ZADABWISA ANTHU AMBIRI ZOMWE CHAKWERA WAYANKHULA PONYANUKA KU AIRPORT ULENDO WAKE OPITA KU USA LERO

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 17 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 173

  • @davidlinerevelation3427
    @davidlinerevelation3427 วันที่ผ่านมา +15

    Peter mutharika said
    We have a president but we don't have a leader

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 13 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ndipo kwambiri

  • @masterkachingwe7448
    @masterkachingwe7448 วันที่ผ่านมา +9

    Holiday after Holiday let's be honest this guy it's living his Best dream life, selling the layman hope 😢

  • @CameronVisser-k7i
    @CameronVisser-k7i วันที่ผ่านมา +13

    Asilikali pofunika uyu akupitaku asakabwelertso, azapedze miyala pa airport ndi jinga za ka banza

  • @kingsleymacheza6733
    @kingsleymacheza6733 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

    Mr. President Chakwera was elected by Malawians to fix the problems left by the previous DPP government. Instead of addressing these issues, he has been busy traveling from one country to another, using our foreign reserves. He claims these trips are for our benefit, yet we see no results. The country is facing serious challenges, and now he wants Malawians to support him despite his failures. It’s a shame that some continue to support wrongdoing, but we will not starve in silence.
    As the president travels, Malawians are suffering. Prices of basic goods are too high, and life is becoming harder every day. We were promised a better life, but things are only getting worse. People are struggling to find food, pay for school, and access healthcare. It feels like the government is ignoring the problems we face. We need a leader who listens to the people and works to fix these challenges instead of focusing on personal benefits.

  • @GiftMwachande
    @GiftMwachande วันที่ผ่านมา +13

    How will i forget SKC? His soul continue rest in peace,

    • @chifundobuledi
      @chifundobuledi วันที่ผ่านมา +3

      Forever in our hears

  • @Jamilahchinyama-y9b
    @Jamilahchinyama-y9b วันที่ผ่านมา +5

    People are dying with hunger the man of country just go there and there god is not sleeping never

  • @JosephFulayi
    @JosephFulayi วันที่ผ่านมา +8

    Ine ndi wa mcp koma palibe chazeru chomwe chikupanga president wathu

    • @peterthawi
      @peterthawi วันที่ผ่านมา +2

      iwe nde munthu.

    • @ChisomoChigaga
      @ChisomoChigaga วันที่ผ่านมา +1

      Bola iwe unaganiza bwino m'bale wanga

    • @DeenesNurudMeke
      @DeenesNurudMeke 13 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Kkkk muzamuvotelebe bas osamutaya kkkk

  • @WezzieChisi-e1g
    @WezzieChisi-e1g วันที่ผ่านมา +2

    Zaziiiii anthu akuvutika ndi njala muzipatala mulibe mankhwala anthu akufa kusowa chithandizo Basi maulendo uku ndi uku ziko osasintha muvaso wagwesa kwacha eeee tilipamavuto ineso basi ndipite konko ku 🇬🇧 💃🏻💃🏻

  • @BerthaMlalama
    @BerthaMlalama วันที่ผ่านมา +8

    Akuchita kufanana ndine wosaphunzira zochitika zake kumangoyendayenda ngati mbuzi yosamagirira pa chingwe mmmm usakabwerenso kumalawi kuno🙆‍♂️🙆‍♂️

    • @WisikiBlack-gj4gu
      @WisikiBlack-gj4gu 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ambuye mupheleni mundege momwemo ameneyo

  • @BarwickSalanje
    @BarwickSalanje วันที่ผ่านมา +3

    What kind of President is this....and he still do promiseles

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 วันที่ผ่านมา +4

    Ndalama zimene akuyendelazo sanga paste anthu tikufa ndi njala,😢

  • @lifnetmakoka2175
    @lifnetmakoka2175 วันที่ผ่านมา +2

    very an unfortunate !!!!!! God give us wisdom Malawi is at Stake

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya วันที่ผ่านมา +3

    Inuyo kuyendako mukungoyenera kutero, cz mpando wa upule munawufunatu abusa,😢 ndiye paja mbuzi imadya pomwe yamangiliridwa, Nanu dyerantuni zanu, inuyo simunabwere kuzatumikira a Malawi ayi,, koma family yanu isangalalale 😢😢😢😢😢

  • @JohnfosterNkusengwa
    @JohnfosterNkusengwa วันที่ผ่านมา +1

    I born in freedom country where there was leaders not president like this nyapape God will deal with this fool president

  • @billymhoni9527
    @billymhoni9527 วันที่ผ่านมา +2

    Malawi Is A Failed State.....under Chakwera......

