Anamiwa musamamize anthu. Ose omwe amasankhindwa mipando mukunenayo eg speaker amakhala andale komaso Richard Msowoya adakhalapo speaker panthawi yomweyo Ali first speaker wa nyumba ya malamulo ndipo sadatule pasi
Pepani a CDEDI akuchita ngati kulankhula mwamwano koma am following every time you are online. Awawa apaneni MACHENDE mpakana aphulike Amongst all these concerned ministers bear 10 culpable homicide each. Chakwera sakupusisidwa ndi wina aliyense pa report yandenge, iyeyo mwini ndi mastermind hence he can't take any action to any suspected Minister. Two!!! Chakwera akuwopa kuti akangochotsa wina wake, atha kukhala pachiwopsezo chopangidwa EXPOSE Awawa chonde mwatonse tiyeni tiapane Ndathokoza a NAMIWA.
Every government is having a strong independent organization that opposes the motion of the ruling government during DPP it was HRDC directed by T. Mtambo more power to these comrades
Mr namiwa you are comrade namiwa Allah azikuyang'anirani thawi zonse
Khaniiyi muibweretsa bwino kobasi tikyyamikileni. Mlungu akudalitse I. Koma tipephenao sizoti mulandile thumba lokutsekani pakamwa pakamwa. Yendetsani chilungamo
Ndipo musasinde maganiso mr namiwa maso patsogolo bas mulungu ali nanu limodzi patsogolo panu osawopa
Iyi sithawi yocheza amalawi tikufuna ufulu, izi tizimange chilili chipanda apo ibuke ibuke, sitikufuna chinyengo achakwera zinthu mnalephera kare siife koma inu nokha,
Mukapeleka masiku akatha simukuchitapo kanthu .kulankhula kokha ndinu akatakwe .koma kuchita
Alonda ,amuchikangawa ,akutipo chani pankhaniyi,kodi mesa munkhalango ,muja muli alonda?
Msatitenge ngat siife amalawi, tipanga ziwoneselo konse konse sitikufuna zausilu tonse ndife amalawi,
Ndipo talimba ntima china chake chichitike basi tionesana pa imfa yii, ndife okwiya ngat simukuziwa
Namiwa umakwan ndpo osadzalandra ndalam zamagaz Mulungu adzakukantha bravo Namiwa always u hit the nail proud of u auncle
Ndipo palibe chopyatira anthuwo ali limoz wonse atule pansi udindo wonse
Nthawi ya DPP kunali human rights vuto ali mbali yasatana mzao paja asatan amayenda asatana okha okha ndye Namiwa wabwera kudzaika poyera chilungam
Koma ma feedback akumabwera? 14 days ija sinathebe kodi?
HRDC yasowa chifukwa analandira ndalama
I remember in RSA period like this in parliament they put the president in front n question him direct
Ngati tinachotsa Dr, Banda Pali chani tisiya bwanji kulankhula sitikuziwa chinachitika iwo Ngati akuopyeza which means akuziwapo katho
Namiwa tapanga changu 14 days yachuluka 5days imakwanila
Atiuze chilungamo za imfa ya beyeni
Ndichifukwa chake otsutsa sapeza mpata
Please boss pitilizani kupanga zinthu zofunikazi
Anamiwa musamamize anthu. Ose omwe amasankhindwa mipando mukunenayo eg speaker amakhala andale komaso Richard Msowoya adakhalapo speaker panthawi yomweyo Ali first speaker wa nyumba ya malamulo ndipo sadatule pasi
Koma sakhala olamula
Cdedi inuyo munabwera kuzatimirira❤
This man hmm very important person ❤
Namiwa 💪💪💪🙏🙏💯💯 ndiwe dolo Activist
Akwanati masiku 14
Nkhani ya bwino iyi😊
Ine kuno ndikuona kuchedwa ndi demo
Zoonadi Mumatiimilira
Anatilakwira koma
Cidet woyeeeee
Mumakwana big...
CDEDI more fire 🔥 be strong guys 👦 chikangawa wachepa uyu we trust you guys more fire 🔥 again chakwera azaimenso next year pls 🙏
❤❤❤❤❤
Pepani a CDEDI akuchita ngati kulankhula mwamwano koma am following every time you are online. Awawa apaneni MACHENDE mpakana aphulike
Amongst all these concerned ministers bear 10 culpable homicide each.
Chakwera sakupusisidwa ndi wina aliyense pa report yandenge, iyeyo mwini ndi mastermind hence he can't take any action to any suspected Minister. Two!!! Chakwera akuwopa kuti akangochotsa wina wake, atha kukhala pachiwopsezo chopangidwa EXPOSE
Awawa chonde mwatonse tiyeni tiapane
Ndathokoza a NAMIWA.
Komatu mulungubwangoti phee kuonelera..ifika nthawi zobisika zibwera poyela..viva Namiwa..mudafooke😊
I salute you comrade. this is not apartheid time
Every government is having a strong independent organization that opposes the motion of the ruling government during DPP it was HRDC directed by T. Mtambo more power to these comrades
Achakwera ngakhale pang'ono osaganiza kukaonapo pamene panagwela v p nkhondotu iyi akuyiyambayi
Komaso mcp kungowauza thawi kapena kuwauza siku lomwe munganene inuyo basi comrade auzeni basi
Mmakwana chief,big up"
Malawi akufunika anthu ngati inuyo Comrade mulungu akupatseni moyo wautali
Atiyankhedi anthu amenewa atikwana kwambili
Namiwa is good Comrade same same Comrade Mtanyiwa ❤❤❤❤❤❤
Mumakwanila big
Mumakwana guys
Proud of you mr namiwa
Achoke watikwana
Chakwera achoka basi
kwaolaaa
Bwanji nthawi ya DPP sided kunalibe koma kungobwera chakwera bas cided ya bwana nanga cholinga chawo ndi chian?
Kudzudzula zolakwika are you against this organization? Are you also chikangawa?
Iwe ndiwe mbuli..ife imfa ya Chilima ikutisowesa mtendere
Useless person
This is the best time for CDEDI. Kunali HRRC lero ndi la CDEDI
Iwe sukudziwa ndiwe mbuli paja
Were together namiwa
This Man called namiwa he's a really comrade
Mumatha guys