NONSE INU MUKUTCHINJIKIZA CHAKWERA PA IFA YA CHILIMA MUDZAKODZEDWA MUKUWONA NGATI 1964 THIS IS 2024 AMALAWIAN ANAPENYA PATALI SIMUNGATI NAMIZE AI OSAVUTIKA NDIKUNENA CHILUNGAMO TINACHIDZIWA KALE CHAKWERA AKUWONONGA NTHAWI CHOTI AZIDZIWA CHAKWERA ALIPAVUTO KWAMBILI
Buzi ya m'busa iwe
Abusa mwaiwala Mulungu Kodi zimene munalonjeza kutumikila ndi zimenezo?
Mmmm koma bundle yanga yathad chizungu chandivutakumva😭
NO MANYAZI KUKULA KONSEKO?
Tinalakwanji amalawi kumangotinaminsa zakha zonse 4 koma siku linsavika likwana la 45
Kodi uyuyu ndi wa mpingo uti Thawale uy?
Izizi chifukwa si m'bale wanga chikhala chilima anali m'bale nditaponya chiphe kalekale kwa agalu amenewa apapa tinganene kuti ndi report or lembetso
NONSE INU MUKUTCHINJIKIZA CHAKWERA PA IFA YA CHILIMA MUDZAKODZEDWA MUKUWONA NGATI 1964 THIS IS 2024 AMALAWIAN ANAPENYA PATALI SIMUNGATI NAMIZE AI OSAVUTIKA NDIKUNENA CHILUNGAMO TINACHIDZIWA KALE CHAKWERA AKUWONONGA NTHAWI CHOTI AZIDZIWA CHAKWERA ALIPAVUTO KWAMBILI
Koma muli ndiuzimu azigalu inu zitsilu za anthu
Nonse ndinu agalu mudziwe kuti mukagona mawa mufela kutulo
Tsiku lizafika anthu awa akubwelesa commission inquiry ya bodzayi mwazola manyi amwini chifukwa inuso muzafusidwa chifukwa chani munalola kupeka report laboza? 2025 ikubwela zonse zizaziwika poyela ndipo muzayimbidwa milandu chifukwa chobisa nkhani anthu inu nanuso mwayingongola nkhaniyi tikumana next year
Ndizomwe adakuuzani Kuti muzanene zimenezi?manyi Eni Eni ,
Akuwerenga ndakatulo kodi
Nthawi izakwana kuti chilungamo chizaziwike
Usatana uli ku Malawi panopa womvesa chison wochitisa manyazi Mulungu akuoneni nonsenu ndpo sadzakukhululukiran or asatana
Nonsense.palibe chikumveka.
Trush lokhalokha anthu mwakalambadi ndithu nthawi yonsei mawadikirirutsa a malawi zau galuzi mxiiiii
Only God knows ndpo misodzi yonse yomwe analira Amalawi onse aja dziwani adzapukuta ndi Mulungu siku lidzafika ndpo u will pay heavy price
LIPOTI ILI MUKAWUZE AMANU
NOSE MWQBWERETSA LIPOTI LABODZALI MUKUDZIYILA MAKALA AMOTO PA BED LANU SIMUDZAKHALA FULU MUNO MALAWI MUDZAZIWUZE NDALAMA ZOMWE CHAKWERA WAKUPATSANI ZOTI MUNAMIZE NAZO AMALAWIAN KOMA MUDZAWONA ANTHU INU MUKUSEWERA KWAMBILI
This person's is killed 9 people in chikangawa
Koma magazi amuthu
It doesn't make sense
At all and they wasting there tym
True zaziiii
Rubbish