-fe9ql 21 วันที่ผ่านมา +1

    Kodi mfana oganiza booo aphulitsa liti mabomba 😂😂😂

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t 21 วันที่ผ่านมา +2

    Wojambula akupanga manyanzi akuonesa modumpha dumpha akuonesa Malo momwe muli anthu basi

  • @user-ul5hh3cz8z
    @user-ul5hh3cz8z 20 วันที่ผ่านมา

    Chakwela ndimbava amalawi akuti Zaka zitatu ndizazingono Kuti iye walemela ndi family yake pazaka zitatu.koma iñu amalawi masauka taganizani mozama amalawi zongoopela Manji tingozipasa mavuto tonkha

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc 19 วันที่ผ่านมา +1

    God can not do that much TO M.C.P again

  • @KondwaniJ.Nkhoma-wt5zo
    @KondwaniJ.Nkhoma-wt5zo 20 วันที่ผ่านมา

    Awaso koma akodzera bulangete sanayanike. Ayiwala kuti usiku ukubweraso

  • @ChimwemweHenry-uw1bq
    @ChimwemweHenry-uw1bq 20 วันที่ผ่านมา

    Komatu peter amayakhula osaonera palipose kumayakhuka zomveka.sono inu bwanj kukikose kumachita kuwerenga.amakupepelesanitu omwe amakulemberaniwo kaya simumaziwa

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 21 วันที่ผ่านมา +1

    Mr President mukulankhula zakumapwa........ mwamva

  • @honourablemcgregorysc97tv
    @honourablemcgregorysc97tv 21 วันที่ผ่านมา +1

    😂😂😂pakamwa chilichonse ndi chotheka

  • @ElizabethMajiga
    @ElizabethMajiga 21 วันที่ผ่านมา +1

    Mulungu amamva mapemphelo ana akee

  • @user-nk5mj5ws8v
    @user-nk5mj5ws8v 20 วันที่ผ่านมา

    achakwela mudziyangula momalidza udindowo mwiniwake a kubwela bola yiweyo walawa nawo koma adzanu achilima eeee wauponda

  • @user-xi2jz8ru1w
    @user-xi2jz8ru1w 21 วันที่ผ่านมา +1

    Komasotu big wa samata kusanga or wa kazi awowatu kungo kala ngati nyapapitu

  • @user-jw5rx9ze8k
    @user-jw5rx9ze8k 20 วันที่ผ่านมา

    Chakwera akudziwa kuti sadzawina , koma angodzilimbitsa mtima hiya.

  • @HafizahHarack-bn3bf
    @HafizahHarack-bn3bf 19 วันที่ผ่านมา

    Amalawi zanga asazakunamizeni kamuzu sanapange China chilinchonse kumalawi zonse zimene akunene chakwela zaboza anamanga ndi atsamunda... Kamuzu amangodziwa kutsitha zithu maina zithu zoti sanamange iyeyo.

  • @patrickscott9086
    @patrickscott9086 20 วันที่ผ่านมา

    Ndizona tizivutikabe bas muziba ndalama muzilemba job aku banja lanu

  • @user-pe2tu1ip3v
    @user-pe2tu1ip3v 21 วันที่ผ่านมา +1

    Peter wa muthalika 2025 boma ❤

  • @scoobymatola8314
    @scoobymatola8314 21 วันที่ผ่านมา

    Gadama
    Matenje
    Chiwanga
    Sangala
    Just to mention a few.
    Sir Joffrey Cody planned Malawi
    😭😭😭
    The list is endless😭😭😭

  • @chigokhalid9420
    @chigokhalid9420 20 วันที่ผ่านมา +1

    He wasn't a malawian

  • @user-jw5rx9ze8k
    @user-jw5rx9ze8k 20 วันที่ผ่านมา

    Koma chakwera mwati ali ndi nzeru? Ndikuona ngati chomwe akuyankhula sakuchidziwa.

