Tiyambe kufufuza imfa ya Chilima ndi Witika. Chifukwa ndiwa MCP ndiye imfa imeneyi ikhale yowawa? Ai kupha ndikwa MCP. Musalire lero. May the soul of Mabvuto rest in peace. Kunkuyu siyani kuononga dziko
Ifesotu tinamva pa misonkhano mukunena zoti pavute bwanji Dr Chilima salamulira ndipo munanenetsa kuti papangidwe sacrifice and munamuphadi pomaliza pake and up to now mukukana kupanga commission of inquiry meaning mukudziwapo kathu amfiti inu achabechabe mwapangitsa Anthu kukhala amkwiyo mdziko muno chifukwa chosachitapo kathu pa zaimfa ya Dr Chilima, witika ndi chipongwe chapa Mbowe omwe anapanga mukuwadziwa koma osawamanga
Iwe ife za imfa iyiyi sikutiwawa kwenikweni koma nkhani ndi ya Biyeni SCK ndi anthu 8 aja osati zoduka mutu ukukambazi ayi Kodi a chipatalawo atayeza thupilo alipeza ndi madala? Kapena kuti mwina anachita kuombeledwa? Lelo mukuti mukufuna mufufuze zoona zenizeni za imfa imeneyi bwanji simukufuna mufufuze za imfa ya yemwe anali wachiwili wa chikangawa lion 🦁🦁🦁🦁
koma maliro tisamawa pangile ndale ndizowona wagona.musayike kuti adale ndi omwe akutele akukuyu khani zaifazi zilipo zingati ku ntcheu ku thyolo ku mangochi ku balaka anthu akufuna kuziwa zoziwika koma tisasatengele ndale ndithu
Inde abwana izi mukuyankhulazi sizikusiya ndi zomwe mumayankhula chilima alimoyo kod inu akubanja la k .s .c .inuyo Akukuonani motani popeza inu ndye ndi mwana yemwe akuchita kudziwiratu kuti .m c p ndiyomwe yapha anthu 9 anja
Mkuthekanso omwewa ndiwo apanga chipongwe chifukwa ndale Zanu ndizotchipa ndizakupha
Ndalama zokuba inuyoooooo anthu akumoto ndinthu 😭😭😭
It's sad chifukwa ndi wa MCP how many people amaphedwa kundirande how sad as a nation on Malawian expenses shame and zachibwana kwambili
Mr Kunkuyu kms MCP yomwe mumve ichi ife kuno ku Ntcheu tikufuna Chilungamo pa imfa ya BIYENI kms anthu 8 aja osaiwala Witika Osati mabi! Ukukamba apawa aiii ndipo Ukamuuze Chimwendo kuti ali ndi masiku owelengeka.
Mbuzi pita page ya chilima not here kuphatikiza zinthu basi ufisi eti
Zachisoni amalawi kt mphaka tiyambe kuphana! zosakhala bwino. Km a kukunkhuyu mawu amenewa munalepeleranji kuyankhula mau amenewa kt kd pazana panayankhulidwa chani ngati mene mukuyankulira apa???? Km zomvesa chisoni!!!!
@@ThandiShandu-l6wndi pa page pa MCP apa??? Nawe pita ku page kwako
a DPP kupha wa MCP 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
We have to start with SKC
Anamwa mowa ameneyo musanamize anthu
We need justice for SKC first
Time will come, koma wina mulife don't run
Ka imfa akaka ndikakang'ono
Tikufuna tchutchu wa imfa ya chilima
Ndipo live why not commission of enquiry
Tiyambe kufufuza imfa ya Chilima ndi Witika. Chifukwa ndiwa MCP ndiye imfa imeneyi ikhale yowawa? Ai kupha ndikwa MCP. Musalire lero. May the soul of Mabvuto rest in peace. Kunkuyu siyani kuononga dziko
Ndipo live
Nawe Garu odya zoola ukamba zosiyana awasimaliro mbuzi iweti
@@ThandiShandu-l6wkoma amayenera kuyamba Kaye commission of inquiry
Where is Allan Witika? Your daya are numbered
Panyo... pako.... Kunkuyu..,.. Osanena... za. imfa .....ya.Witika.... unapha... uja... bwanji... ndiwe..... Chitsilu
