KWACHEMERATU KUSERIKU/ Achakwela VS Aku Blantyre 😱😱😱

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 26 ส.ค. 2024

ความคิดเห็น • 130

  • @user-ec4jo9cu4d
    @user-ec4jo9cu4d หลายเดือนก่อน +3

    Ati sign yoti u president utha ndi Ndilande 😂😂😂

  • @MotrickJamessakah
    @MotrickJamessakah หลายเดือนก่อน +2

    Kung'alura kweneko kkkkk MCP yili mumadzi

  • @nyararaishumba9288
    @nyararaishumba9288 7 หลายเดือนก่อน +10

    Ife sitikumufuna Kuno Ku ndilande chakwera wanuyo tizamupha ndthu asamale

  • @Wyson-bo3sp
    @Wyson-bo3sp 7 หลายเดือนก่อน +4

    Kutsalemekeza msogoleli adayambitsa ndi ndi omwe akulamulilawa. Chomwe umadzala ndi chomwe umakolola. Andele muphunzilepo kanthu. Zilibe kanthu koma president ayenela adzikemekezedwa. Zidachitikadzi zidalakwika

  • @HappyCossmas
    @HappyCossmas หลายเดือนก่อน +1

    Anyamata inuyo mumakwana kkkkkk

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 หลายเดือนก่อน

    😊😊u guys ulemu wanu more fire

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 7 หลายเดือนก่อน +2

    Security yamalawi ili very weak, army comanda akuyenera kutula pansi udindo, izi zikusonyeza malawi defence is very bad, zigawenga zitha kukudilizani mukukanika anthu amaliro opanda nfuti what more zigawenga?

  • @KelvinKandulu-v4y
    @KelvinKandulu-v4y หลายเดือนก่อน +1

    Zinthu szkukomad mMalawi ND2.. Chakwera sindkudziwa kt kod amamva madandowa or iai...

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 หลายเดือนก่อน

    Koma iyi nde the best discussion,,bravo Wonder and a Bishop osaiwala state Brian

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 7 หลายเดือนก่อน +3

    Ndipo Chakwera akuyenera kupeza mavuto oposa awa,, APM anapangidwa zipongwe zoposa izi,, Chomwe anabvala ndi zomwe akukolora lero,, Ndipo I think let's expect more violence between this Government of Chakwera.

    • @tasmania527
      @tasmania527 7 หลายเดือนก่อน

      Musatinyase apa ndi APM wanuyo. You are glorifying APM as if he changed Malawi in his 6 yrs of power. That old man was sleeping on his job, and the only new thing he can bring into government assuming he is given the mantle of leadership, is enriching fools that have surrounded him- the likes of Chimwemwe Chipungu, Namalomba, Chaponda, Mpinganjira Junior, Chisale, and APM's wife. Ask Liberia; they are regretting electing an old man for president. Why are some Malawian minds still stuck in the past? People have really lost their minds to think APM can change malawi's economy. I think our tribalism and regionalism are making us poorer and poorer. A nation that lacks factories to produce things for export can not transform even if it changes 10 leaders in 10 yrs.

    • @patrickmacheso5062
      @patrickmacheso5062 7 หลายเดือนก่อน

      @@tasmania527 I think you have a point but I want to assure you that even APM is old but he's better than Chakwera the Fake Pastor,, People are dying every day with hunger,, and the price of commodities is going up each and every day,, Chakwera is the worst President we never had before.

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f หลายเดือนก่อน +1

    Amene yo ndi pulezidenti wachipaniMCP not wadziko Chifukwa ife tinatopanaye

  • @user-dq9oe8sp8k
    @user-dq9oe8sp8k 7 หลายเดือนก่อน +1

    Abusawo ndee ayankhula za nzeru
    Ndirande sinama akamfunse APM

  • @Phill-nh8ru
    @Phill-nh8ru 7 หลายเดือนก่อน +1

    Malilo akuyenela kupasidwa ulemu osati apresident

  • @user-ir4ph3mp7f
    @user-ir4ph3mp7f 7 หลายเดือนก่อน

    Zinthu zina zimangofunuka strong power achakwera aaaaa alibe nzeru za usogoleri ife amalawi tikulira mokweza 😢😢😢

