THE HOT CURRENT - 24 NOVEMBER 2019
ฝัง
- เผยแพร่เมื่อ 21 ส.ค. 2024
- Land in Malawi is not for Malawians - this is in reference to revelations of public land that has been sold, including Livimbo Primary School in Lilongwe, to Malawians of Indian origin; Brian Banda and George Kasakula discuss this and other issues in this edition of Hot Current.
It is unbelievable kuti brian banda anatisiya # times, timutengera ku zodiak koma achite mwambo oyendtsa zisankho. Zabwino zonse Mr banda happy New year
Brian tachezakoni ndinzimayi uja akutokota zakunyumba yaufumu yathu
Komatu Times please ma camera anu need to be professionally trained, nthawi imene munthu akuyankhula akuoneka ndi omvetsera, please train them properly.
Brian banda amùchtsa ntchito akuti amaba. Banja lake litha kutha chifukwa avutika kudyetsa banja lake. Chachikulu ndimoyo malangizo anga kutelo, ntchito ndimuntengo
Ndzikolidi likulamulidwa ndiasata koma mulungu sakulola kuti satana apitilile kulamulila ndzikoli nchifukwa pano zobisika zonse zikumaululika
Alex Fest1 Always Ndakunyadilan potitumizila Koma mochedwa aTimes mwatani kodi
Guys osalimbana ndi President cos ndakhalako pa mipando yosiyasiyana ndikudziwa momwe umakhalira busy Munthu
Mmmmmm mipando yonsele wakhalayo unathandizapo amalawi motani iwenso unangokhalila kuba nchifukwa wakhala mipando yonseyo
Ku Kenya akanakhala atapeza kale onse omwe asewera game imeneyi, atawathamangitsa kale m'ma office pano
A times poyambilila sinkakuvesesani kama chaka na chinochi mwandisegula mutu pitilizani kutitumizila ndiponso nkhani zanu musamatiyiwalile
Always say "mwatichapa mmaso
Koma ndizoona amalawi ndife otsalira kwambiri. Koma gwero lake ndi atsogoleri athu.
Cubaphidy yemweyoo
Koma malawi aliyese angoba koma why malawian
Koma zikupanga boma ili ndi zoipa ife kuno kumulanje tikusowa malo koma agalu amwenye fucken Muslims are taking our land shame on dpp
Waganiza bwanji kunyoza asilamu,,,mmalo mokamba za amwenye okhawo? Why my dear