ไม่สามารถเล่นวิดีโอนี้
ขออภัยในความไม่สะดวก

KUZUKUTA NKHANI ZOMWE ZACHITIKA.UKU KWATENTHA 🔥🔥🔥🙌🙌

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 25 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 100

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA หลายเดือนก่อน +12

    Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko

  • @macdonaldmunthali9895
    @macdonaldmunthali9895 หลายเดือนก่อน +9

    Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g หลายเดือนก่อน +3

    Kabambe afunampando ku utm koma autm samalanaeni mtsogoleli wanu autm sankhani kaliati ndiponso pamasankho adzawina anthu tilinae ndichikhupililo enawa tawaesa akanika

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l หลายเดือนก่อน +1

    Nkhani ndiyomweyo mwamva bwino zikomo kwambiri pamibawa.. God bless you two guys... Mamakutu wava koma wopanda makutu mawa wazakuwawani

  • @lifayohbenson1994
    @lifayohbenson1994 หลายเดือนก่อน +3

    Ku utm kulibe mphungwe mpungwe
    Winayo chipani chake ndi odya zake alibe mulandu

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f หลายเดือนก่อน +1

    Anapha dala chilima cholinga anthu abalalike koma mulungu ndiwadongosolo a utm osafooka osatopa osaopa

  • @SharifChibwana
    @SharifChibwana หลายเดือนก่อน +5

    Bakili Muluzi tv ndi katundu

  • @user-nv3rf7bl7r
    @user-nv3rf7bl7r หลายเดือนก่อน +2

    Uku nde kuyankhula kopanga umodzi that's y ndimakukondani amibawa chifukwa mumayankhula chilungamo

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale หลายเดือนก่อน +1

    Apa a UTM Mukapanda kumva zanu izo

  • @PeterTembo-zj5jk
    @PeterTembo-zj5jk หลายเดือนก่อน

    Dpp moto❤❤❤

  • @ManzyNgoleka
    @ManzyNgoleka หลายเดือนก่อน

    vuto inu akulu mukukocha ndale mwachidule nanu mulikuseli kwa enaake

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g หลายเดือนก่อน +2

    MCP my vote ❤❤❤❤❤❤

  • @JazzdMonga-v6e
    @JazzdMonga-v6e หลายเดือนก่อน +1

    Kumupeza wina akuti mcp my vote
    Amalawi ndichani

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus หลายเดือนก่อน +1

      Ena si anthu....ndizinyalala tu.

    • @BlessingsNyirenda-ru7ss
      @BlessingsNyirenda-ru7ss หลายเดือนก่อน

      Eti eti amwene mumune mcp yawonongera zinthu ndiye wina akut mcp my vote eeeesh

    • @nellybruhan5834
      @nellybruhan5834 หลายเดือนก่อน

      Anthu ena alibe mzimu... Kuti mwaoneso akuyankhulawo ali mbuuu

    • @pemphokatembe443
      @pemphokatembe443 หลายเดือนก่อน

      Kufuna kuzamva mkhwangwa ili mmutu

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn หลายเดือนก่อน +2

    Khondo Yochita kutiponyera Mcp kumupanga usi
    LET HIM BE THERE WILL MAKE CONVENTION SOON

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 หลายเดือนก่อน

    Aaa manganya ngati mutu mwake dziyendamo bwino ayi musiyeni ku MCP koko afela nayo limodzi

  • @VincentMbeye
    @VincentMbeye หลายเดือนก่อน +1

    Yalakwa UTM kuchoka msanga ....awonesa umbuli kwambili

    • @Aqiec09
      @Aqiec09 หลายเดือนก่อน

      Ndipo usavage wa athu ophunzira umakhumudwisa

  • @daviskamonde4882
    @daviskamonde4882 หลายเดือนก่อน +2

    Don't lie to us.
    You support MCP.

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l หลายเดือนก่อน +1

    Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri
    We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 หลายเดือนก่อน

    Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl หลายเดือนก่อน +2

    UTM motomoto osadandaula

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga หลายเดือนก่อน

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @TonykalicheloKalichelo
    @TonykalicheloKalichelo หลายเดือนก่อน +1

    Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan

  • @lyiemax
    @lyiemax หลายเดือนก่อน

    Proper narration, big up guys ❤❤❤

  • @RegistermoseskashonKashon
    @RegistermoseskashonKashon หลายเดือนก่อน +1

    Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z หลายเดือนก่อน +2

    Mwawathandiza ulemu

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl หลายเดือนก่อน

    Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed

  • @EdsonNjonjo
    @EdsonNjonjo หลายเดือนก่อน +1

    Munthu uyu akunena zoona

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti หลายเดือนก่อน +5

    Athu akuda ndife opanda nzeru

    • @MervinKandoje
      @MervinKandoje หลายเดือนก่อน

      You to be specific

  • @OsmanMasamba-ck4mo
    @OsmanMasamba-ck4mo หลายเดือนก่อน +1

    Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako

  • @FloraBanda-w7t
    @FloraBanda-w7t หลายเดือนก่อน

    Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂

  • @user-ux9ik4zr5x
    @user-ux9ik4zr5x หลายเดือนก่อน

    Probably the best program

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi หลายเดือนก่อน +1

    Ndibwino kt atengane okhaokah

  • @StevieTaiza-r9j
    @StevieTaiza-r9j หลายเดือนก่อน

    Mulungu azikutete bro

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r หลายเดือนก่อน +1

    Akumatibera zathu zomwezi zamisokho

  • @EstherManda-ex3bc
    @EstherManda-ex3bc หลายเดือนก่อน +1

    🤣🤣🤣🤣 nkhani zake

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 หลายเดือนก่อน

    Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw
    @ChiyembekezoPhiri-sv8nw หลายเดือนก่อน

    Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu

  • @Ishriss1999
    @Ishriss1999 หลายเดือนก่อน

    Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo2972 หลายเดือนก่อน

    Gwende u have fairly advised

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w หลายเดือนก่อน

    Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz หลายเดือนก่อน

    Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako

  • @user-rx7cc7tc6b
    @user-rx7cc7tc6b หลายเดือนก่อน +1

    MCP 💥💥💥❣

  • @GiftKaunda-f8j
    @GiftKaunda-f8j หลายเดือนก่อน

    Analysis yanzeru zozama koma imeneyo?

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga หลายเดือนก่อน

    anthu atamalankhura ngati mmene ukuyankhulira lweyo anthu akhoza kumachitazinthu mwanzelu

  • @ChrispinKashosha
    @ChrispinKashosha หลายเดือนก่อน +2

    Mcp ya wina kale

  • @user-he5ol5or7f
    @user-he5ol5or7f หลายเดือนก่อน

    Gwede is the best

  • @dysonmasiye5736
    @dysonmasiye5736 หลายเดือนก่อน

    Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 หลายเดือนก่อน

    Pamaliro wandale athamangitsidwe

  • @JasonMailos
    @JasonMailos หลายเดือนก่อน

    😢😢😢😂 ozuka kumandao
    Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 หลายเดือนก่อน

    First to comment

  • @MasaukoNyirongo
    @MasaukoNyirongo หลายเดือนก่อน +1

    😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b หลายเดือนก่อน

    Kuwechetamwangajimbilambali

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b หลายเดือนก่อน

    Aaaaa
    Malawi

  • @ZioneMkangadzula
    @ZioneMkangadzula หลายเดือนก่อน

    utm igawana zida zafikapa angonamizana

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 หลายเดือนก่อน +5

    MCP 🔥🔥🔥🔥

    • @IshmaelIbrahim-s8c
      @IshmaelIbrahim-s8c หลายเดือนก่อน +4

      Pathako pako 😂

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga หลายเดือนก่อน

      Wabaya ase kkkkkk​@@IshmaelIbrahim-s8c

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga หลายเดือนก่อน +1

      Iwe fisi eti 😢😮

    • @user-he4jv1sb1m
      @user-he4jv1sb1m หลายเดือนก่อน +1

      Mapazi ako nd mcp yomweyo

    • @MaryNyirenda-nq3mh
      @MaryNyirenda-nq3mh หลายเดือนก่อน +1

      Njoka iwe fiti

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b หลายเดือนก่อน

    Umakwana

  • @PociahMack
    @PociahMack หลายเดือนก่อน

    Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂

  • @PhiriChitani
    @PhiriChitani หลายเดือนก่อน

    Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l หลายเดือนก่อน

    Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke หลายเดือนก่อน

    Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke หลายเดือนก่อน

    As government I think abalalika ndithu

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga หลายเดือนก่อน

    vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........

  • @user-gk4nu4xr8r
    @user-gk4nu4xr8r หลายเดือนก่อน

    Of course

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of หลายเดือนก่อน +2

    akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani

    • @RhodaBandah-sh1ir
      @RhodaBandah-sh1ir หลายเดือนก่อน +1

      Tafotokozani mmene akuwonongela ....

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda หลายเดือนก่อน

    Ntchindi mulije mu utm

  • @user-kj7hr2jf1l
    @user-kj7hr2jf1l หลายเดือนก่อน +1

    Zowona utm yisatenge munthu wakunja

  • @atupelemposa4786
    @atupelemposa4786 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂

  • @MayesoKulea-sh8xd
    @MayesoKulea-sh8xd หลายเดือนก่อน +2

    MCP ☑️

  • @YohaneMotison
    @YohaneMotison หลายเดือนก่อน

    😂😂😂😂😂😂

  • @PulayaKalaka
    @PulayaKalaka หลายเดือนก่อน +1

    Mcp mooootooooooooo

  • @user-cb5gh9md4i
    @user-cb5gh9md4i หลายเดือนก่อน

    Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo

    • @officemoyenda-rj2hz
      @officemoyenda-rj2hz หลายเดือนก่อน +1

      Si ntchentche

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂😂

    • @FloraBanda-w7t
      @FloraBanda-w7t หลายเดือนก่อน

      😂😂😂😂esh I think ndi lens

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie หลายเดือนก่อน +1

    Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️
    🙏🙏

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus หลายเดือนก่อน +1

      Ndiwe opembedza mafano
      Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p หลายเดือนก่อน

      Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri

    • @robertkalima874
      @robertkalima874 หลายเดือนก่อน

      @@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c หลายเดือนก่อน

      Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga หลายเดือนก่อน

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus หลายเดือนก่อน

    Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b หลายเดือนก่อน

    Aaaaa
    Malawi