  • @user-hf4xb5ij3o
    @user-hf4xb5ij3o 6 หลายเดือนก่อน +1

    Apm my vote

  • @user-gd5po8fe4b
    @user-gd5po8fe4b หลายเดือนก่อน

    Brian, can you that again 😂😂

  • @emmanuelsambo1158
    @emmanuelsambo1158 7 หลายเดือนก่อน +2

    The principle of sowing and reaping. APM adagendedwa ku Ndilande. Mchitidwe uwu chonde usapitilire, respect the presidency

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 7 หลายเดือนก่อน

      Anayambitsa wokha mcp thawi yomwe amapanga campaign 2020 now kukolola anthu a ayankhulana koma amkazitenga zopanda tchito bola mulowe mu boma lero ndizimenezi. 🔥🔥🔥

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 7 หลายเดือนก่อน +1

      Ndipo Chakwera akuyenera kuphedwa basi akangopitanso ku Blantyre

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i 7 หลายเดือนก่อน +1

    Imfa isanafike pakhomo....ngakhale mphaka, amasowa😢😢😢😢...lero Ma Congo angofa mosadziwika..ntsogoleri kukuwizidwa..azimai kugwidwa ku Cocain...iiiiii.... koma 2024 ithabwino???

  • @FrancisBanda-g9v
    @FrancisBanda-g9v หลายเดือนก่อน

    Afunika kuima poyamba mariro adussa please nakambako cabe ine ndine muzambia ifa ilibe marile

  • @Kamdeukezimbabwesoko
    @Kamdeukezimbabwesoko หลายเดือนก่อน

    Wonderful and nice lesson

  • @HestingsJamu
    @HestingsJamu หลายเดือนก่อน

    Guys musandiseketse, azibusa nde kuti Tatsuya tiyeseko ma sheikh😅

  • @HildatoweraMhango-et4mz
    @HildatoweraMhango-et4mz 7 หลายเดือนก่อน +1

    Achakwera chonde apeweko ku ndilande zoona akudzala zomwe anakoloradi koma mulungu watembenuza flag adziwe zimenezo awa aphaso anthu achakwera chifukwa chokalandira chimanga asabwereso ku 24

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h หลายเดือนก่อน

    Chakwela si president wathu and asamale aziyenda Ku Lilongwe konko osati Ku ndilande tizatseka misewu

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 7 หลายเดือนก่อน +6

    Abishopu ndagwilizana nawo abusa oyamba ndi osiliza kukhala president zithele pa chakwelayu

  • @user-db3pq4nt9z
    @user-db3pq4nt9z หลายเดือนก่อน +1

    Chakwera ndi galu

  • @marthaBisani-vm8ig
    @marthaBisani-vm8ig 7 หลายเดือนก่อน +2

    Alendo 6 aku DRC amwalira anthu 6 amwalira kolandila chimanga zikutani apa? ?

    • @AlexMwalec
      @AlexMwalec 6 หลายเดือนก่อน

      The good thing with democracy is that aliyense amayankhula zimene akufuna

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 7 หลายเดือนก่อน +1

    Borani waziwa kuti amalawi sakumufuna enough is enough tatopa chilulowere muboma palibe cholozeka mavuto Okha Okha 😭😭