Biyeni may his soul continue resting in peace
Man witika fist ok ngati waphedwa sizabwino nooo km wapanga izi sanakhoze inuso akukuyu yakhulani momanga osati momasura
Kunkuyu aligwaaaa ngt sakudya Ndrama zokuba zabomatu😂😂😂😂nkonowo ngt wama ARV
Moses kukuyu machende ake ndipo chisilu chamuthu dpp ikukhuzapo chani wafa wafa bass iweso kukuyu ndichakwera ukudikira zomwezi oky inalilah wainailah rahihuna
Nyimbo ikhale Symon and Kendall..... Nkhoya yobweza iwawila kumsanaku
Apha NDA MCP mwina amamuona kufanana ndi born Kalindo 😂😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂
Mwapha nokha
Akukhuyu hule uja minthu mwawo mumayenda zandale bs kumaliro ndale hule uja apite kusitenji kurowesa ndale
Kulankhula kwabwino(komano akuchikangawa aja bwanji) no inquary
Nanga nkhani yakuchikangawa bwanji si anthu ofunikila
Muyambe kafukufuku wa imfa ya chilima first
Tafufuzani vice president chilima galu iwe kumkuyu
Bwanji maliro apolis ena aja akukhuyu sadapite anali bizy kukatamanga bt ndichikangawa zakunyero basi
Mwaiwala kuti nanu ndiakupha
Na umo mukupulikira apo ntheee ndimo nase tikapulikiranga pa nyifwa za ngozi ya ndege
Sitina iwale khani ya witika
Fufuzana kayr. Za omwe adapha. Achilima muliuze. Sziko agalu inu
Ifiti imazibakirat ngat za nzeru
Muyambisa nkhondo inu ndimisala yanuyo nfundo mulibe
Nanga imfa ya anthu naini ku chikangawa sizinali zopusa?
Mmmmmm basi vomerezan ngat mmene tinavomerezera za chilima,cheteee
Ndiy ngati ndege amaba ma phone uyu ma phone ndi ndalama zinabisala pati
ngani Mr Witika mukuti bwanji nayo iweso muntu wakumpa forsake
Koma ndikudabwa akuyankulawo , akanakhala ena please ,kodi ku mcp kulibe ena?mcp khalani pansi muziona othuma according ndimbili yake please
Ifesotu tinamva pa misonkhano mukunena zoti pavute bwanji Dr Chilima salamulira ndipo munanenetsa kuti papangidwe sacrifice and munamuphadi pomaliza pake and up to now mukukana kupanga commission of inquiry meaning mukudziwapo kathu amfiti inu achabechabe mwapangitsa Anthu kukhala amkwiyo mdziko muno chifukwa chosachitapo kathu pa zaimfa ya Dr Chilima, witika ndi chipongwe chapa Mbowe omwe anapanga mukuwadziwa koma osawamanga
Mawa anthu ena azakambanso choncho pa maliro ako
Yachilima inja bwanji mukuchedwa iwe kukuyu
Speechless 1 million ingagure Moyo wamunthu very shameful
Aaaaaaa akulu bwanji? Simudayankhule za imfa yachilima
Nanga witika analakwa chani?
Iwe ife za imfa iyiyi sikutiwawa kwenikweni koma nkhani ndi ya Biyeni SCK ndi anthu 8 aja osati zoduka mutu ukukambazi ayi Kodi a chipatalawo atayeza thupilo alipeza ndi madala? Kapena kuti mwina anachita kuombeledwa? Lelo mukuti mukufuna mufufuze zoona zenizeni za imfa imeneyi bwanji simukufuna mufufuze za imfa ya yemwe anali wachiwili wa chikangawa lion 🦁🦁🦁🦁
Ndiwe galu bas nkhope yonsayo
Tipange zakuchikangawa osati zopusazo nanu
Mwapha nokha mufuna mupedze dzifukwa kwa ena MCP tikukudziwani
Kd ndarama mwathira mafutazo kupita kumarilo anuyo ndi zanu kapena misokho ya amalawi zopusatu ayi tavana
ameneyo ma battery ake ifa yachili osafufusaza bwanji
Dzikakhala zanu zimbveke za ena ayi?
