kangaude

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 10 ก.ย. 2024

ความคิดเห็น • 162

  • @gladyschisomo4324
    @gladyschisomo4324 ปีที่แล้ว +5

    Bwana Abel tafufuzani akuluakulu alowelelepo anthu osaukafetu tilibe voice mwawamva a OC akuti kaya anthu akumudziwo kusonyeza kuti akumudzi ife tilibe mphamvu a original OC akudziwa ndithu pomwe inayambila ndipomwe inathela zose akuzidziwa koma akubisa

  • @kofibist6845
    @kofibist6845 ปีที่แล้ว +7

    A police achinyengo palibe chanzeru chomwe ayankhulapo andinyasa kobasi anthu anji opanda chisoni ndimomwe akuonekera mwanayo 😢

  • @marynkhata9707
    @marynkhata9707 ปีที่แล้ว +5

    Chisiru ndi bambo wa mwanayo zosenzi zikuchitika chifukwa cha iye ndi abale ake afitiwo mulungu amukhuze mwanayo ndi machiritso 🙏

    • @DanJohn-ws5gl
      @DanJohn-ws5gl 12 วันที่ผ่านมา

      Kwambili zonsezi chifukwa ndi bambo nkhwimayo ndi sister wake nfitiyo

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 ปีที่แล้ว +7

    Anthu mwapasa bail wina akubwera kuzaseketsa mlandu koma opasidwa bail osauzidwa kuti mlandu uja watha 😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 ปีที่แล้ว +6

    Wa police uyo ali ndi vuto akubisa kuyikira ku mbuyo a police ena

  • @BlessingsNyirenda-ru7ss
    @BlessingsNyirenda-ru7ss ปีที่แล้ว +2

    Apolice a police pena muzikhala ngat tonse ndife anthu mukuyankha mozemba zemba pomwe mukuziwa chowona mulungu akukantheni

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 ปีที่แล้ว +7

    Wapolisi uyuyu ngati ntchito akugwira chonchi ndiye kuti akuononga dziko basi

  • @user-yp3um6mf8d
    @user-yp3um6mf8d ปีที่แล้ว +5

    This is a sad development Abel.Please pull up your strings until the end of this case.Both the Officer In charge and the police officer have to be fired and save a curruption case.And unlawful arrest of those victims.When the complainant closed the case the police didn't bother to inform the defendants.Please Malawian Lawyers take this case to court on probno there is money here.The case can be seen that it is on the defendants' side.

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 29 วันที่ผ่านมา

    Kungoyambila Dam lomwe anapanga mamunayo liphwele asowe podalira ndipo amve kuwawa Ngat mmene akumvera mwanayo mu dzina la Yesu.... chemwali wa mamunayo tikupemphera kusauka kuti aziwe za ukulu wa Yesu...OC and corrupt officers ku police imeneyoyo i speak kuchosedwa ntchito kuti aziwe kuwawa kobeleka in Jesus name...I can feel the pain that this family is passing through,this is temporary life tikayankha pa maso pa Mulungu zosezi.

  • @victoriawilliam4490
    @victoriawilliam4490 ปีที่แล้ว +4

    Alibe mfundo a OCwo
    Akuti anthu akumudzi iye ndiwakuti ? Palibe chomwe anganene ndimbava zokhazokha zonsezo

  • @user-di4om7sh8w
    @user-di4om7sh8w ปีที่แล้ว +2

    Ndikumufunila🎉 kuchila mwa nsanga Mwana ameyu

  • @HellenKanyemba
    @HellenKanyemba 3 หลายเดือนก่อน

    Awa akanazisiya apange focus zamwanayo komanso anthu awaonetsa chikondi iwonso mwachikondi akhululuke

  • @costerrobert1519
    @costerrobert1519 ปีที่แล้ว +5

    Wapolice uyu ndi mbudzi yeniyeni ndithu

  • @user-qq6dv2up3w
    @user-qq6dv2up3w 11 หลายเดือนก่อน +1

    Zkundinvekera mwachinyengo choncho aaa koma dzikoli

  • @reginamichael7664
    @reginamichael7664 ปีที่แล้ว +2

    Chilungamo chioneke chifukwa wina aliyense ngat wachoka pantchito kaya wapita ku holiday kukapuma aliyense amamuziwa yemwe wamusiya pa mpando.