  • @MasautsoPatrickKalulu
    @MasautsoPatrickKalulu 7 หลายเดือนก่อน +1

    Inu mkuona ngat muligo umene ummayezara mzako anthu amakuchira chimozmoz 😮

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 7 หลายเดือนก่อน

    Here in blantyre we don't need him now ........😢😢😢we are crying now

  • @user-qq3ln3qr6x
    @user-qq3ln3qr6x 6 หลายเดือนก่อน

    Tikuyenda ndi mikwiyo kwabasi 😂😂😂😂😂😂 asatinyasepo chakwera

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 7 หลายเดือนก่อน +1

    Watizuza kwambili chakwela sitikumufunaso

  • @damianokachingwe3531
    @damianokachingwe3531 7 หลายเดือนก่อน +1

    Kkkkkk naye bishop adalowa mu program yoti siyauzimu ulendo wa ku gahena uyu

    • @lembaniharry8037
      @lembaniharry8037 หลายเดือนก่อน

      Nayeso ndi munthu ali ndi ufulu

    • @damianokachingwe3531
      @damianokachingwe3531 หลายเดือนก่อน

      @@lembaniharry8037 ufulu sitipanga pankhan ya uzimu bwana ngt iyeyo adasankha za uzimu zadziko azisiye kuopa kukhumudwitsa Mulungu

  • @MaxwellChiwaya-tv7kn
    @MaxwellChiwaya-tv7kn 7 หลายเดือนก่อน +1

    Vuto anthu omwe ali mbali mwawo akumva kukoma ndiye kut awauze APRESIDENT zoona zimawavuta

  • @user-gu3mp8uv3y
    @user-gu3mp8uv3y 7 หลายเดือนก่อน +1

    Achoke ameyu

  • @Clyne_Phiri_265
    @Clyne_Phiri_265 7 หลายเดือนก่อน +1

    90% ya apolisi ku Malawi kuno ndi ma savage

  • @kestenlemucha8316
    @kestenlemucha8316 หลายเดือนก่อน

    Bishop-yi waybaponso kuzipangila campaign apa

  • @MosesNjoloma
    @MosesNjoloma 7 หลายเดือนก่อน +1

    Ghetto sitikumufuna chaimayo asamale

  • @user-xo8ms5wh2s
    @user-xo8ms5wh2s 7 หลายเดือนก่อน

    Timalemekeza munthu wanzeru nanga Achakwera nkulemekedwa aaa

  • @jameschibwana2751
    @jameschibwana2751 7 หลายเดือนก่อน

    Chitsanzo ku Malawi kuno cha mtsogoleri yemwe samazolowereka kuti lero kucha bwanji, kawirikawiri samafuna kunamizidwa, even omuzungulira amamuopa, anali Bingu Wa Mutharika, MHSRIP.

  • @JoseKeyaton
    @JoseKeyaton 7 วันที่ผ่านมา

    Mbuzi imeneyi ikadangophedwe kt tiziva Za anthu ena sheet

  • @user-xf8xb2iq9i
    @user-xf8xb2iq9i 7 หลายเดือนก่อน

    Zoona wakhale umaliza m,busa wasakharaso wina oramulira dziko mwanena zoona

  • @user-vx5st6my8i
    @user-vx5st6my8i 7 หลายเดือนก่อน

    Chakwera zamudera ngat alindinzeru awone pamenepa

  • @isaaczuze
    @isaaczuze หลายเดือนก่อน

    Chalwera usiye kupita ku blantyre anthu sitikumufuna olo .pang,ono pomwe .....uzalandila chipongwe osakhala masewela kutsogoloku ...galu iwe munthu wokuba

  • @CrytonMalunga
    @CrytonMalunga 7 หลายเดือนก่อน

    Mthawi ya APM mumati Brian ndi wa MCP lero muzitinso DPP ayi iye amangoima pa chilungamo

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 7 หลายเดือนก่อน

    Ndilande ikalankhula zavuta basi ili ngati ntcheu. Watenga ntcheu pa masankho wawina basi

  • @godfreysingini1508
    @godfreysingini1508 7 หลายเดือนก่อน +1

    Kupepuka basi
    Kuonesa kuti panopo presdent akunyasa bola kusamala malilo

  • @BarnetMwanyula
    @BarnetMwanyula 6 หลายเดือนก่อน

    Anthu akundilande sagawa kamba awa azathera manja!? Ubwinowake anaziyambisa okha time ya muthalika

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 7 หลายเดือนก่อน

    😂😂😂 Wamalizadd busa uyuuu

  • @ManandosiFaluku
    @ManandosiFaluku หลายเดือนก่อน

    akuti alindimuke

  • @OustinYusuf
    @OustinYusuf 6 หลายเดือนก่อน

    Inu Kodi malirowo ndi apulezidenti anuwo chomwe chinali patsogolo ndichani aaaaa?????

