ขนาดวิดีโอ: 1280 X 720853 X 480640 X 360
แสดงแผงควบคุมโปรแกรมเล่น
เล่นอัตโนมัติ
เล่นใหม่
Bon Kalindo yu, tizimutsata bwino bwino.Siwachambatu munthuyu. Acting iyiyi sizama jokes.
Kalindo kupusitsa zitsiru zinzake km zinazi kkkk
Yehova mulungu amene munatilenga zonse tisiya mdzanja la mwana wanu yesu amen.
Kkkkk lero mwabwela ngati mwa drama koma zili zanzeru
Kkkkkk kmatu eeee dzikoli akulamuliladi ndi amafia
The DC number one 😂😂😂😂😂😂😂
Ulemu wanu the DC mumakwanila ifetu mumatiimilira ndipo tikuziwa zitsisi za boma ndipo Mulungu alinafe MCP singawine Mulungu alipo
Kkkkkk the dcc boooooooon kalindo 💪💪💪💪💪💪💪
Kmatu kwachematu 😂😂😂😂😂😂
Vuto ndi a opposition ndimakape kwambiri anthu akuwapasa malangizo Koma makani, mcp ikangowinaso anthu amakhala pa mavuto a nyoo!!
Ndiye inu a Bon KALINDO OSALANDITSA MALAWI.KWA ANTHU AWA OIPÀWA a MCP.WA..INUYO A BON KALINDO PULEZIDENT WA ANTHU OVUTIKA.@NANGA IZIZI SIZIMENE INUYO MUNACITA NDI A CHILIMA AJA .AGAINST PETER MUTHARIKA UJA .
Koma ndeee kalindo 😅😅😅😅😅
Komatu mupengetsa anthu
🤣🤣
Koma ziliko
Misala ikudutse apa aa😅😅😅
Ngati kuli koti azabera nde palibe chifukwa choti a opposition avutike ndikuzavota komwe
Longlive Bon
Koma the D.C
😂😂😂😂😂😂😂😂😅😅ufo
kkkkk koma winiko umantha
😂😂😂taseka mmaso ndipo sindiyankhula
Mulungu atithandize ndithu
Ndiye palibe kuvotatu basi 😒
Unalikotamba ndiwe wopanda nzeru iwe Ku sapota chikangawa wakoyo Za xiii amako akuvutika kumudzi musiyeni Kalindo akutitsegula maso
😂😂😂😂😂 za ziiiii
Nama drama unali kotamba iwe usanamizile maloto
Iweyo galu fiti kod ulibe chisoni ndimeme anthu akumwalilila Malawi kooo manyazi akugwiren bambo
Chokaaaa iweeeee kavule m'chenga
Nde muonatu musegula mimba Chaka chake ndichino 😮😮😮😮😮 muyaluka muonaso 😅😅😅😅😅😅😅
Bon Kalindo yu, tizimutsata bwino bwino.Siwachambatu munthuyu. Acting iyiyi sizama jokes.
Kalindo kupusitsa zitsiru zinzake km zinazi kkkk
Yehova mulungu amene munatilenga zonse tisiya mdzanja la mwana wanu yesu amen.
Kkkkk lero mwabwela ngati mwa drama koma zili zanzeru
Kkkkkk kmatu eeee dzikoli akulamuliladi ndi amafia
The DC number one 😂😂😂😂😂😂😂
Ulemu wanu the DC mumakwanila ifetu mumatiimilira ndipo tikuziwa zitsisi za boma ndipo Mulungu alinafe MCP singawine Mulungu alipo
Kkkkkk the dcc boooooooon kalindo 💪💪💪💪💪💪💪
Kmatu kwachematu 😂😂😂😂😂😂
Vuto ndi a opposition ndimakape kwambiri anthu akuwapasa malangizo Koma makani, mcp ikangowinaso anthu amakhala pa mavuto a nyoo!!
Ndiye inu a Bon KALINDO OSALANDITSA MALAWI.KWA ANTHU AWA OIPÀWA a MCP.WA..INUYO A BON KALINDO PULEZIDENT WA ANTHU OVUTIKA.@NANGA IZIZI SIZIMENE INUYO MUNACITA NDI A CHILIMA AJA .AGAINST PETER MUTHARIKA UJA .
Koma ndeee kalindo 😅😅😅😅😅
Komatu mupengetsa anthu
🤣🤣
Koma ziliko
Misala ikudutse apa aa😅😅😅
Ngati kuli koti azabera nde palibe chifukwa choti a opposition avutike ndikuzavota komwe
Longlive Bon
Koma the D.C
😂😂😂😂😂😂😂😂😅😅
ufo
kkkkk koma winiko umantha
😂😂😂taseka mmaso ndipo sindiyankhula
Mulungu atithandize ndithu
Ndiye palibe kuvotatu basi 😒
Unalikotamba ndiwe wopanda nzeru iwe Ku sapota chikangawa wakoyo Za xiii amako akuvutika kumudzi musiyeni Kalindo akutitsegula maso
😂😂😂😂😂 za ziiiii
Nama drama unali kotamba iwe usanamizile maloto
Iweyo galu fiti kod ulibe chisoni ndimeme anthu akumwalilila Malawi kooo manyazi akugwiren bambo
Chokaaaa iweeeee kavule m'chenga
Nde muonatu musegula mimba Chaka chake ndichino 😮😮😮😮😮 muyaluka muonaso 😅😅😅😅😅😅😅