ANTHU A KU NTCHEU AMULANDILIRA MICHAEL USI CHONCHI POMWE WAFIKA KU NSEMBE YOKUMBUKIRA A CHILIMA

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 13 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 153

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin 2 หลายเดือนก่อน +26

    Anthuwatu mmitima mudakali moto olo muntima mwangamu ndangoona mpando wakhala usiwo zandikumbutsa achilima moyo kuwawa😢😢

    • @JoelMwambira
      @JoelMwambira 2 หลายเดือนก่อน +1

      Saksa

    • @RobertChikawonda
      @RobertChikawonda 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo mmene wawawila wangau esh

  • @NearBanda
    @NearBanda 2 หลายเดือนก่อน +18

    Mary chilima akumvetsa chisoni koma this word 😢😢😢 continue Resting well skc

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya 2 หลายเดือนก่อน +1

      Ndiponso,ine kulira kundimvetsa chisoni

  • @gracemaluwa4674
    @gracemaluwa4674 2 หลายเดือนก่อน +5

    Mai Kaliati pitilizani mtima wanu wabwino ,musasiye Mai Chilima okha munyengo yowawitsayi Amen

  • @MarthaBanda-ye4pt
    @MarthaBanda-ye4pt 2 หลายเดือนก่อน +21

    Ambuye mulimbikitseni mwana wanu Mary Chilima akuvetsa chisoni 😭😭😭

    • @AminahMussah
      @AminahMussah 2 หลายเดือนก่อน +1

      ndipo amphwa kwambili 😭😭😭😭

    • @henrychawinga4639
      @henrychawinga4639 2 หลายเดือนก่อน

      AMEN

    • @mphatsomonjeza4371
      @mphatsomonjeza4371 2 หลายเดือนก่อน

      God is with her 🙏🏻

    • @LywellChilupsa
      @LywellChilupsa 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo ine ngati ndilire

    • @AntinHawile-rw9fj
      @AntinHawile-rw9fj 2 หลายเดือนก่อน

      kulira kosalekeza tikulira nanu mayi mary chilima km ambuye yekha ndiyemwe akuziwa kwezan maso kwa yehova ndpo zonse zizakhala bwino mama😢😢

  • @nysonchapasuka7270
    @nysonchapasuka7270 2 หลายเดือนก่อน +4

    May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.

  • @CharlesChilinde
    @CharlesChilinde 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko.
    Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa
    ❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉

  • @GladysMwantenga
    @GladysMwantenga 2 หลายเดือนก่อน +2

    Apa mpomwe nda ziwa mau aja kuti atatanthauza izi😭😭😭pochoka mzako pali malo💔 continue rest in peace DR.chilima

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 2 หลายเดือนก่อน +9

    Mai Kaliyati pitilizani kufungatira Mary chilima.

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya 2 หลายเดือนก่อน

      Ndipo kwambiri

  • @TizifaBanda-xn5tm
    @TizifaBanda-xn5tm 2 หลายเดือนก่อน +1

    Mai kaliati...is the true politician and kholo.ku UTM musadzapange mistake kutaya Mai ameneyu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 2 หลายเดือนก่อน +9

    Marry kumvetsa chisoni mwana wa eni ake mayo ine😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

    • @WilliamMasula-cb1mg
      @WilliamMasula-cb1mg 2 หลายเดือนก่อน +2

      I feel sorry for her

    • @TamikaKaponya
      @TamikaKaponya 2 หลายเดือนก่อน +1

      ​@WilliamMasula-cb1mg kwambiri tu, Dziko lapansi hmmmm

    • @fannyzimba149
      @fannyzimba149 2 หลายเดือนก่อน

      Koma ndipo zovetsa chisoni 😭😭😭eish

  • @MemoryNyirongo-gt4mn
    @MemoryNyirongo-gt4mn 2 หลายเดือนก่อน

    Palibe chobisika padziko lapasi zingabisike bwanji zidzaulilika (muuse mumtendere achilima tidzakusowani mpaka kalekale) Amen