  • @JafaliAjusa-zg2xi
    @JafaliAjusa-zg2xi 7 หลายเดือนก่อน

    Bishop mukunena zoona kwambili BG up

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 7 หลายเดือนก่อน

    Ndirande ikakwiya u president watha sudzawinanso

  • @MustafaLikaomba
    @MustafaLikaomba 7 หลายเดือนก่อน +1

    Ulemu umapita kwaozipasa ulemu

  • @lupakishomalangaelix6606
    @lupakishomalangaelix6606 7 หลายเดือนก่อน

    Uja amati Aide De Camp

  • @CostanceLalli
    @CostanceLalli หลายเดือนก่อน

    Ine chakwela akundibowa ameneyu mulungu achitepo kanthu mulungu aowonetse mphanvu zake

  • @ConfusedAtv-bs4gc
    @ConfusedAtv-bs4gc 7 หลายเดือนก่อน

    Wina wopepela ndi nkaka Mesa Amati sizinachitike paja Mesa amakana Kuti sizinachitike paja ndiliti mumamufunsa nkanka

  • @DoubtMoyo
    @DoubtMoyo หลายเดือนก่อน

    Mawu obwira mtima

  • @user-jq5oz7cf7k
    @user-jq5oz7cf7k 7 หลายเดือนก่อน +1

    Bigu amapanga zimenezo osat tym iliyose pangan chakut

  • @KenChitete-pg3ws
    @KenChitete-pg3ws หลายเดือนก่อน

    NOT APM KOMA ENOCK CHIHANA 2025 BOMA

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 7 หลายเดือนก่อน

    🔥🔥🔥🔥 Yanyamukaa

  • @user-xc2zm9bu1i
    @user-xc2zm9bu1i หลายเดือนก่อน

    Ife ku ntcheu kuno asadzapondeso mfiti ameneyu

  • @SteveBalakasi-qu5cn
    @SteveBalakasi-qu5cn 7 หลายเดือนก่อน

    Intelligent Conscious (IQ) loooooh kkkkkkkkkkkkkkk

  • @fraiserkapito-yb2ob
    @fraiserkapito-yb2ob 6 หลายเดือนก่อน

    Mukanazuzulanso nthawi yomwe anam'genda Pitala ija

  • @lewisdicksonmlozi130
    @lewisdicksonmlozi130 7 หลายเดือนก่อน

    Inu andemvu zamwayi inu akulu akulu mumatha president siworakwa worako ndi athu amene amayenda ndi president

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw หลายเดือนก่อน

    Mozi wake ndizikhale ng'oma ndi chopeperadi

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 7 หลายเดือนก่อน

    Komatu bwanano aumva uthengawu eeeeee

  • @user-gp7wh9in3m
    @user-gp7wh9in3m หลายเดือนก่อน

    Osanye ngelera amalaw alibezeru.

  • @amoschataika1284
    @amoschataika1284 7 หลายเดือนก่อน +2

    Big up Brothers.

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 5 หลายเดือนก่อน

    Ndi anthu opanda experience anatenga agule okha okha

  • @MakalaSchool
    @MakalaSchool หลายเดือนก่อน

    The president was not wrong but atidyenawo

  • @ClementKhomba
    @ClementKhomba หลายเดือนก่อน

    Achoke basi 5years yake yonunkha

  • @GiftMteteka-f5e
    @GiftMteteka-f5e หลายเดือนก่อน

    Koma yah

  • @mchipengule
    @mchipengule 7 หลายเดือนก่อน

    Zitsilu ndi inuyo pamenepa mumakolezera zinthu zopanda pake. Kodi mulipo angati inuyo? Mwachepa inu ka. Zigwirani ntchito za office. Kodi ndinu andale a Brian Banda? Tulukani mu office. Mumalimbana ndi President bwanji?