  • @GiftMwachande
    @GiftMwachande วันที่ผ่านมา +5

    JB akubwelatu komweko be careful

    • @UthandekireSibande
      @UthandekireSibande 19 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ndithu abwere nsanga
      Ngati akuwelenga comment iyi adziwe kuti ife tikumufuna

  • @JamesALLi-m8i
    @JamesALLi-m8i วันที่ผ่านมา +1

    Guys koma chikangawa atha akuononga ndalama zanthu kwambiri dzabwera ndi kanthu uyu mr president your time is over seriously 😑 will don't need you again go back to chipiku business

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 21 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Chakwera zopanga zako ndizochimwisa kwambiri, ndipo ukhoza kumuyankhulitsa munthu udyo, Chilima uja anali akatundu koma iweyo chakwera panja penipeni.

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm วันที่ผ่านมา +8

    Kd Zina sangamatume anthu ena km chimunthu ichi kukonda kuyenda akatero agwetsa kwacha kapolo uyu tikhara bwanji otukuka akungoyenda yenda komaso kuba ndalama za Malawi chakwera walanga Malawi ndpo waika ziko lathu pamavuto

    • @JosephKamoto-k5j
      @JosephKamoto-k5j วันที่ผ่านมา

      Chadabwisa anthu mu speech ya achakwelayi ndi chani ?

    • @anicakandiado
      @anicakandiado วันที่ผ่านมา

      Ndipo sindikuchiona chodabwitsacho koma ndangoipidwa ndi ulendo opanda phindi kwa a Malawife​@@JosephKamoto-k5j

  • @alicechinyama4155
    @alicechinyama4155 20 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Vote yanga I voted for chakwera but I regret because of the pain he has brought to me

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 วันที่ผ่านมา +3

    Awa atitha ndiithu 😢😢😢😢

  • @ChristopherKawilam
    @ChristopherKawilam วันที่ผ่านมา +1

    Chakwela mmmm ayi ndithu muthuyuakuyenda tisaname ndipo Malawi ali m'mavuto akulu ndipo akadali m'mavuto

  • @WitnessPhiri-y5d
    @WitnessPhiri-y5d 18 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Palibe chingamveke chifukwa anthu akufa ndinjala iyeyo palibe chichitika iye nde phindu ndichan iyeyo akunjoya ndi azibale ale pamene anthu akudya chitedze

  • @MphatsoIshmaeladam
    @MphatsoIshmaeladam วันที่ผ่านมา +1

    Msonkhano wa nambala 80 adziwe kut azapitako ena this is is nonsense kulipo ndikuononga misonkho yathu ndegeyo isakabwelele kuno ife tatopa

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 21 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Apatu chakwela akuchita bwino chifukwa ife amalawi ndi anthu wosayamika munamuchosa peter kuti sakupanga bwino ndiye apa mulungu akukuphunzisa china chake kuti amalawi tinapanga mistake

    • @SamboRuphan
      @SamboRuphan 17 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ngati boza 😂😂😂😂 Peter amalakwa chani

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nchifukwa chani atola nkhani a MBC okha ndiamene amafunsa Chakwera? A Malawi tilibedi mtsogoleri koma President tilinaye. Kuyrndayenda! Mavuto ali phwi!

  • @user-wr3wh8yu2b
    @user-wr3wh8yu2b วันที่ผ่านมา +1

    Pobwela kumeneku sindidabwa kwacha ikagwaso

  • @KestonNGUBO
    @KestonNGUBO วันที่ผ่านมา +1

    Mutukul pakhom umalandila ndiwe t maviako kukuyu mbolo yako pam na chakwera

  • @ElisaNyirongo
    @ElisaNyirongo วันที่ผ่านมา

    Mtukula pakhomoyo kwaenafe kwathu sanafike, kusonyeza Kuti Malawi ndi wawo

  • @billymhoni9527
    @billymhoni9527 วันที่ผ่านมา

    Mtolankhani moti angofunsa koma akuesera kufotokozera zomwe a president akukachita ....what kind of reporters are there at MBC........

  • @felixtembo9602
    @felixtembo9602 วันที่ผ่านมา

    I don't like this guy anymore,God help us please!

