ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
ameneyo azingodikila kubweza chuma chathu bass balibeso kucoteledwa. akumama
Azibusa adyera awa,, angofuna kukhutisa mimba zawo not kufunila a Malawi zabwino,,,
Mwikho 😂😂😂😂 aaaa chakwera
Nkhoma Synod am one of the member CCAP dont pray for Chakwera God will punish you
Musiyeni Mulungu akhale Mulungu musatchule Mulungu pa chabe
Or tipephelele inu mwatulukakale mu boma pepani kwambili
mumuwuze. asatilakwise kuti atimange tikusamala ana ife amalawi. pamene zafikapa Loko kungova Zina lachakwela mimba mukumapweteka chakwela wationesa zokuda sitizamuiwala
Dyela basi zinthu mene zakwelelamo 50kg ya cement Mk35, 000.00, Nima Soap Mk800. 00 Bread Mk3, 500. 00Chakwela alephela
Ndiye dpp ingabwele ndi company
Mwikho
Ine kamanganya ka sindimafuna kukamva mau ake Kamandibowa kwabasi palbe chanzeru chomwe wachita kakumangoba chabe misonkho ya amalawi pamoz ndi chikangawa😮😮😮 kuchikamwa
Azibusa adyera, malo molankhula chilungamo mavuto omwe aMalawi akukumana nawo, koma muli busy kuombera mfiti manja. Mulungu sanyozeka musamale ndithu
Kkkkkk atapembere ndani kod iyeyi mesa amati ndibhusa aphembere yekha
Sanakuuze iwee
Azitsogoleri adyera amafunako ndalama
Why only nkhoma synod
Azibusawo si mulungu chimene mulungu wamanga palibe angamasule angakhale abusawo dyela basi
Ife tikuzavotera chakwera ndipo tilipo ambirikusowa kwa mafuta tinakuuziwa 2012 nthawi ya Bingu
Zawugalu basi achakwela
Palibe chomwe angachite chanzeru .Malangizo sanayambe lero koma samalangizika Miyezi 3 angasithe chachani from 5year kkkkkkkkkkkkkkkk tikakumana kovotako basi kkkkkk
Azibusa awa ndi zitsiru amakasusuka paja azibusa a c c a p kususuka
Umphawi sizinthu , mmene zinthu zili azibusa mumakataniko ku state house ?
Anyapapi adyera😂
Mcp Akumayenda ndi zikwanje a mpingo azipempherera zimenezo
Koma umphawi,ndi usilu,sizabwino
ameneyo azingodikila kubweza chuma chathu bass balibeso kucoteledwa. akumama
Azibusa adyera awa,, angofuna kukhutisa mimba zawo not kufunila a Malawi zabwino,,,
Mwikho 😂😂😂😂 aaaa chakwera
Nkhoma Synod am one of the member CCAP dont pray for Chakwera God will punish you
Musiyeni Mulungu akhale Mulungu musatchule Mulungu pa chabe
Or tipephelele inu mwatulukakale mu boma pepani kwambili
mumuwuze. asatilakwise kuti atimange tikusamala ana ife amalawi. pamene zafikapa Loko kungova Zina lachakwela mimba mukumapweteka chakwela wationesa zokuda sitizamuiwala
Dyela basi zinthu mene zakwelelamo 50kg ya cement Mk35, 000.00, Nima Soap Mk800. 00 Bread Mk3, 500. 00
Chakwela alephela
Ndiye dpp ingabwele ndi company
Mwikho
Ine kamanganya ka sindimafuna kukamva mau ake Kamandibowa kwabasi palbe chanzeru chomwe wachita kakumangoba chabe misonkho ya amalawi pamoz ndi chikangawa😮😮😮 kuchikamwa
Azibusa adyera, malo molankhula chilungamo mavuto omwe aMalawi akukumana nawo, koma muli busy kuombera mfiti manja. Mulungu sanyozeka musamale ndithu
Kkkkkk atapembere ndani kod iyeyi mesa amati ndibhusa aphembere yekha
Sanakuuze iwee
Azitsogoleri adyera amafunako ndalama
Why only nkhoma synod
Azibusawo si mulungu chimene mulungu wamanga palibe angamasule angakhale abusawo dyela basi
Ife tikuzavotera chakwera ndipo tilipo ambiri
kusowa kwa mafuta tinakuuziwa 2012 nthawi ya Bingu
Zawugalu basi achakwela
Palibe chomwe angachite chanzeru .
Malangizo sanayambe lero koma samalangizika
Miyezi 3 angasithe chachani from 5year kkkkkkkkkkkkkkkk tikakumana kovotako basi kkkkkk
Azibusa awa ndi zitsiru amakasusuka paja azibusa a c c a p kususuka
Umphawi sizinthu , mmene zinthu zili azibusa mumakataniko ku state house ?
Anyapapi adyera😂
Mcp Akumayenda ndi zikwanje a mpingo azipempherera zimenezo
Koma umphawi,ndi usilu,sizabwino