May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.
Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko. Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa ❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉
All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed
Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose
Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face
Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh
If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi? Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad. Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal. It's primitive life to fuel enemity for your personal gain. Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse Be civilized guys!!!
Anthuwatu mmitima mudakali moto olo muntima mwangamu ndangoona mpando wakhala usiwo zandikumbutsa achilima moyo kuwawa😢😢
Saksa
Ndipo mmene wawawila wangau esh
Mary chilima akumvetsa chisoni koma this word 😢😢😢 continue Resting well skc
Ndiponso,ine kulira kundimvetsa chisoni
Mai Kaliati pitilizani mtima wanu wabwino ,musasiye Mai Chilima okha munyengo yowawitsayi Amen
Ambuye mulimbikitseni mwana wanu Mary Chilima akuvetsa chisoni 😭😭😭
ndipo amphwa kwambili 😭😭😭😭
AMEN
God is with her 🙏🏻
Ndipo ine ngati ndilire
kulira kosalekeza tikulira nanu mayi mary chilima km ambuye yekha ndiyemwe akuziwa kwezan maso kwa yehova ndpo zonse zizakhala bwino mama😢😢
May the hand of Almighty God keep on strengthening you Mary Chilima in this critical situation you are going through. We are still mourning together. We understand that SKC has created a huge gap in your life Mama and other lives too but we must look up to Jesus Christ who has a final say.
Mzimu AChilima uwuse mumtedere ndi ntchito zonse anati gwirira ngati dziko.
Koma pamwambo umenewu pali ine azikakhala ndi ine mukuwadziwa nokha Mulungu awa Kathe chifukwa Ali ndi mtima osiyana kwambiri ndi momwe AChilima amakondera anthu awo owa tsatira mu U.T.M.ngati chipani. Mulungu odziwa kusunga ndi tothoza ayang'anire Mai Mary Chilima ndi banja lonse Sa
❤❤❤❤❤,, 🎉🎉🎉
Apa mpomwe nda ziwa mau aja kuti atatanthauza izi😭😭😭pochoka mzako pali malo💔 continue rest in peace DR.chilima
Mai Kaliyati pitilizani kufungatira Mary chilima.
Ndipo kwambiri
Mai kaliati...is the true politician and kholo.ku UTM musadzapange mistake kutaya Mai ameneyu
Marry kumvetsa chisoni mwana wa eni ake mayo ine😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
I feel sorry for her
@WilliamMasula-cb1mg kwambiri tu, Dziko lapansi hmmmm
Koma ndipo zovetsa chisoni 😭😭😭eish
Palibe chobisika padziko lapasi zingabisike bwanji zidzaulilika (muuse mumtendere achilima tidzakusowani mpaka kalekale) Amen
All of us we are still shocked and you will see someone saulting on this shameful time,it's better if you don't have something to say just keep quiet coz this is not a time to play with, this is time for the tears respect is needed
Rest well Mr Chilima mayo Marry wanga ine usamale ndi usi chonde ndi mfiti yayikulu iyi😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Guys don't forget that no one knows when you will die, this is by only Him The Lord Almighty
Mulungu ndiwadongosolo azaziona tsiku ndilimoz
Koma imfa ya SKC mmmm I am speechless, Mhsrip
This is like bringing tears again
Myambo yokumbukila SKC izichitika mochuluka mpaka Wina chikumbumtima chimuphe ndithu
😭😭 Ambuye pitirizani kuwusamarira mzimu wa mr chirima 😢😢😢
We need your mercy our father 😢
Corridors of justice shld prevail O, Lord. Rest in peace SKC
Mary khope yake ikadali nchisoni zuchita kuoneka ngatiso alipamalilo lero mzimu wa Saulos Klaus chilima uuse mumtendere ❤️😭😭
Ifa ya skc ma guys ndiyo pweteka paziko la pansi. MCP is a devel goverment.Nkhalani olimba a merry chilima, Kwa ine no vote for mcp mu umoyo wanga wose
Ambuye limbikisani Mary chilima dzikoli ndowawa 😭😭😭😭😭😭
Only Almighty God knows
Azakhari sadaname kutchura bambo a Sikono kuti ndi nkhwari.
