If we cannot stand up and fight for our lives as Malawians, no one is going to fight for us Wake up Malawi. There's no time to fear these idiots. It's time to take our rightful place. Let's unit and fight
Anthu mudana ndi limpopo kumalawi kuno kupanda anthu amenewawa ndindani angalimbe kumayankhula zimenezi its good kuti akuyankhula ali kunja otherwise bwezi pano tikuti afa so zikamalakwika limpopo ikuyenela kuyankhula basi
Ngati Pali anthu opepera ndiye ndife a Malawi mantha too much timakhala always ku ma stand kumaonenelera zinthu zikuonongeka as if we are not here in malawi pambuyo pake tiziyakhurapo very shamefull.
Vuto ndi azisogoleli osusa angoti pheee ngati kuti akumetedwa osalankhula china chilichonse chozuzula mchitidwe olakwika umene akupanga ng'azi ya mcp, koma akuti akufuna kuzavoteledwa 2025 for wat!?, shame on you opposition leaders
Ino mukuti anthu amangidwawo achita bwino panyapano pa amayi ano mashende anu chakwera apha chilima anagwilizana ndi manganya komanso azinduna nose ndino opanda maliseshe panyapano
Zifwamba 30 kulimbana ndi munthu m'modzi walakwa chani ? ndi udindo wathu aamalawi kulira pamaso pa mulungu kumphavu zake agwese upresidernt wa nkhadzawu amen
The main problem is we have weak opposition parties in Malawi and that’s why we will keep exploited like this…. I wish Peter could leave the sit of the presidency for the young and brave person to lead the party, he is the only hope left but very old and he can’t act in these issues but a word would change these an acceptable arrest😎
Amutanyiwa ndi kufunakuti mundi fusireko kwa chakwera kuti Kodi iyeyo chakwera ananena kuti ariyese ayenera kurira mumene angarire amafunakuti seka mumaso? Ine ndi mutumbuka
Iwe wa mcp amene ukuika ma comments opusa usamare iwe chisilu eti bon kalindo amarakwa chani iwe wasateniki mukufuna athu azifa timawako beeeee nyani iwe
Chimene ineyo ndikuona apapa bola kungophwanyanapo ndi MCP chifukwa bomali ndi lathu. komanso zikuoneka MDF yathu ndi yautsilu chifukwa sikuiimilira a Malawi 🇲🇼 koma ikuiimilira a MCP. ndiponso bolaani Valantino Phiri achoke pampando wa ukomanda.
The best Radio station in southern Africa
Apolisi ofoila, asilikali ofoila basi kumangomanga anthu mopanda dongosolo lenileni,chakwera wapha osatiso boza
Keep it up Limpopo ndipo tikudalira inu ndi KALINDO mumatiyimilira kwambiri osafooka ndipo Kalindo mulungu amuyanganile kufikila atuluke ku police
If we cannot stand up and fight for our lives as Malawians, no one is going to fight for us
Wake up Malawi. There's no time to fear these idiots. It's time to take our rightful place.
Let's unit and fight
Mituyanu sigwira ntchito nonse amene mukuikira KUMBUYO mcp poti simunakumane nazo mcp enanu SIMUKUDZIWA ana obadwa ma 2000
Zoonadi achipani atengepo mbali amunthandize bon kalindo atuluke basi chifukwa ndimunthu modzi otinthandiza tonse zikomo 24:38
Anthu mudana ndi limpopo kumalawi kuno kupanda anthu amenewawa ndindani angalimbe kumayankhula zimenezi its good kuti akuyankhula ali kunja otherwise bwezi pano tikuti afa so zikamalakwika limpopo ikuyenela kuyankhula basi
Wandiwechetela bwino
Mulungu wakumwamba onetsani ukulu wanu a Malawi akufuna thandizo lanu kuzela kwa atsogoleli omwe inuyo mudawatsankha. Ndifendani ife popanda inu Mulungu wa moyo. Zikomo chifukwa chokumva mawu athu.
Amen
Bola adzamumpe chonde chifukwatu chipani cha kongelesi ndichakimpa nde chonde ambuye kumwqmbako muwoneni boni kalindo pamosi kalepo kaluwa chonde state🙏🙏🙏🙏🙏
Chakwera adzafa imfa yophweteka kwambiri chifukwa mizimu yambiri mudziko lino ikumudandaula kwambiri ndipo Mulungu mwini Zonse achite nawo bambo Chakwera ndi Nduna zake.