  • @user-je8yo3zy3y
    @user-je8yo3zy3y 7 หลายเดือนก่อน

    Pachikhalidwe a Malawi timalemekeza Malilo A Chakwela ndi MMalawi

  • @user-gu3mp8uv3y
    @user-gu3mp8uv3y 7 หลายเดือนก่อน

    Fertilizer mk4500 kuti mpaka lero

  • @MakalaSchool
    @MakalaSchool หลายเดือนก่อน

    Ndizabodza zimenezo

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 6 หลายเดือนก่อน

    Chakwera usogoleloli wake waumbava

  • @imranhabibu1743
    @imranhabibu1743 7 หลายเดือนก่อน

    Koma nthawi ya Chakwelayu tiona zinthu

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 7 หลายเดือนก่อน

    Koma kuli zinthu yama 2 sau heeeee

  • @user-du8cy6uj5m
    @user-du8cy6uj5m 7 หลายเดือนก่อน

    Atulutseni namalenga awakhululukire

  • @OptimisticTrain-vt9fj
    @OptimisticTrain-vt9fj 7 หลายเดือนก่อน

    President wamalilime ayi

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 7 หลายเดือนก่อน

    Painful truth 😂😂😂😂

  • @AnnieNamalanga-bk8mj
    @AnnieNamalanga-bk8mj 7 หลายเดือนก่อน

    Anger is disappointed love

  • @PrecioushpZawanda-mm2xf
    @PrecioushpZawanda-mm2xf 7 หลายเดือนก่อน

    Muzikamba chirungamo ndinu okondera sadzayenda

  • @user-fs3wc8ue8b
    @user-fs3wc8ue8b 6 หลายเดือนก่อน

    😢😢😢😢😢😢 kape

  • @user-el6kv3uj4p
    @user-el6kv3uj4p 7 หลายเดือนก่อน

    Kkkkk Malawi

  • @ChristopherTsakamile
    @ChristopherTsakamile 6 หลายเดือนก่อน

    Chitsilu kumangonaza anthu sabuside bola bakilimuluzi analidolo

  • @VincentAndrew-jz2gf
    @VincentAndrew-jz2gf หลายเดือนก่อน

    Chakwera Walakwa Chiyani

  • @ChrisyMbewe
    @ChrisyMbewe หลายเดือนก่อน

    Ndipo.asiyedi.kubwela.kuno.

  • @user-ld1js7dt3b
    @user-ld1js7dt3b 7 หลายเดือนก่อน

    Adazala ekha mbeu yoipa muthalika adamutelonsotu mwaiwala?

  • @TiyaMtete
    @TiyaMtete 7 หลายเดือนก่อน

    Vote for adad

  • @ThabisileKanyoza-sr4fz
    @ThabisileKanyoza-sr4fz 7 หลายเดือนก่อน

    Zovuta kumvetsa apule zikuwavuta ndithu

  • @OptimisticTrain-vt9fj
    @OptimisticTrain-vt9fj 7 หลายเดือนก่อน

    Malilime adawapweteka kwambiri

  • @DelightfulComputerChip-rp8gj
    @DelightfulComputerChip-rp8gj 7 หลายเดือนก่อน

    Mukulankhula bwino kwambiri

  • @user-ir4ph3mp7f
    @user-ir4ph3mp7f 7 หลายเดือนก่อน

    22:02

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 7 หลายเดือนก่อน

    Makosana inu mumayakhula zazeru chilungamo chanu mulungu ayelese

  • @user-hf4xb5ij3o
    @user-hf4xb5ij3o 6 หลายเดือนก่อน

    Alibe umunthu amenewo

  • @user-nm8gp1du2m
    @user-nm8gp1du2m 7 หลายเดือนก่อน

    Chakwera kodi ndi kanyama kanji??

  • @Michael-yf1tq
    @Michael-yf1tq 7 หลายเดือนก่อน

    Wafawafa

  • @daviechannel8603
    @daviechannel8603 หลายเดือนก่อน

    Mmmmmmmm