  • @YusufWanck
    @YusufWanck ปีที่แล้ว +3

    Ku police kulibe chilungamo too much kubelekana kma pa chichewa pali mawu "Chaona nzako chapita mawa chili kwa iwe" Ndipo Galu aliyense ali ndi tsiku lake.

  • @user-hg9ye9ux1v
    @user-hg9ye9ux1v ปีที่แล้ว +2

    Kunyasa mawu ngati mamuna ukuwoneka kuti ndiwe oyipa gaku

    • @user-tg1tg8wt8f
      @user-tg1tg8wt8f ปีที่แล้ว

      Mayi oyipa uyu mayi zimbili ndikumuziwa anandimanga ine ndisanalakwe ndizamupeza ubwino wake Ali kwathu tizakupezani komweko

    • @user-yk6qn3hg5i
      @user-yk6qn3hg5i 11 หลายเดือนก่อน

      Ndipo live

  • @MemoryLungu-sp8eq
    @MemoryLungu-sp8eq 4 หลายเดือนก่อน

    Iwe OC chomwe udziwe lungalunga kubadwa chilema chichita kuza uziona ndiwe mzimayi kms Uli ndi ana

  • @user-oq1pz6cv1y
    @user-oq1pz6cv1y 2 หลายเดือนก่อน

    Ndikuva kuti ndiwachinyengi OC

  • @user-ek3tm3su3g
    @user-ek3tm3su3g 3 หลายเดือนก่อน

    Apolice akumalawi ntchito yomwe amagwila siyidziwika mwana momwe akuwonekelamo moti chisoni alibe😢😢😢 kmaso akufuna kwabwino angothandiza mwanayo bola zinazo angozisiya kuweluza ndikwamunuwake mulungu and awakanthila pansi pompano

  • @user-xf1gb5gu3z
    @user-xf1gb5gu3z 5 หลายเดือนก่อน

    I believe the women, they are saying the truth. Apolisi akuno it's there habit, amatenga aliyense accused or locked in behind the bars is a criminal without proper investigations and arrogations.
    Another thing is this, ufiti and satanism here in Malawi zikuchuluka and with those coordinates and networks amongst them when they are together, no truth comes out. They backside each other.
    I can encourage them to do fasting and praying for a breakthrough, there's a living God in Heaven. I am testifying, that's why I am awake by this time. Let's keep on praying everyday, every time and live a Holy life.

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 ปีที่แล้ว +3

    Abel u must no urself that Ur putting urself on the map of the country we need this issue until the end ...Ur doing the GRT job ...I like that question chifukwa chani apolice ndi atolakhani safuna kugwilizana keep it up bro❤

  • @shabaniphiri7261
    @shabaniphiri7261 ปีที่แล้ว +2

    Kodi bambo a Gracious alikuti Albel tawafufuzani abwere azalankhule mbali yake

  • @ericchilinjala481
    @ericchilinjala481 4 หลายเดือนก่อน

    9:27 kunkhozomolaku..tubecho nthawi zina chimasuntha..nkonanso akubanika..ndiofunika chest x ray ..kuti aone ngati tube chili mmalo.

  • @abdulkha7810
    @abdulkha7810 ปีที่แล้ว +4

    Ku malawi wachuluka katangale please 🙏🙏 boma tinthandizeni

  • @user-ws4ue7tf6j
    @user-ws4ue7tf6j ปีที่แล้ว +1

    Mmmmmm koma nzimayi oti kuwawa kwa uchembele ukukudziwa sunga pondeleze khani chonchi kodi police yakwathu kumalawi mumachulutsa kupanga ziphuphu bwanji koma ??? Mulibe manyazi ??? Inetu ndinkayesa kuti
    Police imathandiza komano apapo ndatsimikiza kuti police ndimbava eniyake ziphuphu mudziweni mulungu

  • @brighttomakamanga5370
    @brighttomakamanga5370 ปีที่แล้ว +2

    please amabungwe lowelelanipo mayankhowa sizowona ayi apolice tiyeni tigwire ntchito yathu mowopa mulungu umphawi chisakhale chitozo