Komadi nawo azipani zosusawa akuyenwra kumachitapo kanthu
Ukunena Zoonadi osusawa awonjeza kungoti zii
Eti inu kungoti ndwii zoona mmm
Bon Kalindo amtulutse, ngati boma lawalephela ndi zawo zimezo. Anthu akuvutika kunja uku, iwo akumanga anthu za ziiiii.
Plz let's do something on winikos arrested, we don't have to be silence on this issue
Kodzani mademo tiwone ngat akugona
MCP yafika pa manyi chakwela akupanga zapa nkholo kobas zamanyitu chakwelaiwe manyiako😊
Ngati Pali anthu opepera ndiye ndife a Malawi mantha too much timakhala always ku ma stand kumaonenelera zinthu zikuonongeka as if we are not here in malawi pambuyo pake tiziyakhurapo very shamefull.
DPP sikufuna kulowerera kulephera kwa Tonse Alliance kuti asazaname patsogolo kuti a opposition amawasokoneza. Munali patsogolo kuti DPP ichoke ndiye tiye nazoni ndi nyasi zanuzi. Lero Mulungu wakuikani pambalambanda.
Koma achakwela azachoka boma tizabweza zomanga athu osalakwa OK mulungu alinafe ndithu
Iweyo mene ulilimo ungakwanise kumanga president
Chakwela you mast go watikwana
Vuto ndi azisogoleli osusa angoti pheee ngati kuti akumetedwa osalankhula china chilichonse chozuzula mchitidwe olakwika umene akupanga ng'azi ya mcp, koma akuti akufuna kuzavoteledwa 2025 for wat!?, shame on you opposition leaders
Muzibwelabwela ntanyiwa timadandaula mukapanda kubwela timavela zambili❤❤❤❤❤❤❤
😢😂
I wish I was at my country as Malawian I could have die there too for bon
Kma a Malawi tinagulitsa mtendere wathu ku MCP tilibe ufulu
Mr born kalindo ndi freedom fighter just leave him alone please please release him b4 you put in trouble u a self chakwera
Mr Ntanyiwa munditumileko uthenga Kwa zikhale ng'oma Kuti sarary yamwezi Uno akaguleko malaya
Zipani zosusa boma zaku Malawi ndizopusa kwambiri,zogona
We are malawi , but lets joing together with opposition partie
Mubwelenso amwene mutiwuze amene akufuna kuthawayo , tikamugagade asanathawe
Kkkkkkkk
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂km ku Malawi nkokoma
Lazarus you are aWIZARD
Brz mwayakhula bwino ndithu koma nkhani yayikulu ndiyakuti osutsa boma akugona kwambili
Apatu izi ndizofuna mmachita mademo thawi ya DPP ndiye lelo mukuti dpp yangoti pheee mmayesa mmachosa nonkha
Zoona zake asatana ari umu akubakira amcp zaoizo ife ndife adpp inu tiyeni mademo koma kumzuzu tikhase presidet wanthu osati chakwera uyo ayi nisataniki
Ino mukuti anthu amangidwawo achita bwino panyapano pa amayi ano mashende anu chakwera apha chilima anagwilizana ndi manganya komanso azinduna nose ndino opanda maliseshe panyapano
akuziwalila kt ndizosiyilana ndipo atsala ndi miyezi yochepa
Osawopa Malawi ndi wa tonse
A Chilimaaaaaaaaaaaa😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Atimalizatu chakwera chipani chamwazi ichi
Olo amange bon kalindo bola ife tikuziwabe kuti wapha saulos chilima ndi chakwela from kasiya 😂😂😂
Vuto utm anatiphera chilima manganya ndi chakwera ose ndi a mcp manganya wasangalara anangodekha maliro achilima kmso bon kalindo atulusidwa chilungamo chimapweteka
Ai ndithu zikomo Mcp tikanatiso tizilota kut zizachitikaso izi kachiken sitikanalozedwaso kuvotera manyakawa
Bwanji Sanasankhe. Dausi ..Nsonda ..kapena..uladi Musa Koma chakwera Ali ndi chipongwe
I think apapa akufuna iye ali ku Police mavoti adutse
Boni Kalindo wamangidwa Koma zipani zotsutsa Ali Phee! Osapangako kanthu
Zomvesa chisoni kwambiri mmm
Watching from Nsanje ndikutha kuona ma views akukwera mu ma minutes 😊 ocepa
Ndizofuna izi munkayesa zachibwana munapanga mgwilizano wawumbuli koma muli ophunzira lero mukunong,oneza bondotu
Ndipo ndizoona
Wayankhula bwino nyamatayo akuti osusa Boma akugona aiwala muma 2019 kumapita uko anzawo ankapanga mademo koma zinaliko bwino nthawiyo than Pano..Pano Malawi waipa koma azipani agona tulo..adzakuberani mavoti.
