MNYAMATA WA MCP KUNDIRANDE WAPEZEKA ATAFA KUNYUMBA YAKE NDIPO MOSES KUMKUYU WAYANKHULA IZI PAMALIRO

แชร์
ฝัง
  • เผยแพร่เมื่อ 20 ต.ค. 2024

ความคิดเห็น • 211

  • @Gwedeza-q3f
    @Gwedeza-q3f 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +5

    Mkuthekanso omwewa ndiwo apanga chipongwe chifukwa ndale Zanu ndizotchipa ndizakupha

  • @HamzahTwaib
    @HamzahTwaib 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +4

    Ndalama zokuba inuyoooooo anthu akumoto ndinthu 😭😭😭

  • @geofreysabola5497
    @geofreysabola5497 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

    It's sad chifukwa ndi wa MCP how many people amaphedwa kundirande how sad as a nation on Malawian expenses shame and zachibwana kwambili

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +5

    Mr Kunkuyu kms MCP yomwe mumve ichi ife kuno ku Ntcheu tikufuna Chilungamo pa imfa ya BIYENI kms anthu 8 aja osaiwala Witika Osati mabi! Ukukamba apawa aiii ndipo Ukamuuze Chimwendo kuti ali ndi masiku owelengeka.

    • @ThandiShandu-l6w
      @ThandiShandu-l6w 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Mbuzi pita page ya chilima not here kuphatikiza zinthu basi ufisi eti

    • @adamsmhone
      @adamsmhone 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

      Zachisoni amalawi kt mphaka tiyambe kuphana! zosakhala bwino. Km a kukunkhuyu mawu amenewa munalepeleranji kuyankhula mau amenewa kt kd pazana panayankhulidwa chani ngati mene mukuyankulira apa???? Km zomvesa chisoni!!!!

    • @IshmaelNesta-rb8dx
      @IshmaelNesta-rb8dx ชั่วโมงที่ผ่านมา

      ​@@ThandiShandu-l6wndi pa page pa MCP apa??? Nawe pita ku page kwako

  • @NikolasNanawe
    @NikolasNanawe 23 นาทีที่ผ่านมา +1

    a DPP kupha wa MCP 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @Willardmakande-p2q
    @Willardmakande-p2q ชั่วโมงที่ผ่านมา

    We have to start with SKC

  • @EmmanuelMphande-f4l
    @EmmanuelMphande-f4l 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +3

    Anamwa mowa ameneyo musanamize anthu

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    We need justice for SKC first

  • @juruEzra
    @juruEzra ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Time will come, koma wina mulife don't run

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +4

    Ka imfa akaka ndikakang'ono
    Tikufuna tchutchu wa imfa ya chilima

  • @afropedia_edutainment
    @afropedia_edutainment 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +9

    Tiyambe kufufuza imfa ya Chilima ndi Witika. Chifukwa ndiwa MCP ndiye imfa imeneyi ikhale yowawa? Ai kupha ndikwa MCP. Musalire lero. May the soul of Mabvuto rest in peace. Kunkuyu siyani kuononga dziko

    • @AdamMntonintshi
      @AdamMntonintshi 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ndipo live

    • @ThandiShandu-l6w
      @ThandiShandu-l6w 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Nawe Garu odya zoola ukamba zosiyana awasimaliro mbuzi iweti

    • @Yoxym
      @Yoxym 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

      ​@@ThandiShandu-l6wkoma amayenera kuyamba Kaye commission of inquiry

  • @EdsonKamwendo
    @EdsonKamwendo 28 นาทีที่ผ่านมา

    Where is Allan Witika? Your daya are numbered

  • @SandraBanda-hd1li
    @SandraBanda-hd1li 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Panyo... pako.... Kunkuyu..,.. Osanena... za. imfa .....ya.Witika.... unapha... uja... bwanji... ndiwe..... Chitsilu

  • @MadalitsoChingoma-si5jf
    @MadalitsoChingoma-si5jf 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Biyeni may his soul continue resting in peace

  • @ElsaMalunga
    @ElsaMalunga ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Man witika fist ok ngati waphedwa sizabwino nooo km wapanga izi sanakhoze inuso akukuyu yakhulani momanga osati momasura

  • @MaryNgola
    @MaryNgola 58 นาทีที่ผ่านมา

    Kunkuyu aligwaaaa ngt sakudya Ndrama zokuba zabomatu😂😂😂😂nkonowo ngt wama ARV

  • @IdirissaCharles-s8g
    @IdirissaCharles-s8g ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Moses kukuyu machende ake ndipo chisilu chamuthu dpp ikukhuzapo chani wafa wafa bass iweso kukuyu ndichakwera ukudikira zomwezi oky inalilah wainailah rahihuna