Koma mmene akuyang'anira patrisiayu pavuta apa
Mayi chilima mulungu akutothozeni ndipo akupaseni kulimbika mtima muzakaonana nawo mukachita bwino moyo uno muuse mu mtendele achilima misozi siyikutha kuno eshhhhh
Mzimu wa vice president , continue resting in peace
Pa ifa ya chilima manganya samaoneka lero watenga udindo akuoneka kamunthu koipa kapha mnzake chifukwa cha mpando chitsiru
Mayi kaliati mulungu adzikudalitsan ndithu
Let's only pray for his soul rest in peace but don't create violence because of his death.love one another something bigger gonna come to our nation
Lero nsiku lomwe alengeze zakuchikangawa kod Komatsu alengeze basi lero ausi mmene zinayendela
Koma dzikoli abale Mulungu pitilizan kuwatonthoza Mai Chilima pamodzi ndi ana awo R I P SKC😭😭
Bambo asikonowo musamale nawo ameneyo ndi mbulu akuoneka ngati muli limodzi Koma Ayi makendulo amuontche munthu woyipa
😢😢😢Imfa yosayiwalika
A usi ndiopanda manyazi, kuyandikana ndi Mary
Nkazi wa chilima akunvesa chisoni koma
Manganya 😭😭 pachoka nzako pali Malo, Ambuye mwalolelanj izii?
Ndakumbuka SKC😢😢
Manganya zoona ukumva bwanji muntima mwako pomuona nkazi wanzako akumvetsa chisoni ambuye akukhululukire sukudziwa zomwe ukuchita
Mfiti ilibe chisoni anwene
RIP SKC😢
Ambuye mutonthozeni mwana wanu
Yudasi izi ndizomwe umafuna kuti uzikhala pamenepo. Iwe munthu oyipa kwambiri. Nzimu wa Chilima ukukanthe kosalekeza.
Mzimu wachilima ungokatenga
@@lillianmwanza4218 kkkkk ndipo inu
Lord have mercy
Woyeeeee mama Mary Chilima
Chilima! Eish
Usi ukutaniko uko machende ako anagulisa chilima ulibe manyazi chakwera bwanji wayiopa ntcheu😂😂😂 mapwala ako
Convensiion ngati ingokhala mawa iii.
Km ndizowswa kwambiri zandikhudza mary akuvetsa chisoni
But death 😢
Chifukwa chani awayika moyandikana chonchi? Kulakwa.
Kupepela amugulisa mzawo mukumuyitanatso nose ndinu akupha
Zambili tikaziwa tikazaseka maso zinthu zamundale sizimaveseseka pakufunika mzimu wachiziwitso pamalawi anthu tisekule maso
Zausilu zosezo zitayene , mnavapo wakubanja wa anthu 9 aja akuonesapo action yiliyose yokwiya ,zitayeni zimenezo mngafelezaine
Chisoni chandigarh
Usi Akuma bwanji
Ausi mukumbva bwanji mpando mwakhalilawo zomwe mumafuna ndi zimenezo, Koma mukumbukire kuti lino ndi dziko si inu amuyaya
Usi yu ndisimene ankamvuna simenesi mulungu awawone agalu amenewa
Mulungu apilize kukhala ndi may Mary chilima
Mmmmm mbola fanzi iyiyi ikuoneka yosasangalala
Ndye asangalala bwanji mwambo wachisoni ngati umenewu nanu
anthuwa sakukondwera ndikupezeka Kwa usi mitima yawo ikuwawa ngati ineyo
Manganya yudasi km ukumuwona mery mene akuwonekera agulu lnu nose ndi chikangawa Lazaro aphangaka fiti skcpitilizani kupuma mtendere
Marry maso ndi maso ndi mfiti yomwe idagulitsa mwazi mwamuna wake Ku MCP in exchange for His position,,Marry you are a strong woman trust I wouldn't afford to see USi face to face
Me , I would forget ndine namalira, I could freak out.