Zifwamba 30 kulimbana ndi munthu m'modzi walakwa chani ? ndi udindo wathu aamalawi kulira pamaso pa mulungu kumphavu zake agwese upresidernt wa nkhadzawu amen
Tiyeni tisatope tidziwaikidza ma pemphero Mulungu wathu amamva ndipo atimvera sakhala chete Mulungu wathu
Mmene alongolera Manganya lero wangokhala chete ndipo ndikaonetsetsa plan yompha Chilima imachoka pakamwa pa Manganya sanayenera kuvora kukhala Vice ngati anali ndi chikondi ndi nzake Saulosi Chilima Manganya ndi mfiti too
Olimba mtima anali only chihana palibeso
Ukuchitikawu ndi uchitsiru kwabasi Chakwera ukundinyasa kwabasi
My vote is for Peter mutharika
Koma boma la achakwera mmmm akudziwa ndi mulungu
Mulungu not mulungu
Asatana ali mu ma comments section umu 😂😂😂. Ati kubakila MCP
Sure :DPP+Afford +UDF :::Fire Works
UTM alowe konko
Amalawi mumati munthu akamalankhula mumamuchemelela koma akamangudwa ndiye kumuukilanso ,mutha muona,coz enafetu tili kunja muzivuyika NDINU ngati simukugwilizana,,inafe sangatipeze agalu amenewo siyili maiko okhala amalawi ambiri like south Africa,no koma dziwani mukapanda kugwilana manja mutha ,,matha akuphetsani amalawi
Iwe ndiopusa kwambiri nkana ukulankhula mopusa chonchi
Nzoona ndithu
Kodi nanga United Nation ili kuti? Chifukwa zikuoneka ngati sakunva zimene zikuchitika ku Malawi 🇲🇼. Kodi nanga African Union ili kuti? chimene chikufunika Mr Murder Chakwela achotsedwe basi. Komanso ma MP aku Malawi 🇲🇼 ndi ogona ndipo odontha. Chifukwa ma MP ndiamene angakwanitse kumuchotsa Mr Murder Chakwela mwachangu kupyolera ku parliament
Sangabwele Kuno chifukwa anthu Ake amangoyakhula zopanda mutu
😅😅bon kalindo niamene ali olimba mtima ndithu osati awa
AKULU AKULU A MCP MUSAYIWALE KUTI KULI MULUNGU, PALIBE DOLO OPOTSA MULUNGU. MISOZI YA AMALAWI ILI NDI TANTHAWUZO PAMASO PA MULUNGU NAMALENGA.
A opposition akumalawi agona ndithu kukhalangati adyetsedwa chibanzi chonsecho akufuna kuti amalawi azawavotere mu 2025. Mxm
Inu mkut Peter abwelere muboma koma anthu akumwera mmmm, Kaya zanu izooo
The main problem is we have weak opposition parties in Malawi and that’s why we will keep exploited like this….
I wish Peter could leave the sit of the presidency for the young and brave person to lead the party, he is the only hope left but very old and he can’t act in these issues but a word would change these an acceptable arrest😎
Amutanyiwa ndi kufunakuti mundi fusireko kwa chakwera kuti Kodi iyeyo chakwera ananena kuti ariyese ayenera kurira mumene angarire amafunakuti seka mumaso? Ine ndi mutumbuka
Ulemu wanu a ntanyiwa mumatiyimilila ndithu
Ife kupanda kubvela inu timadandaula kwabasi
Chisankho cha amalawi...paja amafuna change ....change ija ndi imeneyi
Nthanyiwa umakwana bwana
Kunena chilungamo mukamayakhula zowa puta dala afiti amenewa mukuziwa kt azanuwo sakufuna kusokonezedwa pazomwe akucita .