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 2 หลายเดือนก่อน +1

    All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 2 หลายเดือนก่อน +3

    Rest well Mr Chilima mayo Marry wanga ine usamale ndi usi chonde ndi mfiti yayikulu iyi😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 หลายเดือนก่อน

    Guys don't forget that no one knows when you will die, this is by only Him The Lord Almighty

  • @ChristinaNyirenda-zb1if
    @ChristinaNyirenda-zb1if 2 หลายเดือนก่อน +5

    Mulungu ndiwadongosolo azaziona tsiku ndilimoz

  • @stevenkambuku
    @stevenkambuku 2 หลายเดือนก่อน

    Koma imfa ya SKC mmmm I am speechless, Mhsrip

  • @FanscioDancun
    @FanscioDancun 2 หลายเดือนก่อน

    This is like bringing tears again

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j 2 หลายเดือนก่อน +3

    Myambo yokumbukila SKC izichitika mochuluka mpaka Wina chikumbumtima chimuphe ndithu

  • @DolicahGift
    @DolicahGift 2 หลายเดือนก่อน

    😭😭 Ambuye pitirizani kuwusamarira mzimu wa mr chirima 😢😢😢

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl 2 หลายเดือนก่อน

    We need your mercy our father 😢

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 หลายเดือนก่อน

    Corridors of justice shld prevail O, Lord. Rest in peace SKC

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys 2 หลายเดือนก่อน

    Mary khope yake ikadali nchisoni zuchita kuoneka ngatiso alipamalilo lero mzimu wa Saulos Klaus chilima uuse mumtendere ❤️😭😭

  • @eliaskachali-xn2ve
    @eliaskachali-xn2ve 2 หลายเดือนก่อน

    Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose

  • @rhodahjere8747
    @rhodahjere8747 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye limbikisani Mary chilima dzikoli ndowawa 😭😭😭😭😭😭

  • @JoyceChawawa-og1cj
    @JoyceChawawa-og1cj 2 หลายเดือนก่อน

    Only Almighty God knows

  • @Adamuson
    @Adamuson 2 หลายเดือนก่อน

    Azakhari sadaname kutchura bambo a Sikono kuti ndi nkhwari.

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v 2 หลายเดือนก่อน +6

    Koma mmene akuyang'anira patrisiayu pavuta apa

  • @DolothyMussa
    @DolothyMussa 2 หลายเดือนก่อน

    Mayi chilima mulungu akutothozeni ndipo akupaseni kulimbika mtima muzakaonana nawo mukachita bwino moyo uno muuse mu mtendele achilima misozi siyikutha kuno eshhhhh

  • @ChrissieGome
    @ChrissieGome 2 หลายเดือนก่อน

    Mzimu wa vice president , continue resting in peace

  • @CharityMhone-uk9ym
    @CharityMhone-uk9ym 2 หลายเดือนก่อน

    Pa ifa ya chilima manganya samaoneka lero watenga udindo akuoneka kamunthu koipa kapha mnzake chifukwa cha mpando chitsiru

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mayi kaliati mulungu adzikudalitsan ndithu

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 หลายเดือนก่อน

    Let's only pray for his soul rest in peace but don't create violence because of his death.love one another something bigger gonna come to our nation

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula 2 หลายเดือนก่อน

    Lero nsiku lomwe alengeze zakuchikangawa kod Komatsu alengeze basi lero ausi mmene zinayendela

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 หลายเดือนก่อน

    Koma dzikoli abale Mulungu pitilizan kuwatonthoza Mai Chilima pamodzi ndi ana awo R I P SKC😭😭

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 2 หลายเดือนก่อน

    Bambo asikonowo musamale nawo ameneyo ndi mbulu akuoneka ngati muli limodzi Koma Ayi makendulo amuontche munthu woyipa

  • @charleskhomolina2385
    @charleskhomolina2385 2 หลายเดือนก่อน +3

    😢😢😢Imfa yosayiwalika

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 2 หลายเดือนก่อน

    A usi ndiopanda manyazi, kuyandikana ndi Mary

  • @hopembendela
    @hopembendela 2 หลายเดือนก่อน

    Nkazi wa chilima akunvesa chisoni koma

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef 2 หลายเดือนก่อน +1

    Manganya 😭😭 pachoka nzako pali Malo, Ambuye mwalolelanj izii?

