Kutsalemekeza msogoleli adayambitsa ndi ndi omwe akulamulilawa. Chomwe umadzala ndi chomwe umakolola. Andele muphunzilepo kanthu. Zilibe kanthu koma president ayenela adzikemekezedwa. Zidachitikadzi zidalakwika
Security yamalawi ili very weak, army comanda akuyenera kutula pansi udindo, izi zikusonyeza malawi defence is very bad, zigawenga zitha kukudilizani mukukanika anthu amaliro opanda nfuti what more zigawenga?
Ndipo Chakwera akuyenera kupeza mavuto oposa awa,, APM anapangidwa zipongwe zoposa izi,, Chomwe anabvala ndi zomwe akukolora lero,, Ndipo I think let's expect more violence between this Government of Chakwera.
Musatinyase apa ndi APM wanuyo. You are glorifying APM as if he changed Malawi in his 6 yrs of power. That old man was sleeping on his job, and the only new thing he can bring into government assuming he is given the mantle of leadership, is enriching fools that have surrounded him- the likes of Chimwemwe Chipungu, Namalomba, Chaponda, Mpinganjira Junior, Chisale, and APM's wife. Ask Liberia; they are regretting electing an old man for president. Why are some Malawian minds still stuck in the past? People have really lost their minds to think APM can change malawi's economy. I think our tribalism and regionalism are making us poorer and poorer. A nation that lacks factories to produce things for export can not transform even if it changes 10 leaders in 10 yrs.
@@tasmania527 I think you have a point but I want to assure you that even APM is old but he's better than Chakwera the Fake Pastor,, People are dying every day with hunger,, and the price of commodities is going up each and every day,, Chakwera is the worst President we never had before.
Anayambitsa wokha mcp thawi yomwe amapanga campaign 2020 now kukolola anthu a ayankhulana koma amkazitenga zopanda tchito bola mulowe mu boma lero ndizimenezi. 🔥🔥🔥
Zitsilu ndi inuyo pamenepa mumakolezera zinthu zopanda pake. Kodi mulipo angati inuyo? Mwachepa inu ka. Zigwirani ntchito za office. Kodi ndinu andale a Brian Banda? Tulukani mu office. Mumalimbana ndi President bwanji?
Ati sign yoti u president utha ndi Ndilande 😂😂😂
Kung'alura kweneko kkkkk MCP yili mumadzi
Ife sitikumufuna Kuno Ku ndilande chakwera wanuyo tizamupha ndthu asamale
Kutsalemekeza msogoleli adayambitsa ndi ndi omwe akulamulilawa. Chomwe umadzala ndi chomwe umakolola. Andele muphunzilepo kanthu. Zilibe kanthu koma president ayenela adzikemekezedwa. Zidachitikadzi zidalakwika
Anyamata inuyo mumakwana kkkkkk
😊😊u guys ulemu wanu more fire
Security yamalawi ili very weak, army comanda akuyenera kutula pansi udindo, izi zikusonyeza malawi defence is very bad, zigawenga zitha kukudilizani mukukanika anthu amaliro opanda nfuti what more zigawenga?
Zinthu szkukomad mMalawi ND2.. Chakwera sindkudziwa kt kod amamva madandowa or iai...
Koma iyi nde the best discussion,,bravo Wonder and a Bishop osaiwala state Brian
Ndipo Chakwera akuyenera kupeza mavuto oposa awa,, APM anapangidwa zipongwe zoposa izi,, Chomwe anabvala ndi zomwe akukolora lero,, Ndipo I think let's expect more violence between this Government of Chakwera.
Musatinyase apa ndi APM wanuyo. You are glorifying APM as if he changed Malawi in his 6 yrs of power. That old man was sleeping on his job, and the only new thing he can bring into government assuming he is given the mantle of leadership, is enriching fools that have surrounded him- the likes of Chimwemwe Chipungu, Namalomba, Chaponda, Mpinganjira Junior, Chisale, and APM's wife. Ask Liberia; they are regretting electing an old man for president. Why are some Malawian minds still stuck in the past? People have really lost their minds to think APM can change malawi's economy. I think our tribalism and regionalism are making us poorer and poorer. A nation that lacks factories to produce things for export can not transform even if it changes 10 leaders in 10 yrs.