A born kalindo ndamene anali othandizira kusokoneza dziko lino panoso cilango chake chimeneci ali mphuleso okha samene akat zithu zisithe
Anthane nazo aliphule yekhaso . Peter ananyozedwa ndpo ngat wayamba kukula nd peter sibwino ndpo osusa asalowerere anthane nazo
Ndipo sakunama izi zikuchitika izi same like Zimbabwe di tikuziona
Chakwera ndi Bagamoyo
CHAKWERA NDIWOKUPHA
Bwanji kodi osango muphaso nayeso chakwelayo
Why we keep quiet let's stand together and rescue our country please.
boma la zigawenga zokha zokha ili zitsiru asatana
Iweyo bwela udzatitsogolelet ifetu tikuopatu 😂😂😂😂😂😂😂😂
Ambuye Malawi wanga akupita kut? Ambuye tithandizen poti ife timadalila inu patokha sitingathe ndinu Mulungu wachilungamo
Amalawife ndiwogonadi timangolilira mmimbadi
Atule udindo Achakwela kunena mosanyengela ndipo asadikile mpaka 2025 please musaone ngati mupeza mtendele ayi
What you must know " MCP" we are in exile out the country tsiku likubwera muzamuwone mmalawi weniweni wait and see as I said your days are numbered
Limpopo🎉🎉🎉
Zomvesa chisoni kwambiri mmm
Komad a opposition chitanidi kanthu please
Kkkkkkk siuziwa olo pang'ono kupatula kuba
Zonse tikuona bwino ndinthu
Inuyo amranyiwa komanso wa bakili muluzi tv mukungolalata koma munabisala kuopa mcp nde mukut anthu asaope
Iweyo ndiye ndimbuz yamunthu mukifunanso muaphe anachendeinu mboli zaamanu
Ife timadalila munthu yemweyo bon kalindo
Ulemu wanu broo pitilizani kuuza ife amalawi chilungamo, osaopaaa chakwera watikwana kwambiri ana ang'ona awa misokho yathu yakoma
Tatumizani ma message amene ben longwe adatumizawo musamangonamiza anthu inu pazifukwa zanu
MCP 🤔🤔🤔
Malawi😢😢😢😢😢😢
Iwe wa mcp amene ukuika ma comments opusa usamare iwe chisilu eti bon kalindo amarakwa chani iwe wasateniki mukufuna athu azifa timawako beeeee nyani iwe
Km inuyo tapangan zot mademo achitike mosachadwamu ineso ndiphedwele ngat chilima
Tangopitani nokha palibe atapange mademo mwagwanayo
Ndigaireni nambala ya Limpopo fm
thanks me too I want it
Km guys Boma limeneli mmmmm
Amen
Asafetu Born Kalindo sitithanako ku malawi kuno ohooo
Chimene ineyo ndikuona apapa bola kungophwanyanapo ndi MCP chifukwa bomali ndi lathu. komanso zikuoneka MDF yathu ndi yautsilu chifukwa sikuiimilira a Malawi 🇲🇼 koma ikuiimilira a MCP. ndiponso bolaani Valantino Phiri achoke pampando wa ukomanda.
Koma chomwe ndikufuna kudziwa ndi choti kodi momwe zikukhaliramu azisogoleri osusa boma monga ku DPP UDF AFORD AMBEWE simungatengepo gawo pofuna kuthana ndi n'chitidwe ukuchitikawu chifukwa kunena zoona zikuoneseratu kuti 2025 olo chakwera atati asapange campaign atengaso boma potengera ndimomwe wayalira maudindo ku MEC waikako okha okha a M C P mukuganidza kuti inu osusa muzaphulapo ?
naneso ndikudabwa nawo.....Koma onsewa komaso amabungwee kuli ziiiii why dzikoli?????¿😭😭😭😭😭😭
Akuopa chakwala ndioopsa kwambili 😢😢
Kodi mukuti anthu avotere pita muthalika wasintha liti pakutu inu nomwe mukuti MCP sinasinthe pá zaka 30 zomwe yakhala kunja kwa boma.tsono Dpp yakhala kunja kwa boma zaka 4 yasinthila kuti liti????? Sankhani anthu oti sanalamuleko boma .Tamachenjerani a Malawi please.mukutsata zomwe zidachitika ku Brazil?? Pano Lula sakumufunaso koma ankamubwerezetsa .........musapuse a Malawi DPP sinasinthe ndipo zinthu zomwe zidakwera sizidzatsitsidwa mitengo chifukwa chosintha boma
Zoona ndithu simukunama do koma a Malawi kupusa chabe amafunika munthu wina oti sanalamuleko osati pitala
Galu wachifwamba iwe wa mcp mboliyako
Ulowapo iweyo namachendeiwe
Commander wathu Ndi mbudzi yeniyeni😂😂😂😂
Ndiye kuti kumwamba kulibe malo athu, tiyeni tipephere molimba kuti tigonjetse nyasizi