  • @SteliaKolomba
    @SteliaKolomba 2 หลายเดือนก่อน

    Ndakumbuka SKC😢😢

  • @felixjoseph8161
    @felixjoseph8161 2 หลายเดือนก่อน +1

    Manganya zoona ukumva bwanji muntima mwako pomuona nkazi wanzako akumvetsa chisoni ambuye akukhululukire sukudziwa zomwe ukuchita

    • @NatashaBema
      @NatashaBema 2 หลายเดือนก่อน

      Mfiti ilibe chisoni anwene

  • @manzyhetekele8697
    @manzyhetekele8697 2 หลายเดือนก่อน

    RIP SKC😢

  • @JoyceBAllubi
    @JoyceBAllubi 2 หลายเดือนก่อน

    Ambuye mutonthozeni mwana wanu

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 2 หลายเดือนก่อน +1

    Yudasi izi ndizomwe umafuna kuti uzikhala pamenepo. Iwe munthu oyipa kwambiri. Nzimu wa Chilima ukukanthe kosalekeza.

    • @lillianmwanza4218
      @lillianmwanza4218 2 หลายเดือนก่อน

      Mzimu wachilima ungokatenga

    • @amoschataika7440
      @amoschataika7440 2 หลายเดือนก่อน

      @@lillianmwanza4218 kkkkk ndipo inu

  • @Fatima-db8ut
    @Fatima-db8ut 2 หลายเดือนก่อน +1

    Lord have mercy

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn 2 หลายเดือนก่อน

    Woyeeeee mama Mary Chilima

  • @tulimwalwimba6544
    @tulimwalwimba6544 2 หลายเดือนก่อน +1

    Chilima! Eish

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 2 หลายเดือนก่อน

    Usi ukutaniko uko machende ako anagulisa chilima ulibe manyazi chakwera bwanji wayiopa ntcheu😂😂😂 mapwala ako

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 หลายเดือนก่อน +1

    Convensiion ngati ingokhala mawa iii.

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz 2 หลายเดือนก่อน +3

    Km ndizowswa kwambiri zandikhudza mary akuvetsa chisoni

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu 2 หลายเดือนก่อน +3

    Chifukwa chani awayika moyandikana chonchi? Kulakwa.

  • @WestonGawaza
    @WestonGawaza 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kupepela amugulisa mzawo mukumuyitanatso nose ndinu akupha

  • @DavieKidison
    @DavieKidison 2 หลายเดือนก่อน

    Zambili tikaziwa tikazaseka maso zinthu zamundale sizimaveseseka pakufunika mzimu wachiziwitso pamalawi anthu tisekule maso

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa 2 หลายเดือนก่อน

    Zausilu zosezo zitayene , mnavapo wakubanja wa anthu 9 aja akuonesapo action yiliyose yokwiya ,zitayeni zimenezo mngafelezaine

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek 2 หลายเดือนก่อน

    Chisoni chandigarh
    Usi Akuma bwanji

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 หลายเดือนก่อน

    Ausi mukumbva bwanji mpando mwakhalilawo zomwe mumafuna ndi zimenezo, Koma mukumbukire kuti lino ndi dziko si inu amuyaya