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 วันที่ผ่านมา

    AState of emergency under chichewa board leader

  • @JeanfatsanJere
    @JeanfatsanJere วันที่ผ่านมา

    Amathandiza iweyo Ife Siti kuwona phindu eeeee tili pamavuto😢😢😢

  • @AmissKumakanga
    @AmissKumakanga วันที่ผ่านมา

    Machendeako boy uribechison ndidziko rako nde mayiyo arikukamwa nyindu umuze nyero wake ayendebwino😢😢😢😢😢😢

  • @peterthawi
    @peterthawi วันที่ผ่านมา

    ine ndiwa MCP...KOMA at least akanamutuma MAnganya to represent him.chanzeru palibe apa😂😂😂😂

  • @lightwellsilumbu
    @lightwellsilumbu 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Munthuyu zimafunika aitanidwe afusidwe basi. Anthufe tikuvutika iyeyu akkuononga ndalama zathu.

  • @ReginaMulipa
    @ReginaMulipa วันที่ผ่านมา

    Kod koma kumalawiko anayamba wabwerako president waziko Lina kucheza kwanji koyenda Muthu mozi iye samafuna kuyenderedwa kod galu opanda zeru uyu kumangoyendayenda hule lalimuna

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma วันที่ผ่านมา

    Ine ndilibe nthawi yomvetsela zomuyamikila chakwera he is a hartless president mfiti satana uyu anthu akuvutika koma he doesn't care anthu akudya chitedze ku machinga or kukawayendela chitsilu cha president oipa mtima kuposa satana koma Mulungu mwini chilichonse akuonatu one day ayankha kulira kwa ana ake asazione kupambani

  • @GiftNgwira-e8l
    @GiftNgwira-e8l วันที่ผ่านมา

    Rubbish president forever

  • @FelixSomba
    @FelixSomba วันที่ผ่านมา

    Ntchitozo ndi zabwino,kulakwako mkupha ,anthu,
    Ndikumene,kumanyasa Amalawi

  • @Kamwachale
    @Kamwachale 17 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Maulendowa mukuti NDI aphindu, manga nchifukwa ninji chuma chathu sichikupindulila nzika za Malawi Koma nzika za mu MCP zokhazokha. God will at any cost punish us selectivity because of lies on the expense of the poor

  • @EdwardZuze-r7w
    @EdwardZuze-r7w วันที่ผ่านมา

    ndalama zomwe akuonongazo , sangawagulire chakudya amalawi omwe akuvutika ndi zoona,
    Mulungu akuchitile chifundo

  • @EvanceRazaki
    @EvanceRazaki 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Umayakhula fundo zakho ndthu km kt ukwanise.chabe ndthu watikwan ndthu.ndye muwon Peter muthalika sanalonjeze chithu osachitka mayaz ndchifukwat sanayambe sapasidwa zin lodabwisa

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 14 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma Monica naye mwati ndi munthu wanzeru ???Chingovomera zilizonse

  • @user-xc2zm9bu1i
    @user-xc2zm9bu1i 20 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ndege imachagidwa per hour
    How much kukafika ku USA
    Ma allowance
    Bwanjii osangopanga zoom meeting
    Zafuwa basiiii

  • @IbulaMayikolo
    @IbulaMayikolo วันที่ผ่านมา

    Pamenepo akamabwela azitiuza kutimizlngoyatu yagwa chiliga choti abwezele ndalama zomwe walnogazo😂😂😂😂😂

  • @masingatichilumba8263
    @masingatichilumba8263 วันที่ผ่านมา

    Bola mimba za family yake zikukhuta iye vuto alibe, munthu opanda chisoni ndi myoyo ya anthu ena😢

  • @HanifiYaumu
    @HanifiYaumu 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    President ofoira

  • @ChizzaNkhonjera
    @ChizzaNkhonjera วันที่ผ่านมา

    2030 iwetu uzakhara ulipanjatu suzapitiliza kulamlira mtukura pakhomo unapasa ndani

  • @Dee01papa
    @Dee01papa 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    The most stupid headline I've ever seen 😅😢

  • @SteveMasuli
    @SteveMasuli วันที่ผ่านมา

    Can you manage. Sorry brother we are dying because of you

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl วันที่ผ่านมา +1

    Eish komatu kuyenda

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chakwera patumbo pako iwe munthu ochitisa manyazi kwambiri nyasi yamunthu iti

  • @amonechirwa
    @amonechirwa วันที่ผ่านมา

    Chakwara kuyenda Ngati Traspotar Koma chikangawa noses

  • @BenjaminMtima
    @BenjaminMtima วันที่ผ่านมา

    Inunsotu muzibweretsa ma topic a phindu pa page lanuli tizitha bundle nzopusazi?

