Wangodetsedwa mmaso ndi DPP. Usaiwalenso kwakumbutsa anthu za ma Albino aja, anthu 20 aja anaphedwa ndi chipani cha DPP, CHASOWA ku Poly, Njaunju ngozi zimenezo musamayiwalenso kwa kumbutsa a Malawi sachedwa ku iwala
Very well spoken, but don't forget the background of this party, one party system, they don't realize or acknowledge othere parties, they are greedy and rotten
Ndiye inu a DPP mukuzi chita contradict nokha inu siamene mwachititsa UDF isithe kuitana MCP. IWE UKUYANKHULAWE NDI GOTANI MBULI ndindani? Mutaima pamodzi ndi Chimwendo Banda kumuza mwana lozani mbuli pamenepa mukuganiza mwanayo bangalore Chimwendo?
Nonsense
Powerful message 🙌 ulemu wanu big brother 💪 just be strong 💪 mr man 👨 don't be less be strong 💪 🙏 ❤️ 💙 🙌 👍 💪
Ndinu mwamuna waaa triple O
Osaopa,Osatopa,Osafoooka (SKC)
True and Wise words ❤❤❤
Wangodetsedwa mmaso ndi DPP. Usaiwalenso kwakumbutsa anthu za ma Albino aja, anthu 20 aja anaphedwa ndi chipani cha DPP, CHASOWA ku Poly, Njaunju ngozi zimenezo musamayiwalenso kwa kumbutsa a Malawi sachedwa ku iwala
Zoona brother
Nice god protect you,nice words👏👏
Bigy bigy more fire paja kacilungamo kamawawa ngati kapilipiri 😂😂😂😂
Very nice and powerful speech ❤❤❤❤
Exactly this is reality my brother osaopa osafooka osatopa
Opposition iyiyi ikuva kuwawa heavy ndipo sanati akungoyamba
Very well spoken, but don't forget the background of this party, one party system, they don't realize or acknowledge othere parties, they are greedy and rotten
Nice message comrade u too God bless more❤❤❤
Chimwendo ndi galu
Uchitsiru uli ndi a MCP ndiamene akulakwa
Bola ukudziwa mungawidwa basi
Hamas paulendo
Bwana mukuyankhula chilungamo keep it up ❤❤❤❤
❤❤❤ amalawi timakukondani amalawi onse
Ulemu wanu mwayamhura bwino auzeni
Zitsilu za MCP agalu achabe chabe
Manyi awoo onsewo
A bwana mukunena chilungamo
Powerful
Kkkkkkkk munyela 2025 MCP Boma
Auzeni ave zitsiru za mcpzi
Good ng'alurisation
Malawi first ikugwila ntchito yomwee tinayisakhilaaaa
Thank you massage ya mphamvu imenei itaponyedwaso pa FB kuti uthengau upite patali
Eeee😅😅😅😅❤❤❤
❤❤mmmm ndipo zoooona zenizeni
Kkkkkk bone kalindo zaziiii
Zoonadi Brother
Yankhulani big
Ulemu wanu Mr onyozao osadandaula zikhale ngo,oma amagwatu khunyu paja
Kkkkkk
Ngamo
Bad chimwendo
Tilankhuleni
UDF think deep before you do any move failing which it will be your downfall for good
Ndipo ngati kuli mburi ya nduna zikhare ng'oma. Olo speech yake simagwira mtima umburi okha okha.
19:22
God bless you chimwemwe mphepo muzituluka tuluka timakusowa ❤❤❤
Palibe chamzeru chimene akupanga a Richard achimwendo ndi mbuli
Atupele Muluzi akufuna awononga legacy yawo ...Sakudziwa kuti MCP akufuna kwawonongera mbiri...DR TUPELE work up please my brother 🙏 😭
UDF chipani changa will never join MCP yakuphayi😂😂😂
Eish,,l don't understand what z happening
UDF kungoyitana anthu amenewo chipanicho akataye manzi ayiwale zoti azalamulaso malawi chibwana chake chimenecho chipani chipani chimenecho
UDF ziko likukulilirani mukapita ku MCP mukuputa nkwiyo wa anthu osauka ufumu wanu uzalandidwa pakati panu 😭
If you are wise hear what comrade say to you MCP
They don't understand the word democracy
Atupele ngati akuvomeleza zimenezo basi chipani chathera popo
Koma apa mkunene zoona, sabata yathayi, mzuzu ndi Ekwendeni chimozi mozi
Mcp tsogolo ilibe kupanda chilima zitsilu sizikanawina
You are too intelligent for Malawian politicians
Bravo my brother your freedom fighter ya Amalawi
Iyiyi ndiye ngamo💓💓💓ngini iyiyi a opposition atakhala nayo serious akhoza kuzagwesela nayo MCP
Good msgs
Chimwendo banda mutu ngati nkhumba
Fantastic. It's so creare
Well said 💪💪💪🔥
UDF tikulowera kuti??😭😭
Good message ❤Mr
Kunena zoona Atupele Muluzi ndi chitsilu cha munthu kwabasi
Mmmmm kulankhula kumabweza wakhala chitsilu bwanji mudzudzuleni mwachikondi odziwa ndi mulungu basi
🤣🤣🤣komatu kom kutokota🙌🙌
Ulemu wan ❤❤❤❤❤❤
UDF dichipani chopepera
Chimwendo ndi galu kwabasi
❤❤
Azipita ndithu
Well said Mr Mphepo 👏👏
Nonsense
Ndiwanzeru munthuyu onest wanzeru akuziwa izi kuyankhula mopanda nsanje ❤❤❤❤❤❤
Akuluwa ndi anzeru
Nzeru zilipati Nanu inu cadet angayankhule bwanji
Imeneyo ndiye democracy aliyense ali ndi ufulu wopita kumene akufuna kuti akamvere sakakamiza SAVAGE ndi iweyo anthu sachita kuwamanga dzingwe
Nice message