Za witika,zikadzadziwika winadi adzagwetsa nkhope pasi
Chakwela adapha chilima waphindu osati mbuzi yopanda phinduyo
Muyambe mwafufuza za anthu 9 aja kenako imeneyi za Allan witika zili pati
Ndege inagwa bwanji ku Chikangawa musatipondeleze plz mwat muli ndi akadawulo oziwa kufufuza za Saulos Chilima zikukanika pat
Ndiye mukafusa ndani ngat iyeyo amagwila ntchito yowulusa ndege, kakusen aku airport ndi MDF akuyakheni
Witika alikuti
Zagwa mmanja mwanu lero mesa mumati tisalire biyeni wathu
Chimodzimodzi mmene muzagwesele nkhope pazakuchikangawa
Ku nkuyu mutu ngat diwa
Tiyambe kufufuza za chilima ndi Witika
Kukanika za saulos chilima za ziii
Mapwala ake nkunkuyu Nanga imfa ya witikA+9 people's on cruch plane +Raph kasambala
🇲🇼
Kodi mesa Inu akunkuyu mumayankhulira boma? Nanga mukuyankhula ngati mneneri wachipani bwanji?,aa koma
Pa maliro sipolankhula mwa mtundu umeneu nzoyambitsa zipolowe izi kunkuyu akuyenera amangidwe
panyapako kunkuyu ifa ya anthu mudawapha mudenge aja bwanji simukufufuza panyini pamako
Akunkuyu ndinu opepela kwambili, zimenezo simfundo zapamalilo, kumasiyanitsa malilo ndi ndale
Ayambe kukumanga iweyo unapha witika galu iwe
Kodi chilima ndi anthu Ena aja Ana ndi able awo a Alibe,? Commission of inquiry bwanji simukukhazikisa mukuopa chani
Kodi Chilima ndi ena aja analibe ana ndi abale?Inu mukubweretsa mavuto ochulutsa mdziko muno.
Be careful ndi moses chigawenga choopsa chomenechi
koma maliro tisamawa pangile ndale ndizowona wagona.musayike kuti adale ndi omwe akutele akukuyu khani zaifazi zilipo zingati ku ntcheu ku thyolo ku mangochi ku balaka anthu akufuna kuziwa zoziwika koma tisasatengele ndale ndithu
Tiyambe kufufuza ifa yanthu 9 kuchikangawa
Amawaseka tawi yachilimabwaji olilawo ziwanikuti chitoyofufuza siyapolisiayi komaachipatalaalikuti
Kumkuyu chidaz chako
Achakwelaanayakula zamagazi mwachitapochani zadenge akukuyu
Muyambe kufufuza za biyeni..
Aaaaaaa yambani zinazi
Kunkuyu ndi kape uyu saziwa ndale
Mumene munawombela mumanja inu paja wa utm anagwa ndi ndege
Musagamule apolisi asanafufuze zikusalilani
A mkukuyu tayambani za witika chigawenga chinzanucho choipa chamusata
Ukuyankhula zopanda nzeru,chitsiru iwe.
Zifwamba ndi mcp
Uyu ndi mamuziwa ndi wamisala anapengapo
Athuwa mituyawo sikugwila coz m'malomopanga zamaliro akupanga za ndale coz akulimbana ndiachikwanje manga achikwanje kwao ndikundilande????????? Apapa muthuyotu aku mkuyu amupha okha cholonga chofunakuipisa ena.........
..koma sizitheka kut muipise ena anthu akufuna kafukufuku wa ndege ya chilima
Akuluwa mmmmm,apolice ayambile inuyo
Iwenso ndichifwamba unapha witika
Iwe udapha witika. Nyembako
Inde abwana izi mukuyankhulazi sizikusiya ndi zomwe mumayankhula chilima alimoyo kod inu akubanja la k .s .c .inuyo Akukuonani motani popeza inu ndye ndi mwana yemwe akuchita kudziwiratu kuti .m c p ndiyomwe yapha anthu 9 anja
Nambotu baba ajogope mlungu jwakulolaga ya mumtima
Inu kodi zakuchikangawa zikuti bwanji
Ukutinyasa iwe panga zoti muyakhule za cilima osati zimenezo
Imfa ya Witika,zilipati kodi.?
Wafa basi kankwililen pantumbo pale ameneyo
Aaaah koma guys Moti malilo amenewa ndiofunikila kwambiri Ku Boma eti, aaaah chabwino anthu anja muzaonaso kuwawa kwake next year
A Kumkuyu mwaziziwa lero zimenezi?,za anthu9 aja bwanji simunaliudze dziko?.
Imfaa yaa chilima sumukufufuza basi iyiii nde muziti chani chani nkhani iyiii ndiyamalilo osayankhula zogawanitsa anthu mogwilitsa mawu ozembetsa
Mcp ndiyokupha mwayambira kale mukuphana inu musanamizile ena ayi uku kutolana zachibwana izi ndipo muziphanabe inu simunati
Musayiwale kuti nanu munapha chilima APA mukudabwa chani
Osangochita naye bwanji
Iwe mbewa nkukuyu imwe ndimwe wakukoma wa MCP