  • @FelixKachera-je4yk
    @FelixKachera-je4yk 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Nyimbo ikhale Symon and Kendall..... Nkhoya yobweza iwawila kumsanaku

  • @yasiniKalonga
    @yasiniKalonga ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Apha NDA MCP mwina amamuona kufanana ndi born Kalindo 😂😂😂😂😂😂

    • @JudithKatungwe
      @JudithKatungwe 22 นาทีที่ผ่านมา

      😂😂😂😂😂

  • @MaggieBanda-ft5tu
    @MaggieBanda-ft5tu ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mwapha nokha

  • @AdamuKasimu-x5o
    @AdamuKasimu-x5o 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +2

    Akukhuyu hule uja minthu mwawo mumayenda zandale bs kumaliro ndale hule uja apite kusitenji kurowesa ndale

  • @TimeAbilu
    @TimeAbilu ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kulankhula kwabwino(komano akuchikangawa aja bwanji) no inquary

  • @KabikaBuba
    @KabikaBuba 47 นาทีที่ผ่านมา

    Nanga nkhani yakuchikangawa bwanji si anthu ofunikila

  • @LeviChakwira
    @LeviChakwira ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Muyambe kafukufuku wa imfa ya chilima first

  • @lungisanishezi1023
    @lungisanishezi1023 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tafufuzani vice president chilima galu iwe kumkuyu

  • @AdamuKasimu-x5o
    @AdamuKasimu-x5o 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Bwanji maliro apolis ena aja akukhuyu sadapite anali bizy kukatamanga bt ndichikangawa zakunyero basi

  • @KabikaBuba
    @KabikaBuba 46 นาทีที่ผ่านมา

    Mwaiwala kuti nanu ndiakupha

  • @WisemanMvula-c6n
    @WisemanMvula-c6n 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Na umo mukupulikira apo ntheee ndimo nase tikapulikiranga pa nyifwa za ngozi ya ndege

  • @JacquereenPereira
    @JacquereenPereira 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Sitina iwale khani ya witika

  • @TameeraInglis
    @TameeraInglis ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Fufuzana kayr. Za omwe adapha. Achilima muliuze. Sziko agalu inu

  • @RaymondMikondo
    @RaymondMikondo 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ifiti imazibakirat ngat za nzeru

  • @FrankChione-k6m
    @FrankChione-k6m 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Muyambisa nkhondo inu ndimisala yanuyo nfundo mulibe

  • @marthaphiri3600
    @marthaphiri3600 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Nanga imfa ya anthu naini ku chikangawa sizinali zopusa?

  • @Memorymlumbe-j1v
    @Memorymlumbe-j1v 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mmmmmm basi vomerezan ngat mmene tinavomerezera za chilima,cheteee

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh 50 นาทีที่ผ่านมา

    Ndiy ngati ndege amaba ma phone uyu ma phone ndi ndalama zinabisala pati

  • @KeyEnoncent
    @KeyEnoncent 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    ngani Mr Witika mukuti bwanji nayo iweso muntu wakumpa forsake

  • @stevennthukwa
    @stevennthukwa 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Koma ndikudabwa akuyankulawo , akanakhala ena please ,kodi ku mcp kulibe ena?mcp khalani pansi muziona othuma according ndimbili yake please

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ifesotu tinamva pa misonkhano mukunena zoti pavute bwanji Dr Chilima salamulira ndipo munanenetsa kuti papangidwe sacrifice and munamuphadi pomaliza pake and up to now mukukana kupanga commission of inquiry meaning mukudziwapo kathu amfiti inu achabechabe mwapangitsa Anthu kukhala amkwiyo mdziko muno chifukwa chosachitapo kathu pa zaimfa ya Dr Chilima, witika ndi chipongwe chapa Mbowe omwe anapanga mukuwadziwa koma osawamanga

  • @phillimonmaila4269
    @phillimonmaila4269 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mawa anthu ena azakambanso choncho pa maliro ako

  • @KondwaniKholiyo
    @KondwaniKholiyo 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Yachilima inja bwanji mukuchedwa iwe kukuyu

  • @MadalitsoChingoma-si5jf
    @MadalitsoChingoma-si5jf 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Speechless 1 million ingagure Moyo wamunthu very shameful

  • @FrancesPeter-xw3vb
    @FrancesPeter-xw3vb 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Aaaaaaa akulu bwanji? Simudayankhule za imfa yachilima

  • @DanielZunguza
    @DanielZunguza 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nanga witika analakwa chani?