@@tasmania527 I think you have a point but I want to assure you that even APM is old but he's better than Chakwera the Fake Pastor,, People are dying every day with hunger,, and the price of commodities is going up each and every day,, Chakwera is the worst President we never had before.
Amene yo ndi pulezidenti wachipaniMCP not wadziko Chifukwa ife tinatopanaye
Abusawo ndee ayankhula za nzeru
Ndirande sinama akamfunse APM
Malilo akuyenela kupasidwa ulemu osati apresident
Zinthu zina zimangofunuka strong power achakwera aaaaa alibe nzeru za usogoleri ife amalawi tikulira mokweza 😢😢😢
Apm my vote
Brian, can you that again 😂😂
The principle of sowing and reaping. APM adagendedwa ku Ndilande. Mchitidwe uwu chonde usapitilire, respect the presidency
Anayambitsa wokha mcp thawi yomwe amapanga campaign 2020 now kukolola anthu a ayankhulana koma amkazitenga zopanda tchito bola mulowe mu boma lero ndizimenezi. 🔥🔥🔥
Ndipo Chakwera akuyenera kuphedwa basi akangopitanso ku Blantyre
Imfa isanafike pakhomo....ngakhale mphaka, amasowa😢😢😢😢...lero Ma Congo angofa mosadziwika..ntsogoleri kukuwizidwa..azimai kugwidwa ku Cocain...iiiiii.... koma 2024 ithabwino???
Afunika kuima poyamba mariro adussa please nakambako cabe ine ndine muzambia ifa ilibe marile
Wonderful and nice lesson
Guys musandiseketse, azibusa nde kuti Tatsuya tiyeseko ma sheikh😅
Achakwera chonde apeweko ku ndilande zoona akudzala zomwe anakoloradi koma mulungu watembenuza flag adziwe zimenezo awa aphaso anthu achakwera chifukwa chokalandira chimanga asabwereso ku 24
Chakwela si president wathu and asamale aziyenda Ku Lilongwe konko osati Ku ndilande tizatseka misewu
Abishopu ndagwilizana nawo abusa oyamba ndi osiliza kukhala president zithele pa chakwelayu
Chakwera ndi galu
Alendo 6 aku DRC amwalira anthu 6 amwalira kolandila chimanga zikutani apa? ?
The good thing with democracy is that aliyense amayankhula zimene akufuna
Borani waziwa kuti amalawi sakumufuna enough is enough tatopa chilulowere muboma palibe cholozeka mavuto Okha Okha 😭😭
Inu mkuona ngat muligo umene ummayezara mzako anthu amakuchira chimozmoz 😮
Here in blantyre we don't need him now ........😢😢😢we are crying now
Tikuyenda ndi mikwiyo kwabasi 😂😂😂😂😂😂 asatinyasepo chakwera
Watizuza kwambili chakwela sitikumufunaso
Kkkkkk naye bishop adalowa mu program yoti siyauzimu ulendo wa ku gahena uyu
Nayeso ndi munthu ali ndi ufulu
@@lembaniharry8037 ufulu sitipanga pankhan ya uzimu bwana ngt iyeyo adasankha za uzimu zadziko azisiye kuopa kukhumudwitsa Mulungu
Vuto anthu omwe ali mbali mwawo akumva kukoma ndiye kut awauze APRESIDENT zoona zimawavuta
Achoke ameyu
90% ya apolisi ku Malawi kuno ndi ma savage
Bishop-yi waybaponso kuzipangila campaign apa
Ghetto sitikumufuna chaimayo asamale
Timalemekeza munthu wanzeru nanga Achakwera nkulemekedwa aaa
Chitsanzo ku Malawi kuno cha mtsogoleri yemwe samazolowereka kuti lero kucha bwanji, kawirikawiri samafuna kunamizidwa, even omuzungulira amamuopa, anali Bingu Wa Mutharika, MHSRIP.