  • @YusufIbrahim-w1g
    @YusufIbrahim-w1g 2 หลายเดือนก่อน +1

    Usi yu ndisimene ankamvuna simenesi mulungu awawone agalu amenewa

  • @ChifundoSaladechitalo
    @ChifundoSaladechitalo 4 วันที่ผ่านมา

    Mulungu apilize kukhala ndi may Mary chilima

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 2 หลายเดือนก่อน +2

    Mmmmm mbola fanzi iyiyi ikuoneka yosasangalala

    • @maulanaallie6194
      @maulanaallie6194 2 หลายเดือนก่อน

      Ndye asangalala bwanji mwambo wachisoni ngati umenewu nanu

  • @FELIXMAJAWA
    @FELIXMAJAWA 2 หลายเดือนก่อน

    anthuwa sakukondwera ndikupezeka Kwa usi mitima yawo ikuwawa ngati ineyo

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 2 หลายเดือนก่อน

    Manganya yudasi km ukumuwona mery mene akuwonekera agulu lnu nose ndi chikangawa Lazaro aphangaka fiti skcpitilizani kupuma mtendere

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 2 หลายเดือนก่อน

    Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face

    • @mcsellahntv6896
      @mcsellahntv6896 2 หลายเดือนก่อน

      Me , I would forget ndine namalira, I could freak out.

  • @AustinBanda-ee6sb
    @AustinBanda-ee6sb 2 หลายเดือนก่อน

    A Malawi anzanga kuweluzana sibwino chili chonse akudziwa ndi Yahwe kuti zinakhala bwanji ndi chilungamo chizadziwikabe pangatalike maka

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he
    @ChristopherChimbalanga-ez5he 2 หลายเดือนก่อน

    Rest in peace SKC 😭😭😭

  • @Nadeon-y2k
    @Nadeon-y2k 2 หลายเดือนก่อน +1

    Kodi zikatero ndiye kuti Manganya adasiya kuchita zitsuzo

  • @JonathanMsiska
    @JonathanMsiska 2 หลายเดือนก่อน +1

    Koma tiuzane zoona pano Matinitedi tisiye kuvala aliyese nkhope Yake ikhale poyera.Mukazawona munthu wavala tinitedi kumaso ameyo ndi munthu oyipatsitsa.

  • @cmsanyama200
    @cmsanyama200 2 หลายเดือนก่อน +2

    Kutsutsula chilonda chosapola bwanji?

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 2 หลายเดือนก่อน +1

    Rest in peace skc 😭😭

  • @EllenNgoon-nc8vg
    @EllenNgoon-nc8vg 2 หลายเดือนก่อน +1

    😢😢 koma dziko iri

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 2 หลายเดือนก่อน +1

    Akuziona ngati Ali pamwamba yudasi akamayenda akuchita kunja nja

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 2 หลายเดือนก่อน +1

    Only God knows😢

  • @NoelBurton-x1z
    @NoelBurton-x1z 2 หลายเดือนก่อน +2

    SKC forever ❤

  • @vitumbikomateche
    @vitumbikomateche 2 หลายเดือนก่อน

    Skc for life

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 2 หลายเดือนก่อน

    Zimene sitimkaembekezela poti Ambuye munalola tilibe mau ife

  • @JaneMasikini
    @JaneMasikini 2 หลายเดือนก่อน

    Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh

  • @GodsFavourite1
    @GodsFavourite1 2 หลายเดือนก่อน +1

    Usi amabisala mu tinted😮

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 2 หลายเดือนก่อน

    Eee koma anthu kumuyang'ana kwakeko yudas 😂

  • @PatrickViyache
    @PatrickViyache 2 หลายเดือนก่อน +1

    Dzimu wanu ukawutse muntendele skc❤❤❤❤

  • @HestingsZiba-d6k
    @HestingsZiba-d6k 2 หลายเดือนก่อน +1

    Yudas wankulu usi kulandilidwa

  • @SydneyMwale-u9w
    @SydneyMwale-u9w 2 หลายเดือนก่อน

    Nkhalani ntcheru ndi usi uyo ndi fiti

  • @thomasmwitiya1447
    @thomasmwitiya1447 2 หลายเดือนก่อน +1

    Yudas kulandiridwa

  • @mosespemba8822
    @mosespemba8822 2 หลายเดือนก่อน +2

    Is that KABAMBE I'm seeing?