  • @BlessingsMarley-l2x
    @BlessingsMarley-l2x ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iwe ife za imfa iyiyi sikutiwawa kwenikweni koma nkhani ndi ya Biyeni SCK ndi anthu 8 aja osati zoduka mutu ukukambazi ayi Kodi a chipatalawo atayeza thupilo alipeza ndi madala? Kapena kuti mwina anachita kuombeledwa? Lelo mukuti mukufuna mufufuze zoona zenizeni za imfa imeneyi bwanji simukufuna mufufuze za imfa ya yemwe anali wachiwili wa chikangawa lion 🦁🦁🦁🦁

  • @EsnatMeleka
    @EsnatMeleka ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ndiwe galu bas nkhope yonsayo

  • @MagadaleneManjengwa
    @MagadaleneManjengwa ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tipange zakuchikangawa osati zopusazo nanu

  • @TenganiObety
    @TenganiObety 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mwapha nokha mufuna mupedze dzifukwa kwa ena MCP tikukudziwani

  • @ElsaMalunga
    @ElsaMalunga ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kd ndarama mwathira mafutazo kupita kumarilo anuyo ndi zanu kapena misokho ya amalawi zopusatu ayi tavana

  • @JkFosa
    @JkFosa 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    ameneyo ma battery ake ifa yachili osafufusaza bwanji

  • @TenganiObety
    @TenganiObety 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Dzikakhala zanu zimbveke za ena ayi?

  • @GreyMtungama
    @GreyMtungama 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Za witika,zikadzadziwika winadi adzagwetsa nkhope pasi

  • @MagadaleneManjengwa
    @MagadaleneManjengwa ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chakwela adapha chilima waphindu osati mbuzi yopanda phinduyo

  • @ElizabethKumwenda-f5h
    @ElizabethKumwenda-f5h 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Muyambe mwafufuza za anthu 9 aja kenako imeneyi za Allan witika zili pati

  • @danielmagwaya1074
    @danielmagwaya1074 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +4

    Ndege inagwa bwanji ku Chikangawa musatipondeleze plz mwat muli ndi akadawulo oziwa kufufuza za Saulos Chilima zikukanika pat

    • @PociahMack
      @PociahMack 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

      Ndiye mukafusa ndani ngat iyeyo amagwila ntchito yowulusa ndege, kakusen aku airport ndi MDF akuyakheni

  • @Gwedeza-q3f
    @Gwedeza-q3f 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Witika alikuti

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zagwa mmanja mwanu lero mesa mumati tisalire biyeni wathu

  • @aminkums515
    @aminkums515 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Chimodzimodzi mmene muzagwesele nkhope pazakuchikangawa

  • @ArronBenson-g6d
    @ArronBenson-g6d 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ku nkuyu mutu ngat diwa

  • @JACKSONHULUWA-j2n
    @JACKSONHULUWA-j2n ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tiyambe kufufuza za chilima ndi Witika

  • @temwachaima817
    @temwachaima817 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kukanika za saulos chilima za ziii

  • @ThembaniJikah
    @ThembaniJikah 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mapwala ake nkunkuyu Nanga imfa ya witikA+9 people's on cruch plane +Raph kasambala

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh 59 นาทีที่ผ่านมา

    Kodi mesa Inu akunkuyu mumayankhulira boma? Nanga mukuyankhula ngati mneneri wachipani bwanji?,aa koma

  • @EdsonMulendo
    @EdsonMulendo 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Pa maliro sipolankhula mwa mtundu umeneu nzoyambitsa zipolowe izi kunkuyu akuyenera amangidwe

  • @NdamvaScnp
    @NdamvaScnp 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    panyapako kunkuyu ifa ya anthu mudawapha mudenge aja bwanji simukufufuza panyini pamako

  • @raphaelmuliya6362
    @raphaelmuliya6362 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Akunkuyu ndinu opepela kwambili, zimenezo simfundo zapamalilo, kumasiyanitsa malilo ndi ndale

  • @TameeraInglis
    @TameeraInglis ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ayambe kukumanga iweyo unapha witika galu iwe

  • @StephanoRaphael-c7e
    @StephanoRaphael-c7e 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kodi chilima ndi anthu Ena aja Ana ndi able awo a Alibe,? Commission of inquiry bwanji simukukhazikisa mukuopa chani

  • @Chikwawa
    @Chikwawa 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Kodi Chilima ndi ena aja analibe ana ndi abale?Inu mukubweretsa mavuto ochulutsa mdziko muno.

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Be careful ndi moses chigawenga choopsa chomenechi

  • @EmmanuelJesmanphiri
    @EmmanuelJesmanphiri 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    koma maliro tisamawa pangile ndale ndizowona wagona.musayike kuti adale ndi omwe akutele akukuyu khani zaifazi zilipo zingati ku ntcheu ku thyolo ku mangochi ku balaka anthu akufuna kuziwa zoziwika koma tisasatengele ndale ndithu

  • @rajtwaihassan
    @rajtwaihassan 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Tiyambe kufufuza ifa yanthu 9 kuchikangawa

  • @EDSONNAKULENGA
    @EDSONNAKULENGA 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Amawaseka tawi yachilimabwaji olilawo ziwanikuti chitoyofufuza siyapolisiayi komaachipatalaalikuti

  • @RaheemNgoma-pk1ev
    @RaheemNgoma-pk1ev 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kumkuyu chidaz chako

  • @EDSONNAKULENGA
    @EDSONNAKULENGA 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Achakwelaanayakula zamagazi mwachitapochani zadenge akukuyu

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Muyambe kufufuza za biyeni..