Mbuzi imeneyi ikadangophedwe kt tiziva Za anthu ena sheet
Zoona wakhale umaliza m,busa wasakharaso wina oramulira dziko mwanena zoona
Chakwera zamudera ngat alindinzeru awone pamenepa
Chalwera usiye kupita ku blantyre anthu sitikumufuna olo .pang,ono pomwe .....uzalandila chipongwe osakhala masewela kutsogoloku ...galu iwe munthu wokuba
Mthawi ya APM mumati Brian ndi wa MCP lero muzitinso DPP ayi iye amangoima pa chilungamo
Ndilande ikalankhula zavuta basi ili ngati ntcheu. Watenga ntcheu pa masankho wawina basi
Kupepuka basi
Kuonesa kuti panopo presdent akunyasa bola kusamala malilo
Anthu akundilande sagawa kamba awa azathera manja!? Ubwinowake anaziyambisa okha time ya muthalika
😂😂😂 Wamalizadd busa uyuuu
akuti alindimuke
Inu Kodi malirowo ndi apulezidenti anuwo chomwe chinali patsogolo ndichani aaaaa?????
Bishop mukunena zoona kwambili BG up
Ndirande ikakwiya u president watha sudzawinanso
Ukunamatu iwe ukuona ngt udzavota wekha
Ulemu umapita kwaozipasa ulemu
Uja amati Aide De Camp
Ine chakwela akundibowa ameneyu mulungu achitepo kanthu mulungu aowonetse mphanvu zake
Wina wopepela ndi nkaka Mesa Amati sizinachitike paja Mesa amakana Kuti sizinachitike paja ndiliti mumamufunsa nkanka
Mawu obwira mtima
Bigu amapanga zimenezo osat tym iliyose pangan chakut
NOT APM KOMA ENOCK CHIHANA 2025 BOMA
🔥🔥🔥🔥 Yanyamukaa
Ife ku ntcheu kuno asadzapondeso mfiti ameneyu
Intelligent Conscious (IQ) loooooh kkkkkkkkkkkkkkk
Mukanazuzulanso nthawi yomwe anam'genda Pitala ija
Inu andemvu zamwayi inu akulu akulu mumatha president siworakwa worako ndi athu amene amayenda ndi president
Mozi wake ndizikhale ng'oma ndi chopeperadi
Komatu bwanano aumva uthengawu eeeeee
Osanye ngelera amalaw alibezeru.
Big up Brothers.
Ndi anthu opanda experience anatenga agule okha okha
The president was not wrong but atidyenawo
Achoke basi 5years yake yonunkha
Koma yah
Zitsilu ndi inuyo pamenepa mumakolezera zinthu zopanda pake. Kodi mulipo angati inuyo? Mwachepa inu ka. Zigwirani ntchito za office. Kodi ndinu andale a Brian Banda? Tulukani mu office. Mumalimbana ndi President bwanji?
Pachikhalidwe a Malawi timalemekeza Malilo A Chakwela ndi MMalawi
Fertilizer mk4500 kuti mpaka lero
Ndizabodza zimenezo
Chakwera usogoleloli wake waumbava
Koma nthawi ya Chakwelayu tiona zinthu
Koma kuli zinthu yama 2 sau heeeee
Atulutseni namalenga awakhululukire
President wamalilime ayi
Painful truth 😂😂😂😂
Anger is disappointed love
Muzikamba chirungamo ndinu okondera sadzayenda
😢😢😢😢😢😢 kape
Kkkkk Malawi
Chitsilu kumangonaza anthu sabuside bola bakilimuluzi analidolo
Chakwera Walakwa Chiyani
Ndipo.asiyedi.kubwela.kuno.
Adazala ekha mbeu yoipa muthalika adamutelonsotu mwaiwala?
Wachibwana uyu
Vote for adad
Chakwela mutu kt buuuuu 2030
Zovuta kumvetsa apule zikuwavuta ndithu
Malilime adawapweteka kwambiri
Mukulankhula bwino kwambiri
22:02
Makosana inu mumayakhula zazeru chilungamo chanu mulungu ayelese
Ganizani bwino achakwers
Buzi ikakodwa amalonda alipafupi
Alibe umunthu amenewo
Chakwera kodi ndi kanyama kanji??
Opusa iwe
Wafawafa
Mmmmmmmm