  • @aafrogarrix
    @aafrogarrix 2 หลายเดือนก่อน

    KOd uku zimachitikila kutiko

  • @AnusaNkhoma
    @AnusaNkhoma 2 หลายเดือนก่อน

    Mmmmmm😢😢

  • @CosmasChikwindi
    @CosmasChikwindi 2 หลายเดือนก่อน +3

    Tizakhala osauka ovutikitsitsa padziko lapansi chifukwa chakaganizidwe kathu , tinayenela dzinthu zikachitika tizivomeleza maso athu nkupenya kwamulungu koma osati kumalozana zala.

    • @chumasalanje4705
      @chumasalanje4705 2 หลายเดือนก่อน

      Iwe dont say like that its clear USI is the one who plan the death of SKC

    • @GiftKumbweza
      @GiftKumbweza 2 หลายเดือนก่อน

      Ndife anthu omvetsa chisoni kwambiri.Eti in this age and era amwene

    • @WorriedNdhlovu
      @WorriedNdhlovu 2 หลายเดือนก่อน

      Mapwala ambuyako iwe

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 2 หลายเดือนก่อน

      Akanadikira kaye 40 days a Manganyawo bola kuti alemekeza Mzimu wa anzao udindowo pambuyo.

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 2 หลายเดือนก่อน

    If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi?
    Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad.
    Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal.
    It's primitive life to fuel enemity for your personal gain.
    Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse
    Be civilized guys!!!

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 2 หลายเดือนก่อน

    RIP SKC

  • @georgeraphael8198
    @georgeraphael8198 2 หลายเดือนก่อน

    Mwapeza zonena eeeeee😅😅😅😅😅😅

  • @AgathaJerard
    @AgathaJerard 2 หลายเดือนก่อน +2

    Ausiwo kuchibwanoko Ngati apaka ufaaaa 😂😂😂😂😂😂😂

    • @lindaphiri3543
      @lindaphiri3543 2 หลายเดือนก่อน

      😂😂😂 ndipo zosawakhala

  • @AustinBanda-ee6sb
    @AustinBanda-ee6sb 2 หลายเดือนก่อน

    @ Jane ❤❤ ndaikonda comment yako

  • @SalaJawali
    @SalaJawali 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi awa alibe akazi awo mene a kumayenda okhamo

  • @nishanchiwaya4561
    @nishanchiwaya4561 2 หลายเดือนก่อน +2

    Macomentiwo oonesa kuti amalawi mwatopa ndi ulemu😅😅😅😅

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 หลายเดือนก่อน +1

    Yudasi. Satana kumuona akuyenda ndi miyendo. MHSRIP SKC

  • @RichardKuden
    @RichardKuden 2 หลายเดือนก่อน

    Dziko ndilovuta ndithu😂😂😂😂😂

  • @GeoLikwanya-cb9gn
    @GeoLikwanya-cb9gn 2 หลายเดือนก่อน

    Imfa yosaiwalika ku fuko laMalawi 😭🇲🇼

  • @Nunalinn
    @Nunalinn 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi iyeyo akazake sanapite nao

  • @CamlonLogistics-ju6mb
    @CamlonLogistics-ju6mb 2 หลายเดือนก่อน

    Mary chilima akufunika mapemphelo

    • @BlessingsTembenu
      @BlessingsTembenu 2 หลายเดือนก่อน

      Ameneyu anayenera naye kumamupempherela coz Ali munyengo yovuta heavy

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate 2 หลายเดือนก่อน +1

    😭😭😭

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 หลายเดือนก่อน

    Mery chilima usamale ndizopasana moni wamanja zanuzo kuli ma poison kumalawi kaya ayudasiwo musamale nawo

  • @KassimSteven
    @KassimSteven 2 หลายเดือนก่อน

    Mawu tilibe infe chathu ndichison bas