  • @user-mk8cn2no3o
    @user-mk8cn2no3o 5 หลายเดือนก่อน

    Apolice amangofuna ndalama nda mbava zikuluzikulu koma chilungamo chioneke

  • @reginamichael7664
    @reginamichael7664 ปีที่แล้ว +3

    Pagona chinyengo apaaa. Koma chilungamo chioneke bac

  • @ErickDzicco
    @ErickDzicco 2 หลายเดือนก่อน

    Ndikumufunira chithenda chapadera dera wa police ameneyi😢😢

  • @MariaKhowoya-lu5yc
    @MariaKhowoya-lu5yc 20 วันที่ผ่านมา

    Matsiku ano apolice sakuiziwa tchito yao kwao ndikuba basi

  • @user-yk6qn3hg5i
    @user-yk6qn3hg5i 11 หลายเดือนก่อน

    Km mamuna aneneyo komaso ccter wakeyo mulungu awakanthe mu dzina la yesu amen

  • @chifunirosaka9077
    @chifunirosaka9077 ปีที่แล้ว +1

    Mum'dzina la Yesu chilichose chobisika pankhaniyi chibwela poyela ndipo mulungu awapatsa chilango pompano padziko lapasi anthu akumuona amen

  • @user-hc6rc7yr8y
    @user-hc6rc7yr8y 7 หลายเดือนก่อน

    Wapolice oyo malankhulidwe ake akuchita kuoneka mmalankhulidwe ake kuti pali chinyengo

  • @user-di4om7sh8w
    @user-di4om7sh8w ปีที่แล้ว +3

    Km ndikanakonda bamboo oyipayi mutacheza naye onse Ali limodzi

  • @user-ws4ue7tf6j
    @user-ws4ue7tf6j ปีที่แล้ว

    Timadziwatu kuti eniyake ogulitsa chamba ndinu a police ziphuphu ngati mukuyamba inuyo ana anu mungawala ngize bwanji zigawenga zachabechabe

  • @user-od9wh3iu9w
    @user-od9wh3iu9w 5 หลายเดือนก่อน

    Kt apeleke galimoto yokagwilila muthu wa police kumatelo aaaaa

  • @user-lr7ux2ok4t
    @user-lr7ux2ok4t ปีที่แล้ว +3

    Chulungamo chiziwike Ambuye atichitile chisoni

  • @user-od9wh3iu9w
    @user-od9wh3iu9w 5 หลายเดือนก่อน

    Tili pano kuonesetsa khan imeneyi iyende mopanda chinyengo

  • @saukophiri4535
    @saukophiri4535 ปีที่แล้ว

    A police ndi atolankhani zikuoneka kuti sadzagwirizana olo pang'ono chifukwa atolankhani amalondoloza nkhani mpaka olokwa apezeke pamene kumbali ya police amabisana .Zikuonekeratu kuti a oc wo akudziwapo kanthu and vuto ndi iwowo

  • @user-rf7qu1gb3f
    @user-rf7qu1gb3f 7 หลายเดือนก่อน

    Amene angakwanitse kuwathandiza anthuwa kut nkhan ipite chitsogolo pliz do so amene muli ndikuthekera Sizoona zikuchitikazi

  • @BdhfbHdhe-pd7nh
    @BdhfbHdhe-pd7nh ปีที่แล้ว +3

    Abel undipezele bambo amwanayu ndimenyane nawo 1_1

  • @JaneMzengeza
    @JaneMzengeza ปีที่แล้ว +2

    Moyo uno sukufunika kukhala odekha,sukufunika kukhala opusa,sukufunika kumazionela pansi kuti ndine wamkazi,pompo munamuona uyo amadzintcura kuti OC yo mukanapatsa makofi yobu 13 :13 ndipomwe pakanayambika kuoneka cilungamo

  • @mkhokholasamuzonda5094
    @mkhokholasamuzonda5094 ปีที่แล้ว

    kodi iwe wa camera osamujambula wapolisi wopusayo bwa timuone

  • @user-xn6yp2nj8t
    @user-xn6yp2nj8t 8 หลายเดือนก่อน

    Galu oc ameneyo chinyengo kwambili...mbuzi

  • @omarlux3434
    @omarlux3434 ปีที่แล้ว +1

    muzayimalize tizave kuti zili pati?