  • @JamesMussa-do6lc
    @JamesMussa-do6lc 21 วันที่ผ่านมา +3

    Abusa a Chakwera mukuzinamiza simungawine, nthawi yatha mumanga masukulu nthawi yanji..zikoli mwaliononga

  • @MphatsoMannet-uf5nm
    @MphatsoMannet-uf5nm 21 วันที่ผ่านมา

    apm.my vote baba palibe ncanzelu ndikunva.mwainu.sakho.hvy

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo 20 วันที่ผ่านมา

    Ukunama ase ng'ooo udye ndalamazo komaliza wopusa iwe

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936 21 วันที่ผ่านมา

    Mr Pule mwapanga chani choyanjanisa kuposa Kuba ndi katangale nzikomu njala thoo muzikomu

  • @user-ve6yk4cj1e
    @user-ve6yk4cj1e 21 วันที่ผ่านมา +2

    Apm he is the kind 👑

  • @AndersonInnocent
    @AndersonInnocent 21 วันที่ผ่านมา

    Anthu amenewa adyesedwa chani kusekelele Chakwela mbuzi yamunthu anthu akuzunzika zinthu zakwela chakudya kulibe uchokapo pamenepo aise

  • @user-xv3gi9ev9x
    @user-xv3gi9ev9x 20 วันที่ผ่านมา

    Nyali unayasa zowunika ukamaba anthu wokumba mopanda manyazi chisiluyiwe

  • @MadalitsoKondwan
    @MadalitsoKondwan 20 วันที่ผ่านมา

    Awa akuzanimiza asiyeni aledzera mwina ku status house kuli ambuye mtengeni mowa obalalitsa uja

  • @mailosyasin3110
    @mailosyasin3110 21 วันที่ผ่านมา

    Wina aliyense amakondedwa ndi Mulungu. Ndiye osamanyoza mtsogoleri wathu. Ngati inu si a malawi samukani koma ine sindikuona chomwe walakwa pa zomwe wayankhulazi. Tisiye kusankhana mitundu ndipo uthenga uwu wa achakwela ndiowona ndinso omanga dziko.

  • @BHAPPIEKotala
    @BHAPPIEKotala 21 วันที่ผ่านมา

    Ine sindipanga nawo za ndale koma kunena zoona chakwela udindo alinawo nde wa church osakhala dziko. Ndipo akapitilila kukakamila mulungu akwiila dziko lamalawi chifuwa cha utsogoleli wanu. Inuyo mulibe chisomo cha utsogoleli wa ndale

  • @PeterThawi-jc7zl
    @PeterThawi-jc7zl 9 วันที่ผ่านมา

    ,😂😂😂😂ambuye atiyendele...awawa nde ahyi...mmmmhhh

  • @ChrispinJohnson-py5ie
    @ChrispinJohnson-py5ie 21 วันที่ผ่านมา

    kape chilichonse choyankhula kulemba basi kupanda nzeru galuu

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu 21 วันที่ผ่านมา

    Amakulembera ndani Kodi zomwe ukuyankhulazo chidzete iwe? Nose mbuzi

  • @DavidKalumo
    @DavidKalumo 20 วันที่ผ่านมา

    Nonse otsutsa tikuti nonse yiwalani mwamva kodi ?

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 21 วันที่ผ่านมา +1

    Time is over enough is enough mbamva izi

  • @ChifundoChingwalu
    @ChifundoChingwalu 20 วันที่ผ่านมา

    Ngati tili ovota ndiiyeyo
    Sadzadzitha

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m 21 วันที่ผ่านมา +1

    Kuyankhula momveka koma kusamala amalawi mukulephela inu a tonse alliance

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 20 วันที่ผ่านมา

    Iweyo Chakwera ukuona Ngati Dziko la Malawi Ndi lako,kamuzu,chinali chimunthu choipa ngati Iweyo nkhope Ngati mvuwu pa Bumbu pa azibale Ako panopa Malawi aliyense wakalipa msili kariyo una bereka ñdiwe?gondwa mphawi mbava okuba ndalama za amalawi ULI Ndi nyàli iwee basop

  • @HanishaissahKagansa
    @HanishaissahKagansa 21 วันที่ผ่านมา +2

    Nothing you can say about election i will see kungowina iweyo uyembekezele nkhondo chifukwa sitizalola za manyi zakho mwaiweyo mulibe utsogoleri uzaona after all