  • @RaheemNgoma-pk1ev
    @RaheemNgoma-pk1ev วันที่ผ่านมา

    Mr Moyenda eish tizamva ndiumphawi bas

  • @YohaniKachali
    @YohaniKachali วันที่ผ่านมา

    Palibe chanzeru chomwe akuchita chakwera😢

  • @PaulOSBjaulen
    @PaulOSBjaulen 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Akat a Malawi akhala akuvuti panopa tasiya kuvutikako chuma akungononga ameneyi

  • @AnockyDavidd
    @AnockyDavidd 17 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kodi mai chikangawa chidzungu amatha? Why i am asking? Sindinamvepo atalankhula or comment even m'nsonkhano wa chichewa.

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Guys kodi ife amalawi tinatani😂kodi kufansa kwayife kunatani asilikali akumalawi ndi mbunzi ndipo patumbo pawo akuti asilikali apolice ndimanyi eni eni

  • @AgathaJerard
    @AgathaJerard วันที่ผ่านมา

    Nfiti yayikulu mwafiti onse ndameneyu khopezo Ngati akhwezule

  • @mosesnjobvu716
    @mosesnjobvu716 วันที่ผ่านมา

    Economy Ili patio pamenepa mwezi uliwose kuyenda koma zovuta

  • @OwamThoko
    @OwamThoko วันที่ผ่านมา

    Ulendo umenewu ndi wa number 268 chiloweleni m,boma zaka 5 zisanathe eeish that's wy he want to sell island yanthu😢😢😢😢

  • @kondwanimunthali7401
    @kondwanimunthali7401 18 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A very unfortunate nation

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 17 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Paja amkagwira kuchipiku anazolowela kutulusa mushop.ndiye angalephele kudyela ziko

  • @chilingachilinga6059
    @chilingachilinga6059 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Whatever kaya zomwe akupitiliza zopindulira ife km tatopa nazo coz he always asks help kmno what have we done with those helps kmno chomwe unagwetsela kwacha

  • @TecksonKaima-dr6er
    @TecksonKaima-dr6er วันที่ผ่านมา

    Ine kungoti chakwera ndi mbuli kwa mbuli zonse bibulo makate

  • @billymhoni9527
    @billymhoni9527 วันที่ผ่านมา

    Tisiya Bwanji Kumuda .....ameneyo Unga yopita iyeyo yomaliza ndi imeneyoyo

    • @user-ol1hf7ru1v
      @user-ol1hf7ru1v 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Etieti akulemba Mutu waziiii chisamudera nchiyani pamenepo

  • @Legendlandlord-w7y
    @Legendlandlord-w7y วันที่ผ่านมา

    Aaaaa iwe zitithandiza chn wayamba kuyenda 4 years yonsei chilipo chasitha 😅😅😅

  • @HassanMussah-i9j
    @HassanMussah-i9j วันที่ผ่านมา

    Eishee kom chitsilud ndichimene anthu amachilemekeza eishee phindu lake bs ndikutaya misonkho yanthu awa Allah adziku endela mwapadela dela iwe

  • @EstherchavulankhomaNkhoma
    @EstherchavulankhomaNkhoma 21 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ukadakhala iweyo ukadatani kuzolowera kutukwana bas palibepo kumalawi kuno mtsogoleri bas sadzapezeka olo okomera OSE olo utakhala iweyo udzakhumugwitsaso athu

  • @Janaphiri
    @Janaphiri 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Boma lamasomphenya samatuma wina😂 ngakhale wina amufunire imfa akhalabe ndimoyo kaya otukwana sasintha akhalabe chakwera, kodi m'buyomo atsogoleri samapita kunja? Simunamuvotere zisakuwaweni,
    Mwinamudziwe kuti phunzo mumatukwana lija ndi promotion yake 2030 wooooo

  • @blessingssaiti
    @blessingssaiti วันที่ผ่านมา

    Ayende timutisiye sangave sinapalibe anga pange action chaka Chatha kale uyu adzachoke chifukwa chamavoti koma apa sizingatheke inu anthu akufa ndi njala Pano AIP sikudziwika kuti ithekha kapena ai sakusamala zawathu timusiye chaka Chatha kale tithana nae

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 15 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ayi tikonze pamenepa mai chakwera si mayi wa fuko lamalawi siwona ndi mai wa fuko la a nthu aku Lilongwe kukasiya komweko ine ayi,mai wa mtundu wanji osapita kukayamwitsa ana ake ku machinga komwe njala yafika powoosya

  • @JuniorSamalia
    @JuniorSamalia 21 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kodi maiwa a Monica sangakhaleko panyumba ulendo ulionse ali komko eee ai ziliko

  • @JosephFatsani
    @JosephFatsani 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ndie chodabwitsa chomwe chayankhilulidwacho ndichani???