  • @user-hw8ds8oy6i
    @user-hw8ds8oy6i 8 หลายเดือนก่อน

    Chili chose Mulungu akuwona

  • @esteryndau8546
    @esteryndau8546 ปีที่แล้ว +1

    Zikhala bwanji za mkati mwanu poti mwana anamuyika ku cell mayi khalani ndi mtima wachikondi inu m' mene mwafotokozera tanziwano kuti mkuziwapo kanthu

  • @herbartkaphamthengo9978
    @herbartkaphamthengo9978 ปีที่แล้ว +1

    Apolice ambiri kumalawi akufunika zaichosedwa ntchito akapanga zinthu zophera anthu ufulu chifukwa akumazuza anthu ambiri.

  • @LuciasZepete
    @LuciasZepete 5 หลายเดือนก่อน

    Apolice ambiri vuto lake ndi mburi

  • @faithmtika6121
    @faithmtika6121 ปีที่แล้ว +1

    Mulungu amuchitire chifundo mwanayo

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 ปีที่แล้ว

    Ambuye alowelerepo..ndipo awochetse ntchito...komanso wa 70 uja alondoledwe basi..

  • @herbartkaphamthengo9978
    @herbartkaphamthengo9978 ปีที่แล้ว +2

    Nkhani imeneyi ilondolezeni please izikike pothera

  • @EstherZintambira-sq3yy
    @EstherZintambira-sq3yy ปีที่แล้ว

    Palibe chanzelu chayankhidwapo

  • @AkimNyimba
    @AkimNyimba 11 หลายเดือนก่อน

    Mwamuna oyipa mulungu amene analenga iyeyo ndi mwana yo amupase chilango mwamuna yo nkhaza kwamwana

  • @user-xf1gb5gu3z
    @user-xf1gb5gu3z 5 หลายเดือนก่อน

    Officer in charge, "she is even failing to explain of the case, oh my!" she had the mother's file but hear what she's saying 😮😢 oh my!
    Good job Abel, I salute you. This is perfect, keep on doing this good job. We need to correct where things are going wrong by giving out our overviews of what is going on.
    Choonadi sichiola, chilungamo sichimatayika, so watch out when you're doing a bad thing. It comes back to you, from God. There's no secret under Heavens, under the clouds and under the sky.
    Those police are insane, not helping.

  • @user-nx7yz4qo8f
    @user-nx7yz4qo8f ปีที่แล้ว

    Oc yo sangalephere kudziwa yemwe amkagwila ntchito nthaw yomwe iyeyo anali pa holiday,nanga anafufuza bwanji kudziwa za omwe anasekedwawo mayina awo akuwantchula bwa?

  • @giftblack7690
    @giftblack7690 ปีที่แล้ว +1

    Apolice akumalawi ndi amphawi nde sangalondoloze nkhani opanda dziphuphu anthu inu mulungu adzakulangeni kwambili ndipo inu a oc ntchito yanu simumayidziwa koma dyela kukonda ndalama mudzafa mumphawi ndinu otembeleledwa

  • @ErickDzicco
    @ErickDzicco 2 หลายเดือนก่อน

    Koma mfiti wa police iweyo ndwe onyatsa ndi mtima omwe

  • @jumbradoone4164
    @jumbradoone4164 ปีที่แล้ว

    Thumba la Chamba lasokonekela mmanja mwa a Police?

  • @monicabanda7322
    @monicabanda7322 7 หลายเดือนก่อน

    How is the baby now asking from Washington DC.

  • @shabanitendo4781
    @shabanitendo4781 ปีที่แล้ว

    Maiwa ndi hule komaso mfiti khope yakeyo ngt buluz

  • @FosterCement-yn4cj
    @FosterCement-yn4cj ปีที่แล้ว

    Atseka bwanji nkhani abale pangani zoti chilungamo chioneke amaseka bwanji mulandu

  • @chikonjiwe007
    @chikonjiwe007 2 หลายเดือนก่อน

    A police aku Malawi too much corruption fosteki

  • @hucklyrajabu7137
    @hucklyrajabu7137 ปีที่แล้ว +1

    Sambi abale Mmmmmm ai ndithu Allah akhale nanu sister

  • @siskanyirenda
    @siskanyirenda ปีที่แล้ว +1

    Nkhaniyi siingathe choncho apange apilu police Ina iyendeposo apo bii police ilibe ntchito ndi mbava zikuluzikulu zobela anthu akuona

