Population ku north inali bwanjii Who called dead North Infrastructure inalibwanjii Why many people martyred? All these development you are saying North could have been better than central and southern Even Chilembwe did before kamuzu 60yrs of independence gravel road,are you serious? How much have you pocketed?
Kamuzu Banda anali bwino chifukwa,kunali Admark ku Malawi kunali maphunzilo apamwamba kunali chithandidzo mwana akakeelela ku university amatengapo mbali ya school fees,,,zonsedzi pa ma president tsopano awa anapangapo chiyani?????
Aliyense president amakhala ndi ubwino ndi kuipa,,,bakili muluzi anapha oyimba wathu wapamwamba kwambili,, Mr evison matafale,,,,abingo anapha mwana wa school,,,a Robert chasowa analakwa chiyani?????? A Peter Mutharika anaononga Malawi kwambili,,potisithila school yathu ya bwino chifukwa cha nsanje yake ya muntima chimuthu choyipa kwambili ndi brother wake anapanga kota sisitimu kuti aphe maphunzilo kumpoto ndikanva zina loti DPP ndimanyasidwa kwambili.
Kasi mba Rev Mr Tembo, ku Manyamula.
Kamuzu was good. Although everyone has got side effects. Manyamula is my hometown. I like your
Chilima Adakavomeleza Kuluza Last Election Sadakafa Koma Adapanga Ubale Ndichipani Chakupha Chimene Chachotsa Moyo Wake.
Umboni wake kaperekeni kubanja kwawo
Akuziwa ndi Mulungu mwinaso akadafabe imfa yina
Bakili muluzi tv yokuzunguzan mutu
Munagulitsa dziko ndi munthu wakugana Inu .bwanji anachotsa sabject ya chitumbuka? Kamuzu wanuyo
😂😂😂 kamuzu machende ake nanu atumbuka ndinu vindele
Mapwalla ake
Population ku north inali bwanjii
Who called dead North
Infrastructure inalibwanjii
Why many people martyred?
All these development you are saying North could have been better than central and southern
Even Chilembwe did before kamuzu
60yrs of independence gravel road,are you serious?
How much have you pocketed?
Mbutsa iwe machende ako wamvaa
Kamuzu Banda anali bwino chifukwa,kunali Admark ku Malawi kunali maphunzilo apamwamba kunali chithandidzo mwana akakeelela ku university amatengapo mbali ya school fees,,,zonsedzi pa ma president tsopano awa anapangapo chiyani?????
Aliyense president amakhala ndi ubwino ndi kuipa,,,bakili muluzi anapha oyimba wathu wapamwamba kwambili,, Mr evison matafale,,,,abingo anapha mwana wa school,,,a Robert chasowa analakwa chiyani?????? A Peter Mutharika anaononga Malawi kwambili,,potisithila school yathu ya bwino chifukwa cha nsanje yake ya muntima chimuthu choyipa kwambili ndi brother wake anapanga kota sisitimu kuti aphe maphunzilo kumpoto ndikanva zina loti DPP ndimanyasidwa kwambili.
Kathyali
Kwambiri