  • @TamalaKambanje
    @TamalaKambanje 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Aaaaaaa yambani zinazi

  • @AlfredTengani
    @AlfredTengani 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Kunkuyu ndi kape uyu saziwa ndale

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Mumene munawombela mumanja inu paja wa utm anagwa ndi ndege

  • @EDSONNAKULENGA
    @EDSONNAKULENGA 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Musagamule apolisi asanafufuze zikusalilani

  • @ChiwaloWilliams
    @ChiwaloWilliams 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A mkukuyu tayambani za witika chigawenga chinzanucho choipa chamusata

  • @OwenchangnyaMkandawire
    @OwenchangnyaMkandawire 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Ukuyankhula zopanda nzeru,chitsiru iwe.

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Zifwamba ndi mcp

  • @wellington-w2e
    @wellington-w2e 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Uyu ndi mamuziwa ndi wamisala anapengapo

  • @wisdomblack-u8n
    @wisdomblack-u8n 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Athuwa mituyawo sikugwila coz m'malomopanga zamaliro akupanga za ndale coz akulimbana ndiachikwanje manga achikwanje kwao ndikundilande????????? Apapa muthuyotu aku mkuyu amupha okha cholonga chofunakuipisa ena.........
    ..koma sizitheka kut muipise ena anthu akufuna kafukufuku wa ndege ya chilima

  • @StephanoEbele
    @StephanoEbele 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Akuluwa mmmmm,apolice ayambile inuyo

  • @IsaqueFernandoAntônioAntônio
    @IsaqueFernandoAntônioAntônio 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iwenso ndichifwamba unapha witika

  • @ChisomoBanda-jo4ix
    @ChisomoBanda-jo4ix 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iwe udapha witika. Nyembako

  • @JohnChauma
    @JohnChauma 26 นาทีที่ผ่านมา

    Inde abwana izi mukuyankhulazi sizikusiya ndi zomwe mumayankhula chilima alimoyo kod inu akubanja la k .s .c .inuyo Akukuonani motani popeza inu ndye ndi mwana yemwe akuchita kudziwiratu kuti .m c p ndiyomwe yapha anthu 9 anja

  • @BlessingsSeleman
    @BlessingsSeleman 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Nambotu baba ajogope mlungu jwakulolaga ya mumtima

  • @StephanoRaphael-c7e
    @StephanoRaphael-c7e 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Inu kodi zakuchikangawa zikuti bwanji

  • @SeyaniTrouble
    @SeyaniTrouble 5 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Ukutinyasa iwe panga zoti muyakhule za cilima osati zimenezo

  • @AnnieMandala-z7o
    @AnnieMandala-z7o 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Imfa ya Witika,zilipati kodi.?

  • @SamisonLevison-z5p
    @SamisonLevison-z5p 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Wafa basi kankwililen pantumbo pale ameneyo

  • @AshanAlexx
    @AshanAlexx 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Aaaah koma guys Moti malilo amenewa ndiofunikila kwambiri Ku Boma eti, aaaah chabwino anthu anja muzaonaso kuwawa kwake next year

  • @WonderfulMaulana-q6d
    @WonderfulMaulana-q6d 2 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    A Kumkuyu mwaziziwa lero zimenezi?,za anthu9 aja bwanji simunaliudze dziko?.

  • @JacklineNiwahereza-ni3pm
    @JacklineNiwahereza-ni3pm 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Imfaa yaa chilima sumukufufuza basi iyiii nde muziti chani chani nkhani iyiii ndiyamalilo osayankhula zogawanitsa anthu mogwilitsa mawu ozembetsa

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 4 ชั่วโมงที่ผ่านมา +1

    Mcp ndiyokupha mwayambira kale mukuphana inu musanamizile ena ayi uku kutolana zachibwana izi ndipo muziphanabe inu simunati

  • @michaelchimwala-x8t
    @michaelchimwala-x8t 48 นาทีที่ผ่านมา

    Musayiwale kuti nanu munapha chilima APA mukudabwa chani

  • @phillimonmaila4269
    @phillimonmaila4269 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Osangochita naye bwanji

  • @PhilimonThegha
    @PhilimonThegha 3 ชั่วโมงที่ผ่านมา

    Iwe mbewa nkukuyu imwe ndimwe wakukoma wa MCP