    • @user-gz3mi5bl1f
      @user-gz3mi5bl1f 21 วันที่ผ่านมา

      Ukunama

    • @HanishaissahKagansa
      @HanishaissahKagansa 21 วันที่ผ่านมา

      @@user-gz3mi5bl1f let,s see after election because is not so far

    • @wisdom20mkango49
      @wisdom20mkango49 20 วันที่ผ่านมา

      Nkhondo😂😂😂😂😂😂 akulodza eti....umaidziwa nkhondo iwe

    • @HanishaissahKagansa
      @HanishaissahKagansa 20 วันที่ผ่านมา

      @@wisdom20mkango49 let's see

  • @MustafaLikaomba
    @MustafaLikaomba 21 วันที่ผ่านมา

    Ndiye iye wapanga chan ,zongoone likasa

  • @AmaChidzinga
    @AmaChidzinga 21 วันที่ผ่านมา

    ❤❤❤. My vote m.c.p ennanu mwazolowerakudya zopempha

    • @JosephyNdeule
      @JosephyNdeule 20 วันที่ผ่านมา

      Dziko likamayenda bwino anthu amasangalala koma izizi ndiye ai mbuzi

  • @user-ce6hy6tp7e
    @user-ce6hy6tp7e 21 วันที่ผ่านมา

    Chakwera iweyo ukalamulira 2025 nyumba ya nkazako ndi ana ako pamtumbo pamako wamva

  • @EmanuelPaul-io2hk
    @EmanuelPaul-io2hk 6 วันที่ผ่านมา

    Ine zandale simbali yanga,chakwera samaopa Mlengi mwachidule mkulu wasanaki.

  • @ibrahmdoka7486
    @ibrahmdoka7486 19 วันที่ผ่านมา

    Azivotera yekha ndi nduna zakezo ...olo atabera zizitheka....

  • @user-jr7bq8sw6t
    @user-jr7bq8sw6t 20 วันที่ผ่านมา

    Ndipo ine utu sindimamva mfundo zzomwe amayankhula Koma mukuti olo ulaliki wake unali omveka bwino bwino?

  • @thandiseweza
    @thandiseweza 21 วันที่ผ่านมา

    zitsiru ndi zomwe zimanama zatelemu chakwera ndi. garu bass
    😂😢😢

  • @user-cp8rz3qs8l
    @user-cp8rz3qs8l 21 วันที่ผ่านมา +2

    Tangoziwona nduna zakozo kukwiyako akuziwa kuti kwatha basi next year kusowa wakumuzi basi

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 20 วันที่ผ่านมา

    Zaziiiii Chakwera ndi chitsiru kwambiri

  • @user-nl5rq9to2s
    @user-nl5rq9to2s 21 วันที่ผ่านมา +1

    ukupita wayambakulila galu ukupita u like or not u are going time is up

  • @user-ul5hh3cz8z
    @user-ul5hh3cz8z 20 วันที่ผ่านมา

    Çhakwela is good on preaching he thinking that Malawians are in church

  • @GreshamDaniel-hu5ht
    @GreshamDaniel-hu5ht 21 วันที่ผ่านมา

    Galuyii achoka bas afune asafune

  • @usumanidaudi
    @usumanidaudi 21 วันที่ผ่านมา

    This man is mede

  • @khumalonyirenda4437
    @khumalonyirenda4437 20 วันที่ผ่านมา

    Chakwera boma ,salute

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo 20 วันที่ผ่านมา

    Mulungu atithandize munthu uyu woipa mtima

  • @andrewbanda99
    @andrewbanda99 21 วันที่ผ่านมา

    Ukunama ndiweyo ife sitikupeleka mpata opeleka boma. Timalize zabwino zomwe tinayambazi

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u 21 วันที่ผ่านมา

    Mbuzi galu ngati iwe munthu umagwila ku chipiku ndiye ungakwanitse kukhala president panyo pako ukagwele

  • @Hastings-on9is
    @Hastings-on9is 21 วันที่ผ่านมา

    God will work it out next year,,,, we are tired with you Mr,, kungotiphaka phara pano....

  • @GloryRudraksh
    @GloryRudraksh 15 วันที่ผ่านมา

    Aliyetse angozifutsa kuti kwanthu kuno ndi chitukuko chiti chomwe alupanga ameneyu

  • @thomluciouss7360
    @thomluciouss7360 20 วันที่ผ่านมา

    Chenjezo kwa Malawi azanga gwileni mtima vote ndi chaka chamawa, uku mwapita uku mwapita punsi anagwa chagwada

  • @BaldwinBanda-gd9zo
    @BaldwinBanda-gd9zo 15 วันที่ผ่านมา

    Chakwera ndiwe mbuzi yamano pasi

  • @jemasmasimbi8109
    @jemasmasimbi8109 21 วันที่ผ่านมา

    kodi afiti kumalawi kuno tilibee,, akanangolozako nyaniyu iyaa😜

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b 20 วันที่ผ่านมา

    Chimwendo pemphero lakolo mulungu waanthu sangayankhe ndiponso upresidernt wa chakwera chaka chamawa ukutha mukulamulira kunyini kwamanu