  • @joicemartin-ji5zu
    @joicemartin-ji5zu ปีที่แล้ว +1

    Ndi cisiru ameneyo wachinyengo ameneyo

  • @jennifermbewe9684
    @jennifermbewe9684 ปีที่แล้ว

    Murungu adzaurura zisisi zose zobisika murungu ndiwo Oshwa kwambiri

  • @mrsnsuzilenardil4827
    @mrsnsuzilenardil4827 ปีที่แล้ว +2

    Mmmmmm Sambi chinyengo

  • @user-oq1pz6cv1y
    @user-oq1pz6cv1y 2 หลายเดือนก่อน

    Kodi anawamanga chifukwa chani😢

  • @namondwejohn9354
    @namondwejohn9354 4 หลายเดือนก่อน

    Mmmm koma amayi awa mulungu awaone mai odziwa ululu pobereka kukhara satana chonchi,atolankhan musaisiye panjila mkhan kufikira chilungamo chiyende ngati madzi,kuti ena atengerepo phuzilo

  • @peterchunga8990
    @peterchunga8990 8 หลายเดือนก่อน

    Iyi ndinkhani yomvetsa chisoni kwambili koma OC wapa luchenza wachulukitsa katangale and nkhani ngati izi ndizija apolice amapezelapo mavuto chifukwa chamchitidwe waukatangale koma ine zitandichitikila zimene wayankha OC ameneyu straight mpakana ndimpanga chiwembu kuti ena atengelepo phunzilo mmayi opusa kwambili.

  • @yassinjanna9564
    @yassinjanna9564 ปีที่แล้ว +1

    Wa police yi ndiwamwano

  • @AishaPanjira-od9hg
    @AishaPanjira-od9hg ปีที่แล้ว +1

    Apolisi akumalawi ndi zisilu

  • @towellabanda2218
    @towellabanda2218 ปีที่แล้ว

    Ndi Ameyo mayiyo 😂😂😂😂😂
    Wazomera kale

  • @Ibrahim-m1d8t
    @Ibrahim-m1d8t ปีที่แล้ว +1

    AC Odyssey Samantha Road indore

    • @Ibrahim-m1d8t
      @Ibrahim-m1d8t ปีที่แล้ว +1

      Cesar bueno bellissima Bangor Georgia

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 ปีที่แล้ว

    Azimai ndinu anthu oipa kwambiri mukangoyerekeza kuidwa paudindo mumazuza kwambiri azanu zoona mulibe chisoni ndimwana wanzanu momwe akuvutikira mmm Oc oipa kwambiri mulungu akulange sure

  • @user-hn7sc3ft1f
    @user-hn7sc3ft1f 8 หลายเดือนก่อน

    That case need justice up to the end of story please Abell go ahead on that case may good Lord be with the concerned family

  • @user-yk6qn3hg5i
    @user-yk6qn3hg5i 11 หลายเดือนก่อน

    Mayi oyipa iwe mulungu akukanthe galu wamayi ngati subeleka

  • @sharrifgwape7169
    @sharrifgwape7169 ปีที่แล้ว +1

    Zovuta ndithu

  • @thokochilimba-bs2mm
    @thokochilimba-bs2mm ปีที่แล้ว +1

    This woman chilungamo akuchidziwa

  • @user-nf2fh2zr8u
    @user-nf2fh2zr8u 10 หลายเดือนก่อน

    Apolice akusogoza ndalama Koma Mmmmm zosayenda😢😢😢

  • @jennifermbewe9684
    @jennifermbewe9684 ปีที่แล้ว

    Ndipo azibambo sazindikira ndithu Nkazi okongora bwino Ngati ameneyo kumamuzuza ndithu ayi zikomo murungu akuyendere bambo iwe pomuchita chipongwe Nkazi ndimwana murungu ngwama chiritso achira mwanayo osadandaura

    • @user-rh3ts4yh4z
      @user-rh3ts4yh4z 11 หลายเดือนก่อน

      Ndipo mmene wakongolera nkaziyo ndikuzifunsa Kuti bwanji mulungu sanatikumanise ndi mayi odekha ngati uyu 😢akuchita kuoneka kuti ndiolifuna banja ndipo alindichikondi mayi uyu ❤..anyway ambuye achitepo kanthu ndithu