A Malawi anzanga kuweluzana sibwino chili chonse akudziwa ndi Yahwe kuti zinakhala bwanji ndi chilungamo chizadziwikabe pangatalike maka
Rest in peace SKC 😭😭😭
Kodi zikatero ndiye kuti Manganya adasiya kuchita zitsuzo
Koma tiuzane zoona pano Matinitedi tisiye kuvala aliyese nkhope Yake ikhale poyera.Mukazawona munthu wavala tinitedi kumaso ameyo ndi munthu oyipatsitsa.
Kutsutsula chilonda chosapola bwanji?
Rest in peace skc 😭😭
😢😢 koma dziko iri
Akuziona ngati Ali pamwamba yudasi akamayenda akuchita kunja nja
Only God knows😢
SKC forever ❤
Skc for life
Zimene sitimkaembekezela poti Ambuye munalola tilibe mau ife
Ma comment ali apa eee mphawi kuchulutsa zochita matukutuku aeni ake akubanja azisiya zonse mmanja mwa mulungu koma wina busy kumuloza chala munthu eishh
Usi amabisala mu tinted😮
Eee koma anthu kumuyang'ana kwakeko yudas 😂
Dzimu wanu ukawutse muntendele skc❤❤❤❤
Yudas wankulu usi kulandilidwa
Nkhalani ntcheru ndi usi uyo ndi fiti
Yudas kulandiridwa
Is that KABAMBE I'm seeing?
Yes
Yes with his madam
Yes he is
Yes
KOd uku zimachitikila kutiko
Mmmmmm😢😢
Tizakhala osauka ovutikitsitsa padziko lapansi chifukwa chakaganizidwe kathu , tinayenela dzinthu zikachitika tizivomeleza maso athu nkupenya kwamulungu koma osati kumalozana zala.
Iwe dont say like that its clear USI is the one who plan the death of SKC
Ndife anthu omvetsa chisoni kwambiri.Eti in this age and era amwene
Mapwala ambuyako iwe
Akanadikira kaye 40 days a Manganyawo bola kuti alemekeza Mzimu wa anzao udindowo pambuyo.
If usi was not eppointed as VP.....would you people continue to say he is yudasi?
Where the name yudasi has come from? Do not hate someone because you head from someone that he is bad.
Usi has been with our president the late Dr SKC and we have never heardbof any disloyal.
It's primitive life to fuel enemity for your personal gain.
Sorry for all of you who want Usi to fall and also you want him to feel like he is hated and leave utm.when he leaves you will also talk so much nosesnse
Be civilized guys!!!
RIP SKC
Mwapeza zonena eeeeee😅😅😅😅😅😅
Ausiwo kuchibwanoko Ngati apaka ufaaaa 😂😂😂😂😂😂😂
😂😂😂 ndipo zosawakhala
@ Jane ❤❤ ndaikonda comment yako
Kodi awa alibe akazi awo mene a kumayenda okhamo
Macomentiwo oonesa kuti amalawi mwatopa ndi ulemu😅😅😅😅
Yudasi. Satana kumuona akuyenda ndi miyendo. MHSRIP SKC
Dziko ndilovuta ndithu😂😂😂😂😂
Imfa yosaiwalika ku fuko laMalawi 😭🇲🇼
Kodi iyeyo akazake sanapite nao
Mary chilima akufunika mapemphelo
Ameneyu anayenera naye kumamupempherela coz Ali munyengo yovuta heavy
😭😭😭
Mery chilima usamale ndizopasana moni wamanja zanuzo kuli ma poison kumalawi kaya ayudasiwo musamale nawo
Mawu tilibe infe chathu ndichison bas