  • @EstherBair
    @EstherBair วันที่ผ่านมา

    Kod kulibe Muthu Wina Kuti Atha kumutuma kod

  • @MiracleDamiano
    @MiracleDamiano 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma Bambo ameneyi nzeru alibe ndpo nd manyaka enieni🚮🚮🚮

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Boma ndi lomweli chikangawa pile, kwacha ikugwa ndipo mafuta akwela oye ali kuunga phew judy's misonkho yathu

  • @PearsonZachariah
    @PearsonZachariah 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chakwera ndi munthu wovetsa chisoni

  • @IssahAluba
    @IssahAluba วันที่ผ่านมา

    Zaziiii iyaaaaa

  • @PetrusTlhokwane
    @PetrusTlhokwane วันที่ผ่านมา

    Chingogwa kumwamba nachoso mesa chinatigwesela wathu chikanagwa kumeneko Ambuye talolani uyo ndioyipa kuyenda yenda mmmm

  • @JoannaNAMA
    @JoannaNAMA วันที่ผ่านมา

    Koma Munthu uyu mmmm chokamba chagwera mkati watikwana kwambiri

  • @lightwellsilumbu
    @lightwellsilumbu 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    moti amipingo mabungwe anthu tonsefe kulephera kumufusa munthuyu?.

  • @ChisomDevison
    @ChisomDevison วันที่ผ่านมา

    Oyendetsa umugwetsele ku chikagawa

  • @VajraBanda
    @VajraBanda วันที่ผ่านมา +1

    🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @EliasMoya-i5s
    @EliasMoya-i5s วันที่ผ่านมา

    mpakA misonkhano 79 😮

  • @Yoxym
    @Yoxym วันที่ผ่านมา

    Boma ndilomweli 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂🎉🎉🎉😂😂😂😂😂😂😂

  • @NaomieBanda-t6g
    @NaomieBanda-t6g วันที่ผ่านมา

    Simuchotsa black box

  • @KareemYahaya-ey6tf
    @KareemYahaya-ey6tf วันที่ผ่านมา

    Munthu akuchuta kufanana ndi falawo

  • @EdwinKachepa
    @EdwinKachepa วันที่ผ่านมา

    Onena analipo, koma kusamva kwathu

  • @mphatsomonjeza4371
    @mphatsomonjeza4371 วันที่ผ่านมา

    Koma amaiwa anayamba apangako zachitukuko kapena kutsegula timabungwe ngati mai wafuko? Kapena nawo 😂ndi atinkenawo oti alibe focus ina iliyonse ? Chifukwa sindinamveko chomwe amapanga amaiwa koposera kumango londola kulikonse ngati chikwama chapule

  • @ChisomDevison
    @ChisomDevison วันที่ผ่านมา

    Moses ndw galu uzion zoyakhula ulimbe manyaz kd

  • @IjilanMwalija
    @IjilanMwalija 20 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Bola ndengeyo ingosowa mmalele mommo

  • @BarwickSalanje
    @BarwickSalanje วันที่ผ่านมา

    Apa ndie mukuona kuti zinthu zilibwino or pali kutukuka apa....or mukungosamala zamimba yanu basi

  • @azunguauskay4903
    @azunguauskay4903 23 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Galu wa president

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu 22 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chitukuko chanji galu iwe mfiti , umangolakhula ngati uli ndi nzeru koma uli muthu ofoila, iwe yako ndiyakhupha basi yomwe taona ife , amalawi inetu uyu ndiphaa akundinyasa kwambili

  • @FulasesiJaseteni
    @FulasesiJaseteni วันที่ผ่านมา

    😢koma uyu yekha nde 0 pa 10

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy วันที่ผ่านมา

    Bola usaduse ku chikangawa otherwise

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r วันที่ผ่านมา

    Mbuzi yamuthu kukonda kunyenda mbava hiiii