  • @user-ci5nc7mm8w
    @user-ci5nc7mm8w ปีที่แล้ว

    0c opanda mzelu ngati ameneyo sinamuonepo akubisa komaso akufuna kukomza zina lake chi m,mayi choipa ngati iwe sinakuonepo

  • @FlyingSquadz-nz5cl
    @FlyingSquadz-nz5cl ปีที่แล้ว +1

    For just my opinion u can go whatever you can if you have no money or if you're poor 😭 big problem and behind bars is for the people who doesn't have money

  • @user-wg5lp9zt2w
    @user-wg5lp9zt2w 6 หลายเดือนก่อน

    Kurakwa koma😢

  • @leonardkaumphawi2858
    @leonardkaumphawi2858 ปีที่แล้ว

    Apolice akumalawi amakhala ndimwano .and akakumanga omangidwa umakhala ngati chitsiru and ngati opanda ntchito kuziko..the way mmene amakulankhulira.

  • @brasiobrasio2113
    @brasiobrasio2113 ปีที่แล้ว

    Wankulu wapolisi openda nzeru ameneyo corruption inawawapweteka kuyankha mopanda nzeru ngati si mmayi

  • @chikonjiwe007
    @chikonjiwe007 2 หลายเดือนก่อน

    Lucheza police has messed up big time kodi munthu osauka usakhale ndi voice why Malawi..the child is so innocent muzikhala ndi mzimu. Azimai kodi bwanji mumakhala olimba mtima. Ndi dzikotu ili..God will punish you. Stop oppressing the voiceless..A Police munakhala njibwa kukonda ndalama..bambo wa mwana ndi sister wake muli kuti..could you please come out in the open we need to hear your side of a story..Dam la nsomba.mwayambalo will soon dry up and you will suffer for the rest of your life.

  • @giftphiri1533
    @giftphiri1533 ปีที่แล้ว

    Aaaaa inu bwanj chilungamo mukuchibitsa apa osawapanikiza mafuso iwowo akuoneka akuziwa chilungamo

  • @towellabanda2218
    @towellabanda2218 ปีที่แล้ว

    Bwanji sanawayimbire Fon?
    Amafuna kukawabela??

  • @user-cs5ss4rj7g
    @user-cs5ss4rj7g ปีที่แล้ว

    Mwaonatu amalawi tipepha mulungu alowelelepo

  • @mailosyasin3110
    @mailosyasin3110 ปีที่แล้ว

    And mkuwona kwanga pakuyenda chinyengo apa kulibwino nkhaniyi ipite kukhoti kuti apolisi ngati away atengelepo phunziro komanso chilungamo chikawoneke. Amabungwe omenyera ufulu loweleranipo basi anamiwa mulikuti

  • @FosterCement-yn4cj
    @FosterCement-yn4cj ปีที่แล้ว

    Kumwamba zikaoneka Mai Ngati kumapemphera APA mukutero Koma kumwamba mukazivera chisoni Mai mulingalire muli inu mungatani mwana Ali wanu

    • @FaithKasonjola-dj4qx
      @FaithKasonjola-dj4qx ปีที่แล้ว

      Mayi wopanda mzelu ngobeleka koma ameneyi Mulungu adzakukatha zimayi iwe phaka kunena kuti athu akumudzi iwe ndewakutawn

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 ปีที่แล้ว +2

    Mu katundu munali katundu ooopsya koma ziliko ku Malawi

  • @FosterCement-yn4cj
    @FosterCement-yn4cj ปีที่แล้ว

    Akambirana bwanji kumbali Palibe zimenezo

  • @user-cs5ss4rj7g
    @user-cs5ss4rj7g ปีที่แล้ว

    Yes mayio akunena zoona apoliceo ndiooputsa anawapasa ndalama a .o.c

  • @herbartkaphamthengo9978
    @herbartkaphamthengo9978 ปีที่แล้ว +1

    Koma Aubrey umatha kufusa mafuso komaso wapolice sakuyankha moveka

  • @user-tg1tg8wt8f
    @user-tg1tg8wt8f ปีที่แล้ว

    Mayi oyipa uyu mayi zimbili ndizakupezani wasala pang'ono

  • @chikuchimbatata3169
    @chikuchimbatata3169 10 หลายเดือนก่อน

    The officer palibe chomwe wayakha chazeru ... i wish khaniyi itatsatiridwa to the end